< Aisaia 4 >

1 Amo esoga uda fesuale da dunu afadafa gagulaligili, ema amane sia: mu, “Ninisu da ninia ha: i manu amola ninia abula lamu. Be ninia da gawa hame fiba: le, gogosiasa: besa: le, di ninia gawa esaloma.”
Tsiku limenelo akazi asanu ndi awiri adzagwira mwamuna mmodzi, nʼkunena kuti, “Ife tizidya chakudya chathuchathu, ndi kuvala zovala zathu; inu mungotilola kuti tidziyitanidwa ndi dzina lanu. Tichotseni manyazi aumbeta!”
2 Amo esoga, Hina Gode Ea Amoda da ida: iwane amola hadigiwane ba: mu. Amola Isala: ili dunu hame bogole esalea da soge ea ha: i manu gami amo hahawane bagade ba: mu.
Tsiku limenelo Nthambi ya Yehova idzakhala yokongola ndi yaulemerero, ndipo chipatso cha mʼdziko chidzakhala chonyaditsa ndi chopereka ulemerero kwa onse opulumuka mu Israeli.
3 Dunu huluane amo Gode da mae bogoma: ne ilegei, Yelusaleme amo ganodini esala, ilia da hadigiwane hamoi dagoi ba: mu.
Iwo amene adzatsale mu Ziyoni, amene adzatsalire mu Yerusalemu, adzatchedwa oyera, onse amene mayina awo alembedwa pakati pa anthu amoyo okhala mu Yerusalemu.
4 Hina Gode da Ea gasa amoga Isala: ili dunu fi ilima fofada: nanu, ilia wadela: i hou dodofemu amola Yelusaleme fi ilia gogosia: i fadegale, maga: me huluane amo moilai bai bagade ganodini asi, amo huluane dodofemu.
Ambuye adzasambitsa akazi a Ziyoni ndi kuchotsa zonyansa zawo. Adzatsuka magazi amene anakhetsedwa mu Yerusalemu ndi mzimu wachiweruzo ndiponso mzimu wamoto.
5 Amasea, Hina Gode da Saione Goumi amola dunu da amogawi gilisi, amo dedeboma: ne esomogoa mu mobi hahamomu amola gasia lalu mobi amola lalu sawa: hadigi bagade ba: mu. Gode Ea Hadigi da moilai bai bagadega dedebosu gaga: su liligi agoane ba: mu.
Tsono Yehova adzayika mtambo wake pamwamba ponse pa phiri la Ziyoni, ndipo pa onse amene asonkhana masana padzakhala mtambo wa utsi ndipo usiku padzakhala malawi amoto. Pamwamba pa zonse padzakhala ulemerero wa Yehova.
6 Hina Gode Ea hadigi da esosea gia: i amoga ougi noga: iwane hahamomu. Moilai bai bagade da gaga: i dagoi ba: mu, amola gibu amola isu amoga gagili sali dagoi ba: mu.
Ulemerero wake udzakhala mthunzi wothawiramo kutentha kwa masana, udzakhala malo opeweramo mphepo ndi owusiramo mvula.

< Aisaia 4 >