< Yelemaia 5 >

1 Yelusaleme fi dunu! Dilia logoga hehenama! Ba: le gagama! Dilisu ba: ma! Bidi lasu soge amo ganodini hogoi helema! Dilia da moloidafa hamosu dunu afae ba: ma: bela: ? Dilia Godema mae hohonone moloidafa fa: no bobogesu dunu afae ba: ma: bela: ? Hame mabu! Be dilia agoaiwane dunu afae ba: sea, Hina Gode da Yelusaleme fi ilia wadela: i hou gogolema: ne olofomu.
“Pitani uku ndi uku mʼmisewu ya Yerusalemu, mudzionere nokha, funafunani mʼmabwalo ake. Ngati mungapeze munthu mmodzi amene amachita zachilungamo ndi kufunafuna choonadi, ndipo ndidzakhululukira mzinda uno.
2 Dilia da Hina Godema nodone sia: ne gadosa, dilisu da sia: sa. Be dilia da ogogosa.
Ngakhale anthu akulumbira kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’ komabe akungolumbira mwachinyengo.”
3 Hina Gode da mae hohonone moloidafa fa: no bobogesu hou hogosa. E da dili fai dagoi, be dilia amo hame dawa: i galu. E da dili goudale fasi, be dilia da amoba: le dilia hou hame hahamoi. Dilia da ga: nasi hamoiba: le, dilia wadela: i hou fisimusa: hame dawa: iou.
Inu Yehova, kodi suja mumafuna anthu onena zoona? Inu munawakantha anthuwo, koma sanamve kupweteka; munawaphwanya anthuwo, koma sanatengepo phunziro. Anawumitsa mitima yawo ngati mwala ndipo anakaniratu kulapa.
4 Amalalu, na da agoane dawa: i, “Amo da hame gagui amola hame dawa: su dunu fawane. Ilia da gagaoui agoane hamosa. Ilia Gode Ea hanai amo hame dawa:
Ndiye ndinati, “Awa ndi amphawi chabe; anthu ochita zopusa. Sadziwa njira ya Yehova, sazindikira zimene Mulungu wawo amafuna.
5 Amaiba: le, na da ouligisu hou gagui dunu ilima asili, ilima sia: mu. Na da agoane dawa: , ‘Ilia da Gode Ea hanai dawa: mu. Ilia hamoma: ne, Hina Gode Ea sia: i liligi ilia da dawa: mu.’ Be ilia huluane da Hina Gode Ea ouligisu hou amo higale yolesi dagoi. Ilia da Ea sia: nabimu higasa.
Tsono ndidzapita kwa atsogoleri ndi kukayankhula nawo; ndithu iwo amadziwa njira ya Yehova, amadziwa zomwe Mulungu wawo amafuna.” Koma ayi, iwonso anathyola goli la Yehova ndipo anadula msinga zawo.
6 Amaiba: le, iwilaga esalebe laione wa: me da ili medole legemu. Hafoga: i sogega esalebe ‘wufi’ wa: me da ili medole legele, dadalega: mu. Amola ‘lebade’ wa: me da ilia moilai amo ganodini wamowane manebe ba: mu. Amo dunu da ilia diasu gadili ahoasea, ilia da: i da gadelale fofonoboi dagoi ba: mu. Bai ilia wadela: i hou hamoi da bagohame. Amola eso huluane, mae fisili, ilia da Godema baligi fa: su.
Choncho mkango wochokera ku nkhalango udzawapha, mmbulu wochokera ku thengo udzawawononga, kambuku adzawabisalira pafupi ndi mizinda yawo kuti akhadzule aliyense amene adzayesera kutuluka mʼmizindamo pakuti kuwukira kwawo ndi kwakukulu ndipo abwerera mʼmbuyo kwambiri.
7 Hina Gode da amane adole ba: i, “Na da abuliba: le Na fi ilia wadela: i hou gogolema: ne olofoma: bela: ? Ilia da Na yolesili, ogogosu ‘gode’ ilima nodone sia: ne gadosu. Na fi dunu sadima: ne, Na da ha: i manu iligili i. Be ilia da inia uda adole lasu hou hamosu amola hina: da: i bidi lasu uda ilima fa: no bobogei.
Yehova akuti, “Kodi ndingakukhululukireni bwanji ndi zimene mwachita? Ana anu andisiya Ine ndipo amapembedza milungu imene si milungu konse. Ine ndinawapatsa zonse zimene ankasowa, komabe iwo anachita chigololo namasonkhana ku nyumba za akazi achiwerewere.
8 Ilia da hosi gawali amo da sadi dagoi amola aseme amoma fima: ne nimi bagade hamosa, amo defele gala. Ilia afae afae ea na: iyado idua amo lale, gilisili golamu hanai bagade.
Monga amachitira akavalo onenepa akamamemesa, aliyense wa iwo ankathamangira mkazi wa mnzake.
