< Mui 30 >

1 Be La: isele da Ya: igobe ea mano hame laiba: le ea dalusima mudasu ba: i. E da Ya: igobema amane sia: i, “Di da nama mano hame iasea na da bogomu.”
Rakele ataona kuti sakumuberekera Yakobo ana, anayamba kumuchitira nsanje mʼbale wake. Choncho anati kwa Yakobo, “Undipatse ana kapena apo ayi ndingofa!”
2 La: isele ea sia: nababeba: le, Ya: igobe da ougi ba: i. E amane sia: i, “Na da Gode Ea sogebi lamu da hamedei galebe. Hi fawane da dia mano lamu logo ga: sisa.”
Yakobo anapsera mtima Rakele ndipo nati, “Kodi ine ndalowa mʼmalo mwa Mulungu amene wakulepheretsa iwe kukhala ndi ana?”
3 La: isele da amane sia: i, “Di da na udigili hawa: hamosu a: fini Biliha, amo lama. Di amola e gilisili golama. Amasea, e da mano lasea, na da amo mano ea ame esalumu.”
Pamenepo Rakele anati kwa Yakobo, “Mdzakazi wanga Biliha nayu. Lowana naye kuti mwina nʼkundibalira mwana, ndipo kudzera mwa iyeyu nanenso nʼkukhala ndi ana.”
4 E da Biliha amo egoama i. Amalalu, Ya: igobe da e amola gilisili golai.
Ndipo anamupatsa Yakobo wantchito wake Biliha kuti alowane naye. Choncho Yakobo analowana ndi Biliha,
5 Biliha da abula agui, dunu mano lalelegei.
ndipo Bilihayo anatenga pathupi namubalira Yakobo mwana wamwamuna.
6 La: isele da amane sia: i, “Gode da na fidima: ne fofada: i dagoi. E da na sia: ne gadosu nabalu, dunu mano nama i dagoi.” Amaiba: le, e da ea manoma Da: ne (Fidima: ne fofada: su) dio asuli dagoi.
Pamenepo Rakele anati, “Mulungu waweruza mondikomera mtima, wamva kupempha kwanga ndipo wandipatsa mwana wa mwamuna.” Choncho anamutcha Dani.
7 Biliha da bu abula agui, Ya: igobe ea dunu mano eno amola lalelegei.
Biliha, wantchito wa Rakele, anatenganso pathupi nabalira Yakobo mwana wa mwamuna wachiwiri.
8 La: isele da amane sia: i, “Na da na dalusima bagadewane gegei galu. Be na da osa: le heda: i dagoi. Amaiba: le e da amo manoma Na: badalai (Gegesu) dio asuli.
Pamenepo Rakele anati, “Ndakhala ndikulimbana kwambiri ndi mʼbale wanga ndipo ndapambana.” Choncho anamutcha Nafutali.
9 Lia da ea mano lamu logo ga: i dagoi amo dawa: beba: le, e da ea udigili hawa: hamosu a: fini Siliba amo Ya: igobema i.
Pamene Leya anaona kuti waleka kubereka ana, iye anatenga wantchito wake Zilipa namupereka kwa Yakobo kuti alowane naye.
10 Amalalu, Siliba da Ya: igobe ea dunu mano lalelegei.
Zilipa, wantchito wa Leya, anaberekera Yakobo mwana wamwamuna.
11 Lia da amane sia: i, “Na da hahawane udigili lai!” Amaiba: le e da Ga: de (Hahawane udigili Lai) dio ema asuli.
Pamenepo Leya anati, “Mwayi wangawo!” Choncho anamutcha Gadi.
12 Siliba da Ya: igobe ea dunu mano eno lai.
Zilipa, wantchito wa Leya anamubalira Yakobo mwana wa mwamuna wachiwiri.
13 Lia da amane sia: i, “Na da hahawane bagade! Eno uda da na da hahawane sia: mu. Amaiba: le, e da amo manoma A: sie (Hahawane) dio asuli.
Pamenepo Leya anati, “Ndakondwa bwanji! Amayi adzanditcha ine wokondwa.” Choncho anamutcha Aseri.
