< Yelemaia 52 >

1 Sedegaia ea lalelegei ode21 gidigili, e da Yuda hina bagade hamoi dagoi ba: i. E da ode gidayale gala, Yelusaleme amo ganodini esalu, Yuda soge ouligi. Ea ame dio da Hamiudale (e da Libina dunu Yelemaia amo ea idiwi).
Zedekiya anali wa zaka 21 pamene analowa ufumu, ndipo analamulira zaka 11 ku Yerusalemu. Amayi ake anali Hamutali mwana wa Yeremiya wa ku Libina.
2 Hina bagade Sedegaia da hina bagade Yihoiagimi ea hou defele, Hina Godema wadela: le hamoi.
Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Yehoyakimu.
3 Hina Gode da Yelusaleme amola Yuda fi ilima bagadewane ougiba: le, E da ili mae ba: ma: ne, mugululi masa: ne, sefasi. Sedegaia da Ba: bilone hina bagade, Nebiuga: denese, ema odoga: i.
Chifukwa cha zonse zimene zinachitika ku Yerusalemu ndi ku Yuda Yehova anakwiyira anthu ake mpaka kuwachotsa pamaso pake. Tsono Zedekiya anawukira mfumu ya ku Babuloni.
4 Amaiba: le, Nebiuga: denese amola ea dadi gagui wa: i da misini, eso nabuane amola oubi nabuane Sedegaia ea Yuda soge ouligisu ode sesegeyalega, Yelusalemema doagala: i. Ilia wa: i fisisu diasu moilai gadili gagui, amalu doagala: musa: osobo gasa: le lelegela heda: le,
Choncho mʼchaka cha chisanu ndi chinayi cha ulamuliro wa Zedekiya, mwezi wakhumi, pa tsiku la khumi, Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni anabwera ndi ankhondo ake onse kudzathira nkhondo Yerusalemu. Anamanga misasa ndi mitumbira yankhondo kunja kuzungulira mzindawo.
5 doagala: lalu, Sedegaia ea ouligisu ode gida gala amoga hasali.
Mzindawo unazingidwa mpaka chaka cha khumi ndi chimodzi cha ulamuliro wa Mfumu Zedekiya.
6 Amo ode amogawane, eso sesege amola oubi biyadu amoga, Yelusaleme dunu da ha: i bagadeba: le, ha: i manu hame ba: i.
Pa tsiku lachisanu ndi chinayi la mwezi wachinayi njala inakula kwambiri mu mzindamo kotero kuti munalibe chakudya choti anthu nʼkudya.
7 Amo esoga, Ba: bilone dunu da gagoi dobea mugului dagoi. Ba: bilone dadi gagui dunu da Yelusalemega sisiga: le esalebe ba: i. Be Yuda dadi gagui dunu huluane da gasia hobea: i. Ilia da hina bagade ea ifabi golili sa: ili, logo holei amo da dobea aduna ela disisu amoga diala, amoga asili, Yodane fago amoga doaga: musa: hobea: i.
Tsono linga la mzindawo linabowoledwa, ndipo ankhondo onse anathawa. Iwo anatuluka mu mzindamo usiku kudzera pa chipata cha pakati pa makoma awiri a pafupi ndi munda wa mfumu, ngakhale kuti Ababuloni anali atazinga mzindawo. Ndipo anathawira ku Araba,
8 Be Ba: bilone dadi gagui wa: i da hina bagade Sedegaia ema fa: no bobogele, umi soge Yeligou moilai bai bagade gadenene, amoga e gagulaligi. Amalalu, Sedegaia ea dadi gagui dunu huluane da e yolesili hobea: i.
koma gulu la ankhondo la ku Babuloni linalondola mfumu Zedekiya ndi kumupeza mʼchigwa cha ku Yeriko. Ankhondo onse anamusiya yekha nabalalika.
9 Ilia da Sedegaia amo hina bagade Nebiuga: denesema oule asi. E da Libila moilai bai bagade Ha: ima: de soge ganodini diala amogawi esalebe ba: i. Amogawi, Nebiuga: denese da Sedegaiama se ima: ne fofada: i.