9 Ilia da amo hou hamobeba: le, Na da ilima se imunu da defea. Agoaiwane fi ilima dabe imunu da defea.
Tsono ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi?” akutero Yehova. “Kodi nʼkuleka kuwulipsira mtundu woterewu?
10 Na da ha lai dunu amo Na fi dunu ilia waini sagai hedofama: ne asunasimu. Be amo da dafawane wadela: lesi ebelei dagoi hame ba: mu. Na da ha lai amoma, e da amoda huluane gole fasima: ne Na da sia: mu. Bai amo amoda da Na: hame.
“Pitani ku minda yake ya mipesa ndi kukayiwononga, koma musakayiwononge kotheratu. Sadzani nthambi zake pakuti anthu amenewa si a Yehova.
11 Isala: ili dunu amola Yuda dunu da Na dafawanedafa hohonoi. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
Nyumba ya Israeli ndi nyumba ya Yuda onse akhala osakhulupirika kotheratu kwa Ine.”
12 Hina Gode Ea fi dunu da E yolesi. Ilia da amane sia: sa, “Gode da ninima se hame imunu. Ninia da gasa bagade hou hame ba: mu. Ninia da gegesu amola ha: su hame ba: mu.”
Iwowa ankanama ponena za Yehova kuti, “Yehova sangachite zimenezi! Choyipa sichidzatigwera; sitidzaona nkhondo kapena njala.
Mawu a aneneri azidzangopita ngati mphepo; ndipo mwa iwo mulibe uthenga wa Yehova. Choncho zimene amanena zidzawachitikira okha.”
14 Ilia da amane sia: sa, “Balofede dunu ilia sia: da fo fawane. Ilia da Hina Gode Ea sia: hame gaguli maha.” Hina Gode Bagadedafa da nama amane sia: i, “Yelemaia! Amo dunu da agoane sia: beba: le, Na da sia: dia lafiga gala amo lalu agoane hamomu. Na fi dunu da lalu ifa agoane ba: mu, amola Na agoane sia: nanu ili da nei dagoi ba: mu.”
Chifukwa chake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse akuti, “Popeza kuti anthu awa ayankhula mawu amenewa, tsono mawu anga ndidzawasandutsa moto mʼkamwa mwako ndipo anthu awa ndidzawasandutsa nkhuni zimene moto udzapserezeretu.
15 Isala: ili dunu! Dilia! Hina Gode da fi sedagaga esalebe, amo dilima doaga: la: ma: ne, oule misunu. Amo fi da gasa bagade hemone fi amola dilia da ilia sia: hame dawa:
Inu Aisraeli,” Yehova akuti, “Ndikukubweretserani mtundu wa anthu ochokera kutali, ndi mtundu umene sunagonjetsedwepo, mtundu wakalekale umene chiyankhulo chawo inu simuchidziwa, zimene akunena inu simungazimvetse.
16 Ilia dadi gagui dunu da gasa bagade. Ilia da mae asigili medole lelegelala.
Zida zawo za nkhondo zapha anthu ambirimbiri; onsewo ndi ankhondo amphamvu okhaokha.
17 Ilia da dilia ha: i manu amola bugi huluane na dagomu. Ilia da dilia dunu mano amola uda mano huluane medole lelegemu. Ilia da dilia sibi amola bulamagau gilisisu medole legemu. Amola dilia waini efe amola figi ifa ilia da wadela: lesimu. Dilia gagili sali moilai da dili gaga: mu, dilia dawa: sa. Be ilia dadi gagui da amo huluane mugululi wadela: lesimu.”
Adzakudyerani zokolola zanu ndi chakudya chanu, adzapha ana anu aamuna ndi aakazi; adzakupherani nkhosa zanu ndi ngʼombe zanu, adzawononga mpesa wanu ndi mikuyu yanu. Ndi malupanga awo adzagwetsa mizinda yanu yotetezedwa imene mumayidalira.
18 Hina Gode da amane sia: sa, “Be amo se nabasu esoga, Na da Na fi dunu huluanedafa hame wadela: lesimu. Afae afae da esalebe ba: mu.
“Komabe pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu,” akutero Yehova.
19 Amola, Yelemaia, di! Ilia da Na da abuliba: le amo hou hamobela: le adole ba: sea, ilima bu adole ima, ‘Bai ilia da Na yolesili, ilia soge ganodini ga fi ogogosu ‘gode’ ilima hawa: hamosu, amo defele ilia da eno fi dunu ilia soge ganodini, amo ga fi dunu ilia se iasu hawa: hamosu hamonanumu.’”
Ndipo pamene anthu adzafunsa Yehova kuti, “Chifukwa chiyani Yehova Mulungu wathu wachita zimenezi?” Iwe udzawawuze kuti, “Monga momwe mwasiyira Ine ndi kutumikira milungu yachilendo mʼdziko mwanu, momwemonso mudzatumikira anthu a mʼdzikonso lachilendo.”