14 Widi faisu eso amoga, Liubene da gisi sogega asili, sogea liligi amo mano lasu fidisu liligi ilia da dawa: i galu, (ma: nadala: igi) amo fili, ea: me Liama gaguli misi. La: isele da Lia ema amane sia: i, “Dia mano ea sogea lai liligi amo mogili nama ima.”
Pa nthawi yokolola tirigu, Rubeni anapita ku munda ndipo anapezako zipatso za mankhwala wobereketsa. Tsono anatengerako mayi wake Leya. Rakele anati kwa Leya, “Chonde patseko mankhwala wakupezera mwana wakowo.”
15 Lia da bu adole i, “Di da nagoa wamolai dagoi. Amo da hamedei liligi di da dawa: bela: ? Be wali di da na mano ea sogea liligi amo amola lamusa: dawa: lala. La: isele da amane sia: i, “Di da dia mano ea sogea liligi amo nama iasea, di amola Ya: igobe da wali gasia gilisili golamu da defea.”
Koma iye anati kwa Rakele, “Kodi sizinakukwanire kulanda mwamuna wanga? Ukuti utengenso mankhwala a mwana wangawa.” Iye anati, “Chabwino, agone ndi iwe usiku uno kuti tisinthane ndi mankhwala a mwana wakowo.”
16 Daeya, Ya: igobe da ifabi amoga misini, Lia da logoga e yosia: musa: asi. Lia da amane sia: i, “Ania da wali gasia gilisili golamu galebe. Na da na mano ea sogea amoga di bidi lai dagoi.” Amaiba: le, Ya: igobe da e amola gilisili golai.
Choncho pamene Yakobo ankabwera kuchokera ku munda madzulo, Leya anapita kukakumana naye nati, “Lero mukagona ku nyumba chifukwa ndakubwerekani ndi mankhwala wobereketsa a mwana wanga.” Choncho usiku umenewo Yakobo anakalowa kwa Leya.
17 Gode da Lia ea sia: ne gadosu nabi dagoi. E da abula agui, Ya: igobe ea dunu mano eno - amo da mano bi gala lalelegei.
Mulungu anamva pemphero la Leya ndipo anatenga pathupi nabalira Yakobo mwana wa mwamuna wachisanu.
18 Lia da amane sia: i, “Na da na hawa: hamosu a: fini nagoama i dagoiba: le, Gode da nama hahawane bidi i dagoi. Amaiba: le, e da ea manoma Isiga (Dunu Bidiga Lai) amo dio asuli.
Pamenepo Leya anati, “Mulungu wandipatsa mphotho chifukwa chopereka wantchito wanga kwa mwamuna wanga.” Choncho anamutcha Isakara.
19 Lia da bu abula agui ba: i. E da Ya: igobe ea dunu mano gafe lalelegei dagoi.
Leya anatenganso pathupi nabalira Yakobo mwana wa mwamuna wachisanu ndi chimodzi.
20 E amane sia: i, “Gode da nama hahawane udigili iasu i dagoi. Wali, na da nagoama dunu mano gafeyale ia dagoiba: le, e da na hahawane lamu. Amaiba: le, e da amo manoma Sebiulane (Hahawane Iasu Lai) dio asuli.
Pamenepo Leya anati, “Mulungu wandipatsa mphatso yapamwamba. Tsopano mwamuna wanga adzandilemekeza chifukwa ndamubalira ana aamuna asanu ndi mmodzi.” Choncho anamutcha Zebuloni.
21 Fa: no, Lia da uda mano lai dagoi. E da ema Daina dio asuli.
Patapita nthawi Leya anabereka mwana wamkazi ndipo anamutcha Dina.
22 Amalalu, Gode da bu La: isele dawa: i. E da ea sia: ne gadosu nabi. E da ea mano lamu logo doasi dagoi.
Kenaka, Mulungu anakumbukira Rakele namva pemphero lake ndi kulola kuti akhale ndi mwana.
23 E da abula agui, dunu mano lalelegei. E amane sia: i, “Gode da nama dunu mano ia dagoiba: le, na gogosiasu fadegai dagoi.
Rakele anatenga pathupi nabala mwana wamwamuna ndipo anati, “Mulungu wandichotsera manyazi anga.”
