< Yelemaia 50 >

1 Hina Gode da Ba: bilone moilai bai bagade fi ilima Ea sia: ne iasu ilegei amo nama amane olelei,
Uthenga umene Yehova anayankhula ndi mneneri Yeremiya wonena za mzinda wa Babuloni ndi anthu ake ndi uwu:
2 “Fifi asi gala ilima olelema! Ha: giwane sisia: ma! Dawa: digima: ne hahamosu olelelalu, sisia: ma! Amo sia: mae wamolegema! Ba: bilone da dafai dagoi! Ea ogogosu ‘gode’ Madage da goudane sali! Ba: bilone loboga hamoi ogogosu ‘gode’ da gogosiasu lai dagoi! Ea wadela: idafa loboga hamoi ‘gode’ huluane da goudai dagoi!
“Lengeza ndi kulalika pakati pa anthu a mitundu ina, kweza mbendera ndipo ulengeze; usabise kanthu, koma uwawuze kuti, ‘Babuloni wagwa; mulungu wawo Beli wachititsidwa manyazi, nayenso Mariduku wagwidwa ndi mantha. Milungu yake yagwidwa ndi mantha ndipo mafano ake adzagwidwa ndi mantha.’
3 Gagoe (north) esalebe fi da Ba: bilone fi ilima doagala: musa: amola hafoga: i soge defele hamoma: ne wadela: musa: , misi dagoi. Dunu amola ohe da hobeamu, amola dunu da amogawi bu hame esalebe ba: mu.”
Mtundu wa anthu wochokera kumpoto wadzathira nkhondo Babuloni ndi kusandutsa bwinja dziko lake. Kumeneko sikudzakhalanso munthu kapena nyama.
4 Hina Gode da amane sia: sa, “Amo eso doaga: sea, Isala: ili fi dunu amola Yuda fi dunu da gilisili, diginiwane, Na, ilia Gode, amo bu hogomusa: misunu.
“Masiku amenewo, nthawi imeneyo,” akutero Yehova, “anthu a ku Israeli ndi anthu a ku Yuda onse pamodzi adzabwera akulira. Adzafunitsitsa kuchita zimene Yehova Mulungu wawo akufuna.
5 Ilia da Saione Goumi amoga ahoasu logo Nama adole ba: mu. Amola ilia da amo logoga masunu. Ilia da eso huluane dialoma: ne Gousa: su Nama hamomu, amola ilia da amo hamedafa fimu.
Adzafunsa njira ya ku Ziyoni ndi kuyamba ulendo wopita kumeneko. Iwo adzadzipereka kwa Yehova pochita naye pangano lamuyaya limene silidzayiwalika.
6 Na fi dunu da sibi amo ilia ouligisu dunu da noga: le hame ouligibiba: le, goumia fisi dagoi agoane ba: sa. Ilia da sibi agoane, goumi afae yolesili, eno goumia ahoasu, agoane asili, ilia da ilia sogebidafa amo gogolei dagoi.
“Anthu anga ali ngati nkhosa zotayika; abusa awo anawasocheretsa mʼmapiri. Iwo anayendayenda mʼmapiri ndi mʼzitunda mpaka kuyiwala kwawo.
7 Nowa da ili ba: sea da ilima doagala: sa. Ilia ha lai da amane sia: sa, ‘Ilia da ilia Hina Godema wadela: le hamoi dagoi. Amaiba: le, ninia da ilima doagala: mu da defea, wadela: i hame. Ilia aowa fi da Hina Gode Ea hou dafawaneyale dawa: i. Ilia amola da mae yolesili, Ema fa: no bobogemu da defea galu.’
Aliyense amene anawapeza anawawononga; adani awo anati, ‘Ife si olakwa, chifukwa iwo anachimwira Yehova, amene ali mpumulo wawo weniweni ndi amene makolo awo anamukhulupirira.’
