< Yoube 19 >

1 Yoube da amane sia: i,
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Dilia da abuliba: le sia: ga nama se iahabela: ?
“Kodi mudzakhala mukundizunza mpaka liti, ndi kundilasa ndi mawu anuwo?
3 Dilia da mae fisili, nama sisa: nonana. Amola dilia da nama wadela: le hamobeba: le, hame gogosiasa.
Inuyo mwandinyoza kwambiri; mwanditsutsa mopanda manyazi.
4 Be amomane, na da wadela: i hou hamoi ganiaba, amo da dilima se hame ia: noba.
Ngati ndi zoona kuti ine ndasochera, cholakwachotu nʼchanga.
5 Dilia da dilia noga: i hou da na hou baligiliyale dawa: sa. Dilia da nama doaga: i bidi hamosu da na wadela: i hou olelebeyale dawa: sa.
Ngati ndithudi mukudziyika nokha pamwamba panga, ndi kugwiritsa ntchito kunyozedwa kwanga polimbana nane,
6 Gode da amo bidi hamosu nama iasi dagoi. Dilia abuliba: le amo hou hame ba: sala: ? Gode da na sa: ima: ne efegelesi.
pamenepa dziwani kuti Mulungu wandilakwira ndipo wandizinga ukonde wake.
7 Na da Ea nama ha lai hou higabeba: le, egasa. Be dunu afae da na egasu hame naba. Na da moloidafa fofada: ma: ne wele sia: sa, be dunu afae da hame naba.
“Ngakhale ndifuwule kuti, ‘Akundizunza!’ Palibe wondiyankha; ngakhale ndipemphe thandizo, palibe wondichitira zolungama.
8 Gode da na logo ga: i dagoi amola na da amoga bu masunu hame dawa: E da na logo gasiga uligilisi dagoi.
Mulungu wanditsekera njira yanga kotero sindingathe kudutsa; waphimba njira zanga ndi mdima.
9 E da na gagui liligi huluane samogei dagoi. Musa: , eno dunu da na da mimogo dunuyale dawa: i. Be wali ilia na higasa.
Iye wandilanda ulemu wanga ndipo wandivula chipewa chaufumu pamutu panga.
10 E da na da: i la: idi la: idi fanana. E da na udigili bioma: ne amola bogoma: ne yolesisa.
Wandiphwanyaphwanya mbali zonse ndipo ndatheratu; Iye wazula chiyembekezo changa ngati mtengo.
11 Gode da ougi bagade, E da nama ha: giwane halasa. E da Ea ha laidafa dunuma hamosa, amo defele nama hamosa.
Wandikwiyira ndipo akundiyesa mmodzi mwa adani ake.
12 E da Ea dadi gagui wa: i, nama doagala: musa: , asunasisa. Ilia da gegemusa: osobo hagali dogonana, amola na abula diasuga doagala: sa.
Ankhondo ake akubwera kwa ine mwamphamvu, akonzekera zodzalimbana nane ndipo azungulira nyumba yanga.
13 Gode Ea hamobeba: le, na olalali da na yolesi dagoi. Dunu amo da musa: na dawa: digi, da wali na da ga fi dunu agoai ba: sa.
“Mulungu wandisiyanitsa ndi abale anga; wasandutsa odziwana nane kukhala achilendo kwa ine.
14 Na fi dunu amola na: iyado dunu huluane da asi dagoi.
Abale anga andithawa; abwenzi anga andiyiwala.
15 Dunu amo na da na diasuga aowai, ilia huluane da na gogolei. Na hawa: hamosu uda ilia ga fi dunuma hamobe defele, nama hamosa.
Anthu odzacheza ku nyumba kwanga ndiponso antchito anga aakazi andisandutsa mlendo; ndasanduka mlendo mʼmaso mwawo.
