< Aisaia 41 >

1 Gode da amane sia: sa, “Dilia sedaga soge fi! Ouiya: ma! Na sia: nabima! Dilia fofada: su diasu ganodini sia: ma: ne, dilia fofada: su sia: momagema. Dilia da bu sia: mu logo ba: mu. Dilia amola Na da moloidafa hou dawa: ma: ne, fofada: mu da defea.
“Khalani chete pamaso panga, inu mayiko a mʼmbali mwa nyanja! Alekeni ayandikire ndi kuyankhula; tiyeni tikhale pamodzi kuti atiweruze.
2 Nowa da gusugoe amoga hasalasu dunu oule misibela: ? Nowa da soge huluane e da asi amoga ema hasalasu hou iabela: ? E da hina bagade amola fifi asi gala ilima hasanasima: ne, nowa da ema hasalasu hou iabela: ? Ea gobihei amoga e da fifi asi gala dunu osobo su defele wadela: sa. Ea dadi amoga gala: beba: le, ilia da gisi da foga afafasu defele afafasa.
“Ndani anadzutsa wochokera kummawa uja amene ananka napambana kulikonse kumene ankapita? Iye amapereka anthu a mitundu ina mʼmanja mwake ndipo ndi lupanga lake anagonjetsa ndi kusandutsa mafumu kukhala ngati fumbi nawamwaza ngati mankhusu ndi uta wake.
3 E da ilia hobeasu amoma fa: no bobogesa amola mogodigili ahoa. E da hehenabeba: le, gadenenewane hagili ahoa.
Amawalondola namayenda mosavutika, mʼnjira imene mapazi ake sanayendemo kale.
4 Nowa da amo hou misa: ne hamobela: ? Nowa da osobo bagade hou huluane ouligibala: ? Na, Hina Gode, da osobo bagade hemosu eso amoga esalebe ba: i, amola Na, Hina Gode da osobo bagade wadela: mu eso amoga esalebe ba: mu.
Ndani anachita zimenezi ndi kuzitsiriza, si uja amene anayambitsa mitundu ya anthu? Ine Yehova, ndine chiyambi ndipo potsiriza pake ndidzakhalapo.”
5 Soge sedaga fi dunu da Na hamobe ba: beba: le, bagadewane beda: beba: le, yagugusa. Amaiba: le, ilia huluane da gilisili, maha.
Mayiko amʼmbali mwa nyanja aona zimenezi ndipo akuopa; anthu a ku mathero a dziko lapansi akunjenjemera. Akuyandikira pafupi, akubwera;
6 Liligi hahamosu dunu ilia enoenoi fidisa amola dogo denesisa.
aliyense akuthandiza mnzake ndipo akuwuza mʼbale wake kuti, “Limba mtima!”
7 Ifa hahamosu dunu da gouli hahamosu dunuma, “Dia da noga: le hamoi,” sia: sa. Dunu amo da ‘gode’ agoaila enemema: ne hamosu da dunu amo da ‘gode’ agoaila gafesiga dabagala: sa amoma dogo denesima: ne sia: sa. Ilia da amane sia: sa, “Gouli madelagisu da defea.” Amasea, ilia da amo loboga hamoi ‘gode’ ea sogebi dialoma: ne, amo gafesiga dabagala: sa.
Mʼmisiri wa matabwa amalimbikitsa mʼmisiri wa golide, ndipo iye amene amasalaza fano ndi nyundo amalimbikitsa amene amalisanja pa chipala. Ponena za kuwotcherera iye amati, “Zili bwino.” Iye amalikhomerera fanolo ndi misomali kuti lisagwe.
8 Be di, Isala: ili, Na hawa: hamosu dunu. Dilia da Na fi dunu Na da ilegei dagoi. Dilia da Na dogolegei A: ibalaha: me, amo egaga fi esala.
“Koma Iwe Israeli mtumiki wanga, Yakobo amene ndakusankha, Ndiwe chidzukulu cha Abrahamu bwenzi langa.
9 Na da dili osobo bagade bega: bega: amoga dilima wele sia: nanu, oule misini, gilisi. Na da dilima amane sia: i, “Dilia da Na hawa: hamosu dunu. Na da dili hame higasu, be dili Na fi hamoma: ne ilegei dagoi.
Ndinakutengani kuchokera ku mapeto a dziko lapansi, ndinakuyitanani kuchokera ku mbali za kutali za dziko lapansi. Ine ndinati, ‘Iwe ndiwe mtumiki wanga;’ Ndinakusankha ndipo sindinakutaye.
10 Mae beda: ma! Ani esala. Na da dilia Gode! Liligi huluane amoma mae beda: ma. Na da dilima gasa imunu amola dili fidimu. Na da dili gaga: mu.