8 Isala: ili fi dunu! Ba: bilone soge yolesili, hobeama! Dilia degabo amo soge yolesima!
“Thawaniko ku Babuloni; chokani mʼdziko la Ababuloni. Muyambe inu kutuluka ngati atonde amene amatsogolera ziweto.
9 Na da gagoe (north) esalebe fi gilisisu ilima sia: beba: le, ilia da Ba: bilone amoga doagala: musa: misunu. Ilia da gegemusa: dadalele, Ba: bilone fi ilima doagala: le, hasalimu. Ilia da benea ahoasu dunu noga: idafa. Ilia dadiga gala: sea, giadofamu hame dawa:
Taonani, ndidzaukitsa gulu lankhondo lamphamvu la mitundu ina ndi kubwera nalo kuchokera kumpoto kudzamenyana ndi Babuloni. Iwo adzandandalika ankhondo awo ndi kugonjetsa Babuloni. Mivi yawo ili ngati ya ankhondo aluso, yosapita padera.
10 Ilia da Ba: bilone fi ilia liligi huluane gesowale lamu. Ilia hanai liligi ilia da udigili lamu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
Motero Ababuloni adzafunkhidwa; ndipo onse omufunkha adzakhuta,” akutero Yehova.
11 Hina Gode da amane sia: sa, “Ba: bilone fi dunu! Dilia da Na fi dunu ilima doagala: le, ilia liligi huluane gesowale lai dagoi. Dilia da hahawane ahoa. Fedege agoane, dilia da bulamagau amo gagoma ha: i manu lamusa: ososa: gisa o hosi amo da gogona: ahoabe, agoane ba: sa.
“Inu Ababuloni, munawononga anthu anga osankhika. Ndiye pano mukukondwa, mukusangalala. Mukulumphalumpha mokondwa ngati mwana wangʼombe wopuntha tirigu ndiponso mukulira monyada ngati ngʼombe zazimuna.
12 Be dilia moilai bai bagade (Ba: bilone) da dafane gogosia: i dagoi ba: mu. Amola Ba: bilone fi da fifi asi gala amo ganodini gududafa dialebe ba: mu. Ba: bilone soge da wadela: i hafoga: i soge hamoi dagoi ba: mu.
Koma mzinda wanu udzachititsidwa manyazi kwambiri. Mzinda umene uli ngati mayi wanu udzanyazitsidwa. Babuloni adzasanduka chitsirizira cha anthu onse. Mzinda wawo udzakhala ngati thengo, ngati dziko lowuma lachipululu.
13 Bai Na da ougi bagadeba: le, dunu afae Ba: bilone soge ganodini esalebe da hame ba: mu. Ba: bilone da mugului dagoi dialebe ba: mu, amola nowa dunu da amo soge baligimusa: ahoasea, da bagadewane fofogadigimu.
Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova Babuloni adzakhala wopanda anthu ndipo adzakhala chipululu chokhachokha. Onse odutsa kumeneko adzachita mantha ndipo azidzangotsonya chifukwa cha chiwonongeko chake chachikulu.
14 Dilia dadi gagui dunu! Ba: bilone amoma doagala: musa: dadalema! E eale sisiga: ma! Dilia dadi huluane amoga, e gala: ma! Bai Ba: bilone fi da Na, Hina Gode, Nama wadela: le hamoi.
“Inu okoka uta, konzekani kuti muthire nkhondo mzinda wa Babuloni mbali zonse. Muponyereni mivi yanu yonse chifukwa anachimwira Yehova.
15 Moilai bai bagade amo eale sisiga: le, gegemusa: halama! Wali Ba: bilone da fama: ne olei dagoi! Ea gagoi dobea da fili, mugului dagoi ba: sa. Na da Ba: bilone fi ilima dabe iaha. Amaiba: le, ha lai dunu! Ilima dabe ima! Ilia da eno dunuma hamoi, amo defele, ilima dabe bu ima.