Anagwidwa napita naye kwa mfumu ya ku Babuloni ku Ribula mʼdziko la Hamati, kumene anagamula mlandu wake.
10 Libila moilai bai bagadega e da Sedegaia ba: ma: ne, egefelali medole legema: ne sia: i. Amola, ea sia: beba: le, ilia da Yuda eagene ouligisu dunu medole lelegei.
Ku Ribulako mfumu ya ku Babuloni inapha ana aamuna a Zedekiya iyeyo akuona; ndiponso inapha akuluakulu onse a ku Yuda.
11 Amalalu, ea sia: beba: le, ilia da Sedegaia ea si aduna duga: le fasili, e efega la: gili, Ba: bilone sogega hiouginana asi. Sedegaia da Ba: bilone soge gagili ga: i diasu ganodini esalu, amogainini e da amogawi bogoi.
Ndipo inamukolowola maso Zedekiya, ndi kumumanga ndi maunyolo a mkuwa nʼkupita naye ku Babuloni kumene inakamuyika mʼndende kuti akhalemo moyo wake wonse.
12 Oubi bi, eso nabu, Ba: bilone hina bagade ea ode19 ouligibiga, Nebiusala: ida: ne (hina bagade ea fada: i sia: su dunu amola ea dadi gagui wa: i ouligisu dunu) da Yelusaleme moilai bai bagade golili sa: i.
Mwezi wachisanu, pa tsiku lakhumi, chaka cha 19 cha ulamuliro wa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni, Nebuzaradani mtsogoleri wa ankhondo a mfumu, amene amatumikira mfumu ya ku Babuloni, anabwera ku Yerusalemu.
13 E da Debolo diasu amola hina bagade diasu amola Yelusaleme dunu mimogo ilia diasu huluane laluga ulagi dagoi.
Ndipo anatentha Nyumba ya Yehova, nyumba ya mfumu ndi nyumba zonse za mu Yerusalemu. Anatentha nyumba iliyonse.
14 Amola ea dadi gagui dunu da moilai dobea gadelale sali.
Tsono gulu lonse lankhondo la Ababuloni limene linali ndi mtsogoleri wa ankhondo a mfumu uja linagwetsa malinga onse ozungulira Yerusalemu.
15 Amalalu, Nebiusala: ida: ne da dunu amo moilai bai bagade ganodini esala, amola bagade dawa: su hawa: hamosu dunu hame bogoi esala, amola dunu amo da hohonone, Ba: bilone ilia la: idi amoga asi, amo huluane Ba: bilone sogega oule asi.
Nebuzaradani mtsogoleri wa ankhondo anatenga anthu amene anatsala mu mzindamo, anthu aluso pamodzi ndi amene anadzipereka kale kwa mfumu ya ku Babuloni kupita nawo ku ukapolo ku Babuloni.
16 Be baligili hame gagui dunu amo da soge hame gagui, amo e da waini sagai amola ifabi ganodini hawa: hamomusa: , Yuda sogega esaloma: ne yolesi.
Komabe Nebuzaradani mtsogoleri wa ankhondo anasiya anthu ena onse osaukitsitsa a mʼdzikomo kuti azigwira ntchito mʼminda ya mpesa ndi minda ina.
17 Ba: bilone dunu da balasega hamoi duni bugi amola ‘gaguli fula ahoasu’ amola balasega hamoi sisiga: i ofodo sugi bagade (hano nasu bagade) Debolo diasu ganodini dialu, amo fifili, balase huluane Ba: bilone sogega gaguli asi.
Ababuloni anaphwanya nsanamira za mkuwa, maphaka ndi chimbiya chamkuwa zimene zinali mʼNyumba ya Yehova. Anatenga mkuwa wonsewo nʼkupita nazo ku Babuloni.
18 Amola ilia da safala amola nasubu ofodo (amo da oloda dodofemusa: gala) amola gamali hahamosu liligi, amola ofodo amoga ilia da gobele salasu maga: me lasu, amola ofodo amoga ilia da gabusiga: manoma gobesisu, amola balase liligi huluane amoga ilia da Debolo diasuga hawa: hamosu, amo huluane ilia da gaguli asi.
