< Yelemaia 19 >
1 Hina Gode da nama na da laga osoboga hamoi ganagu bidi lamusa: masa: ne sia: i. Amola na da dunu fi ilia asigilai dunu mogili amola asigilai gobele salasu dunu mogili, amo oule masa: ne sia: i.
Yehova anandiwuza kuti, “Pita ukagule mʼphika wadothi kwa munthu wowumba. Utenge akuluakulu ena a anthuwa ndi ansembe
2 Na da Bodesehede Logo Holei amoga ga asili, Hinome Fagoga doaga: le, Ea sia: alofele olelema: ne, E sia: i.
ndipo mupite ku Chigwa cha Hinomu chimene chili pafupi ndi pa chipata cha mapale. Pamenepo ukalengeze mawu amene ndikakuwuze.
3 Hina Gode da na da amane alofele sia: ma: ne sia: i, “Yuda fi hina bagade dilia amola Yelusaleme fi dunu dilia Na, Hina Gode Bagadedafa, Isala: ili fi ilia Gode, amo Na sia: nabima. Na da amo sogega wadela: su bagade iasimu. Nowa dunu da amo hou ba: sea, da bagadewane fofogadigimuba: le sidi agoai ba: mu.
Ukanene kuti, ‘Imvani mawu a Yehova, inu mafumu a ku Yuda ndi anthu a ku Yerusalemu. Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akuti: Tamverani! Ine ndibweretsa mavuto pa malo pano mwakuti aliyense amene adzamve adzadzidzimuka.
4 Dunu huluane da Na yolesi dagoiba: le, amola ogogosu ‘gode’ amo ilia amola ilia aowalalia amola Yuda hina bagade da hame dawa: i galu, ilima gobele salasu hou hamoiba: le, sogebi wadela: lesi dagoiba: le, amola amo sogebi ganodini wadela: i hame hamosu dunu bagohame udigili medole legeiba: le, Na da amo soge wadela: mu.
Pakuti anthu andikana Ine ndipo ayipitsa malo ano. Afukiza lubani pa malo ano kwa milungu imene iwo ngakhale makolo awo ngakhalenso mafumu a ku Yuda sanayidziwe. Iwo adzaza malowa ndi magazi a anthu osalakwa.
5 Ilia da ilia mano laluga gobele salimusa: , ogogosu ‘gode’ Ba: iele ea oloda hamoi dagoi. Amo hou hamoma: ne Na da hamedafa sia: i. Na da amo hamedafa dawa: i.
Amanga nsanja zopembedzerapo Baala, kuperekapo ana awo kuti akhale nsembe zopsereza kwa Baala, chinthu chimene Ine sindinalamule kapena kuchiyankhula, ngakhalenso kuchiganizira.
6 Amaiba: le, eso da misunu amoga amo sogebi ea dio da Doubede o Hinome Fago ilia da bu hame sia: mu. Be dio gaheabolo amo Medole Legesu Fago asuli dagoi ba: mu.
Nʼchifukwa chake taonani, masiku akubwera, akutero Yehova, pamene anthu sadzatchulanso malo ano kuti Tofeti kapena Chigwa cha Hinomu, koma Chophera anthu.
7 Amo sogebi ganodini Na da Yuda fi dunu amola Yelusaleme fi dunu ilia ilegei huluane hedofamu. Ilia ha lai da ilima hasalima: ne, amola gegesu ganodini ili medole legema: ne, Na da logo doasimu. Na da ilia bogoi da: i hodo amo sio fi amola sigua ohe amo ili moma: ne imunu.
“‘Pamalo pano ndidzasokoneza maganizo a anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu. Ndidzachititsa kuti adani awo awaphe ku nkhondo. Ndidzawakanthitsa kwa anthu amene akuwazonda. Mitembo yawo ndidzayipereka kwa mbalame za mlengalenga ndi zirombo za kutchire kuti ikhale chakudya chawo.
