< Aisaia 45 >

1 Hina Gode da Sailase hina bagade hamoma: ne ilegei dagoi. E da Sailase amo fifi asi gala ilima hasanasima: ne ilegei dagoi. Sailase da hina bagade eno ilia gasa wadela: lesimu. Hina Gode da Sailase golili sa: ima: ne, moilai bai bagade ilia ga: su doasimu. Hina Gode da Sailasema amane sia: sa,
Yehova akuyankhula ndi wodzozedwa wake Koresi amene anamugwira dzanja lamanja kuti agonjetse mitundu ya anthu ndi kuwalanda mafumu zida zawo zankhondo, ndi kutsekula zitseko kuti zipatazo zisadzatsekedwenso ndi ichi:
2 “Na Nisu da dia logo fodomu. Na da goumi amola agolo mugululi, umi hamomu. Na da “balase” logo ga: su mugulumu amola ouli galiamo agoai ga: su liligi goudamu.
Ine ndidzayenda patsogolo pako, ndi kusalaza mapiri; ndidzaphwanya zitseko za mkuwa ndi kuthyola mipiringidzo ya chitsulo.
3 Na da liligi noga: idafa gasi agoai sogebi ganodini wamolegei, amo dima imunu. Amasea, Na da Hina Gode amo di da dawa: mu. Amola Isala: ili Godedafa da dia dio dawa: beba: le, dima wele sia: i dagoi.
Ndidzakupatsa chuma chobisika mu mdima, katundu wa pamalo obisika, kotero kuti udziwe kuti Ine ndine Yehova Mulungu wa Israeli, amene ndakuyitana pokutchula dzina.
4 Di da Na hawa: hamosu dunu amo Isala: ili (Na ilegei dunu fi) amo fidima: ne, Na da di ilegei dagoi. Di da Na hame dawa: , be eno dunu ilia da dima nodoma: ne, Na da ilegei dagoi.
Chifukwa cha mtumiki wanga Yakobo, chifukwa cha wosankhidwa wanga Israeli, Ine ndakuyitana pokutchula dzina ndipo ndakupatsa dzina laulemu ngakhale iwe sukundidziwa Ine.
5 Na da Hina God! Eno ‘gode’ da hame gala. Dia da Na hame dawa: , be Na da dia hawa: hamomu defele, gasa dima imunu.
Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina; kupatula Ine palibenso Mulungu wina. Ndidzakupatsa mphamvu, ngakhale sukundidziwa Ine,
6 Dunu huluanedafa, osobo bagade bega: asili eno bega: doaga: sa, amo huluane ilia da Na da Hina Gode amola eno ‘gode’ da hame gala amo dawa: ma: ne, Na da agoane hamomu.
kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo anthu adzadziwa kuti palibe wina koma Ine ndekha. Ine ndine Yehova, ndipo palibenso wina.
7 Na da hadigi amola gasi hahamosa. Na da hahawane hou amola gugunufinisisu hou gaguli maha. Na, Hina Gode, da amo hou huluane hamonana.
Ndimalenga kuwala ndi mdima, ndimabweretsa madalitso ndi tsoka; ndine Yehova, amene ndimachita zonsezi.
8 Na da muagado mabe gibu defele hasalasu hou iasimu. Fedege agoane, osobo bagade da ea lafi dagale, amo hou da: gimu. Amasea, sogea fudagala: su defele, hahawane dogolegele ahoasu hou amola moloidafa hou da osobo bagadega dialebe ba: mu. Na, Hina Gode da amo hou misa: ne, hamomu.
“Iwe thambo gwetsa mvula kuchokera kumwamba; mitambo ivumbwe mivumbi ya chilungamo. Dziko lapansi litsekuke, ndipo chipulumutso chiphuke kuti chilungamo chimereponso; Ine Yehova, ndine ndalenga zimenezi.
9 Laga osoboga hamoi ofodo, amo ofodo eno huluane defele da ea hahamosu dunuma sia: ga gegemu da defeala: ? Laga osobo da ofodo hahamosu dunuma ea hamobe adole ba: sala: ? Laga osoboga hamoi ofodo da e hahamosu dunu amoma, “Di da hahamosu hou hame dawa: !” amo sia: sia: sala: ?