Ankhondowo anatenganso mbiya, zochotsera phulusa, zozimitsira nyale, mbale zofukizira lubani, zikho pamodzi ndi ziwiya zina zonse za mkuwa zimene ankagwiritsira ntchito mʼNyumba ya Yehova.
19 Ilia da liligi huluane amo da gouli o silifa amoga hamoi, (ofodo fonobahadi, ofodo amoga ilia da laluso gaguli ahoasu, ofodo amoga ilia da gobele salasu maga: me lasu, nasubu ofodo, gamali ilia bai, ofodo amo ganodini ilia da gabusiga: manoma gobesisu, amola faigelei amoga ilia da waini hano iasu sogadigisu, amo liligi huluane Ba: bilone dunu da ilia sogega gaguli asi.
Nebuzaradani uja anatenganso mabeseni, ziwiya zosonkhapo moto, mbale zowazira madzi, zoyikapo nyale, zipande zofukizira lubani ndi zikho ndi zina zonse zagolide ndi siliva.
20 Balasega hamoi liligi amo hina bagade Soloumane da Debolo diasu ganodini amoga hawa: hamoma: ne hamoi (duni bugi aduna, ‘gaguli fula ahoasu’, hano nasu bagade [sisiga: i ofodo sugi bagade] amola bulamagau gawali fagoyale gala amo hagudu dialu) amo da dioi bagadeba: le, ilia dioi defei dawa: mu da hamedei ba: i.
Nsanamira ziwiri zija, chimbiya, maphaka ndi ngʼombe khumi ndi ziwiri za mkuwa zochirikizira chimbiyacho zimene mfumu Solomoni anapangira Nyumba ya Yehova kulemera kwake kunali kosawerengeka.
Nsanamira imodzi kutalika kwake kunali mamita asanu ndi atatu, akazunguliza chingwe inali mamita asanu ndi theka; mʼkati mwake munali bowo ndipo kuchindikala kwake kunali zala zinayi.
22 Duni bugi aduna ela da defele ba: i. Ela gado defei da 8 mida amola sisiga: le defei da 5.3mida. Ilia dogoa da gelabai amola balase ea gadugagi defei da 75milimida ba: i. Duni bugi afae afae amo da: iya balasega hamoi habuga agoane dialebe ba: i. Ela gado defei da 2.2mida. Amola ea baiga da balase esa agoane. Amoga da ‘bomegala: nidi’ fage balasega hamoi dialebe ba: i.
Pamwamba pa nsanamira iliyonse panali mutu wamkuwa umene kutalika kwake kunali mamita awiri. Pozungulira pake panali ukonde ndi makangadza, zonsezo za mkuwa. Nsanamira inayo inalinso ndi makangadza ake ndipo inali yofanana ndi inzake ija.
23 Duni bugi afae afae ea gigiadomai amoga ‘bomegala: nidi’ fage100agoane dedei dialebe ba: i. Dunu da osoboga lelu, amo huluane ba: musa: dawa: i.
Mʼmbali mwake munali makangadza 96; makangadza onse pamodzi analipo 100 kuzungulira ukonde onse.
24 Nebiusala: ida: ne, dadi gagui ouligisudafa, da gobele salasu ouligisudafa Sila: ia, amola e bagia gobele salasu dunu Sefanaia, amola Debolo ouligisu dunu bagade udiana eno, amo gagulaligili, se iasu diasu hawa: hamomusa: afugili asi.
Mtsogoleri wa ankhondo uja, anagwira Seraya mkulu wa ansembe ndi Zefaniya, wachiwiri wa mkulu wa ansembe ndi alonda atatu apachipata.
25 E da Yelusalemega Yuda dadi gagui ilia ouligisudafa, hina bagade ea fada: i sia: ne iasu dunu fesuale (amo da moilai amo ganodini esalebe ba: i), dadi gagui ouligisudafa ea fidisu dunu (amo da dadi gagui wa: i ilia meloa dedei ouligisu) amola dunu mimogo60 agoane eno amo Ba: bilone hina bagade Libila moilai bai bagade, Ha: ima: de soge ganodini amoga esalu, ema oule asi. Hina bagade da sia: beba: le, ilia da amo dunu huluane fananu, medole legei dagoi. Yuda dunu huluane da ilia sogedafa amoga fadegale, Ba: bilone sogega mugululi asi dagoi ba: i.
