< Mui 20 >

1 A: ibalaha: me da Ma: melei soge yolesili, Ga: ina: ne soge ga (south) la: idiga asi. E da diasu aduna amo Ga: idesie amola Sie amoga dogoa moilai bai bagade ea dio amo Gila esalu.
Abrahamu anachokako kumeneko napita ku Negevi ndipo anakakhala ku dziko la Gerari, limene lili pakati pa mzinda wa Kadesi ndi mzinda wa Suri. Anakhala ku Gerari kwa kanthawi,
2 Amoga, A:ibalaha: me da ea uda Sela amo da ea dalusi sia: i. Amalalu, Gila hina bagade dunu amo Abimelege da Sela ema misa: ne sia: i. E da ea diasuga esaloma: ne lai.
ndipo Abrahamu ankawawuza za Sara kuti, “Iyeyu ndi mlongo wanga.” Choncho Abimeleki, mfumu wa ku Gerari anamutenga Sara uja.
3 Be Gode da simasia ganodini Abimelegema amane sia: i, “Di da bogoi dunu defele. Bai amo uda di da lai, amo da dunu eno idua.”
Koma usiku, Mulungu anafika kwa Abimeleki kutulo nati, “Ufatu iwe chifukwa cha mkazi amene watengayu popeza ndi wokwatiwa.”
4 Be Abimelege da Sela amoma hame doaga: i galu. Amaiba: le, e amane sia: i, “Hina Gode! Di da fi amo wadela: le hame hamoi amo wadela: ma: bela: ?
Nthawi imeneyi nʼkuti Abimeleki asanamukhudze mkaziyo, kotero kuti anati, “Ambuye, kodi mudzawonongadi mtundu wolungama?
5 A: ibalaha: me da nama amane sia: i, ‘E da na dalusi,’ amola uda da nama amane sia: i, ‘E da na ola’. Na da amo sia: da dafawane dawa: beba: le, wadela: le hame hamoi.”
Kodi Abrahamu sanandiwuze kuti iyeyu ndi mlongo wake? Ndiponso mkaziyu ankanena kuti Abrahamu ndi mlongo wake. Choncho ine pochita izi, ndinkachita moona mtima ndiponso mopanda chinyengo.”
6 Amalalu, Gode da amo simasia ganodini ema amane sia: i, “Dafawane! Na dawa: Di da asigi dawa: su dodofei dagoi amoga hamoi. Amaiba: le, Na da dia wadela: i hamomu logo damui dagoi. Bai di da e mae digili ba: ma: ne, Na da amo logo ga: i.
Tsono kumaloto komweko Mulungu anati kwa iye, “Inde ndikudziwa kuti wachita izi moona mtima, ndipo Ine sindinafune kuti undichimwire. Nʼchifukwa chake sindinakulole kuti umukhudze.
7 Be wali amo dunu ea uda ema bu ima. E da balofede dunu amola e da di fidima: ne sia: ne gadomu. Amasea, di da hame bogole esalumu. Be ema bu hame iasea, di amola dia fi huluane da bogogia: mu, amo noga: le dawa: ma.”
Tsopano kabwezere mkaziyo kwa mwamuna wake. Iyeyu ndi mneneri, ndipo adzakupempherera kuti ukhale ndi moyo. Koma ukapanda kukamupereka, udziwiretu kuti udzafa pamodzi ndi onse a pa banja pako.”
8 Hahabedafa, Abimelege da ea eagene ouligisu dunu huluane misa: ne sia: i. Amo hou huluane ilima olelelalu, ilia da bagadewane beda: i.
Mmamawa mwake Abimeleki anayitanitsa akuluakulu ake onse, ndipo atawafotokozera zimene zinachitika, iwo aja anachita mantha kwambiri.
9 Amalalu, Abimelege da A: ibalaha: me misa: ne sia: i. E da ema amane sia: i, “Di da ninima adi hamobela: ? Dia hou hamoiba: le, na amola na fi da se bagade nabi. Na da dima adi wadela: i hou hamobela: ? Di da ninima hou hamoi da defea hame.”
