< Yelemaia 46 >

1 Hina Gode da fifi asi gala ilia hou nama olelei.
Yehova anamupatsa Yeremiya uthenga wonena za anthu a mitundu ina.
2 E da hidadea Idibidi fi ilia hou olelei. E da Idibidi hina bagade Nigou ea dadi gagui wa: i amo ilia hou olelei. Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese da Yuda hina bagade Yihoiagimi ea ouligisu ode biyaduga, e da Gagimisi moilai bai bagade Iufala: idisi Hano gadenene amoga hina bagade Nigou ea dadi gagui wa: i amoga hasalasi. Hina Gode da amane sia: i,
Kunena za Igupto: Yehova ananena za gulu lankhondo la Farao Neko mfumu ya ku Igupto limene Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni analigonjetsa ku Karikemesi ku mtsinje wa Yufurate mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa Yosiya mfumu ya Yuda,
3 “Idibidi dadi gagui ouligisu dunu da amane wele sia: sa, ‘Dilia da: igene ga: su momagele, gegemusa: mogodigili masa.
anati, “Konzani zishango zanu ndi malihawo, ndipo yambanipo kupita ku nkhondo!
4 Dilia hosi liligi momagele, ili da: iya fila heda: ma! Dadalema! Ouli habuga figisima! Dilia goge agei debema! Dilia da: igene ga: su liligi gasisalima!’
Mangani akavalo, ndipo kwerani inu okwerapo! Khalani pa mzere mutavala zipewa! Nolani mikondo yanu, valani malaya anu ankhondo!
5 “Be Na da adi ba: sala: ?” Hina Gode da amane sia: sa. “Ilia da beda: iba: le sinidigisa. Ilia ha lai da ili fanana. Ilia da bagadewane beda: iba: le, mae beba: le hobeasa.
Yeremiya anati: Kodi ndikuona chiyani? Achita mantha akubwerera, ankhondo awo agonjetsedwa. Akuthawa mofulumirapo osayangʼananso mʼmbuyo, ndipo agwidwa ndi mantha ponseponse,” akutero Yehova.
6 Be hedolodafa hehenasu dunu da baligili hobeamu hame dawa: Dadi gagui dunu da hobeale masunu hamedei ba: sa. Gagoe (north) sogega, Iufala: idisi Hano gadenene, ilia da emo udagaguli dafasa.
Waliwiro sangathe kuthawa ngakhale wankhondo wamphamvu sangathe kupulumuka. Akunka napunthwa ndi kugwa kumpoto kwa mtsinje wa Yufurate.
7 Fi amo da Naile Hano defele heda: le ea bega: nabale aduga: le daha, amo fi da nowala: ?
“Kodi ndani amene akukwera ngati Nailo, ngati mtsinje wa madzi amkokomo?
8 Amo fi da Idibidi. E da Naile Hano defele heda: le, ea bega: nabane aduga: le daha. Idibidi da amane sia: i, ‘Na da heda: le, osobo bagade dedebomu. Na da moilai amola amo ganodini esalebe dunu amo wadela: lesimu.
Igupto akusefukira ngati Nailo, ngati mitsinje ya madzi amkokomo. Iye akunena kuti, ‘Ndidzadzuka ndi kuphimba dziko lapansi; ndidzawononga mizinda ndi anthu ake.’
9 Hosi masa: ne sia: ma! Sa: liode masa: ne sia: ma! Dadi gagui dunu gadili asunasima! Ilia da Suda: ne amola Libia soge, ilia da: i ga: su gaguiwane maha. Amola dadia gegesu bagade dawa: su dunu Lidia sogega misi, amo asunasimu.’”
Tiyeni, inu akavalo! Thamangani inu magaleta! Tulukani, inu ankhondo, ankhondo a ku Kusi ndi Puti amene mumanyamula zishango, ankhondo a ku Ludi amene mumaponya uta.
10 Wali eso da Ouligisudafa Hina Gode Bagadedafa Ea Eso. Wali eso E da dabemu. Wali eso E da Ea ha lai ilima se imunu. Fedege agoane, Ea gobihei da sadima: ne, Ea ha lai na dagomu. Amola sadima: ne, ilia maga: me manu. Wali eso, gagoe (north) soge Iufala: idisi Hano gadenene, Hina Gode Bagadedafa da gobele salasu hamomu.