“Tsoka kwa wokangana ndi mlengi wake, ngakhale kuti ali ngati phale chabe pakati pa mapale anzake. Kodi dongo lingafunse munthu wowumba kuti, ‘Kodi ukuwumba chiyani?’ Kodi ntchito yako inganene kuti, ‘Ulibe luso?’
10 Nowa da ea ada amola ame elama, “Ali da abuliba: le na agoane hahamobela: ?” Elama agoane adole ba: sala: ?
Tsoka kwa wofunsa abambo ake kuti, ‘Kodi munabereka chiyani?’ Kapena amayi ake kuti, ‘Kodi mufuna kubereka chiyani?’
11 Hina Gode, Isala: ili ea Hadigi Gode da dunu ilia hobea misunu hou hahamonana, amola e da amane sia: sa, “Dilia da Na manolali ilima Na hamosu, amo da noga: i hame sia: mu da defea hame galebe. Dilia da Nama, “agoane hamoma!” sia: mu da hamedei.
“Yehova Woyerayo wa Israeli, ndiponso Mlengi wake akunena, zokhudza zinthu zimene zikubwera ndi izi: Kodi iwe ukundifunsa za ana anga, kapena kundilamula pa zokhudza ntchito zanga?
12 Na fawane da osobo bagade amo ganodini dunu fi esaloma: ne, hahamoi dagoi. Na gasaga Na da mu fadegale gai. Na da eso amola oubi amola gasumuni ouligisa.
Ndine amene ndinapanga dziko lapansi ndikulenga munthu kuti akhalemo. Ine ndi manja anga ndinayalika thambo; ndimalamulira zolengedwa zonse za mlengalenga.
13 Na Nisu da Sailasema Na hanai hamoma: ne, amola hou huluane moloma: ne, sia: i dagoi. Ea logo ahoabe huluane, Na da molomu. E da Na moilai bai bagade Yelusaleme amo bu gagumu. Amola Sailase da Na fi dunu (amo da wali udigili hawa: hamonana, ) amo ilia halegale masa: ne logo doasimu. Dunu eno da amo hamoma: ne, ema bidi o hano suligili hame iasu.” Hina Gode Bagadedafa da sia: i dagoi.
Ndine amene ndidzawutsa Koresi kuti chilungamo changa chikwaniritsidwe: ndipo ndidzawongolera njira zake zonse. Iye adzamanganso mzinda wanga ndi kumasula anthu anga amene ali mu ukapolo, wopanda kupereka ndalama kapena mphotho, akutero Yehova Wamphamvuzonse.”
14 Hina Gode da Isala: ili fi ilima amane sia: sa, “Dilia da Idibidi amola Sudane ilia gagui liligi huluane lamu. Amola Siba dunu sedade da dilia udigili hawa: hamosu dunu ba: mu. Ilia da sia: ine amoga la: gili, dilima fa: no bobogemu. Ilia da dilima beguduli, amane sia: mu, ‘Gode da dili esala - Hi fawane da Godedafa.
Yehova akuti, “Chuma cha ku Igupto ndi chuma cha malonda cha Kusi chidzakhala chanu. Anthu amphamvu zawo ndi athanzi a ku Seba adzabwera kwa inu ndipo adzakhala anthu anu; iwo adzidzakutsatani pambuyo panu ali mʼmaunyolo. Adzakugwadirani ndi kukupemphani, ponena kuti, ‘Ndithudi Mulungu ali ndi inu, ndipo palibenso wina; palibenso mulungu wina.’”
15 Isala: ili fi ilia Gode, ilia Gaga: su dunu, E da hou agoane hamosa. E da wamoaligisa.
Zoonadi inu muli ndi Mulungu wobisika amene ali Mulungu ndi Mpulumutsi wa Israeli.
16 Dunu amo da ogogosu ‘gode’ hahamobe da gogosiasu ba: mu. Dunu eno da ili higamu.
Onse amene amapanga mafano adzawachititsa manyazi ndi kuwanyozetsa. Adzakhala osokonezeka maganizo.
17 Be Hina God da Isala: ili dunu gaga: i dagoi. Ilia hasalasu hou da mae fisili dialalalumu. Amola ilia da gogosiasu hamedafa ba: mu.’”
Koma Yehova adzapulumutsa Israeli ndi chipulumutso chamuyaya; simudzachitanso manyazi kapena kunyozeka mpaka kalekale.