Kenaka Abimeleki anayitana Abrahamu ndipo anati, “Kodi wachita chiyani? Ndakulakwira chiyani kuti undibweretsere ine pamodzi ndi anthu anga chilango chachikulu chotere? Wandichitira zinthu zimene sizinayenera kuchitika.”
10 Amola Abimelege da A: ibalaha: mema amane adole ba: i, “Adi baiga di da amo hou hamobela: ?”
Ndipo Abrahamu anafunsa Abimeleki kuti, “Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”
11 A: ibalaha: me da bu adole i, “Na da na dogo ganodini amane sia: i, ‘Amo soge ganodini, dunu fi da Godema hame beda: sa. Ilia da na uda ba: sea, na fane legemu.’
Abrahamu anayankha nati, “Ndinkaganiza kuti kuno kulibiretu munthu woopa Mulungu. Ndiye ndimati mwina adzandipha chifukwa cha mkazi wanga.
12 Amola, amo uda da dafawane na dalusi. E da na ada ea mano be eme ea mano hame. Amola amo na da lai dagoi.
Komabe kunena zoona, iyeyu ndi mlongo wangadi, mwana wamkazi wa abambo anga ngakhale kuti si ife a mayi mmodzi. Tsono akhoza kukhala mkazi wanga.
13 Amola Gode da nama nada ea fi amo fisili ga masa: ne sia: noba, na da Selama amane sia: i, ‘Di da dia nama asigi hou agoane olelema. Soge huluane ani ahoasea, na hou agoane olelema; E da na ola!’”
Ndiye pamene Mulungu anati ndichoke ku nyumba ya abambo anga, ndinawuza mkazi wangayu kuti, ‘Kuti uwonetse kuti ndiwe mkazi wokoma mtima, uziwuza anthu kulikonse kumene tingapite kuti ndine mlongo wako.’”
14 Amalalu, Abimelege da sibi, bulamagau, udigili hawa: hamosu dunu amola udigili hawa: hamosu uda, amo oule misini, A:ibalaha: mema i. Amola ea uda Sela amo ema bu i.
Tsono Abimeleki anapereka nkhosa, ngʼombe ndi antchito aamuna ndi aakazi kwa Abrahamu. Ndipo anamubwezeranso Abrahamu Sara, mkazi wake.
15 Amola Abimelege da ema amane sia: i, “Na soge huluane ba: ma. Dia hanaiga amogai fima.”
Tsono Abimeleki anati kwa Abrahamu, “Dziko langa ndi limene ukulionali; ukhale paliponse pamene ufuna.”
16 E da Selama amane sia: i, “Na da dia olama silifa muni 1000 amo iaha. Amo da dunu huluane ilima di da wadela: i hame hamoi amo olelema: ne. Dunu huluane da di da wadela: i hame hamoi amo dawa: mu.”
Ndipo kwa Sara, iye anati, “Ndikumupatsa mlongo wakoyu makilogalamu khumi ndi awiri a siliva kutsimikiza kuti iwe ndi wosalakwa pamaso pa onse amene ali ndi iwe; ulibedi mlandu.”
17 Amalalu, A:ibalaha: me da Godema sia: ne gadoi. Amola Gode da Abimelege, ea uda amola ea udigili hawa: hamosu a: fini huluane uhinisi dagoi. Amalalu, ilia da mano eno bu lamu hou dawa: i.
Tsono Abrahamu anapemphera kwa Mulungu ndipo Mulunguyo anachiritsa Abimeleki, mkazi wake pamodzi ndi adzakazi ake kuti athenso kubereka ana.
18 Bai Hina Gode da A: ibalaha: me idua Selama asigiba: le, Abimelege ea fi uda ilia mano lamu logo amo huluane ga: si dagoi. Be wali bu doasi.
Paja Yehova nʼkuti atatseka akazi onse a mʼbanja la Abimeleki kuti asabereke ana chifukwa cha Sara, mkazi wa Abrahamu.

< Mui 20 >