< Aisaia 10 >
1 Dilia da se iasu bagade ba: mu! Dilia da Na fi dunu se nabima: ne, sema moloihame hamonana.
Tsoka kwa anthu amene amapanga malamulo opanda chilungamo, kwa iwo amene amalemba zongovutitsa anzawo,
2 Amoga, hame gagui dunu ilia hou moloidafa hame ba: sa. Amo sema moloihame hamobeba: le, dilia da didalo amola guluba: mano ilia soge amola liligi wamolaha.
kuwalanda anthu osauka ufulu wawo ndi kumana chilungamo osautsidwa pakati pa anthu anga, amalanda zinthu za akazi amasiye ndi kubera ana amasiye.
3 Gode da dilima se iasea, dilia da adi hamoma: bela: ? Gode da dili wadela: musa: , sedaga esala ga fi oule masea, dilia da adi hamoma: bela: ? Dilia da eno dunu dili fidima: ne, habidili hobeama: bela: ? Dilia muni amola noga: i liligi, habodili wamolegema: bela: ?
Kodi mudzatani pa tsiku la chilango, pofika chiwonongeko chochokera kutali? Kodi mudzathawira kwa yani kuti akuthandizeni? Nanga chuma chanu mudzachisiya kuti?
4 Dilia da gegesu ganodini fane legei dagoi ba: mu. Mogili, dilia da enoga afugili, se iasu diasuga hawa: hamoma: ne mugululi asi dagoi ba: mu. Be amo hamonanu, Hina Gode Ea ougi da hame gumi ba: mu. E da se eno ima: ne, Ea lobo ililua: le lelebe ba: mu.
Kudzatsala nʼkungozolika mwamanyazi pakati pa anthu ogwidwa kapena kufa pamodzi ndi ophedwa. Komabe pa zonsezi mkwiyo wake sunawachokere, mkono wake uli chitambasulire.
5 Hina Gode da amane sia: i, “Na da Asilia hina bagade amo dunu amoma Na da ougi gala ilima se ima: ne, Na da Asilia hina bagade ogoma agoane hamoi.
“Tsoka kwa mfumu ya ku Asiriya, chikwapu cha mkwiyo wanga, iye ndiye ndodo ya mkwiyo wanga!
6 Na da Asilia dunu amo dunu fi da Na fisibiba: le amoma Na da ougi gala, ilima doagala: musa: asunasi. Ilia da amo dunu ilia liligi wamolale, amola ilima osobo agoane osa: gili, hasanasima: ne, Na da Asilia dunu amo asunasi dagoi.
Ndidzamutuma kukalimbana ndi mtundu wosapembedza Mulungu, ndidzamutumiza kukalimbana ndi anthu amene amandikwiyitsa Ine, kukafunkha ndi kulanda chuma, ndi kuwapondereza pansi ngati matope a mʼmisewu.
7 Be Asilia hina bagade, e da hi nimi bagade hi hanai hou hamomusa: dawa: lala. E da dunu fifi asi gala bagohame wadela: musa: dawa: lala.
Koma izi si zimene akufuna kukachita, izi si zimene zili mʼmaganizo mwake; cholinga chake ndi kukawononga, kukapulula mitundu yambiri ya anthu.
8 E da gasa fili agoane sia: sa “Na dadi gagui ouligisu dunu afae afae huluane da hina bagade gala.
Iye akuti, ‘Kodi atsogoleri anga ankhondo si mafumu okhaokha?’
9 Na da Ga: lanou, Gagimisi, Ha: ima: de, Aba: de, Samelia amola Dama: sagase, amo moilai bai bagade huluane hasali dagoi.
‘Kodi Kalino sanagonjetsedwe monga Karikemesi? Kodi Hamati sali ngati Aripadi, nanga Samariya sali ngati Damasiko?
10 Na da fifi asi gala amo da loboga hamoi ‘gode’ ilima sia: ne gadosa, (ilia loboga hamoi liligi idi da Yelusaleme amola Samelia ilia ‘gode’ hamoi liligi idi baligisa) ilima se ima: ne, na da doagala: i.
Dzanja langa linakantha maufumu a anthu opembedza mafano, mafumu amene mafano awo ndi aakulu kupambana Yerusalemu ndi Samariya;
11 Na da Samelia dunu fi amola ilia loboga hamoi ‘gode’ amo wadela: lesi dagoi. Amola na da Yelusaleme amola, ilia loboga hamoi liligi amoma ilia sia: ne gadosa, amo defele gugunufinisimu.”
nanga Ine nʼkulephera kodi kuwononga Yerusalemu pamodzi ndi mafano ake monga ndinakanthira Samariya pamodzi ndi mafano ake?’”
12 Be Hina Gode da amane sia: sa, “Na da wali hamobe Saione Goumi amola Yelusaleme amo ganodini amo dagosea, Na da Asilia hina bagade ema se bidi imunu. Bai e da hidale gasa fi bagade hamosa.”