Mufuwulireni mbali zonse pakuti wagonja. Nsanja zake zagwa. Malinga ake agwetsedwa. Kumeneku ndiko kulipsira kwa Yehova. Mulipsireni, mumuchite zomwe iye anachitira anthu ena.
16 Amo soge ganodini, ha: i manu bugima: ne amola faima: ne logo mae doasima! Ga fi dunu Ba: bilone soge ganodini esala, ilia da dadi gagui wa: i Ba: bilone fi ilima doagala: musa: manebe, ilima beda: iba: le, hi sogega bu masunu.”
Chotsani ku Babuloni munthu wofesa mbewu aliyense, ndiponso wodula tirigu ndi chikwakwa chake pa nthawi yokolola. Poona lupanga la ozunza anzawo, aliyense adzabwerera kwa anthu ake; adzathawira ku dziko la kwawo.
17 Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili fi dunu da sibi amo laione wa: mega sefasi amola afagogoi dagoi, amo agoane ba: sa. Degabo, Asilia hina bagade da ilima doagala: i. Amasea, fedege agoane, Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese, da ilia gasa gagisu.
“Aisraeli ali ngati nkhosa zomwe zabalalika pothamangitsidwa ndi mikango. Mfumu ya ku Asiriya ndiye inayamba kuwapha Aisraeliwo. Wotsiriza anali Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni amene anachita ngati kuphwanya mafupa ake.”
18 Amaiba: le, Na, Hina Gode Bagadedafa, Isala: ili fi ilia Gode, da Asilia hina bagade ema se iasu defele, hina bagade Nebiuga: denese amola ea fi ilima se imunu.
Nʼchifukwa chake Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, “Ndidzalanga mfumu ya ku Babuloni pamodzi ndi dziko lake monga momwe ndinalangira mfumu ya ku Asiriya.
19 Na da Isala: ili fi ilia sogega buhagima: ne, logo doasimu. Ilia da ha: i manu amo da Gamele Goumia amola Ba: isia: ne sogega heda: lebe amo manu, amola ha: i manu bugi Ifala: ime soge amola Gilia: de sogega gala, amoga ilia hanaiga defele manu.
Koma ndidzabwezera Israeli ku msipu wake ndipo adzadya mʼminda ya ku Karimeli ndi Basani; adzadya nakhuta ku mapiri a ku Efereimu ndi Giliyadi.
20 Amo eso da doaga: sea, Isala: ili fi amola Yuda fi amo ganodini da wadela: i hou dialebe hame ba: mu. Bai dunu amo ilia esalusu Na da gaga: i, ilia wadela: i hou amola Na da gogolema: ne olofomu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
Masiku amenewo, nthawi imeneyo,” akutero Yehova, “anthu adzafunafuna zolakwa za Israeli koma sadzapeza nʼchimodzi chomwe, ndipo adzafufuza machimo a Yuda, koma sadzapeza ndi limodzi lomwe, chifukwa otsala amene ndawasiya ndidzawakhululukira.
21 Hina Gode da amane sia: sa, “Melada: ime fi amola Bigode fi (ela da Ba: bilone fi) ilima doagala: ma! Ilia huluane medole legele wadela: lesima! Na sia: i liligi huluane hamoma! Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.
“Lithireni nkhondo dziko la Merataimu ndi anthu okhala ku Pekodi. Muwaphe ndi lupanga ndi kuwawonongeratu,” akutero Yehova. “Chitani zonse monga momwe ndakulamulani.
22 Ba: bilone soge ganodini gegemusa: ha lasu da naba. Amola wadela: su bagade ba: sa.
Mʼdziko muli phokoso la nkhondo, phokoso la chiwonongeko chachikulu!
23 Ba: bilone da ‘ha: ma’ (hammer) agoane, fifi asi gala huluane fifima: ne fananu. Be wali amo ‘ha: ma’ da fifilasi dagoi. Ema doaga: i hou ba: beba: le, fifi asi gala huluane da bagadewane fofogadigisa.
