< Yelemaia 14 >
1 Hina Gode da esoi bagade ea hou olelema: ne, nama amane sia: i,
Awa ndi mawu amene Yehova anamuwuza Yeremiya onena za chilala:
2 “Yuda soge da da: i dioiwane didigia: su. Ea moilai bai bagade huluane da bogogia: lala. Ea fi dunu huluane da da: i dione, osoboga dia dafia: sa. Amola Yelusaleme da enoga fidima: ne wele sia: nana.
“Yuda akulira, mizinda yake ikuvutika; anthu ake adzigwetsa pansi mwachisoni, kulira kwa Yerusalemu kwakula.
3 Bagade gagui dunu da ilia hawa: hamosu dunu hano dima: ne asunasisa. Ilia da hano si amoga asili, hano hame dialebe ba: sa. Ilia hano nasu ganagu hano hamedei hagiwane bu gaguli maha. Ilia da: i dioiwane amola gagoudanu, gogosiane ilia odagi dedebole, buhagisa.
Anthu awo wolemekezeka akutuma antchito awo kuti akatunge madzi. Apita ku zitsime osapezako madzi. Choncho amabwerera ndi mitsuko yopanda madzi. Amanyazi ndi othedwa nzeru adziphimba kumaso.
4 Gibu da hame sa: iba: le, amola osobo huluane da hafoga: iba: le, ifabi ouligisu dunu da baligili da: i dione heawisa. Ilia amola odagi dedebosa.
Popeza pansi pawumiratu chifukwa kulibe madzi, alimi ali ndi manyazi ndipo amphimba nkhope zawo.
5 Sogega, “dia” ohe ame da ea gaheabolo lalelegei mano amo fisiagasa. Bai gisi hame galebeba: le.
Ngakhale mbawala yayikazi ikusiya mwana wake wakhanda ku thengo chifukwa kulibe msipu.
6 Sigua ‘dougi’ da agolo da: iya lela. Ilia sigua wa: me defele ha: ha: sa. Ilia da ha: i manu hameba: le, ilia si da wadela: sa.
Mbidzi zikuyima pa zitunda zopanda kanthu nʼkumapuma wefuwefu ngati nkhandwe; maso awo achita chidima chifukwa chosowa msipu.”
7 Na fi dunu da Nama amane wele sia: sa, ‘Dafawane! Ninia wadela: i hou da ninima diwane udidisa. Be Hina Gode! Dia musa: ilegele sia: i defele, nini fidima! Ninia da eso bagohame Di baligi fa: sea, wadela: le hamoi ba: sa.
Anthu akuti, “Ngakhale machimo athu akutitsutsa, koma Inu Yehova chitanipo kanthu chifukwa cha dzina lanu. Pakuti kusakhulupirika kwathu nʼkwakukulu; ife takuchimwirani.
8 Be Di fawane da Isala: ili fi gaga: musa: dawa: Di fawane da nini mae wadela: lesima: ne, gaga: musa: dawa: Di da abuliba: le ga fi dunu amo da gasi afadafa fawane ninia soge ganodini esalebe, agoane ba: sala: ?
Inu Yehova amene Aisraeli amakukhulupirirani ndi amene mumawapulumutsa pa nthawi ya masautso, chifukwa chiyani mukukhala ngati mlendo mʼdziko muno? Chifukwa chiyani muli ngati wapaulendo amene akungogona tsiku limodzi?
9 Di da abuliba: le, dunu da fofogadigibi agoane ba: sala: ? Abuliba: le, gasa hame dadi gagui nini fidimusa: hame dawa: agoane ba: sala: ? Hina Gode! Di da dafawane ninimagale esala! Ninia da Dia fi dunu! Nini mae yolesima!’”
Chifukwa chiyani muli ngati munthu amene wadzidzimutsidwa, kapena ngati wankhondo amene alibe mphamvu yopulumutsa? Komabe Inu Yehova, muli pakati pathu, ndipo tikudziwika ndi dzina lanu; musatitaye ife!”