24 E da nama eno dunu mano imunu da defea. Amaiba: le, e da amo manoma Yousefe (Eno imunu da defea) dio asuli.
Iye anamutcha mwanayo Yosefe, ndipo anati, “Mulungu andipatsenso mwana wina.”
25 Yousefe da lalelegei dagoloba, Ya: igobe da La: iba: nema amane sia: i, “Na da na diasuga masunu. Na masa: ne logo doasima.
Rakele atabereka Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, “Ndimasuleni kuti ndizipita ku dziko la kwathu.
26 Na uda amola mano amo na da dia hawa: hamosu hamoiba: le bidi lai, amo huluane nama ianu na da masunu galebe. Di dawa: Na da dia hawa: hamosu noga: le hamoi.
Patseni akazi anga ndi ana anga, amene ndinakugwirirani ntchito, ndipo ndidzanyamuka ulendo. Inu mukudziwa ntchito imene ndakugwirirani.”
27 La: iba: ne da ema amane sia: i, “Na da ba: la: lusu dunu agoane. Na agoane ba: i. Dia hawa: hamobeba: le, Gode da nama hahawane dogolegele hamoi.
Koma Labani anati kwa iye, “Chonde, ngati mungandikomere mtima musapite chifukwa ndadziwa kudzera mwa kuwombeza kwanga kuti Yehova wandidalitsa chifukwa cha inu.”
28 Dima bidi imunu defei, amo di fawane sia: ma. Amasea, na da amo dima imunu”
Anapitiriza kunena kuti, “Tchula malipiro ako ndipo ndidzakupatsa.”
29 Ya: igobe da amane sia: i, “Di da na hawa: hamosu dawa: Na da dia sibi noga: le ouligisu. Amaiba: le, ilia idi da noga: le heda: i amola di da bagade gaguiwane ba: sa.
Koma Yakobo anati kwa iye, “Inu mukudziwa mmene ine ndakugwirirani ntchito ndi mmene ziweto zanu zaswanira pamene ine ndimazisamalira.
30 Musa: na da mae misini, dia sibi da bagahame galu. Be wali bagohame ba: sa. Na da fidibiba: le, Gode da dima hahawane dogolegele fidisu. Wali na da ni liligi amo dawa: mu.”
Poyamba munali nazo zochepa ine ndisanabwere, koma tsopano zachuluka. Yehova wakudalitsani chifukwa cha ine. Ndi nthawi tsopano kuti nane ndisamalire banja langa.”
31 La: iba: ne da amane sia: i, “Na da dima adi ima: bela: ?” Ya: igobe da bu adole i, “Na da muni hame lamu. Di da na adole ba: su hahawane ba: sea, na da dia sibi bu ouligimu.
Labani anafunsa, “Ndikupatse chiyani?” Yakobo anayankha, “Musandipatse kanthu. Koma mungondichitira izi ndipo ndidzapitiriza kusamalira nkhosa zanu ndi kuziyangʼanira:
32 Be wali eso na da dia sibi fi amoga bunumai sibi mano, amola goudi hoholei o daginisisi, amo huluane na da lamu. Amo bidi fawane na da lamu.
Mundilole ndiyendeyende pakati pa ziweto zanu lero ndi kuchotsamo mwana wankhosa wamkazi aliyense wakuda, mbuzi iliyonse yamathothomathotho ndi yamawangamawanga. Zimenezi ndiye zikhale malipiro anga.
33 Amola hobea di da na hou hedolo ba: mu. Di da na hou ba: la masea, hoholei o daginisisi hame hamoi goudi o bunumai hame sibi ba: sea, amo da wamolai dagoi di da dawa: mu.”
Ndipo chilungamo changa chidzaoneka mʼtsogolo, pamene inu mudzabwere kudzaona malipiro angawo. Ngati mudzapeza mbuzi mʼgulu langa imene si yamawangamawanga, kapena mwana wankhosa wamkazi amene si wakuda ndiye kuti zimenezo zidzakhala kuti ndinakuberani.”
34 La: iba: ne da bu adole i, “Defea! Dia sia: defele ninia da hamomu.”
Labani anati, “Ndavomera, zikhale monga mmene wayankhuliramu.”
