< Ha:ga:iai 1 >

1 Be ode ageyadu amoga, Da: liase da Besia soge amo hina bagade hamone ouligi esalu, amola oubi gafe amoga eso agega, Hina Gode da Ha: ga: iai ema sia: sia: i. Amola Ha: ga: iai da alofele, amo sia: Yuda eagene ouligisu dunu amola Selababele (Sia: lediele egefe) amola gobele salasu ouligisu dunu Yosiua (Yihosada: ge egefe), ilima bu sia: i.
Chaka chachiwiri cha Mfumu Dariyo, tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chimodzi, Yehova anapatsa mneneri Hagai uthenga wopita kwa Zerubabeli mwana wa Sealatieli, bwanamkubwa wa Yuda, ndiponso kwa mkulu wa ansembe Yoswa mwana wa Yehozadaki:
2 Hina Gode Bagadedafa da Ha: ga: iaima amane sia: i, “Isala: ili dunu ilia da amane sia: sa, ‘Debolo Diasu bu gagumu esodafa da hame doaga: i.’”
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu awa amanena kuti, ‘Nthawi sinafike yoti nʼkumanga Nyumba ya Yehova.’”
3 Amalalu, Hina Gode Ea sia: amo da dunu huluane ilia nabima: ne, balofede dunu Ha: ga: iaima sia: ne i.
Tsono Yehova anayankhula ndi mneneri Hagai kuti,
4 Hina Gode da amane sia: i, “Na dunu fi abuliba: le ilila: diasu amo noga: le gaguli esala, amola Na Sia: ne Gadosu Diasu amo bu wadela: lesi dagoi ba: sala: ?
“Kodi ino ndi nthawi yoti inuyo muzikhala mʼnyumba zomanga bwino, pamene Nyumba yangayi ikanali bwinja?”
5 Dilia da abuliba: le dilima hou doaga: ga: lalebe amo hame ba: sala: ?
Tsono zimene Yehova Wamphamvuzonse akunena ndi izi, “Ganizirani bwino njira zanu.
6 Dilia da gagoma bagade sagai galu, be amomane bagade hame fai. Dilia da ha: i manu gala be dili sadini manu defele hame gala. Dilia da waini hano manu gala, be dilia da waini hano hanai gumimu defele hame gala. Dilia da abula gala, be bagahameba: le, dilia da: i hame hougala: sa. Dunu da muni lamusa: hawa: hamosa, be amomane esaloma: ne lamu liligi amo defele hame ba: sa.
Mwadzala zambiri, koma mwakolola zochepa. Mumadya, koma simukhuta. Mumamwa, koma ludzu lanu silitha. Mumavala, koma simumva kutentha. Mumalandira malipiro, koma ndalama zanu zimatha ngati mwaziyika mʼthumba lobowoka.”
7 Di da abuliba: le, amo hou doaga: be hame ba: bela: ?
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ganizirani bwino njira zanu.
8 Defea, wahadafa agoloba: le heda: le, diasu gagusu ifa lidima, amola Na Debolo Diasu mugului amo bu buga: le gaguma. Amasea Na da dilima nodomu amola dilia da Nama defele nodone sia: ne gadomu.
Pitani ku mapiri ndipo mukatenge matabwa oti mudzamangire Nyumba yanga, kuti ndikondwere nayo ndi kulandiramo ulemu,” akutero Yehova.
9 Dilia da ifabi ganodini ha: i manu bagade lamusa: dawa: i galu. Amomane ha: i manu da dadamini aguni manoba, Na da amo dadami fulabole fasi dagoi. Abuliba: le, Na agoane hamobela: ? Bai Na Debolo Diasu da mugululi sia: i dagoiba: le. Be dilia da mae dawa: le, dilia diasu fawane gagulala.
“Mumayembekezera zambiri, koma taonani mwapeza pangʼono pokha. Zimene munazibweretsa ku nyumba, Ine ndinazimwaza. Nʼchifukwa chiyani?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Chifukwa Nyumba yanga ikanali bwinja, pamene aliyense wa inu watanganidwa kumanga nyumba yake.
10 Amaiba: le, Na da diligili gibu amola ha: i manu hame iaha.
Choncho, chifukwa cha inu, mitambo yaleka kugwetsa mvula ndipo dziko lapansi laleka kutulutsa zomera.
11 Na da dilia sogega esoi bagade i dagoi. Dilia soge agolo, gagoma sagai, waini sagai, olefe ifa sagai, dilia sagai liligi huluane amola dunu fi amola ohe fi huluane amo da esoi bagade ba: sa.
Ndabweretsa chilala pa minda ndi pa mapiri, chilala chawumitsa tirigu, mphesa, mafuta a olivi ndi chilichonse chimene chimamera pa nthaka, pa anthu ndi pa ngʼombe, ndi pa ntchito zonse za manja anu.”
12 Amalalu, Selababele, Yosiua amola dunu fi huluane (amo da Ba: bilone mugului asili buhagi), ilia Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele hamoi. Ilia da beda: ne, balofede dunu Ha: ga: iai (Hina Gode Ea Sia: Alofesu dunu) amo ea sia: nabawane hamoi.
Pamenepo Zerubabeli mwana wa Sealatieli, mkulu wa ansembe Yoswa mwana wa Yehozadaki, ndi anthu onse otsala anamvera mawu a Yehova Mulungu wawo ndi uthenga wa Hagai, chifukwa anatumidwa ndi Yehova Mulungu wawo. Ndipo anthuwo anaopa Yehova.
13 Amalalu, Ha: ga: iai da Hina Gode Ea sia: amo Isala: ili dunuma alofele adoi, amane, “Na da dafawane ilegesa. Na da dili hamedafa yolesimu.”
Tsono Hagai, mthenga wa Yehova, anapereka kwa anthuwo uthenga uwu wa Yehova: “Ine ndili nanu,” akutero Yehova.
14 Hina Gode da Selababele, Yuda eagene ouligisu dunu, gobele salasu ouligisu dunu Yosiua amola dunu huluane amo da mugululi asili buhagi, amo ilia da Debolo Diasu bu gaguma: ne, Hina Gode da ilia a: silibu denesi dagoi. Ilia da ilia Hina Gode Bagadedafa Ea Debolo Diasu gaguma: ne, hawa: hamosu mui.
Kotero Yehova anakhudza mtima wa Zerubabeli mwana wa Sealatieli, bwanamkubwa wa Yuda, mtima wa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndiponso mitima ya anthu onse otsala. Iwo anabwera ndi kuyamba ntchito yomanga Nyumba ya Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wawo,
15 Ilia da oubi gafeale amola eso 24 amo Da: liase ea hina bagade ouligisu eso amoga, amo hawa: hamosu mui.
pa tsiku la 24 la mwezi wachisanu ndi chimodzi, wa chaka chachiwiri cha Mfumu Dariyo.

< Ha:ga:iai 1 >