Taonani mʼmene waphwanyikira ndi kuwonongekera uja amati ndi nyundo ya dziko lonse lapansi. Mzinda wa Babuloni wasanduka chinthu chochititsa mantha pakati pa mitundu ina!
24 Ba: bilone fi! Dilia da nama gegenanu. Be wali dilia da sani amo Na da dili sa: ima: ne gei, amoga sa: i dagoi. Dilia da mae dawa: iwane amoga sa: i dagoi.
Ndinakutchera msampha, iwe Babuloni, ndipo wakodwamo iwe wosazindikira kanthu; unapezeka ndiponso unakodwa chifukwa unalimbana ndi Yehova.
25 Na da Na gegesu liligi lidiligalei diasu amo doasili amola Na da ougiba: le, amo liligi gagui dagoi. Bai Na, Ouligisu Hina Gode Bagadedafa, da Ba: bilone sogega hawa: hamomu galaiou.
Yehova watsekula nyumba ya zida zake ndipo watulutsa zida za ukali wake, pakuti Ambuye Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ntchito yoti agwire mʼdziko la Ababuloni.
26 La: ididili huluane amoga Ba: bilonema doagala: ma! Ea widi amola gagoma legesu diasu fima! Lai liligi amo widi lelegela heda: i agoane lelegela heda: ma! Soge wadela: ma! Liligi huluanedafa wadela: lesima!
Mumenyane naye Babuloni mbali zonse. Anthu ake muwawunjike ngati milu ya tirigu. Muwawononge kotheratu ndipo pasakhale wopulumuka ndi mmodzi yemwe.
27 Ba: bilone dadi gagui dunu huluane medole legema! Medole legema! Ba: bilone dunu da wadela: lesi dagoi ba: mu! Ilima se iasu eso da doaga: i dagoi.
Iphani ankhondo ake onse. Onse aphedwe ndithu. Tsoka lawagwera pakuti tsiku lawo lachilango lafika.
28 (Mugululi asi dunu da Ba: bilone soge yolesili, hobeale, Yelusaleme diasuga doaga: sa. Ilia da sia: ne iasu amo ninia Hina Gode da Ba: bilone dunu ilima dabe i dagoi - bai ilia da Ea Debolo diasu wadela: lesi - amo ilia da olelesa.)
Tikumva anthu othawa nkhondo ochokera ku Babuloni akulengeza mu Yerusalemu za kulipsira kwa Yehova Mulungu wathu. Iye akulipsira chifukwa chowononga Nyumba yake.
29 Dadi gagui dunu ilima ilia Ba: bilone fi doagala: ma: ne sia: ma! Dunu huluane amo da dadiga gala: su dawa: , amo gadili asunasima! Moilai sisiga: le, dunu afae mae hobeama: ne, logo huluane ga: ma! Ba: bilone fi ilima dabe ima. Ilia hou eno fi ilima hamoi, amo defele ilima hamoma! Bai ilia da Na, Isala: ili ilia Hadigi Gode, Nama gasa fili hamoi.
“Itanani anthu oponya mivi kudzathira nkhondo Babuloni. Muyitanenso onse amene amakoka mauta. Mangani misasa ya nkhondo momuzungulira; musalole munthu aliyense kuthawa. Muchiteni monga momwe iye anachitira anthu ena. Iyeyu ananyoza Yehova, Woyera wa Israeli.
30 Amaiba: le, ilia ayeligi dunu da moilai logoga medole legei dagoi ba: mu. Amola amo esoga, ilia dadi gagui dunu da medole legei dagoi ba: mu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.
Nʼchifukwa chake, anyamata ake adzaphedwa mʼmabwalo ake; ankhondo ake onse adzaphedwa tsiku limenelo,” akutero Yehova.
31 Ba: bilone! Di da gasa fi hou amoga nabai gala. Amaiba: le, Na, Ouligisudafa Hina Gode Bagadedafa, da dima ha lai hamoi dagoi. Na da dima se imunu eso ilegei, amo da doaga: i dagoi.
