< Aisaia 57 >

1 Moloidafa dunu da bogosa, be eno dunu da dawa: hame laha, amola ilia da hame asigisa. Be moloi dunu da bogosea, bidi hamosu da ilima se hame iaha.
Anthu olungama amafa, ndipo palibe amene amalingalira mu mtima mwake; anthu odzipereka amatengedwa, ndipo palibe amene amamvetsa chifukwa chake. Anthu olungama amatengedwa kuti tsoka lisawagwere.
2 Nowa da noga: iwane esalea da bogosea, olofosu amola helefisu ba: mu.
Iwo amene amakhala moyo wolungama amafa mwamtendere; amapeza mpumulo pamene agona mu imfa.
3 “Dilia wadela: i hamosu dunu! Guiguda: fofada: musa: misa! Dilia hou da wamuni dawa: su dunu, amola inia uda adole lasu dunu, amola hina: da: i bidi lasu uda, ilia hou defele wadela: idafa.
“Bwerani kuno, anthu ochita zoyipa, inu muli ngati zidzukulu za mkazi wachigololo ndi wadama!
4 Dilia da nowama oufesega: sala: ? Dilia ogogosu dunu! Nowama oufesega: sala: ?
Kodi inu mukuseka yani? Kodi mukumunena ndani ndi kupotoza pakamwa panu? Kodi inu si ana owukira, zidzukulu za anthu abodza?
5 Dilia da ogogosu ‘gode’ ilima nodone sia: ne gadomusa: , sema gosa: su ifa haguduga wadela: i udigili uda lasu hou hamonana. Dilia da magufu gelabo hano gadenene diala, amo ganodini dilia mano gobele salimusa: medole legesa.
Inu mumapembedza mafano pamene mumalobodoka ndi zilakolako zanu pakati pa mitengo ya thundu, ndiponso pa tsinde pa mtengo uliwonse wa nthambi zambiri. Mumapereka ana anu ngati nsembe mu zigwa ndiponso mʼmingʼalu ya mʼmatanthwe.
6 Dilia da enemei igi amo hanoga lasea, amoma ‘gode’ dio asuli, nodone sia: ne gadosa. Dilia da ilima gobele salimusa: , waini hano sogadigisa amola ilima ima: ne gagoma gaguli maha. Dilia adi dawa: bela: ? Na da amo hou hahawane ba: sala: ? Hame mabu!
Mafano a pakati pa miyala yosalala ya mu zigwa ndiye chuma chanu. Inde, ndiye gawo lanu. Mumapereka chopereka cha chakumwa kwa mafanowo, ndipo mumaperekanso chopereka cha chakudya. Kodi zimenezi zingandichititse kuti ndikukomereni mtima?
7 Dilia da ogogosu ‘gode’ ilima gobele salasu hamoma: ne amola wadela: i ledo uda lasu hou hamoma: ne, goumi sedade amoba: le heda: sa.
Inu munayiwala bedi lanu pa phiri lalitali ndi looneka kutali. Mumapita kumeneko kukapereka nsembe zanu.
8 Dilia da ledo bagade loboga hamoi ‘gode’ amo dilia logo ga: su amo ganodini legesa. Dilia da Na fisisa. Dilia da abula gisa: le, dilia amola wadela: i hina: da: i bidi lasu uda gilisili da: i nabadowane diaheda: su bagade amoga fila heda: sa. Amola amogawi dilia da dilia wadela: i uda hanai hou gumisa.
Mʼnyumba mwanu mwayika mafano kuseri kwa zitseko ndiponso pa mphuthu. Mwandisiya Ine, mwavula zovala zanu. Bedi lanu mwalikulitsa ndipo mwakwera ndi zibwenzi zanu, ndiye mwazilipira kuti mugone nazo. Kumene mwakwaniritsa zilakolako zanu zoyipa.
9 Dilia da gabusiga: manoma legelalu, ogogosu ‘gode’ amo Moulege amoma nodone sia: ne gadomusa: ahoa. Dilia da ‘gode’ liligi eno ilima sia: ne gadomusa: amo hogoma: ne, dilia da sia: ne iasu dunu soge sedagaga asuna ahoa. Amola amo hogomusa: dilia da osobo bagade baligili, bogosu sogebi amoga ahoa. (Sheol h7585)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol h7585)
10 Dilia da eno ‘gode’ hogomusa: , hele bagade naba. Be amo hogosu hou dilia fisimusa: hame dawa: Dilia ledo bagade loboga hamoi ‘gode’ da dilima gasa iaha amo dawa: beba: le, dilia gasa da bu gaheabolo laha.”
Inu mumatopa ndi maulendo anu, koma simunathe kunena kuti, ‘Nʼzopanda phindu.’ Munapezako kumeneko zokhumba zanu nʼchifukwa chake simunalefuke.
11 Hina Gode da amane sia: sa, “Amo ‘gode’ ilia da nowala: ? Dilia da ilima beda: iba: le, Nama ogogosa, amola dilia da Na gogoleidafa. Na da eso bagohame ouiya: le, esalebeba: le, dilia da Nama nodosu hou yolesila: ?