Tsono usaope, pakuti Ine ndili nawe; usataye mtima chifukwa Ine ndine Mulungu wako. Ndidzakupatsa mphamvu ndipo ndidzakuthandiza, ndidzakutchinjiriza ndi dzanja langa lamanja logonjetsa.
11 Dilia da nowa da dilima ougi galea, ilima hasanasibiba: le, ilia da gogosiamu. Nowa da dilima gegesea da bogole,
“Onse amene akupsera mtima adzachita manyazi ndithu ndi kunyazitsidwa; onse amene akukangana nawe sadzakhalanso kanthu, adzawonongeka.
12 osobo bagadega bu hame ba: ma: ne alalolesimu.
Udzafunafuna adani ako, koma sadzapezeka. Iwo amene akuchita nawe nkhondo sadzakhalanso kanthu.
13 Na da Hina Gode amo dilia Gode. Na da dilima gasa iaha amola dilima amane sia: sa, “Mae beda: ma! Na da dili fidimu.”
Pakuti Ine Yehova, ndine Mulungu wako, amene ndikukugwira dzanja lako lamanja ndipo ndikuti, usaope; ndidzakuthandiza.
14 Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili fi! Dilia da fonobahadi fi amola gasa hame galebe. Be mae beda: ma! Na da dili fidimu. Na, Isala: ili fi ilia Hadigi Gode, Na da dilia gaga: su dunu esala.
Usachite mantha, iwe Yakobo wofowoka ngati nyongolotsi, iwe wochepa mphamvu Israeli, chifukwa Ine ndidzakuthandiza,” akutero Yehova Mpulumutsi wako, Woyerayo wa Israeli.
15 Na da dilia hou afadenene, widi fasu ifa agoane hamomu. Amoga sosu liligi gaheabolo amola agei dagoi agoane ba: mu. Amoga dilia da goumi amo fananu, wadela: lesimu. Dilia da agolo goudane, ilia da osobo su agoane ba: mu.
“Taona, ndidzakusandutsa ngati chipangizo chopunthira tirigu chatsopano, chakunthwa ndi cha mano ambiri. Udzanyenya mapiri ndi kuwaphwanyaphwanya, ndipo zitunda adzazisandutsa ngati mankhusu.
16 Dilia da amo goumi gadodi gasa: le gadosea, ilia da foga mini asi dagoi ba: mu, amola isula bobodobe amoga afafai dagoi ba: mu. Amasea, dilia da hahawane ba: mu. Bai Na da dilia Gode esala. Dilia da Na, Isala: ili fi ilia Hadigi Gode, Nama nodomu.
Udzawapeta ndipo adzawuluka ndi mphepo komanso adzamwazika ndi kamvuluvulu. Koma iwe udzakondwera chifukwa Ine ndine Mulungu wako, ndipo udzanyadira chifukwa cha Ine Woyerayo wa Israeli:
17 Na fi dunu da hano hanaiba: le, hano hogosea, ilia asogoa da hafoga: i galea, Na, Hina Gode da ilia sia: ne gadosu amoma bu adole imunu. Na, Isala: ili fi ilia Gode, da ili hamedafa yolesimu.
“Pamene amphawi ndi osauka akufunafuna madzi, koma sakuwapeza; ndipo kummero kwawo kwawuma ndi ludzu. Ine Yehova ndidzayankha pemphero lawo; Ine, Mulungu wa Israeli, sindidzawasiya.
18 Na da hafog: ai agolo sogega, hano yogosa: ima: ne hamomu. Amola hafoga: i soge ganodini, gu hano hamomu. Na da hafoga: i soge afadenene, bu hano wayabo hamomu. Amola hafoga: i soge gu hano bubuga: su hamomu.
Ndidzayendetsa mitsinje mʼmalo owuma, ndi akasupe adzatumphuka mu zigwa. Ndidzasandutsa chipululu kukhala dziwe la madzi ndipo dziko lowuma kukhala akasupe a madzi.
19 Dolo ifa amola “aga: isia” ifa amola “medili” ifa da hafoga: i soge ganodini heda: lalebe ba: mu. “Baine” ifa amola “yuniba” ifa amola “saibalase” ifa da hafoga: i sogega heda: mu.
Mʼchipululu ndidzameretsa mkungudza, kasiya mchisu ndi mtengo wa Olivi. Mʼdziko lowuma ndidzaza mitengo ya payini, ya mkuyu ndi ya mlombwa,
20 Dunu da amo hou ba: beba: le, ilia da Na, Hina Gode, da amo hou hamoi dagoi, dawa: mu. Ilia da Isala: ili fi ilia Hadigi Gode da amo hou hamoi dagoi ba: mu.” Hina Gode da Ogogosu ‘gode’ liligi ilima Fofada: sa
kuti anthu aone ndi kudziwa; inde, alingalire ndi kumvetsa, kuti Yehova ndiye wachita zimenezi; kuti Woyera wa Israeli ndiye anakonza zimenezi.