16 Na da na hawa: hamosu dunu, e na fidima: ne nama misa: ne ha: giwane edegesea, e da nama hame adole iaha.
Ndikayitana wa ntchito wanga, iye sandiyankha, ngakhale ndikapempha ndi pakamwa panga sandichitira kanthu.
17 Na uda da na lafi holo ahoabe, amo ea gaha bagade higasa. Amola nolalidafa ilia da nama hame gadenena maha.
Mpweya wanga umamunyansa mkazi wanga; ndine chinthu chonyansa kwa abale anga a mimba imodzi.
18 Mano fonobahadi da na higale ba: sa. Ilia da naba: le habosesele oufesega: sa.
Inde, ngakhale ana amandinyoza; akandiona amandinyodola.
19 Na na: iyadodafa dunu ilia da na higale ba: sa. Nama dogolegei ilia da sinidigili nama ha lai hamoi.
Anzanga onse apamtima amanyansidwa nane; iwo amene ndinkawakonda andiwukira.
20 Na gadofo da udigili abula agoane, na gasaga gosagisi dialebe ba: sa. Na da gadenenewane bogoi dagoi.
Ndangotsala khungu ndi mafupa okhaokha; ndapulumuka lokumbakumba.
21 Dilia da na samalali! Amaiba: le, nama asigima! Gode da na dafama: ne fai dagoi.
“Mvereni chisoni, inu abwenzi anga, mvereni chisoni, pakuti dzanja la Mulungu landikantha.
22 Gode da nama se bagade iaha. Dilia abuliba: le, Ea hou defele, nama se iahabela: ? Dilia da nama se nabasu defele i dagoi!
Chifukwa chiyani mukundilondola ngati Mulungu? Kodi simunatope nalo thupi langa?
23 Na da agoane hanai gala. Dunu afae da na sia: mae gogolema: ne, meloa bioi amoga dedene legemu da defea.
“Aa, achikhala mawu anga analembedwa, achikhala analembedwa mʼbuku,
24 O e da ouliga hamoi nusi (chisel) amoga igi da: iya dedemu da defea. Amasea, na sia: da mae fisili, eso huluane dialumu.
akanalembedwa pa mwala ndi chitsulo, akanalembedwa pa thanthwe kuti sangathe kufufutidwa!
25 Be na dawa: ! Na esalusu Bu Bidi Lamu dunu da Hebene ganodini esalalala. E da dagomu esoga osobo bagade da: iya, na gaga: ma: ne lelumu.
Koma ndikudziwa kuti mpulumutsi wanga ali ndi moyo, ndipo pa nthawi yomaliza adzabwera kudzanditeteza.
26 Amola na da: i da wadela: lesi dagoi ba: mu. Be na da na osobo bagade da: i hodo ganodini esalea, na da Gode ba: mu.
Ndipo khungu langa litatha nʼkuwonongeka, mʼthupi langa lomweli ndidzamuona Mulungu.
27 Na da na sidafa amoga E ba: mu. Amola E da ga fi dunu agoane hame ba: mu.
Ine ndemwe ndidzamuona Iye ndi maso angawa, ineyo, osati wina ayi. Ndithu mtima wanga ukufunitsitsadi!
28 Dilia da nama se ima: ne amola doagala: ma: ne, logo hogoi helei. Amaiba: le, na da beda: i galu.
“Koma inu mukuti, ‘Haa! Tingamuzunze bwanji, popeza kuti zonsezi zaoneka chifukwa cha iye yemweyo?’
29 Be wali, dilia beda: mu da defea. Gode da wadela: i houba: le ougi bagadedafa, amola Ea ougi hou da gegesu gobihei bagade agoane. Dilia amoga beda: ma! Bai fa: no dilia da Moloidafa Fofada: su Dunu da esalebe dawa: mu.
Inu muyenera kuopa lupanga; pakuti mkwiyo wake umalangadi ndi lupanga; zikadzatero muzadziwa kuti chiweruzo chilipo ndithu.”

< Yoube 19 >