Mu mzindamo anagwiramo mkulu amene ankalamulira ankhondo, ndi alangizi amfumu asanu ndi awiri. Anagwiranso mlembi wa mtsogoleri wa ankhondo, amene ankalemba anthu mʼdzikomo, pamodzi ndi anthu ena 60 amene anali mu mzindamo.
Nebuzaradani, mtsogoleri wa ankhondoyo anawatenga onse napita nawo kwa mfumu ya ku Babuloni ku Ribula.
Ku Ribulako, mʼdziko la Hamati, mfumu ya ku Babuloniyo inalamula kuti anthuwo aphedwe. Motero anthu a ku Yuda anapita ku ukapolo, kutali ndi dziko lawo.
28 Ba: bilone hina bagade, Nebiuga: denese da amo hagudu dedei dunu udigili hawa: hamoma: ne mugululi asi: Ea ouligibi ode fesuale amoga, e da3,023dunu agoane mugululi asi.
Chiwerengero cha anthu amene Nebukadinezara anawatenga kupita nawo ku ukapolo ndi ichi: Mʼchaka cha chisanu ndi chiwiri cha ulamuliro wake, anatenga Ayuda 3,023;
29 Ea ouligibi ode18 amoga e da Yelusaleme fi dunu832 agoane amo mugululi asi.
mʼchaka cha 18 cha ulamuliro wa Nebukadinezara, anatenga anthu 832 kuchokera mu Yerusalemu;
30 Ea ouligibi ode23 amoga e da dunu 745 agoane mugululi asi. Nebiusala: ida: ne da amo dunu745 agoane Ba: bilone amoga oule asi. Mugululi asi dunu huluane ilia idi da 4,600agoane ba: i.
mʼchaka cha 23 cha ulamuliro wa Nebukadinezara, Nebuzaradani, mtsogoleri wa ankhondo a mfumu anagwira Ayuda 745 kupita ku ukapolo. Onse pamodzi analipo anthu 4,600.
31 Ode amoga Nebiuga: denese egefe Ifilimelouda: ge da Ba: bilone soge ouligisu lai, e da hina bagade Yihoiagimi ema asigiba: le, ea gagili ga: i logo doasi. Yihoiagimi da Ba: bilone soge ganodini ode37agoane gagili ga: i diasu ganodini esalu. Eso 25amola oubi fagoyale gala amo odega, Ifilimelouda: ge da ea gagili ga: i logo doasi.
Mʼchaka chimene Evili-Merodaki analowa ufumu wa Babuloni, iye anakomera mtima Yehoyakini mfumu ya ku Yuda, namutulutsa mʼndende. Izi zinachitika pa tsiku la 25 la mwezi wa khumi ndi chiwiri zitatha zaka 37 chitengedwere Yehoyakimu ku ukapolo.
32 Ifilimelouda: ge da ema asigiwane hamosu. E da Yihoiagimi e da eno hina bagade gilisili Ba: bilone sogega mugululi asi, amo mimogo sogebi amoga gaguia gadoi.
Evili-Merodaki anakomera mtima Yehoyakini, namupatsa malo aulemu kuposa mafumu ena amene anali naye ku Babuloni.
33 Amaiba: le, ea sia: beba: le, Yihoiagimi da ea udigili hawa: hamosu abula gisa: le, eno abula salawane, e da esalea, Ba: bilone hina bagade ea ha: i nasu fafai amoga gilisili ha: i nanu.
Choncho Yehoyakini analoledwa kuvula zovala zake za ku ndende ndipo tsiku ndi tsiku ankadya ndi mfumu pa moyo wake wonse.
34 Eso huluane, e da osobo bagadega esalebe gowane, Ba: bilone hina bagade da ea esaloma: ne lamu liligi defele, muni amola liligi ema i. Sia: ama dagoi
Tsiku ndi tsiku mfumu ya ku Babuloni inkamupatsa Yehoyakini phoso lake nthawi yonse ya moyo wake, mpaka pa nthawi ya imfa yake.

< Yelemaia 52 >