Koma tsikulo ndi la Ambuye Yehova Wamphamvuzonse; tsiku lolipsira, lolipsira adani ake. Lupanga lake lidzawononga ndi kukhuta magazi, lidzaledzera ndi magazi. Pakuti Yehova, Yehova Wamphamvuzonse, adzapereka adani ake ngati nsembe mʼdziko la kumpoto mʼmbali mwa mtsinje wa Yufurate.
11 Idibidi dunu! Manoma hogomusa: , Gilia: de sogega masa! Dilia manoma da udigili hamedei agoane ba: i dagoi. Dilia da uhimu da hamedei.
“Pita ku Giliyadi ukatenge mankhwala iwe namwali Igupto. Wayesayesa mankhwala ambiri koma osachira; palibe mankhwala okuchiritsa.
12 Fifi asi gala huluane da dilia gogosiasu ba: i, amo nabi dagoi. Dadi gagui afae afae da ea sama amoma emo udagaguli, ela gilisili osoboga dafasa.
Anthu a mitundu ina amva za manyazi ako; kulira kwako kwadzaza dziko lapansi. Ankhondo akunka nagwetsanagwetsana, onse awiri agwa pansi limodzi.”
13 Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese da Idibidi doagala: musa: manoba, Hina Gode da nama amane sia: i,
Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za kubwera kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni kudzathira nkhondo Igupto ndi uwu:
14 “Idibidi moilai bai bagade (Migidole, Memefisi amola Daha: banisi) amo ganodini ha: giwane amane olelema, ‘Dilila: gaga: ma: ne, momagema! Dilia huluane gegesu ganodini wadela: lesi dagoi ba: mu.
“Mulengeze ku Igupto. Mulengeze ku Migidoli. Mulengezenso ku Mefisi ndi ku Tapanesi. Muwawuze anthu akumeneko kuti, ‘Imani pamalo panu ndi kukhala okonzeka kudziteteza, chifukwa lupanga lidzawononga zonse zimene muli nazo.’
15 Dilia gasa bagadedafa dadi gagui dunu da abuliba: le dafabela: ? Bai Hina Gode da ili fane legei dagoi.
Chifukwa chiyani mulungu wanu wamphamvu uja Apisi wathawa? Iye sakanatha kulimba chifukwa Yehova anamugwetsa.
16 Dilia dadi gagui dunu da emo udagaguli dafai dagoi. Ilia enoma enoma amane sia: daha, ‘Hedolo! Ninia ha lai amoga medole legesu mae ba: ma: ne, ninia fi dunu diasuga ahoa: di.’
Ankhondo anu apunthwa ndi kugwa. Aliyense akuwuza mnzake kuti, ‘Tiyeni tibwerere kwathu, ku dziko kumene tinabadwira, tithawe lupanga la adani athu.’
17 Idibidi hina bagade ema amo gaheabolo dio asulima, ‘Sia: Bagade Hidasu Dunu, E da Hasalasisu Giadofai.’
Kumeneku iwo adzafuwula kuti, ‘Farao, mfumu ya ku Igupto mupatseni dzina lakuti, Waphokoso, Wotaya mwayi wake.’
18 Na, Hina Gode Bagadedafa, da Hina Bagade! Na da Gode Esala! Da: ibo Goumi da goumi huluane baligisa. Amola Gamele Goumi da hano wayabo bagade amoga bagade heda: i dagoi ba: sa. Amo defele, dilima doagala: su dunu ea gasa da dilia gasa bagadewane baligimu.
“Pali Ine wamoyo,” ikutero Mfumu, imene dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse, “wina adzabwera amene ali ngati Tabori phiri lopambana mapiri ena, ngati phiri la Karimeli loti njoo mʼmbali mwa nyanja.
19 Dilia Idibidi fi dunu! Udigili hawa: hamomusa: masa: ne momagema! Memefisi moilai bai bagade da wadela: i hafoga: i soge amo ganodini dunu esalebe hame ba: mu, agoai ba: mu galebe.
Konzani katundu wanu wopita naye ku ukapolo inu anthu a ku Igupto, pakuti Mefisi adzasanduka chipululu ndipo adzakhala bwinja mopanda wokhalamo.
20 Idibidi da bulamagau aseme noga: idafa agoane ba: sa. Be gagoe (north) amoga gasonasu awinimi ema doagala: musa: manebe ba: sa.