8 Na da Yelusaleme amoma wadela: su baligili iasimuba: le, nowa da baligimusa: ahoasea da bogomuwane fofogadigimu.
Mzinda uno ndidzawusakaza ndi kuwusandutsa chinthu chochititsa mantha ndi chonyansa. Onse odutsamo adzadabwa ndi kupukusa mitu yawo chifukwa cha kuwonongeka kwake.
9 Ha lai dunu da dunu huluane medole legemusa: , moilai sisiga: mu. Amo doagala: su da baligili gasa bagade ba: beba: le, dunu amo moilai ganodini esalebe da ilia na: iyado amola hina: mano amola ili hei manu.”
Adani awo adzawuzinga mzindawo kufuna kuwapha motero kuti anthu a mʼkatimo adzafika pomadyana wina ndi mnzake. Adzadya ana awo aamuna ndi ana awo aakazi.’
10 Amasea, Hina Gode da nama amane sia: i, “Dunu amo di da oule asi, amo ilia midadi ganagu goudane,
“Tsono iwe udzaphwanye mtsukowo anthu amene udzapite nawowo akuona,
11 ilima Hina Gode Bagadedafa da amane sia: sa olelema, ‘Na da amo moilai amola ea fi dunu goudamu. Amola amo laga osoboga hamoi ganagu da bu hahamomu hamedei, amo defele dilia fi bu hahamomu da hamedei ba: mu. Dunu da bogoi dunu uli dogomusa: sogebi hogoi helele, ba: mu hamedeiba: le, ilia da Doubede sogebi amoga uli dogomu.
ndipo ukawawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse akuti, Ine ndidzaphwanya dziko lino ndi mzinda uno ngati momwe wowumba amaphwanyira mbiya yake ndipo sangathe kuyikonzanso. Adzayika anthu akufa ku Tofeti chifukwa padzasowa malo ena owayika.
12 Na amo moilai amola amo ganodini esalebe dunu amo Doubede isu salasu defele hamomu. Amo Na da dafawane ilegesa.
Umu ndi mmene ndidzachitire ndi malo ano pamodzi ndi anthu okhalamo, akutero Yehova. Ndidzasandutsa mzindawu kukhala ngati Tofeti.
13 Yelusaleme diasu huluane amola Yuda hina bagade ilia diasu huluane amola diasu huluane amo da: iya ilia da gasumunima nodoma: ne gabusiga: manoma ulagisu amola ogogosu ‘gode’ ilima nodoma: ne, waini hano sogadigisu, amo diasu huluane da Doubede defele, ledo bagade hamoi ba: mu.”
Nyumba za mu Yerusalemu ndi za mafumu a ku Yuda ndidzazisandutsa ngati za ku Tofeti chifukwa ndi nyumba zimene pa madenga ake ankafukiza lubani kwa zolengedwa zamlengalenga ndi kuthira nsembe zachakumwa kwa milungu ina.’”
14 Amalalu, na da Doubede (Hinome Fago amoga Hina Gode da Ea sia: alofele olelema: ne, na asunasi) amo fisili asi. Na da asili, Debolo gagoi amo ganodini lelu, dunu huluane nabima: ne, Hina Gode Bagadedafa Isala: ili fi dunu ilia Gode, amo Ea sia: amane alofele sia: i,
Kenaka Yeremiya anabwerako ku Tofeti, kumene Yehova anamutuma kuti akanenere, nakayimirira mʼbwalo la Nyumba ya Yehova ndi kuwawuza anthu kuti,
15 “Na da amo moilai amola moilai huluane gadenene gala, amoga se iasu Na musa: olelei amo iasimu. Bai dilia dogo da ga: nasi dagoi, amola dilia da Na sia: hamedafa naba.”
“Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akuti, ‘Tamverani! Ine ndidzabweretsa masautso amene ndinanena aja pa mzinda uno ndi pa mizinda yozungulira, chifukwa anthu ake ndi nkhutukumve ndipo sanamvere mawu anga.’”