< Hosia 4 >
1 Hina Gode da Ea fi dunu Isala: ili soge ganodini esala, ilima diwaneya udidisa. Isala: ili fi! Ea sia: nabima! E da amane sia: sa, “Noga: i fa: no bobogesu hou amola asigi hou da Isala: ili soge ganodini hamedafa gala. Amola Na fi dunu da Na da Godedafa hame sia: sa.
Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova, chifukwa Yehova ali ndi mlandu ndi inu amene mumakhala mʼdzikoli: “Mʼdziko mwanu mulibe kukhulupirika, mulibe chikondi mulibe kulabadira za Mulungu.
2 Ilia da sia: dafawane ilegei amo giadofasa. Ilia da ogogosa amola fane legesa amola wamolasa amola inia uda adole laha. Wadela: i hou da bagade heda: sa amola ilia da fane legesu hou mae fisili hamonana.
Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha. Kuba ndi kuchita chigololo; machimo achita kunyanya ndipo akungokhalira kuphana.
3 Amaiba: le, ilia soge da hafoga: i hamoi dagoi ba: mu amola liligi huluane amogawi esalebe da bogogia: i dagoi ba: mu. Ohe huluane amola sio amola menabo huluanedafa da bogogia: i dagoi ba: mu.”
Chifukwa chake dziko likulira ndipo onse amene amakhalamo akuvutika; zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga ndiponso nsomba zamʼnyanja zikufa.
4 Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili dunudafa ilima mae diwaneya udidima amola gagabole mae sia: ma: ma! Na da dili gobele salasu dunu dilima fawane egane sia: sa.
“Koma wina asapeze mnzake chifukwa, wina aliyense asayimbe mlandu mnzake, pakuti anthu ako ali ngati anthu amene amayimba mlandu wansembe.
5 Esohaga amola gasia dilia da udigili gagaoui agoane hawa: hamonana amola balofede dunu da dili defele hamosa. Na da dilia ame Isala: ili amo wadela: lesimu.
Mumapunthwa usana ndi usiku ndipo aneneri amapunthwa nanu pamodzi. Choncho ndidzawononga amayi anu.
6 Na fi dunu da Nama Na da Godedafa hame sia: beba: le, ilia da wadela: lesi dagoi ba: mu. Dilia gobele salasu dunu da Nama Na da Godedafa hame sia: sa amola Na olelesu hame naba. Amaiba: le, Na da dilia gofelalia Nama gobele salasu hamoma: ne hame ilegemu.
Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa. “Pakuti mwakana kudziwa, Inenso ndidzakukanani monga ansembe anga; chifukwa mwayiwala lamulo la Mulungu wanu, Inenso ndidzayiwala ana anu.
7 Dilia gobele salasu dunu idi da heda: sea, dilia Nama wadela: i hou hamobe da amo defele heda: sa. Amaiba: le, Na da wali dunu da dilima nodosu hou hamosa amo afadenene, ilia dilima higamu, amola dilia da gogosiamu.
Ansembe ankati akachuluka iwo ankandichimwiranso kwambiri; iwo anasinthanitsa ulemerero wawo ndi chinthu china chonyansa.
8 Na fi dunu da wadela: le hamobeba: le, dilia da bagade gaguiwane ba: sa. Amaiba: le, dilia da ili baligiliwane wadela: i hou hamoma: ne, dilia da hanai.
Amalemererapo pa machimo a anthu anga ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azipitiriza kuchimwa.
9 Dilia da Isala: ili dunu ilia se nabasu defele lamu. Na da dilima se imunu. Amola dilia wadela: i hou hamobeba: le, dilima dabemu.
Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe. Ndidzawalanga onsewo chifukwa cha njira zawo, ndidzawabwezera chifukwa cha machitidwe awo.
10 Dilia da gobele salasu amoga dilia la: idi amo nanu, bu ha: i ba: mu. Dilia da mano lasu ‘gode’ ilima nodone sia: ne gadomu, be dilia da mano hame lamu. Bai dilia da Nama baligi fa: le, eno ogogosu ‘gode’ ilima fa: no bobogelala.”
