< Yelemaia 12 >
1 Hina Gode! Na da Dima fofada: loba, Di da moloidafa ba: la: loba. Be na da moloidafa hou hisu hisu Dima adole ba: ma: mu. Abuliba: le wadela: i hamosu dunu da bagade gagui amola hahawane esalabala? Abuliba: le ogogosu wamolasu dunu da didili hamosala: ?
Yehova, Inu mumakhala wokhoza nthawi zonse ndikati nditsutsane nanu. Komabe ndikufuna kuyankhula nanu za mlandu wanga. Chifukwa chiyani anthu oyipa zinthu zimawayendera bwino? Chifukwa chiyani anthu achinyengo amakhala pabwino?
2 Di da amo wadela: i hamosu dunu bugisa. Ilia difi da gudu sa: ili, ilia heda: sa amola fage legesa. Ilia da ogogole eno dunuma Dia hou nodone sia: sa. Be ilia da Dima hame asigisa.
Inu munawadzala ndipo anamera mizu; amakula ndi kubereka zipatso. Dzina lanu limakhala pakamwa pawo nthawi zonse, koma mitima yawo imakhala kutali ndi Inu.
3 Be Hina Gode! Di da na hou dawa: Di da na hawa: hamosu ba: lala! Na da Dima bagade asigisa. Amo di dawa: Dunu da sibi medole legemusa: hiouginana ahoa, amo defele Dia amo wadela: i dunu hiouginana masa. Dia ili medole legemusa: eso ilegema! Amola ilia da amo esoga doaga: mane, Dia noga: le sosodo aligima!
Koma Inu Yehova, ine mumandidziwa; mumandiona ndipo mumayesa zolingalira zanga. Akokeni anthu oyipawo ngati nkhosa zokaphedwa! Ayikeni padera mpaka tsiku loti akaphedwe!
4 Eso habodane ninia soge da hafoga: i dagoi amola gisi sogebi huluane ganodini bioi dagoi ba: ma: bela: ? Ohe fi amola sio fi amola da bogogia: lala. Bai ninia fi dunu da wadela: le hamonana. Amola ilia da amane sia: daha, “Gode da ninia hamobe hame ba: lala.”
Kodi dziko lidzakhala likulirabe mpaka liti ndipo udzu mʼmunda uliwonse udzakhalabe ofota mpaka liti? Nyama ndi mbalame kulibiretu chifukwa anthu amene amakhalamo ndi oyipa. Iwo amati: “Yehova sangathe kuona ntchito zathu.”
5 Hina Gode da amane sia: i, “Yelemaia! Di da dunu baligimusa: hehenanebeba: le, helesa. Di da habodane hosi baligimusa: hehenama: bela: ? Di da ifa hamedene umi amoga leloma: ne hame dawa: beba: le, habodane Yodane hano gadenene iwila amo ganodini leloma: bela: ?
Yehova anayankha kuti, “Ngati kukutopetsa kuthamanga pamodzi ndi anthu nanga ungapikisane bwanji ndi akavalo? Ngati ukupunthwa ndi kugwa pa malo abwino, udzatha bwanji kuthamanga mʼnkhalango za ku Yorodani?
6 Dunu huluane, amola dia sosogodafa, diolalali da di hohonoi dagoi. Dunu eno da dima doagala: sea, ilia amola da dima doagala: musa: gilisisa. Ilia da dima asigi sia: sia: sea, ilia hou mae dafawaneyale dawa: ma.”
Ngakhale abale ako ndi anansi akuwukira, onsewo amvana zokuyimba mlandu. Usawakhulupirire, ngakhale ayankhule zabwino ndi iwe.
7 Hina Gode da amane sia: sa, “Na da Isala: ili yolesi dagoi. Na ilegei fi amo Na da higale yolesi. Dunu fi amoma Na da asigisa, Na da ilia ha lai dunu amo ilia lobo da: iya ligisi dagoi.
“Ine ndawasiya anthu anga; anthu amene ndinawasankha ndawataya. Ndapereka okondedwa anga mʼmanja mwa adani awo.
8 Na ilegei fi da Nama baligi fa: su. Ilia da laione wa: me iwilaga esala defele Nama husu. Amaiba: le, wali Na da Na fi higasa.
Anthu amene ndinawasankha asanduka ngati mkango wa mʼnkhalango. Akundibangulira mwaukali; nʼchifukwa chake Ine ndikudana nawo.
