< Yelemaia 41 >
1 Oubi fesu amo odega, Isama: iele (Nedanaia egefe amola Ilisiama ea aowa [Ilisiama da hina bagade ea fi dunu amola hina bagade ea eagene ouligisu dunu afae galu]) e da Misiba moilaiga Gedalaia gousa: musa: asi. Ilia huluane da gilisili ha: i nanoba,
Pa mwezi wachisanu ndi chiwiri Ismaeli mwana wa Netaniya, mdzukulu wa Elisama amene anali wa banja laufumu ndiponso mmodzi wa atsogoleri a ankhondo a mfumu, anabwera ku Mizipa kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ndi anthu khumi. Pamene ankadya naye kumeneko,
2 Isama: iele amola dunu nabuane ea sigi misi amo, ilia gegesu gobihei sedade duga: le gadole, Gedalaia medole legei.
Ismaeli mwana wa Netaniya pamodzi ndi anthu khumi aja anayimirira ndi kupha ndi lupanga Gedaliya mwana wa Ahikamu, mdzukulu wa Safani. Choncho anapha munthu amene mfumu ya ku Babuloni inamusankha kukhala bwanamkubwa wa dzikolo.
3 Amola Isama: iele da Isala: ili dunu huluane Misiba amoga Gedalaia sigi esalu, amola Ba: bilone dadi gagui dunu amogawi esalu, amo huluane medole lelegei.
Ismaeli anaphanso Ayuda onse amene anali pamodzi ndi Gedaliya ku Mizipa, kuphatikizanso asilikali a Ababuloni amene anali ku Mizipako.
4 Aya esoga, dunu huluane da Gedalaia ea medole lelegei amo hame nabi galu,
Mmawa mwake, anthu asanadziwe kuti Gedaliya waphedwa,
5 dunu 80agoane da Siegeme amola Siailou amola Samelia amoga misini, Misiba amoga doaga: i. Ilia da mayabo waga: ne, abula gadelale, ilisu da: i fa: ginisiwane misi. Ilia da gagoma amola gabusiga: manoma amo Debolo diasuga gobele salimusa: gaguli manebe ba: i.
kunafika anthu 80 ochekera ku Sekemu, Silo ndi Samariya, amene anali atameta ndevu zawo, atangʼamba zovala zawo ndi kudzichekacheka. Iwowa anatenga chopereka cha ufa ndi lubani kuti adzapereke ku Nyumba ya Yehova.
6 Amalalu, Isama: iele da Misiba amoga digini, ili gousa: musa: asi. E da ilima doaga: le, amane sia: i, “Sama misa! Gedalaia ba: musa: misa!”
Ismaeli mwana wa Netaniya anachoka ku Mizipa akulira kupita kukakumana nawo. Atakumana nawo, iye anati, “Bwerani mudzaonane ndi Gedaliya mwana wa Ahikamu.”
7 Ilia da Misiba moilai amo ganodini golili sa: ili, Isama: iele amola ea fa: no bobogesu dunu da hedolowane ili medole lelegele, ilia bogoi da: i hodo amo hano uli dogoi ganodini sanasisi.
Atafika pakati pa mzinda, Ismaeli mwana wa Netaniya pamodzi ndi anthu amene anali naye anawapha anthuwo ndi kuwaponya mʼchitsime.
8 Be amo gilisisu ganodini, dunu nabuane gala ilia da Isama: ielema ha: giwane edegei, “Nini mae medole legema! Ninia da widi, bali, olife susuligi amola agime hano, soge ganodini wamolegei diala.” Amaiba: le, e da amo dunu hame medole legei.
Koma anthu khumi a gululo anawuza Ismaeli kuti, “Musatiphe! Tili ndi tirigu ndi barele, mafuta ndi uchi, zimene tabisa mʼmunda.” Choncho anawasiya ndipo sanawaphere pamodzi ndi anzawo aja.
9 Hano uli dogoi amo ganodini Isama: iele da dunu e medole legei amo ilia da: i hodo ha: digi, amo da uli dogoi bagade. Musa: , Isala: ili hina bagade Ba: iasia da Yuda hina bagade A: isa ema doagala: beba: le, A:isa da amo uli dogoma: ne sia: i. Isama: iele da amo uli dogoi, bogoi dunu ilia da: i hodo ha: digi amola uli dogoi da nabai ba: i.