20 Hina Gode da amane sia: sa, “Ya: igobe egaga fi, amola Yuda fi dunu ilima amane sia: ma,
“Lengeza izi kwa ana a Yakobo ndipo mulalikire kwa anthu a ku Yuda kuti,
21 ‘Dilia gagaoui amola hame dawa: su dunu! Dawa: ma: i! Dilia da si gala be ba: mu gogolei! Dilia da ge gala be hame naba!
Imvani izi, inu anthu opusa ndi opanda nzeru, inu amene maso muli nawo koma simupenya, amene makutu muli nawo koma simumva.
22 Na da Hina Gode! Dilia abuliba: le Nama hame nodone beda: bela: ? Dilia da abuliba: le Na midadi hame yagugusala: ? Na da sa: iboso amo hano wayabo bagade ea alalo legei dagoi. Amo alalo legesu da eso huluane dialumu, amola hano bagade da amo baligimu hame dawa: Hano bagade da gafulusa be amo alalo legesu hame baligisa. Hano gafului da fugala: sa, be osoba amo ganodini golili misunu hame dawa:
Kodi simuyenera kuchita nane mantha?” Akutero Yehova. “Kodi simuyenera kunjenjemera pamaso panga? Ine ndinayika mchenga kuti ukhale malire a nyanja, malire a muyaya amene nyanjayo singadutsepo. Mafunde angawombe motani, koma sangathe kupitirira malirewo; mafunde angakokome motani, koma sangadutse malirewo.
23 Be dilia Na fi dunu! Dilia da gasa fili, odoga: su dunu. Dilia da la: ididili asili, Na yolesi.
Koma anthu awa ndi nkhutukumve ndiponso a mitima yowukira; andifulatira ndipo andisiyiratu.
24 Na da woufo gibu amola mugi gibu dilima iasu amola dilia hahawane bugi gamini moma: ne eso dilima iasu. Be dilia da Nama nodomu hame dawa: i galu.
Sananenepo mʼmitima mwawo kuti, ‘Tiyeni tizipembedza Yehova Mulungu wathu. Kodi suja amatipatsa pa nthawi yake mvula yachizimalupsa ndi yamasika. Iye salephera konse kutipatsa nyengo ya kholola.’
25 Be dilia da wadela: le hamobeba: le, amo liligi ida: iwane hame ba: i.
Koma zolakwa zanu zalepheretsa zonsezi; ndipo machimo anu akumanitsani zabwino.
26 Na fi dunu gilisisu ganodini da wadela: idafa dunu esalebe. Ilia da dunu ilia sio sa: ima: ne sanebe, amo defele dunu dafama: ne, sanigesa.
“Pakati pa anthu anga pali anthu ena oyipa amene amabisalira anzawo monga amachitira mlenje mbalame ndiponso ngati amene amatchera misampha kuti akole anthu anzawo.
27 Benea ahoasu dunu da sio lale, ea gagili amo ganodini sala, amo defele ilia inia liligi lale, ilia diasu nabama: ne ligisisa. Amaiba: le, ilia da bagade gagui amola gasa bagade ba: sa.
Nyumba zawo zadzaza ndi chuma chochipeza mwa chinyengo ngati zikwere zodzaza ndi mbalame. Nʼchifukwa chake asanduka otchuka ndi olemera.
28 Ilia da sadi dagoi amola dunu basului agoane ba: sa. Ilia da baligili, mae yolele, wadela: i hou hamonana. Ilia da guluba: mano hame fidisa, amola hame gagui banenesi dunu ilima moloidafa fofada: su imunu hame dawa:
Ndipo ananenepa ndi kukhala ndi matupi osalala. Ntchito zawo zoyipa nʼzopanda malire; saweruza mwachilungamo nkhani ya ana amasiye kuti iyende bwino, sateteza ufulu wa anthu osauka.
29 Be Na, Hina Gode, da ilia wadela: i hou hamobeba: le, ilima se imunu. Na da amo fima dabe imunu.
Kodi Ine ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi? Kodi ndisawulipsire mtundu woterewu? Akutero Yehova.
30 Yuda soge ganodini, fofogadigisu wadela: i houdafa da doaga: i dagoi.
“Chinthu chothetsa nzeru ndi choopsa kwambiri chachitika mʼdzikomo:
31 Balofede dunu da ogogole fawane sia: sa. Gobele salasu dunu da balofede dunu ilia sia: defele ouligisa, amola Na fi dunu da ilia wadela: i logo hame hedofasa. Be amo hou ea dabe doaga: sea, ilia da adi hamoma: bela: ?’”
Aneneri akunenera zabodza, ndipo ansembe akuvomerezana nawo, ndipo anthu anga akukonda zimenezi. Koma mudzatani potsiriza?

< Yelemaia 5 >