“Igupto ali ngati mwana wangʼombe wokongola, koma chimphanga chikubwera kuchokera kumpoto kudzalimbana naye.
21 Idibidi muni hawa: hamosu dadi gagui dunu amola da bulamagau mano fonobahadi defele, gasa hame ba: sa. Ilia da bu gegemusa: hame lelu. Ilia da sinidigili, hobea: i. Ilia wadela: mu eso da doaga: i dagoi.
Ngakhale ankhondo aganyu amene ali naye ali ngati ana angʼombe onenepa. Nawonso abwerera mʼmbuyo, nathawa pamodzi. Palibe amene wachirimika. Ndithu, tsiku la tsoka lawafikira; ndiyo nthawi yowalanga.
Aigupto akuthawa ndi liwu lawo lili ngati la njoka yothawa pamene adani abwera ndi zida zawo, abwera ndi nkhwangwa ngati anthu odula mitengo.
23 Ha lai dadi gagui wa: i da manebe ba: loba, Idibidi da sania agoane soiya afia: i. Ilia ha lai da dunu amo da goaheiga ifa aba amola iwila bagade wadela: su, amo defele ilima doagala: sa. Ha lai dadi gagui da idimu hame gala. Ilia idi da danuba: wa: i ilia idi baligisa.
Iwo adzadula nkhalango ya Igupto,” akutero Yehova, “ngakhale kuti ndi yowirira. Anthuwo ndi ochuluka kupambana dzombe, moti sangatheke kuwerengeka.
24 Idibidi dunu da gogosiasu ba: sa. Gagoe (north) fi dunu da ilima hasalasi dagoi. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
Anthu a ku Igupto achita manyazi atengedwa ukapolo ndi anthu a kumpoto.”
Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akunena kuti, “Ndili pafupi kulanga Amoni mulungu wa Tebesi. Ndidzalanganso Farao ndi Igupto pamodzi ndi milungu yake yonse, mafumu ake ndi onse amene amamukhulupirira.
26 Hina Gode Bagadedafa, Isala: ili fi ilia Gode, da amane sia: sa, “Na da Dibisi moilai bai bagade ea ogogosu ‘gode’ A: imone amola Idibidi fi huluane (ilia ‘gode’ amola hina bagade) ilima se bagade imunu. Na da Idibidi hina bagade amola dunu huluane ema fa: no bobogesa, amo lale, dunu amo da ili medole legemusa: hanai ilima imunu. Na da ili amo Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese amola ea dadi gagui wa: i ilima imunu. Be hobea, dunu da musa: Idibidi soge ganodini esalu, amo defele, dunu da bu amo ganodini esalumu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
Ndidzawapereka kwa amene akufuna kuwapha, ndiye kuti kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi atsogoleri ake ankhondo. Komabe, mʼtsogolomo Igupto adzakhalanso ndi anthu monga kale,” akutero Yehova.
27 Hina Gode da amane sia: i, “Na fi dunu! Mae beda: ma! Dilia da soge sedaga amo ganodini udigili hawa: hamonana. Be amoga Na da dili gaga: le, fadegamu. Dilia da dilia sogedafa amoga buhagili, olofole esalumu. Amasea, dilia da gaga: iwane, mae beda: iwane, amo ganodini esalumu.
“Iwe mtumiki wanga Yakobo, usachite mantha; usataye mtima, iwe Israeli. Ndithu Ine ndidzakupulumutsa kuchokera ku mayiko akutali, ndidzapulumutsanso zidzukulu zako kuchokera ku mayiko kumene anapita nazo ku ukapolo. Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala motakasuka ndi pa mtendere, ndipo palibenso wina amene adzamuopsa.
28 Na da dilima misini, dili gaga: mu. Na da fifi asi gala amoga Na da dili afagogoi dagoi, amo huluane wadela: lesimu. Be Na da dili hame wadela: lesimu. Na da dilima se imunu. Be amo se iasea, moloidafa se fawane imunu. Na, Hina Gode, Na da sia: i dagoi.”
Iwe mtumiki wanga Yakobo, usachite mantha, pakuti Ine ndili nawe,” akutero Yehova. “Ndidzawonongeratu mitundu yonse ya anthu a ku mayiko kumene ndakupirikitsira, Koma iwe sindidzakuwononga kotheratu. Ndidzakulanga iwe ndithu koma moyenerera; sindidzakulekerera osakulanga.”

< Yelemaia 46 >