18 Hina Gode da mu hahamoi. Hi fawane da Godedafa. E da osobo bagade hahamoi-E da amo mae muguluma: ne, gasawane hamoi. E da soge wadela: i hame be noga: idafa hamoi, Amola dunu da hahawane ganodini esaloma: ne, hamoi dagoi. Hi fawane da amane sia: sa, “Na da Hina Gode. Eno ‘gode’ da hamedafa.
Yehova analenga zinthu zakumwamba, Iye ndiye Mulungu; amene akulenga dziko lapansi, ndi kulikhazikitsa, sanalipange kuti likhale lopanda kanthu, koma analipanga kuti anthu akhalemo. Iyeyu akunena kuti: Ine ndine Yehova, ndipo palibenso wina.
19 Na da wamowane hame sia: i. Amola Na hanai hame wamolegei. Na da Isala: ili dunu ilia gugunufinisi soge amo ganodini Na hogomu, hame sia: i. Na da Hina Gode amola Na sia: da dafawane. Na da moloidafa hou olelesa.
Ine sindinayankhule mwachinsinsi, pamalo ena a mdima; Ine sindinaziwuze zidzukulu za Yakobo kuti, “Ndifunefuneni ku malo kopanda kanthu.” Ine Yehova, ndimayankhula zoona; ndikunena zolungama.
20 Hina Gode da amane sia: sa, “Dilia fifi asi gala huluane! Gilisima! Nowa da Ba: bilone ea dafai mae bogole esala. Dilia fofada: musa: misa! Dunu ilia da ifaga hamoi ‘gode’ liligi gaguli, mogodigili ahoa amola amo ‘gode’ liligi ilima sia: ne gadosa, amo dunu ilia asigi dawa: su da hamedeidafa.
Yehova akuti, “Sonkhanani pamodzi ndipo mubwere; yandikirani, inu amene munapulumuka pothawa nkhondo kwa anthu a mitundu ina. Ndinu opanda nzeru amene mumanyamula mafano a mitengo, amene mumapemphera kwa milungu imene singathe kupulumutsa.
21 Dilia sia: sia: musa: fofada: su diasuga misa. Dilia da Nama fofada: sea, dunu enoenoi gilisili sia: sa: ima. Nowa da musa: hemonega hobea misunu hou amo dawa: beba: le, olelebela: ? Na, Ni fawane, Hina Gode Ea fi Gaga: su dunu, da amo hou ba: la: lusu.
Fotokozani mlandu wanu, mupatsane nzeru nonse pamodzi. Kodi ndani ananeneratu zimenezi kalekale? Ndani anazifotokozeratu zimenezi nthawi yamakedzana? Kodi si Ineyo Yehova? Ndipo palibenso Mulungu wina kupatula Ine, Mulungu wolungama ndi Wopulumutsa, palibenso wina kupatula Ine.
22 Osobo bagade fifi asi gala dunu huluane! Nama sinidigima! Amasea, dilia Na Gaga: su ba: mu. Ni fawane da Godedafa, eno hame.
“Tembenukirani kwa Ine kuti mupulumuke, inu anthu onse a pa dziko lapansi, pakuti Ine ndine Mulungu ndipo palibenso wina.
23 Na ilegei sia: da dafawane, amola Na da amo afedenemu hame dawa: Na da Na hou huluane amoga Na ilegei sia: i defele hamoma: ne sia: sa. Dunu huluanedafa da Nama misini, muguni bugili, Na mae yolesima: ne ilia da sia: mu.
Ndalumbira ndekha, pakamwa panga patulutsa mawu owona, mawu amene sadzasinthika konse akuti, bondo lililonse lidzagwada pamaso panga; anthu onse adzalumbira potchula dzina langa.
24 Na hamobeba: le fawane, hasalasu hou amola gasa bagade hou da ba: mu, amo ilia da sia: mu. Be huluane da Na higasea da gogosiamu.
Iwo adzanene kwa Ine kuti, ‘Chilungamo ndi mphamvu zimapezeka mwa Yehova yekha.’” Onse amene anamuwukira Iye adzabwera kwa Iye ndipo adzachita manyazi.
25 Na, Hina Gode, da Ya: igobe egaga fi huluane gaga: mu. Amasea, ilia da Nama nodosu imunu.”
Koma mwa Yehova zidzukulu zonse za Israeli zidzapambana ndi kupeza ulemerero.

< Aisaia 45 >