35 Be amo eso La: iba: ne da goudi gawali hoholei amola aseme fifi amola daginisisi huluane, amola bunumai sibi amo fadegale, egefelali ili ouligima: ne oule asi.
Tsiku lomwelo Labani anachotsa atonde onse ndi mbuzi zazikazi zonse zimene zinali ndi mawangamawanga kapena zamathothomathotho, ndiponso zonse zabanga loyera. Anachotsa ana onse ankhosa aakazi akuda, napereka ziweto zonsezi kwa ana ake aamuna kuti aziweta.
36 Amalalu, e da Ya: igobe fisili, eso udiana asili, eno sogega doaga: i. Be Ya: igobe da La: iba: ne ea sibi eno ouligisu.
Kenaka Labani anayenda mtunda wa masiku atatu kutalikirana ndi Yakobo koma Yakobo anapitiriza kuweta nkhosa zina zonse za Labani.
37 Ya: igobe da ifa amoda lale, ea gadofo mogili amo gobiheiga gagaselele, amoda da ahea: iai amola bunumai, amo fifi agoane ba: i.
Tsono Yakobo anatenga nthambi zaziwisi za mitengo ya mkundi, alimoni ndi puleni nazisenda kuchotsa makungwa ake mpaka mtengo woyera wamʼkati kuonekera.
38 Amo ifa amoda e da sibi gilisisu ilia hano nasu ofodo gadenene ligisi. Bai fofoi ohe da hano na misini, mano lama: ne agusu.
Atatero anayika nthambi zija mʼmagome omwera madzi molunjika ziweto zija kuti pakumwa madziwo ziweto zazikazi ziziyangʼana nthambi zija popeza kuti pakumwa madzi ziweto zija zinkakwerana.
39 Amaiba: le, goudi da mano hamoma: ne ifa ba: le gaidiga hamosu, ilia mano da fa: no lalelegeloba hoholei amola fifi daginisisi ba: su.
Ndiye kuti nkhosa zija zinkatenga mawere pakumwa madzi molunjika nthambi zija, ndipo zinkaswa ana a mawangamawanga kapena a mathothomathotho.
40 Ya: igobe da sibi amola goudi afafai. Sibi da mano lasu hou hamonoba, e da ea sibi amo La: iba: ne ea fifi amola bunumai lai gebo amo ba: la masa: ne olelei. Amalalu, ea lai gebo da bagade hamoi, amola e da ea lai gebo fi amo La: iba: ne ea lai gebo fi ilima afafai.
Yakobo anayika padera ana a ziweto zija. Koma ziweto zina anaziyika kuti ziyangʼanane ndi za Labani, zimene zinali za mawangamawanga ndi zakuda. Motero anapeza ziweto zakezake, ndipo sanazisakanize ndi za Labani.
41 Noga: i dagumui lai gebo da mano lama: ne hamonoba, e da ifa hamoi ilia ba: ma: ne hano ofodo gadenene ligisisu.
Yakobo ankayika nthambi zija momwera madzi pamene ziweto zamphamvu zazikazi zinkakweredwa pofuna kuti zitenge mawere pakumwa madzi moyangʼanana ndi nthambi zija.
42 Be gasa hame lai gebo da mano lama: ne hamonanoba, e da ifa hame ligisisu. Amalalu, La: iba: ne ea lai gebo da gasa hame ba: i. Be Ya: igobe ea lai gebo huluane da gasa bagade dagumui ba: i.
Koma sankayika nthambizo pamene ziweto zofowoka zazikazi zinkakweredwa pakumwa madzi. Choncho ziweto zofowoka zonse zinakhala za Labani, ndi ziweto zamphamvu zinakhala za Yakobo.
43 Amalalu, Ya: igobe da bagade gagui dunu agoane ba: i. E da sibi gilisisu bagohame, udigili hawa: hamosu dunu, ga: mele, lai gebo, sibi, amola dougi bagohame gagui galu.
Mwa njira imeneyi, Yakobo analemera kwambiri ndipo anali ndi ziweto zochuluka kwambiri, antchito aakazi ndi aamuna, ngamira ndi abulu.

< Mui 30 >