“Taona, ndikukuthira nkhondo, iwe wodzikuzawe,” akutero Ambuye Yehova Wamphamvuzonse, “chifukwa tsiku lako lafika, nthawi yoti ndikulange yakwana.
32 Dia hidale hamosu gasa fi da sadenane dafamu. Amola, dunu eno di wa: legadolesimu hamedafa ba: mu. Na da dia moilai bai bagade huluane laluga ulagimu. Amola liligi huluane sisiga: le dialebe da wadela: lesi dagoi ba: mu.”
Wodzikuzawe udzapunthwa nʼkugwa ndipo palibe amene adzakudzutse; ndidzayatsa moto mʼmizinda yake umene udzanyeketsa onse amene amuzungulira.”
33 Hina Gode Bagadedafa da amane sia: sa, “Isala: ili fi amola Yuda fi da banenesiwane esalebe ba: sa. Dunu amo da ili gagulaligi, da ili ha: giwane sosodo aligisa. Amola ilia da ili se iasu udigili hawa: hamosu logo doasimusa: hame dawa:
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu a ku Israeli akuzunzidwa, pamodzi ndi anthu a ku Yuda, ndipo onse amene anawagwira ukapolo awagwiritsitsa, akukana kuwamasula.
34 Be ilia gaga: su dunu da gasa bagadewane esala. Ea dio da Hina Gode Bagadedafa. Hisu da ilimagale gegemu. E da osobo bagade fifi asi gala ilima olofosu iasimu. Be E da Ba: bilone fi ilima bidi hamosu iasimu.”
Koma Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu; dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse. Iye adzawateteza molimba pa mlandu wawo nʼcholinga choti abweretse mtendere mʼdziko lawo, koma adzavutitsa okhala ku Babuloni.”
35 Hina Gode da amane sia: sa, “Ba: bilone soge da bogosu ba: ma! Ea fi dunu amola ouligisu dunu amola bagade dawa: su dunu da bogosu ba: mu.
Yehova akuti, “Imfa yalunjika pa Ababuloni, pa akuluakulu ake ndi pa anthu ake a nzeru!
36 Ea ogogosu balofede dunu da bogosu ba: mu. Ilia da gagaoui dunu. Ea dadi gagui dunu da bogosu ba: mu. Ilia da bagadewane beda: i.
Imfa yalunjika pa aneneri abodza kuti asanduke zitsiru. Imfa yalunjika pa ankhondo ake kuti agwidwe ndi mantha aakulu.
37 Ea hosi amola sa: liode huluane wadela: lesima! Ea ga fi muni lama: ne hawa: hamosu dadi gagui dunu da bogosu ba: mu. Ilia da gasa hamedafa ba: sa. Ba: bilone liligi ida: iwane gala huluane wadela: lesima! Huluane gesowale lale dagoma!
Imfa ilunjike pa akavalo ake ndi magaleta ake. Ilunjikanso pa magulu ankhondo achilendo amene ali pakati pawo kuti asanduke ngati akazi. Chiwonongeko chilunjikenso pa chuma chake kuti chidzafunkhidwe.
38 Ea sogega esoi bagade iasima. Ea hano huluane hafoga: ma! Ba: bilone soge ganodini da loboga hamoi ogogosu ‘gode’ bagohame. Ea fi dunu da ilima beda: iba: le, gagaoui agoane ba: sa.
Chilala chilunjike pa madzi ake kuti aphwe. Babuloni ndi dziko la mafano, ndipo anthu afika poyaluka nawo mafanowo.
39 Amaiba: le, Ba: bilone soge ganodini, Fio liligi amola wadela: i a: silibu amola ledo hamoi sio bagohame ba: mu. Dunu fi da amo soge ganodini hamedafa esalumu.
“Nʼchifukwa chake nyama zakuthengo ndi afisi zidzakhala kumeneko ndipo kudzakhalanso akadzidzi. Kumeneko sikudzapezekako anthu, ndithu anthu sadzakhalako pa mibado yonse.