10 Hina Gode da Ea fi dunu ilia hou olelema: ne, amane sia: sa, “Ilia da Na fisimusa: hobeamu hanai gala. Ilia da ilia hou amoma hina esaloma: ne hame dawa: Amaiba: le, Na da ilima hahawane hame. Na da ilia wadela: i hou bu dawa: mu amola amoba: le, se ilima imunu.”
Zimene Yehova akunena za anthuwa ndi izi: “Iwo amakonda kuyendayenda kwambiri; samatha kudziretsa. Nʼchifukwa chake Ine Yehova sindingawalandire, ndipo tsopano ndidzakumbukira zoyipa zawo ndi kuwalanga chifukwa cha machimo awo.”
11 Hina Gode da nama amane sia: i, “Amo dunu fidima: ne, Nama mae adole ba: ma!
Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Usawapempherere anthu awa kuti zinthu ziwayendere bwino.
12 Ilia da ha: i mae nawane sia: ne gadosea, Na da ili fidima: ne wele sia: su hame nabimu. Amola ilia da Nama ohe gobele salasu amola gagoma iasu iasea, Na da ili hahawane hame ba: mu. Be amo mae dawa: le, Na da gegesu amola ha: naba amola olo ilima iasili, ili medole lelegemu.”
Ngakhale asale zakudya, Ine sindidzamva kulira kwawo; ngakhale apereke nsembe zopsereza ndi chopereka cha chakudya, sindidzazilandira. Mʼmalo mwake, ndidzawapha ndi lupanga, njala ndi mliri.”
13 Amalalu, na da amane sia: i, “Ouligisudafa Hina Gode! Di dawa: ! Balofede dunu da Dia fi dunu da ha: i bagade amola gegesu hame ba: mu, amo ilima agoane sia: sa. Bai Di da sia: i dagoi, olofosu fawane da Dia soge amo ganodini ba: mu, ilia sia: sa.”
Koma ine ndinati, “Aa, Ambuye Yehova, aneneri amawawuza anthuwo kuti, sadzaphedwa ndi lupanga kapena kuvutika ndi njala. Koma kuti Inu mudzawapatsa mtendere wokhawokha pamalo pano.”
14 Be Hina Gode da nama bu adole i, “Amo balofede dunu da Na Dioba: le ogogosa. Na da ili hame asunasi amola ilia da Na sia: alofele olelema: ne, Na da hamedafa sia: i. Ilia esala ba: su olelebe amo da Nama hame misi. Ilia ba: la: lusu liligi da hamedei liligi amo ilisu ilia asigi dawa: su ganodini hamoi.
Ndipo Yehova anandiwuza kuti, “Ndi zabodza kuti aneneriwa akunenera mʼdzina langa. Ine sindinawatume kapena kuwasankha kapenanso kuyankhula nawo. Iwo amakuwuzani zinthu zabodza zomwe amati anaziona mʼmasomphenya, kapena pogwiritsa ntchito mawula achabechabe. Zimene amayankhula ndi zongopeka mʼmutu mwawo.
15 Na, Hina Gode, da dima olelemu. Amo balofede dunu (amo Na da hame asunasi, be ilia da Na Dioba: le gegesu amola ha: i bagade da hame misunu ogogole sia: sa) Na da ili gegesu amola ha: i bagade amoga medole legemu.
Nʼchifukwa chake Ine Yehova ndikuti aneneri amenewa akulosera mʼdzina langa pamene Ine sindinawatume. Iwo amati simudzafa pa nkhondo kapena ndi njala mʼdziko muno. Koma tsono ndi iwowo, aneneriwa amene adzafe pa nkhondo kapena ndi njala.
16 Dunu amoma ilia amo liligi ogogole sia: i, ilia amola da gegesu amola ha: i bagade amoga medole legei ba: mu. Ilia bogoi da: i hodo da Yelusaleme logoga ha: digi dagoi ba: mu, amola amo uli dogoma: ne, dunu afae da hame ba: mu. Amo hou da ili huluanema doaga: mu. Amoga ilia uda amola dunu mano amola uda mano, huluane medole legei dagoi ba: mu. Ilia wadela: i hou hamoiba: le, dabe lamu.”