“Iwo azidzadya koma sadzakhuta; azidzachita zachiwerewere koma sadzachulukana, chifukwa anasiya Yehova kuti adzipereke
11 Hina Gode da amane sia: sa, “Na fi dunu da waini hano yaolo amola gaheabolo bagade nabeba: le, gagaoui agoane hamosa.
ku zachiwerewere, ku vinyo wakale ndi watsopano, zimene zimachotsa nzeru zomvetsa zinthu
12 Ilia da udigili ifa amoga hobea misunu hou adole ba: sa. Ifa da ilia dawa: mu hanai liligi ilima adole iaha. Ilia da Na yolesi dagoi. Uda amo da hina: da: i bidi lasu defele, ilila: da: i ilia da ogogosu ‘gode’ ilima i dagoi.
za anthu anga. Anthu anga amapempha nzeru ku fano lamtengo ndipo ndodo yawo yamtengo imawayankha. Mzimu wachiwerewere umawasocheretsa; iwo sakukhulupirika kwa Mulungu wawo.
13 Ilia goumi da: iya sema sogebi amoga gobele salasu hou hamonana amola agolo da: iya ifa sedade amomodai haguduga gabusiga: manoma gobesisa. Bai amo ifa ilia ougiha: i da hisi noga: idafa. Amo hamobeba: le, didiwilali da hina: da: i bidi lasu uda agoane hawa: hamonana, amola dilia nawi ilia da inia dunu adole lasu hou hamosa.
Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri ndi kufukiza lubani pa zitunda, pa tsinde pa mtengo wa thundu, mnjale ndi mkundi, pamene pali mthunzi wabwino. Nʼchifukwa chake ana anu aakazi akuchita zachiwerewere ndipo akazi a ana anu akuchita zigololo.
14 Be amo hamobeba: le, Na da ilima se hame imunu. Bai dilisu amola da sia: ne gadosu diasu hina: da: i bidi lasu uda amola gilisili lalala amola ili gilisili, hame lalegagui dunu defele, ogogosu gobele salasu hou hamonana. Musa: malasu defele, ‘Dunu fi da asigi dawa: su hame galea, ilia da wadela: lesi dagoi ba: mu.’
“Ine sindidzalanga ana anu aakazi pamene iwo adzachita zachiwerewere, kapena akazi a ana anu pamene adzachita zigololo. Paja inu nomwe amunanu mumayenda ndi akazi achiwerewere, ndipo mumapereka nsembe pamodzi ndi akazi achiwerewere a ku malo opembedzerako. Anthu amene alibe nzeru adzawonongeka ndithu!
15 Dilia Isala: ili fi dunu da Nama baligi fa: i dagoi. Be Yuda fi dunu da amo defele hamomu da defea hame. Dilia Giliga: le o Bedele amoma nodone sia: ne gadosu hou mae hamoma. Amola amogawi, Esalalalusu Hina Gode Ea Dioba: le, dafawane ilegele sia: mae sia: ma.
“Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli, Yuda asapezeke ndi mlandu wotere. “Usapite ku Giligala. Usapite ku Beti-Aveni. Ndipo usalumbire kuti, ‘Pali Yehova wamoyo!’
16 Isala: ili dunu da ‘miule’ (dougi agoai) amo ilia gawamaga: i hou defele gala. Dunu da gisi noga: i sogega sibi mano ilima ha: i nasu iaha. Be Na da habodane amo defele, Isala: ili dunuma ha: i manudafa ima: bela: ?
Aisraeli ndi nkhutukumve, ngosamva ngati ana angʼombe. Kodi Yehova angathe kuwaweta bwanji ngati ana ankhosa pa msipu wabwino?
17 Isala: ili dunu da loboga hamoi ‘gode’ amo ilia gasaga gagulaligi dagoi. Defea! Ilisu ilia logo fodoi amoga masa: ne yolesima!
Efereimu waphathana ndi mafano; mulekeni!
18 Ilia waini hano bagade nalu, hahawane hina: da: i bidi lasu hou defele hamonana. Ilia da ilima nodosu hou mae dawa: le, gogosiasu fawane hanai gala.
Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha, amapitiriza kuchita zachiwerewere; atsogoleri awo amakonda kwambiri njira zawo zochititsa manyazi.
19 Ilia da foga mini masunu agoai ba: mu. Amola ilia da hame lalegagui ogogosu gobele salasu hou hamobeba: le, gogosiamu.”
Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zawo.