< Hosia 13 >

1 Musa: , Ifala: ime fi da sia: beba: le, Isala: ili fi eno da beda: i galu. Ilia da Ifala: ime fi ilima nodone ba: i. Be ilia da Ba: ilema nodone sia: ne gadobeba: le, wadela: le hamoi. Amo hamobeba: le, ilia da bogosu dabe lamu.
Kale Efereimu ankati akayankhula, anthu ankanjenjemera; anali wolemekezeka mu Israeli. Koma analakwa popembedza Baala, motero anafa.
2 Ilia da wadela: i hou hamonana. Ilia da loboga ogogole ouli ‘gode’ hamone, ilima nodone sia: ne gadomusa: , hamosa. Ilia silifaga ogogole ‘gode’ hamosa. Amo ilia da asigi dawa: su ganodini dawa: le, loboga hamosa. Amasea, ilia da amane sia: sa, “Amoga gobele salasu hou hamoma!” Mafua dunu da habodane udigili loboga hamoi bulamagau gawali amo nonogoma: bela: ?
Tsopano akunka nachimwirachimwirabe; akudzipangira mafano pogwiritsa ntchito siliva wawo, zifanizo zopangidwa mwaluso, zonsezo zopangidwa ndi amisiri. Amanena za anthu awa kuti, “Amatenga munthu ndi kumupereka nsembe ndipo amapsompsona fano la mwana wangʼombe.”
3 Amaiba: le, amo dunu da hahabe mobi defele hedolowane geamu. Ilia da hahabe oubi baea geabe defele, hedolo alalolesi dagoi ba: mu. Ilia da hafoga: i gisi amo dadabisu sogebiga foga mini ahoa amola mobi amo da mobi heda: suga ahoabe, agoane ba: mu.
Choncho adzakhala ngati nkhungu yammawa, ngati mame amene amakamuka msanga, ngati mungu wowuluka kuchokera pa malo opunthira tirigu, ngati utsi umene ukutulukira pa zenera.
4 Hina Gode da amane sia: sa, “Na da dilia Hina Gode! Na da dili Idibidi sogega esalu fisili masa: ne gadili asunasi. Dilia da eno Gode hame, Na fawane. Nisu da dilia Gaga: su Dunu.
Koma Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani mu Igupto. Simuyenera kudziwa Mulungu wina, koma Ine ndekha, palibe Mpulumutsi wina kupatula Ine.
5 Na da hafoga: i wadela: i soge ganodini dili ouligi.
Ndinakusamalira mʼchipululu, mʼdziko lotentha kwambiri.
6 Be dilia da soge noga: idafa amo ganodini golili sa: ili, hedolowane sadi dagoi ba: i. Amalalu, dilia da gasa fili, dilia Na gogolei.
Pamene ndinawadyetsa, iwo anakhuta; iwo atakhuta anayamba kunyada; ndipo anandiyiwala Ine.
7 Amaiba: le, Na da laione wa: me defele, dilima doagala: mu. Na da ‘lebade’ wa: me defele, dilima doagala: musa: logo legei dialumu.
Motero ndidzawalumphira ngati mkango, ndidzawabisalira mu msewu ngati kambuku.
8 Bea wa: me amo ea mano fisi defele, Na da dilima doagala: le, dilia da: i dudugale fasimu.
Ngati chimbalangondo cholandidwa ana ake, ndidzawambwandira ndi kuwathyolathyola. Ndidzawapwepweta ngati mkango; chirombo chakuthengo chidzawakhadzula.
9 Isala: ili fi dunu! Na da dili wadela: lesimu. Amasea, dili fidima: ne, nowa esalabala?
“Iwe Israeli, wawonongedwa, chifukwa ukutsutsana ndi Ine, ukutsutsana ndi mthandizi wako.
10 Dilia da hina bagade amola ouligisu dunu lama: ne adole ba: su. Be ilia da habodane dilia fi gaga: ma: bela: ?
Kodi mfumu yako ili kuti, kuti ikupulumutse? Olamulira ako a mʼmizinda yonse ali kuti, amene iwe unanena za iwo kuti, ‘Patseni mfumu ndi akalonga?’
11 Na da dilima ougiba: le, hina bagade ili dilima i. Amola Na da baligiliwane ougiba: le, amo hina bagade ili fadegai.
Choncho Ine ndinakupatsani mfumu mwachipseramtima, ndipo ndinayichotsa mwaukali.
12 Isala: ili ea wadela: i hou da dedena sa: i dagoi, amola amo dedena sa: i da noga: le momagele legei diala.
Kulakwa kwa Efereimu kwasungidwa, machimo ake alembedwa mʼbuku.
13 Isala: ili da fifi masunu gala. Be e da gagaouiba: le, fifi masunu da hamedei ba: mu. E da mano dudubu lalelegemu gadenei gala, amo da ea ame ea hagomo yolesimu hihini dialebe, amo agoaiwane gala.
Zowawa zonga za mayi pa nthawi yobala mwana zamugwera, koma iye ndi mwana wopanda nzeru, pamene nthawi yake yobadwa yafika iyeyo safuna kutuluka mʼmimba mwa amayi ake.
14 Na da amo fi dunu da bogoi soge amoga mae sa: ima: ne amola bogosu ea gasaga mae fama: ne, hamedafa gaga: mu. Bogosu! Dia olo gia: su amo oule misa! Bogoi soge! Dia wadela: su oule misa! Na da amo dunu fi ilima bu hame asigimu. (Sheol h7585)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol h7585)
15 Be Isala: ili da wadela: i gagalobo defele, hahawane heda: i dagoi ba: sa ganiaba, Na da gia: i bagade gusudili mabe fo hafoga: i sogega misi amo iasili, amo da ilia gu hano bubuga: su amola hano uli dogoi hafoga: mu. Amo fo da ilia noga: i liligi huluanedafa mini fasimu.
ngakhale Efereimu akondwe pakati pa abale ake, mphepo ya kummawa yochokera kwa Yehova idzabwera, ikuwomba kuchokera ku chipululu. Kasupe wake adzaphwa ndipo chitsime chake chidzawuma. Chuma chake chonse chamtengowapatali chidzafunkhidwa ndipo chidzatengedwa.
16 Samelia fi da Nama lelei dagoiba: le, ilia da se dabe iasu ba: ma: mu. Samelia fi dunu da gegesu ganodini bogomu. Mano dudubu da osoba gisalugala: i dagoi ba: mu. Amola abula agui uda ilia da: i da dudugai dagoi ba: mu.”
Anthu a ku Samariya adzalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo, chifukwa anawukira Mulungu wawo. Adzaphedwa ndi lupanga; ana awo adzaphedwa mowamenyetsa pansi, akazi awo oyembekezera adzatumbulidwa pa mimba.”

< Hosia 13 >