Ambuye akadzamaliza ntchito yonse yolanga phiri la Ziyoni ndi Yerusalemu adzalanganso mfumu ya ku Asiriya chifukwa cha kudzitama ndi kunyada kwake.
13 Asilia hina bagade da hidale agoane sia: sa, “Na nisu agoane hamoi. Na da gasa bagade amola bagade dawa: su. Na da fifi asi gala ilia alalo legesu mugululi, ilia ha: i manu amola liligi legesu amo lai dagoi. Na da bulamagau gawali defele, dunu amogawi esalu amoga osa: gi dagoi.
Pakuti mfumuyo ikuti, “‘Ndachita zimenezi ndi dzanja langa, ndiponso ndi nzeru zanga, chifukwa ndine wozindikira zinthu. Ndinachotsa malire a mitundu ya anthu, ndinafunkha chuma chawo; ndinagonjetsa mafumu awo monga munthu wamphamvu.
14 Osobo bagade fifi asi gala da sio bibi agoane ba: i. Na da sio ea oso labe defele, asabole fifi asi gala ilia liligi huluane lai dagoi. Na beda: ma: ne, ougia afae yagugui hame ba: i. Nama gua: ma: ne, misu afae da hame dagai.”
Dzanja langa lagwira chuma cha mitundu ya anthu ngati momwe munthu amagwirira chisa cha mbalame, ngati momwe anthu amatolera mazira osiyidwa, motero inenso ndinasonkhanitsa mayiko onse; palibe mbalame imene inakupiza mapiko ake, kapena kuyasama kukamwa kuti ilire.’”
15 Be Hina Gode da amane sia: sa, “Goahei da dunu amoga hawa: hamosa, amo ea hou baligisala: ? So hedofasu da dunu amoga hawa: hamosa, amo ea hou baligisala: ? Ogoma da dunu hame gaguia gadosa. Be dunu da ogoma gaguia gadosa.”
Kodi nkhwangwa ingathe kudzikuza kupambana woyigwiritsa ntchito, kapena macheka angathe kudzikuza kupambana wowagwiritsa ntchito? Ndiye kukhala ngati kuti chikwapu chikuzunguza munthu amene wachinyamula, kapena ngati kuti ndodo ikuopseza amene wayinyamula!
16 Hina Gode Bagadedafa da dunu amo da wali sadi gala ilima se ima: ne, olo iasimu. Ilia da olo madelabeba: le, ilia da: i hodo ganodini, lalu mae ha: ba: done nenanumu.
Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova Wamphamvuzonse adzatumiza matenda owondetsa kwa ankhondo amphamvu; kunyada kwa mfumuyo kudzapsa ndi moto wosazima.
17 Gode da Isala: ili fi ilima hadigi gamali agoane. Be E da afadanene bu lalu agoane hamomu. Isala: ili ilia Hadigi Gode da lalu gona: su agoane ba: mu. Amo da eso afadafa amoga, liligi huluane amola aya: gaga: nomei amola gagalobo nei dagomu.
Mulungu, Kuwala kwa Israeli, adzakhala ngati moto, Woyera uja wa Israeli adzakhala ngati malawi a moto. Motowo udzawatentha ndi kuwapsereza ngati minga ndi mkandankhuku pa tsiku limodzi.
18 Iwila ida: iwane gala amola ifabi nasegagi amola da bogosu olo da dunu wadela: sa defele, amo wadela: lesi dagoi ba: mu.
Ankhondo ake adzawonongedwa ngati nkhalango yayikulu ndi ngati nthaka yachonde.
19 Isala: ili sogega da ifa bagahame dialebeba: le, mano fonobahadi ilia idimu da defele ba: mu.
Mitengo yotsalira ya mʼnkhalango zake idzakhala yochepa kwambiri, yoti ndi mwana yemwe ndi kuyiwerenga.
20 Eso da misunu, amoga Isala: ili dunu amo da mae bogole esala, ilia da dunu fi da ilia fi wadela: lesi, ilima hame fa: no bobogemu. Be ilia da Hina Gode, Isala: ili fi ilia Hadigi Gode, amo Ea hou dafawaneyale dawa: beba: le, lalegagumu.
Tsiku limenelo otsalira a ku Israeli, opulumuka a nyumba ya Yakobo, sadzadaliranso anthu amene anawakantha, koma adzadalira Yehova, Woyerayo wa Israeli.
21 Isala: ili dunu mogili bagahame da ilia Gode Bagadedafa Ema sinidigimu.
Otsalira adzabwerera, otsalira a Yakobo adzabwerera kwa Mulungu Wamphamvu.
22 Wali Isala: ili dunu ilia idi da hano wayabo bagade bega: sa: iboso dialebe, amo ea idi defele ba: sa. Be dunu bagahame fawane da buhagimu. Isala: ili dunu fi da wadela: lesi dagoi ba: mu. Amola ilia da amo dabe ba: mu da defeadafa.