21 Hina Gode, Isala: ili ilia Hina bagade, da amane sia: sa, “Dilia fifi asi gala ‘gode’ liligi! Dilia hou gaga: ma: ne Nama fofada: ma! Sia: gasa bagade dilia hou gaga: ma: ne fofada: ma!
“Yehova akuwuza milungu ina kuti, ‘Fotokozani mlandu wanu.’ Mfumu ya Yakobo ikuti, ‘Perekani umboni wanu.’
22 Misa! Amola hobea misunu hou ba: la: loma! Amo dilia sia: i liligi da doaga: sea, amo ea bai ninia dawa: ma: ne, ninima olelema. Musa: hamoi liligi amo fofada: su dunuma olelema amola amo ea dawa: loma: ne ninima olelema.
Bwerani ndi milungu yanu kuti idzatiwuze zomwe zidzachitike mʼtsogolo. Tifotokozereni zinthu zamakedzana tiziganizire ndi kudziwa zotsatira zake. Kapena tiwuzeni zimene zidzachitike mʼtsogolo,
23 Hobea misunu hou ninima olelema. Amasea, dilia da dafawane ‘gode’ esala, amo ninia da dawa: mu. Hou noga: iwane hamoma o ninia baligiliwane beda: ma: ne, wadela: lesisu liligi afae hamoma!
tiwuzeni kuti kutsogolo kuli zotani, ndipo ife tidziwa kuti ndinu milungu. Chitani chinthu chabwino kapena choyipa, ndipo mutidabwitsa ndi kutichititsa mantha.
24 Dili amola dilia hamonana huluane da hamedei liligi. Dunu amo da dilima nodone sia: ne gadosa, amo da gogosiasu wadela: idafa.
Koma inu sindinu kanthu ndipo zochita zanu nʼzopandapake; amene amapembedza inu ali ngati chinthu chokanidwa chifukwa ndi choyipa.
25 Na da dunu amo da gusugoe esala, amo e ilegei dagoi. E da gagoe (north) amoga doagala: musa: misunu. E da ouligisu dunu amo ososa: gisa. Ilia da fafu agoai ba: sa, amola e da osoboga ofodo hamosu dunu Amo da fafu ososa: gisa agoane ba: sa.
“Ndinawutsa munthu wina kumpoto ndipo anabwera, munthu wochokera kummawa amene ndinamuyitana. Amapondaponda olamulira ngati matope, ngati ndi wowumba mbiya amene akuponda dongo.
26 Amo hou da doaga: ma: ne, dilia gilisisu ganodini, da nowa ba: la: lobala: ? Dilia da amo sia: sia: noba, ninia da dilia da dafawane sia: i dawa: la: loba. Be dilia huluane da hamedafa sia: i. Dunu afae da dilia amane sia: i, hamedafa nabi.
Ndani anawululiratu zimenezi poyamba pomwe, kuti ife tidziwe, kapena kutiwuziratu zisanachitike kuti ife tinene kuti, ‘Analondola?’ Palibe amene ananena, palibe analengeza zimenezi, palibe anamva mawu anu.
27 Na, Hina Gode, da hidadea Saione fi ilima amo sia: olelei. Na da sia: ne iasu dunu Yelusaleme dunu fi hahawane sia: adoma: ne asunasi. Na da ilima amane adole iasi, ‘Dilia fi da ilia sogedafa amoga bu manebe.’
Ine ndinali woyamba kumuwuza Ziyoni kuti, ‘Taona, si awa akubwera apawa!’ Ndinatumiza mthenga wa nkhani yabwino ku Yerusalemu.
28 Be Na da ogogosu ‘gode’ liligi amo ganodini hogoi helebeba: le, moloi sia: su hamedafa ba: i. Ilia da Na adole ba: su amoma bu adole imunu gogolei galu.
Koma ndikayangʼana palibe ndi mmodzi yemwe, palibe ndi mmodzi yemwe pakati pawo wotha kupereka uphungu, palibe woti ayankhe pamene ine ndawafunsa.
29 Amo ‘gode’ liligi da hamedeidafa. Ilia da hawa: hamomu gogolesa. Ilia da gasa hamedafa.”
Taonani, milungu yonseyi ndi yachinyengo! Zochita zawo si kanthu konse; mafano awo ali ngati mphepo yachabechabe.

< Aisaia 41 >