9 Na ilegei fi dunu da sio afae amo da la: idi la: idi buhibaga doagala: i, amo defele ba: sa. Sigua ohe huluane, ilia amo moma: ne misa: ne wele sia: ma!
Anthu anga amene ndinawasankha asanduka ngati mbalame yolusa yamawangamawanga imene akabawi ayizinga. Pitani, kasonkhanitseni nyama zakuthengo. Mubwere nazo kuti zidzadye mbalameyo.
10 Ga fi ouligisu dunu bagohame da Na waini efe sagai wadela: lesi. Ilia da Na ifabi huluane amo ososa: gi. Na soge ida: iwane gala ilia wadela: lesili, bu hafoga: i soge agoane hamosu.
Abusa ambiri anawononga munda wanga wa mpesa, anapondereza munda wanga; munda wanga wabwino uja anawusandutsa chipululu.
11 Na da Na soge ba: sea, wadela: i hafoga: i soge agoane ba: sa. Soge huluanedafa da wadela: i hafoga: i soge agoane hamoi, amola dunu huluane da amo asigiwane hame dawa: digisa.
Unawusandutsadi chipululu. Ukanali wokhawokha chomwecho ukundilirira Ine. Dziko lonse lasanduka chipululu chifukwa palibe wolisamalira.
12 Hafoga: i agolo soge amoga dunu da gegele lamusa: maha. Na da soge huluane wadela: lesimusa: gegesu dunu asunasi dagoi. Dunu huluane da olofole esalumu hame dawa:
Anthu onse owononga abalalikira ku zitunda zonse za mʼchipululu. Yehova watuma ankhondo ake kudzawatha kuyambira kumalire ena a dziko mpaka ku malire enanso a dziko, ndipo palibe amene adzakhale pa mtendere.
13 Na fi dunu da widi hawa: bugi, be gagalobo fawane faisa. Ilia da gasa bagadewane hawa: hamoi, be bidi hame ba: i. Na da ilima ougi bagadeba: le, ilia sagai da ha: i manu hame legei.”
Anthu anafesa tirigu koma anatuta minga; anadzitopetsa kugwira ntchito koma osapeza phindu lililonse. Choncho mudzachita manyazi ndi zokolola zanu chifukwa cha mkwiyo wa Yehova.”
14 Hina Gode da amane sia: sa, “Na da Isala: ili ilia na: iyado fi dunu ilima sia: gala. Bai ilia da soge amo Na da Na fi Isala: ili dunu ilima i, amo wadela: lesi dagoi. Dunu da bugi amo a: le fasibi defele, Na da amo dunu ilia soge amoga a: le fasimu. Na da Yuda fi dunu gaga: mu.
“Anthu oyipa oyandikana ndi anthu anga Aisraeli, akuwalanda Aisraeliwo dziko, cholowa chimene ndinawapatsa. Nʼchifukwa chake ndidzawachotsa mʼdziko limenelo, ndipo ndidzachotsa banja la Yuda pakati pawo.
15 Be Na da amo fi dunu fadegale fasili ga gaguli ahoasea, fa: no Na da bu ilima asigili, ilia sogedafa amoga bu oule masunu.
Komabe nditawachotsa, ndidzawachitiranso chifundo, ndipo ndidzabwezera aliyense cholowa chake ndi dziko lake.
16 Ilia da dafawanedafa Na fi dunu ilia sia: ne gadosu hou lalegagusia amola ‘Hina Gode da esala’ amo sia: dafawane ilegesea (musa: ilia da Na fi ilima Ba: iele ea dio amoma dafawane ilegema: ne sia: su olelei), amasea ilia da Na fidafa amoga gilisi dagoi ba: mu, amola ilia da hahawane bagade gaguiwane esalumu.
Ndipo ngati iwo adzaphunzira bwino njira za anthu anga ndi kulumbira mʼdzina langa, namanena kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’ monga iwo anaphunzitsira anthu anga kulumbira mʼdzina la Baala, Ine ndidzawakhazikitsa pakati pa anthu anga.
17 Be nowa fi da Na sia: hame nabasea, Na da amo fi fadegale fasili, wadela: lesimu. Na, Hina Gode da sia: i dagoi.”
Koma ngati mtundu wina uliwonse sudzamvera, Ine ndidzawuchotsa ndi kuwuwonongeratu,” akutero Yehova.