“Kodi ndani amene mwachita naye mantha ndi kumuopa, kotero kuti mwakhala mukundinamiza, ndipo Ine simundikumbukira nʼkomwe, kapena kuganizirapo mʼmitima yanu za Ine? Kodi mwaleka kundiopa chifukwa choti ndakhala chete nthawi yayitali?
12 Dilia hou da moloidafa dilisu dawa: lala. Be Na da dunu huluane ba: ma: ne, dilia wadela: i hou olelemu. Amola dilia loboga hamoi ‘gode’ da dili fidimu gogolemu.
Koma ndaonetsa poyera ntchito zanu zomwe mumati nʼzolungama, ndi mafano anu kuti nʼzosathandiza.
13 Dilia fidima: ne wele sia: ne disia, dilia loboga hamoi ‘gode’ liligi dili fidimu da defea. Fo fonobahadi da amo liligi mini masa: ne dawa: Be nowa da Na dafawaneyale dawa: beba: le da Isala: ili sogega esalumu amola Na Debolo diasu ganodini Nama nodone sia: ne gadomu.”
Pamene mufuwula kupempha thandizo, mafano anu amene munasonkhanitsawo ndiyetu akupulumutseni! Mphepo idzanyamula mafano anu onsewo, mpweya chabe udzawulutsa mafanowo. Koma munthu amene amadalira ine adzalandira dziko lokhalamo. Phiri langa lopatulika lidzakhala lakelake.”
14 Hina Gode da amane sia: sa, “Na fi dunu Nama bu sinidigima: ne, ilia logo fodole, momagema! Logo ga: su liligi huluane fadegama.
Ndipo panamveka mawu akuti, “Undani, undani, konzani msewu! Chotsani zotchinga pa njira yoyendamo anthu anga.”
15 Na da gaguia gadoi amola Hadigi Gode, eso huluane Fifi Ahoanusu Gode esala. Na da gadodafa amola hadigi sogebi amo ganodini esala. Be Na da asaboi dunu ilia wadela: i hou fofada: nanu Nama sinidigisa, agoaiwane dunu ilima Na da gilisili esala. Bai Na da ilima hame beda: su hou, amola hobea misunu hou da noga: idafa amo dafawane esaloma: beyale dawa: su hou, ilima bu iaha.
Pakuti Iye amene ali Wamkulu ndi Wopambanazonse, amene alipo nthawi zonse, amene dzina lake ndi Woyerayo, akunena kuti, “Ndimakhala pamalo aulemu ndi opatulika, koma ndimakhalanso ndi munthu wodzichepetsa ndi wosweka mtima kuti odzichepetsawo ndiwalimbitse ndi kuwachotsa mantha osweka mtima.
16 Na da Na fi dunu ilima esalusu i dagoi, amola ilia da da: i dioiba: le dafasa: besa: le, Na da eso huluane ilima diwaneya hame udidimu, amola eso huluane ilima hame ougimu.
Sindidzawatsutsa anthu mpaka muyaya kapena kuwapsera mtima nthawi zonse, popeza kuti ndinalenga anthu anga ndi kuwapatsa mpweya wamoyo.
17 Ilia da wadela: i hou amola uasu hou hamobeba: le, Na da ilima ougi galu. Amaiba: le, Na da ilima se iasu amola ili yolesiagai. Be ilia da amo sisasu mae dawa: le, hi hanaiga udigili asi.
Ine ndinakwiya kwambiri chifukwa cha tchimo lawo ladyera; ndinawalanga ndi kuwafulatira mokwiya, koma iwo anapitirirabe kuchita ntchito zawo zoyipa.
18 Na da ilia hou ba: i dagoi, be Na da ili uhinisimu. Na da ili bisili masunu, amola ili fidimu, amola nowa da da: i dioiba: le, dinana, amo Na da ilia dogo denesinisimu.
Ndaona zochita zawo, komabe ndidzawachiritsa; kuwapumulitsa ndi kuwapatsa mtendere,
19 Na da gadenene dunu fi esala, amola fi eno sedaga esala ilima olofosu ima: ne sia: mu. Na da Na fi dunu uhinisimu.
anthu olira a mu Israeli adzanditamanda ndi milomo yawo. Anthu amene ali kutali ndi apafupi pomwe ndidzawapatsa mtendere,” “Ndipo ndidzawachiritsa.” Akutero Yehova.
20 Be wadela: i hamosu dunu da hano wayabo bagade, ea gafului agoane yagugusa. Ilia helefisu hame dawa: , amola gafului da fafu amola ledo bibiagosa.
Koma anthu oyipa ali ngati nyanja yowinduka, yosatha kukhala bata, mafunde ake amaponya matope ndi ndere.
21 Be wadela: i hamosu dunu da olofosu hamedafa ba: mu,” Hina Gode da amane sia: sa.
“Palibe mtendere kwa oyipa,” akutero Mulungu wanga.

< Aisaia 57 >