< Aisaia 25 >
1 Hina Gode! Di da na Gode! Na da dima nodone dawa: mu amola Dia Dio amoma nodone sia: ne gadomu. Di da fofogadigisu hou hamoi dagoi. Amola mae giadofale, Dia hemonega hamomu ilegei amo Dia hamoi dagoi.
Yehova ndinu Mulungu wanga; ine ndidzakukwezani ndi kutamanda dzina lanu, pakuti mwachita zodabwitsa zimene munakonzekeratu kalekale mokhulupirika kwambiri.
2 Di da moilai bai bagade bagohame mugululi, amola ilia gaga: su gagoi wadela: lesi dagoi. Ninia ha lai hina bagade ilia diasu gagui, amo da wadela: lesi dagole, bu hamedafa ba: mu.
Inu mwasandutsa mzinda uja kukhala mulu wamiyala. Ndipo mzinda wamalinga wasanduka bwinja, linga la anthu achilendo lero si mzindanso ndipo sidzamangidwanso.
3 Dunu amo da gasa bagade fifi asi gala ganodini esala da Dima nodomu. Nimi bagade hame asigi fifi asi gala ilia moilai bai bagade amo ganodini, ilia da Diba: le bagade beda: mu.
Nʼchifukwa chake anthu amphamvu adzakulemekezani; mizinda ya mitundu ya anthu ankhanza idzakuopani.
4 Hame gagui amola gasa hame hahani dunu da bidi hamosu eso amoga, Dima hobeale, gaga: su noga: i ba: su. Isu bagade manoba, Di da ili gaga: sa. Amola eso bagade gia: sea, Dia da ilima ougi olelesa. Hame asigi nimi bagade dunu da anegagi eso isu mabe agoane eno dunu doagala: sa.
Inu mwakhala ngati populumukira pa anthu osauka, mwakhala ngati kobisalirako munthu wovutika pa nthawi ya masautso ake. Mwakhala ngati pobisalirapo pa nthawi ya mphepo yamkuntho ndi mthunzi pa nthawi ya dzuwa. Pakuti anthu ankhanza ali ngati mphepo yamkuntho yowomba pa khoma,
5 Amola ilia da esoi bagade agoane doagala: sa. Be Di, Hina Gode, da ninia ha lai dunu ouiya: lesi dagoi. Mu mobi da eso gia: i anegagisa, amo defele Di da hame asigi nimi bagade dunu ilia halasu ouiya: ma: ne hedofasa.
ndiponso ngati kutentha mʼdziko lowuma. Inu mumaletsa phokoso la anthu achilendo. Monga momwe mthunzi wa mtambo umachepetsa kutentha, inu munaletsa nyimbo za anthu ankhanza.
6 Guiguda: , Saione Goumiga, Hina Gode Bagadedafa da osobo bagade fifi asi gala huluane misa: ne, Lolo Nabe hahamomu. Amoga, ilia da ha: i manu noga: idafa amola waini hano ida: iwane gala manu.
Pa phiri ili Yehova Wamphamvuzonse adzakonzera anthu a mitundu yonse madyerero a zakudya zokoma ndi vinyo wabwino. Phwando la nyama yonona ndi vinyo wabwino kwambiri.
7 Guiguda: , E da hedolowane da: i dioi amo da fifi asi gala huluane mu mobi agoane dedebosa, amo fadegale fasimu.
Iye adzachotsa kulira kumene kwaphimba anthu ngati nsalu. Adzachotsa chinsalu chimene chakuta mitundu yonse ya anthu.
8 Ouligisudafa Hina Gode da bogosu hou amo bu mae ba: ma: ne gugunufinisimu. E da dunu huluane ilia disu si hano doga: mu. Ea fi dunu da osobo bagadega fifi asi gala huluane ganodini, gogosiane se nabasu amo nabaha. Be Hina Gode da amo gogosiasu fadegale fasimu. Hina Gode Hisu da sia: i dagoi.
Yehova adzathetsa imfa mpaka muyaya, Ambuye Yehova adzapukuta misozi mʼmaso mwa munthu aliyense; adzachotsa manyazi a anthu ake pa dziko lonse lapansi, Yehova wayankhula.
9 Amo hou doaga: sea, dunu huluane da amane sia: mu, “E da ninia Gode! Ninia da Ea hou dafawaneyale dawa: beba: le amola lalegaguiba: le, E da nini gaga: i dagoi. E da Hina Godedafa! Ninia da Ea hou lalegagui dagoi. Amaiba: le, ninia da wali hahawane bagade. Bai E da nini gaga: i dagoi.”
Tsiku limenelo iwo adzati, “Ndithudi, uyu ndiye Mulungu wathu; ife tinamudalira ndipo anatipulumutsa. Uyu ndiye Yehova, ife tinamudalira; tiyeni tikondwe ndi kusangalala chifukwa watipulumutsa.”
10 Hina Gode da Saione Goumi fi amo gaga: mu. Be Moua: be fi da gisi bulamagau iga amo ganodini osa: gili banenesi dagoi ba: sa, amo defele ilia da osa: gili, banenesi dagoi ba: mu.
Yehova adzateteza phiri limeneli ndi dzanja lake; ndipo Amowabu adzawapondereza pomwe alilipo, ngati mmene amapondera manyowa mʼdzenje.
11 Ilia da dasi sa: imusa: defele ilia lobo ilua: mu, be Gode da ili gogosiama: ne banenesimu, amola ilia lobo da gasa hameba: le, gasi gudumu.
Amowabuwo adzatambasula manja awo mʼmenemo, ngati mmene amachitira munthu wosambira. Koma Mulungu adzathetsa kunyada kwawo ngakhale luso la manja awo.
12 Moua: be fi da ilia gaga: su gagoi sedadewane gagula heda: i. Be amo huluane, Gode da mugululi wadela: lesili, ilia sa: ili osobo su amoga doaga: mu.
Iye adzagumula malinga awo ataliatali ndipo adzawagwetsa ndi kuwaponya pansi, pa fumbi penipeni.