Tsono chitsime chimene anaponyamo mitembo ya anthu amene anawaphawo pamodzi ndi mtembo wa Gedaliya chinali chimene mfumu Asa anachikumba poopsedwa ndi Baasa mfumu ya Israeli. Ismaeli mwana wa Netaliya anachidzaza ndi mitembo.
10 Amalalu, e da hina bagade ea idiwi huluane amola Misiba dunu (amo Ba: bilone dadi gagui ouligisu Nebiusala: ida: ne da Gedalaia ema ouligima: ne sia: i) amo huluane afugili, ili udigili hawa: hamoma: ne, A:mone sogega hiouginana asi.
Pambuyo pake Ismaeli anatenga ukapolo anthu ena onse amene anali ku Mizipa: ana aakazi a mfumu pamodzi ndi ena onse amene anatsalira kumeneko, amene Nebuzaradani mtsogoleri wa asilikali olonda mfumu anapatsa Gedaliya mwana wa Ahikamu kuti akhale bwanamkubwa wawo. Ismaeli mwana wa Netaliya anatenga ukapolo anthuwa ndi kuwoloka nawo kumapita ku dziko la Aamoni.
11 Youha: ina: ne amola Yuda dadi gagui ouligisu dunu ema sigi esalu, ilia da Isama: iele ea wadela: i hou amo nabi dagoi.
Pamene Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye pamodzi anamva zoyipa zonse zimene Ismaeli mwana wa Netaniya anachita,
12 Amaiba: le, ilia da ilia fa: no bobogesu dunu gagadole, ema fa: no bobogele, hano wayabo Gibione moilai bai bagade gadenene amoga Isama: ielema doagala: i.
anatenga ankhondo awo onse kupita kukamenyana ndi Ismaeli mwana wa Netaniya. Anakamupeza kufupi ndi chidziwe chachikulu cha ku Gibiyoni.
13 Dunu amo da Isama: iele da gagulaligi ilia da Youha: ina: ne amola ea dadi gagui ouligisu dunu ba: beba: le, hahawane bagade ba: i.
Pamene anthu onse amene Ismaeli anawagwira anaona Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri a ankhondo amene anali naye, anasangalala.
14 Ilia da sinidigili, ilima hehenai.
Anthu onse amene Ismaeli anawagwira ukapolo ku Mizipa anabwerera ndi kupita kwa Yohanani mwana wa Kareya.
15 Be Isama: iele amola ea dunu godoane gala da Youha: ina: nema hobeale, A:mone sogega hobea: i.
Koma Ismaeli pamodzi ndi anthu ake asanu ndi atatu, anathawa Yohanani ndi kuthawira kwa Aamoni.
16 Amalalu, Youha: ina: ne amola ea dadi gagui ouligisu dunu da dadi gagui dunu amola uda amola mano amola gulusu danai dunu amo Isama: iele da udigili hawa: hamomusa: lai, amo ouligi.
Kenaka Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye anatsogolera anthu onse otsala a ku Mizipa amene anawapulumutsa kwa Ismaeli mwana wa Netaniya atapha Gedaliya mwana wa Ahikamu. Anthu amenewa anali: asilikali, akazi, ana ndi amuna ofulidwa otumikira mfumu amene anawatenga ku Gibiyoni.
Ndipo ananyamuka nayima ku Geruti Kimuhamu pafupi ndi Betelehemu pa ulendo wawo wopita ku Igupto
18 Ilia da Ba: bilone fi ilima bagade beda: i galu. Bai Ba: bilone hina bagade da Gedalaia amo Yuda soge ouligima: ne ilegei dagoi, amola Isama: iele da Gedalaia amo medole legei dagoi. Amaiba: le, ilia da Ba: bilone dunu ilima hobeamusa: , Idibidi sogega masusa: asi. Logoga ahoanoba, ilia da Gimiha: me moilai, Bedeleheme gadenene, ouesalu.
kuthawa Ababuloni. Iwo anaopa Ababuloniwo chifukwa Ismaeli mwana wa Netaniya anapha Gedaliya mwana wa Ahikamu, amene mfumu ya ku Babuloni inamuyika kukhala bwanamkubwa wa dzikolo.