< Yoube 10 >

1 Na da esalumu hihi gala. Na egasu sia: nabima!
“Ine ndatopa nawo moyo wanga; choncho ndidzanena zodandaula zanga momasuka ndipo ndidzayankhula mwa kuwawidwa mtima kwanga.
2 Gode! Na bogoma: ne, mae fofada: ma! Nama adoma! Na da adi hamoiga fofada: bela: ?
Ndidzati kwa Mulungu wanga: Musandiweruze kuti ndine wolakwa, koma mundiwuze chifukwa chimene Inu mukukanganira ndi ine.
3 Di da nama mae asigiliwane se ianumu da defeala: ? Di da na hamoi dagoi. Amaiba: le, Dia wali na higamu da defeala: ? Amola Di da wadela: le hamosu dunu ilia wadela: i ilegesu hahawane ba: mu da defeala: ?
Kodi mumakondwera mukamandizunza, kunyoza ntchito ya manja anu, chonsecho mukusekerera ndi zochita za anthu oyipa?
4 Di da nini osobo bagade dunu ninia hou defele, liligi ba: sala: ?
Kodi maso anu ali ngati a munthu? Kodi mumaona zinthu monga momwe amazionera munthu?
5 Dia esalebe ode da ninia esalebe ode defele dunumunihadi ganabela: ? Hame mabu!
Kodi masiku anu ali ngati masiku a munthu, kapena zaka zanu ngati zaka za munthu,
6 Amaiba: le, Dia da abuliba: le na wadela: i hou huluane hogosala: ? Amola na giadofai huluane benea ahoasu defele ba: sala: ?
kuti Inu mufufuze zolakwa zanga ndi kulondola tchimo langa,
7 Di dawa: ! Na da wadela: le hame hamoi. Amola Di da nama doagala: sea, enoga na gaga: mu da hamedei.
ngakhale mukudziwa kuti sindine wolakwa ndiponso kuti palibe amene angandilanditse mʼdzanja lanu?
8 Di da Dia loboga na da: i hamoi dagoi. Be wali Di da Dia loboga, na gugunufinisisa.
“Munandiwumba ndi kundipanga ndi manja anu. Kodi tsopano Inu mudzatembenuka ndi kundiwononga?
9 Di da na osoboga hamoi dagoi, amo mae gogolema! Be wali Di da na goudane, bu gulu hamoma: bela: ?
Kumbukirani kuti munandipanga ndi dothi, kodi tsopano mundibwezeranso ku fumbi?
10 Di da na ada na hamoma: ne, ema gasa i. Dia na ame ea hagomo ganodini, na hamoi dagoi.
Suja munapatsa abambo anga mphamvu zoti andibale, suja munandikuza bwino mʼmimba mwa amayi anga?
11 Di da na da: i hodo amola gasa amola momoge hamoi. Di da na gasa amo huga amola gadofoga dedebolesi.
Munandikuta ndi khungu ndi mnofu ndi kundilumikiza pamodzi ndi mafupa ndi mitsempha?
12 Di da nama esalusu amola asigi hou i dagoi. Di da na noga: le ouligibiba: le, na da esalebe goea.
Munandipatsa moyo ndi kundionetsa chifundo chanu, ndipo munasamalira bwino moyo wanga.
13 Be na da wali dawa: Amo musa: esoga, Di da wamowane na wadela: musa: ilegelalu.
“Koma izi ndi zimene munabisa mu mtima mwanu, ndipo ndikudziwa kuti zinali mʼmaganizo anu:
14 Di da na wadela: le hamosa: besa: le, eso huluane na hou ha: giwane sosodosu. Amola na da wadela: le hamoi ganiaba, Di da amo hou hame gogolema: ne olofomu dawa: la: loba.
Kuti ngati ndingachimwe mudzakhala mukundipenyetsetsa ndipo kuti simudzalola kuti ndisalangidwe chifukwa cha kulakwa kwanga.
15 Na da fonobahadi fawane wadela: le hamosea, na da Dia se dabe iasu ba: sa. Be na da moloidafa hamosea, Dia hahawane iasu hame ba: sa. Na da da: i dioi bagade amola bagadewane gogosiasa.
Ngati ndili wolakwa, tsoka langa! Koma ngakhale ndili wosalakwa sindingathe kutukula mutu wanga, pakuti ndagwidwa ndi manyazi ndipo ndamizidwa mʼmavuto anga.
16 Na da noga: le didili hamosea, dunu da laione wa: me fane legemusa: benea ahoabe amo defele, Di da na sebobogesa. Di da na se nabima: ne, musa: hame ba: su gasa bagade hou amolawane hamosa.
Ndipo ndikatukula mutu wanga, Inu mumandisaka ngati mkango ndiponso mumandiopseza ndi mphamvu yanu.
17 Di da eso huluane na dafama: ne, ba: su dunu ilegesa. Dia ougi hou da nama doagaga: sa heda: sa. Di da eso huluane nama gaheabolo doagala: musa: ilegesa.
Mumabweretsa mboni zatsopano potsutsana nane ndipo mkwiyo wanu pa ine umanka nukulirakulira ndi magulu anu olimbana nane amanka nachulukirachulukira.
18 Gode! Dia da abuliba: le na lalelegema: ne hamobela: ? Na dunu enoga mae ba: le bogomu da defea galu.
“Chifukwa chiyani Inu munalola kuti ndibadwe? Ndi bwino ndikanafa diso lililonse lisanandione.
19 Na da hamedafa lalelegemu da defea galu. Be amai hame galea, na da lalelegeloba, hedolo bogomu da defea galu.
Ndikanapanda kubadwa, kapena akanangonditenga nditabadwa kupita nane ku manda!
20 Na esalusu da gadenene agoane dagobela: ? Na yolesima! Na da fonobahadi fawane bu esalumu. Amaiba: le, amo eso bagahamega hahawane esalumusa: , Dia logo doasima!
Kodi masiku anga owerengeka sali pafupi kutha? Ndilekeni kuti ndipumule pangʼono pokha
21 Na da gadenenewane ahoabe goea. Na da bu hame misunu. Na da gasi galebe sogega masunu.
ndisanapite ku malo amene munthu sabwererako ku dziko la imfa ndi kwa mdima wandiweyani,
22 Amo soge da gasi bagade. Amo ganodini baba bagohame gala. Amo soge da ededenasu soge. Amola amoga hadigi da gasi agoane ba: sa.”
ku dziko la mdima wandiweyani ndi chisokonezo, kumene kuwala kumakhala ngati mdima.”

< Yoube 10 >