40 Musa: hemonega, Na da Sodame amola Goumola amola amo sisiga: le dialebe moilai fonobahadi huluane amo wadela: lesi dagoi. Amo hou defele da Ba: bilone fi ilima doaga: mu. Dunu afae da amo ganodini wali amola eso huluane hame esalebe ba: mu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.
Monga momwe Mulungu anawonongera Sodomu ndi Gomora pamodzi ndi mizinda yonse yozungulira,” akutero Yehova, “momwemonso palibe amene adzakhale kumeneko; anthu sadzayendanso mʼmenemo.
41 Gagoe (north) soge amoga fi bagadedafa da gegemusa: manebe. Hina bagade bagohame da gegemusa: momagesa.
“Taonani! Gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto; mtundu wa anthu amphamvu pamodzi ndi mafumu ambiri, wanyamuka kuchokera kumathero a dziko lapansi.
42 Ilia da ilia dadi amola gegesu gobihei gagui dagoi. Ilia da nimi bagade hame asigi dunu. Ilia da hosi da: iya fila heda: le ahoasea, ilia ha lasu da hano wayabo bagade ea gafululi fugala: sa agoane naba. Ilia da Ba: bilone fi ilima doagala: musa: momagei dagoi.
Atenga mauta ndi mikondo; ndi anthu ankhanza ndipo alibe chifundo. Phokoso lawo likumveka ngati mkokomo wa nyanja. Akwera pa akavalo awo, ndipo akonzekera kudzakuthira nkhondo iwe Babuloni.
43 Ba: bilone hina bagade da ilia manebe sia: nabasea, ea lobo da bodola: le gudusa. E da uda da mano lalelegemu gadenesea se naba, amo defele e da se naba.
Mfumu ya ku Babuloni yamva za mbiri yawo, ndipo yalobodokeratu. Ikuda nkhawa, ikumva ululu ngati wa mayi pa nthawi yake yochira.
44 Laione wa: me da Yodane Hano bega: iwila amo yolesili, bulamagau ha: i manu mola: ya: i gisi soge amoga manebe, amo defele Na, Hina Gode da Ba: bilone dunu ilima doagala: musa: misunu. Amasea, Ba: bilone dunu da ilia moilai yolesili, hobeamu. Nowa da Na agoanela: ? Nowa da Nama doagala: mu dawa: bela: ? Nowa ouligisu dunu da Nama gegemusa: dawa: bela: ? Nama hasalasimu da hamedeidafa.
Taonani, monga mkango wochokera ku nkhalango ya ku Yorodani kupita ku msipu wobiriwira, momwemonso ine ndidzapirikitsa Babuloni mʼdziko lake mwadzidzidzi. Pambuyo pake ndidzawayikira wowalamulira amene ndamufuna Ine. Wofanana nane ndani ndipo ndani amene angalimbane nane? Ndi mtsogoleri wa dziko uti amene anganditengere ku bwalo la milandu?”
45 Amaiba: le, Na da Ba: bilone soge amola ea fi dunu ilima hamoma: ne ilegesu amo nabima! Ilia huluane amola ilia mano da ga hiouginana asi dagoi ba: mu. Amasea, dunu huluane da bagadewane beda: mu.
Nʼchifukwa chake imvani. Izi ndi zimene Ine Yehova ndakonza zolangira anthu a ku Babuloni. Ngakhale ana omwe adzatengedwa ukapolo ndipo aliyense adzachita mantha chifukwa cha iwo.
46 Ba: bilone da dafasea, sia: bagade nababeba: le, osobo bagade da igugumu. Amola fifi asi gala huluane da ilia beda: ga wele sia: nebe nabimu.
Akadzagwa Babuloni padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera, ndipo kulira kwawo kudzamveka pakati pa mitundu yonse ya anthu.

< Yelemaia 50 >