Ndipo anthu amene anawaloserawo adzaponyedwa mʼmisewu ya mu Yerusalemu atafa ndi njala ndi lupanga. Sipadzapezeka wowayika mʼmanda popeza iwowo, akazi awo, ana awo aamuna, onse adzakhala atafa. Ine ndidzawagwetsera chilango chowayenera.
17 Hina Gode da na da Ea fi dunu ilima na da: i dioi ilima olelema: ne sia: i. Ea sia: beba: le, na da ilima amane sia: i, “Haga amola gasia amola na si hano da gudu sa: imu da defea. Na dibi da hamedafa dagomu. Bai na fi dunu da oso dogone fa: ginisi amola se bagade naba.
“Awuze mawu awa: “‘Maso anga akugwetsa misozi kosalekeza usana ndi usiku; chifukwa anthu anga okondedwa apwetekeka kwambiri, akanthidwa kwambiri.
18 Na da moifufu amoga ahoasea, na da dunu gegesu ganodini medole legei ilia bogoi da: i hodo ba: sa. Na da moilai gagagai amo ganodini ahoasea, na da dunu ha: ga bogogia: lalebe ba: sa. Balofede amola gobele salasu dunu amola da mugululi, soge amo ilia hame dawa: soge amoga afugili asi.”
Ndikapita kuthengo, ndikuona amene aphedwa ndi lupanga; ndikapita mu mzinda, ndikuona amene asakazidwa ndi njala. Ngakhale aneneri pamodzi ndi ansembe onse atengedwa.’”
19 Hina Gode! Di da dafawanedafa Yuda fi fisiagabela: ? Di da Saione dunu higasala: ? Di da abuliba: le nini mae uhima: ne ninima se bagadedafa ibala: ? Ninia da olofosu hogoi helei, be hahawane hou da hame doaga: i. Ninia da uhinisisu hogoi helei, be beda: su bagade fawane ba: i.
Kodi anthu a ku Yuda mwawakana kwathunthu? Kodi mtima wanu wanyansidwa nawo anthu a ku Ziyoni? Chifukwa chiyani mwatikantha chotere kuti sitingathenso kuchira? Ife tinayembekezera mtendere koma palibe chabwino chomwe chabwera, tinayembekezera kuchira koma panali kuopsezedwa kokhakokha.
20 Hina Gode! Ninia da dima wadela: le bagade hamoi. Ninia wadela: i hou amola ninia aowalalia ilia wadela: i hou, amo ninia Dima fofada: nana.
Inu Yehova, ife tikuvomereza kuyipa kwathu ndiponso kulakwa kwa makolo athu; ndithu ife tinakuchimwiranidi.
21 Dia hahawane ninima imunu sia: i ilegesu amo bu dawa: ma! Dia nini mae higama! Yelusaleme da Dia hadigi fisu ea sogebi. Amaiba: le, Yelusaleme da gogosiasa: besa: le, gaga: ma. Dia gousa: su ninima hamoi amo mae fima.
Musatikane kuopa kuti dzina lanu linganyozedwe; musanyoze mpando wanu waufumu waulemerero. Kumbukirani pangano lanu ndi ife ndipo musachiphwanye.
22 Fifi asi gala ilia loboga hamoi ogogosu ‘gode’ da gibu iasimu hame dawa: Mu hisu da gibu hamomu hame dawa: Ninia Hina Gode! Di fawane da amo hamomusa: dawa: Amaiba: le, ninia dafawaneyale esaloma: beyale dawa: lusu da Di fawane.
Mwa milungu yachabechabe ya anthu a mitundu ina, kodi pali mulungu amene angagwetse mvula? Ife chikhulupiriro chathu chili pa Inu, popeza Inu nokha ndinu Yehova Mulungu wathu amene mukhoza kuchita zimenezi.