< Hosia 11 >

1 Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili ea goi hadini esoga, Na da ema asigisu. Na da e Nagofe agoane e Idibidi sogega esalu amo gadili welegai.
“Israeli ali mwana, ndinamukonda, ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto.
2 Na ema bagohame wei, be e da Nama bagohame baligi fa: i. Na dunu da Ba: ilema gobele salasu. Ilia da loboga hamoi ogogole ‘gode’ ilima gabusiga: manoma gobele salasu.
Koma ndimati ndikamapitiriza kuyitana iwo amandithawa kupita kutali. Ankapereka nsembe kwa Abaala ndipo ankafukiza lubani kwa mafano.
3 Be Na Nisu da Isala: ilima ahoasu hou olelei. Na da Na fi dunu Nima sogoba: le guda: i. Na da ili noga: le ouligi. Be ilia da Nama hame nodoi.
Ndi Ine amene ndinaphunzitsa Efereimu kuyenda, ndipo ndinawagwira pa mkono; koma iwo sanazindikire kuti ndine amene ndinawachiritsa.
4 Na da asigiliwane ili Nima hiougia guda: i. Na da youge ilia mugia galu amo fadegai amola Na da ilima ha: i manu imunusa: begudui.
Ndinawatsogolera ndi zingwe zachifundo cha anthu ndi zomangira za chikondi; ndinachotsa goli mʼkhosi mwawo ndipo ndinawerama nʼkuwadyetsa.
5 Ilia Nama sinidigimu higasa. Amaiba: le, ilia da Idibidi sogega dafawane buhagima: ma. Amola Asilia fi da ili ouligimu.
“Sadzabwerera ku Igupto, koma Asiriya ndiye adzakhala mfumu yawo pakuti akana kutembenuka.
6 Gegesu da ilia moilai ganodini doasa: ili, moilai logo ga: su da mugululi sa: imu. Na fi dunu da ilia hanaiga hamobeba: le, gegesu da ili wadela: lesimu.
Malupanga adzangʼanima mʼmizinda yawo, ndipo adzawononga mipiringidzo ya zipata zawo nadzathetseratu malingaliro awo.
7 Ilia da dafawane Nama baligi fa: lala. Youge da ilia mugi da: iya dialebeba: le, ilia da a: iya gusa: mu. Be enoga da amo youge hame gaguia gadolesimu.
Anthu anga atsimikiza zondifulatira Ine. Ngakhale atayitana Wammwambamwamba, sizidzatheka kuti Iye awakwezenso.
8 Isala: ili! Na da habodane di yolesima: bela: ? Na da habodane di fisima: bela: ? Na da A: dama moilai bai bagade amola Siboime moilai bai bagade Amo wadela: lesi dagoi. Be Na da habodane amo defele di gugunufinisima: bela: ? Na dima bagadewane asigisa. Amaiba: le, Na da di gugunufinisimu hamedei ba: sa.
“Kodi ndingakusiye bwanji iwe Efereimu? Kodi ndingakupereke bwanji iwe Israeli? Kodi ndingakuchitire bwanji zimene ndinachitira Adima? Kodi ndingathe bwanji kukuchitira zimene ndinachitira Zeboimu? Mtima wanga wakana kutero; chifundo changa chonse chikusefukira.
9 Na da dima ougili se bidi hame imunu. Na da Isala: ili bu hame wadela: lesimu. Bai Na da mafua dunu hame, Na da Gode. Na, Hadigi Gode, Na da ani esala. Na ougiliwane dima hame misunu.
Sindidzalola kuti ndikulange ndi mkwiyo wanga woopsa, kapena kutembenuka ndi kuwononga Efereimu. Pakuti Ine ndine Mulungu osati munthu, Woyerayo pakati panu. Sindidzabwera mwaukali.
10 Na da Na fi ilia ha lai dunu ilima laione wa: me agoane gogonomomu. Amasea, Na fi da Nama fa: no bobogemu. Ilia da guma: dini esalu, hedolo Nama misunu.
Iwo adzatsatira Yehova; Iye adzabangula ngati mkango. Akadzabangula, ana ake adzabwera akunjenjemera kuchokera kumadzulo.
11 Ilia da Idibidi ganini, sio agoane hedolo hagili misunu, amola Asilia ganini, ‘dafe’ sio defele hedolo hagili misunu. Na da ilia ilila: diasudafa amoga bu oule misunu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
Adzabwera akunjenjemera ngati mbalame kuchokera ku Igupto, ngati nkhunda kuchokera ku Asiriya. Ine ndidzawakhazikanso mʼnyumba zawo,” akutero Yehova.
12 Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili dunu ilia ogogosu hou da Na sisiga: sa. Na da Dafawanedafa amola Hadigi Gode. Be Yuda fi dunu da Nama lelesu hou gebewane hamonana.”
Efereimu wandizungulira ndi mabodza, nyumba ya Israeli yandizungulira ndi chinyengo. Ndipo Yuda wawukira Mulungu, wawukira ngakhale Woyerayo amene ndi wokhulupirika.

< Hosia 11 >