Iwe Israeli, ngakhale anthu ako achuluke ngati mchenga wa ku nyanja, otsala okha ndiwo adzabwerere. Chiwonongeko chalamulidwa, chidzaonetsa chilungamo chosefukira.
23 Dafawane! Ouligisudafa Hina Gode Bagadedafa da Ea sia: i defele soge huluane amo ganodini, gugunufinisisu fawane iasimu.
Ambuye Yehova Wamphamvuzonse adzawononga ndithu dziko lonse monga momwe analamulira.
24 Ouligisudafa Hina Gode Bagadedafa da Ea dunu ilia Saione Goumi amoga esala, ilima amane sia: sa, “Asilia dunu da Idibidi dunu defele, dilima se imunu. Be iliba: le mae beda: ma.
Nʼchifukwa chake, Ambuye Yehova Wamphamvuzonse akunena kuti, “Inu anthu anga okhala mu Ziyoni, musawaope Asiriya, amene amakukanthani ndi ndodo nakumenyani ndi zibonga monga mmene Igupto anachitira.
25 Na da eso bagahame fawane dilima se ianu, dagomu. Amasea, Na da Asilia dunu gugunufinisimu.
Patsala pangʼonongʼono kuti mkwiyo wanga uchoke pa inu ndipo ndidzaonetsa ukali wanga pa iwo mpaka kuwawononga.”
26 Na, Hina Gode Bagadedafa, da Na fegasuga Midia: ne dunu Oulebe Igi sogega fasu. Amo defele Na da Asilia dunu Na fegasuga famu. Na da Idibidi fi dunu ilima se iasu amo defele, Na da Asilia dunuma se bidi imunu.
Yehova Wamphamvuzonse adzawakwapula ndi chikwapu, monga momwe anakwapulira Amidiyani ku thanthwe la Orebu; ndipo adzatukula ndodo yake pa madzi ndikuwalanga monga analangira Igupto pa nyanja.
27 Amo esoga, Na da Asilia ilia gasa bagade hou amo da wali dilima hasanasisa, amo Na da gugunufinisimu. Ilia dioi bagade “youge” da fa: no dilia gidagi bu hame banenesimu.”
Tsiku limenelo katundu wawo adzachotsedwa pa mapewa anu, goli lawo lidzachoka mʼkhosi mwanu; golilo lidzathyoka chifukwa cha kunenepa kwambiri.
28 Isala: ili dunu ilia ha lai da A: iai moilai bai bagade suguli lai dagoi. Ilia da Migalone moilai golili sa: ili baligi dagoi. Ilia momagei liligi ilia da Migema: se moilaiga legele yolesi.
Adani alowa mu Ayati apyola ku Migironi; asunga katundu wawo ku Mikimasi.
29 Ilia da goumi logo holei goulosu amo baligili, wali gasia Giba moilai bai bagadega diaha. Lama moilai fi dunu da bagadewane beda: be amola hina bagade Solo ea moilai (Gibia) amo ea fi dunu huluane da hobea: i dagoi.
Adutsa pa mpata uja, ndipo akuti, “Tikagona ku Geba” Rama akunjenjemera; Gibeya, mzinda wa Saulo ukuthawa.
30 Ga: limi moilai dunu! Wema mabu! La: isia moilai bai bagade dunu! Nabima! A: nadode moilai dunu! Bu adole ima!
Lilani mokweza, inu anthu a ku Galimu! Tchera khutu, iwe Laisa! Iwe Anatoti wosauka!
31 Ma: damina moilai dunu da hobeale asi dagoi. Gibimi moilai dunu da hobeale, wamoaligisa.
Anthu a ku Madimena akuthawa; anthu a ku Gebimu bisalani.
32 Wali eso, ninia ha lai dunu da Noube moilai bai bagadega doaga: le, ilia lobo usunawane, Saione Goumi amola Yelusaleme, amoga yagugusa.
Lero lomwe lino adaniwo adzayima ku Nobu; adzagwedeza mikono yawo, kuopseza anthu a ku Ziyoni, pa phiri la Yerusalemu.
33 Be Hina Gode Bagadedafa da dunu ilia da ifa amoda abasea, ilia osoboga gisalugala: sa, amo defele E da Asilia dunu gisalugala: mu. Gasa fi dunu gado bagade heda: i, amo huluane da hedofai dagoi ba: beba: le, gogosiasu lamu.
Taonani, Ambuye Yehova Wamphamvuzonse, adzadula mwamphamvu nthambi za mitengo, mitengo yodzikweza idzadulidwa, mitengo yayitali idzagwetsedwa.
34 Dunu ilia da iwila ifa amola ifa noga: iwane Lebanone soge ganodini gala, amo goaheiga abasu, amo defele, Hina Gode da Asilia dunu abimu.
Yehova adzadula ndi nkhwangwa mitengo ya mʼnkhalango yowirira; Lebanoni adzagwa pamaso pa Wamphamvu.