< Esela 4 >

1 Yuda fi dunu amola Bediamini fi dunu ilia ha lai dunu da mugululi asi dunu da buhagili, Isala: ili Hina Gode Ea Debolo diasu gagubi nabi.
Adani a Yuda ndi Benjamini anamva kuti anthu obwera ku ukapolo aja akumangira Nyumba Yehova, Mulungu wa Israeli.
2 Amaiba: le, ilia da Selubabele amola Isala: ili fi ouligisu dunu ilima asili, amane adole ba: i, “Ninia amola da Debolo diasu gagumusa: fidimu da defeala: ? Ninia Godema sia: ne gadosu da dilia Godema sia: ne gadosu amo defele sia: ne gadosa. Amola Asilia hina bagade Isaha: done da sia: beba: le ninia guiguda: misi, amo fa: no ninia da Godema gobele salasu hou huluane hamonana.”
Tsono anapita kwa Zerubabeli ndi kwa atsogoleri a mabanja awo ndi kunena kuti, “Mutilole kuti tikuthandizeni kumangaku chifukwa ife timapembedza Mulungu wanu monga momwe mumachitira inu, ndipo takhala tikupereka nsembe kwa Iye kuyambira nthawi ya Esrahadoni, mfumu ya ku Asiriya, amene anabwera nafe kuno.”
3 Selubabele, Yosiua amola Isala: ili fi ouligisu dunu da ilima amane adole i, “Ninia da Hina Gode Ea Debolo diasu gagusia, eno fidisu dunu hame lamu. Ninisu amo Besia hina bagade Sailase amo ea sia: i defele, gagumu.”
Koma Zerubabeli, Yesuwa ndi atsogoleri ena otsala a mabanja a Aisraeli anayankha kuti, “Inu simungatithandize kumangira Nyumba Yehova, Mulungu wathu. Tokha tidzamumangira Nyumba Yehova, Mulungu wa Aisraeli, monga mfumu Koresi, mfumu ya Perisiya inatilamulira.”
4 Amalalu, dunu da musa: Isala: ili sogega esalu da Yu dunu beda: ma: ne gasa fi hamosu. Ilia da Yu dunu ilia Debolo gagumu hawa: hamosu hedofamusa: dawa: i galu.
Tsono anthu a mʼdzikomo anayamba kuchititsa ulesi anthu a ku Yuda, ndi kuwachititsa mantha kuti aleke ntchito yomangayo.
5 Ilia da Besia eagene dunu amo Yu dunu ilia Debolo gagusu hawa: hamosu hedofama: ne, hano suligili muni ilima i. Amo hou ilia da Sailase ea Besia soge ouligisia amola fa: no Da: liase da Besia soge ouligisia, amo esoha ilia da mae fisili hamosu.
Analemba alangizi ena kuti alepheretse cholinga chawo pa ntchitoyo pa nthawi yonse ya Koresi, mfumu ya ku Perisiya, ndiponso mpaka pamene Dariyo mfumu ya ku Perisiya ankalamulira dzikolo.
6 Hina bagade amo Segesisi da Besia ouligisu hou lai dagoi. Ea ouligisu degabo laloba, dunu amo Yuda soge amola Yelusaleme ganodini esalu, ilima ha lai dunu da ilima fofada: musa: meloa dedene i.
Mfumu Ahasiwero atangoyamba kulamulira dzikolo, adani aja analemba kalata yoneneza anthu a Yuda ndi Yerusalemu.
7 Fa: no, hina bagade eno amo Adasegesisi da Besia soge ouligisia, ha lai dunu amo Bisila: me, Mililida: de amola Da: ibia: le ilia da Adasegesisima meloa dedene i. Amo meloa ilia da A: lama: ia: ge sia: ga dedei. Idisia, ilia da bu Besia sia: amoga afadenema: ne sia: i.
Ndiponso mʼnthawi ya Aritasasita mfumu ya Perisiya, Bisilamu, Mitiredati, Tabeeli ndi anzawo ena analemba kalata inanso kwa Aritasasita. Kalatayo inalembedwa mʼChiaramu ndipo ankatanthauzira poyiwerenga.
8 Amola eagene hina dunu amo Lihame amola soge dedesu dunu amo Simisai, ela da Adasegesisi ema Yelusaleme ea hou olelemusa: meloa dedene i, amane,
Rehumu mkulu wankhondo ndi Simisai mlembi, nawonso analemba kalata yawo yoneneza anthu a ku Yerusalemu kwa mfumu Aritasasita. Anayilemba motere:
9 “Lihame (eagene hina dunu), Simisai (soge dedesu dunu), ela fidisu dunu, fofada: su dunu amola ouligisu dunu eno huluane (amo huluane da musa: Ila: me soge moilai bai bagade amo Ilege, Ba: bilone amola Susa amoga misi) amola
Kalata yochokera kwa Rehumu, mkulu wa gulu lankhondo, mlembi Simisai ndi anzawo awa: oweruza, nduna, akuluakulu ena, anthu a ku Peresiya, Ereki, Babuloni, Susa mʼdziko la Elamu,
10 dunu eno amo gasa bagade hina Asoba: niba: le da ilia moilaia mugululi, ilia da Samelia moilai bai bagade amola eno sogebi Guma: dini Iufala: idisi Soge amo ganodini fima: ne oule asi, da amo meloa dedene iaha.”
ndi mitundu ina imene mkulu wolemekezeka, Osanipara anayisamutsa ndi kuyikhazika mʼmizinda ya Samariya ndi mʼmadera ena apatsidya la Yufurate.
11 Ilia da meloa agoane dedene i, “Ninia da di, hina bagade Adasegesisi, ninia da dia hawa: hamosu dunu Guma: dini Iufala: idisi soge amo ganodini esala, dima meloa dedene iaha.
Mawu a mʼkalata ya kwa Aritasasita anali awa: Kwa mfumu Aritasasita: Kuchokera kwa atumiki anu, anthu a kutsidya kwa Yufurate:
12 Hina bagade! Di da Yelusaleme amoma doaga: i hou dawa: mu da defea. Yu dunu da dia soge eno amoga misini, Yelusaleme amo ganodini fili, ilia amo wadela: i amola hame nabasu moilai bai bagade amo bu gagulala. Ilia amo moilai bai bagade gagoi gagulala amola ea gagui da gadenenewane dagomu ba: sa.
Amfumu tati mudziwe kuti Ayuda amene anabwera kuno kuchokera kwanuko apita ku Yerusalemu ndipo akumanganso mzinda wa anthu owukira ndi oyipa uja. Akumaliza makoma ake ndipo akukonzanso maziko.
13 Hina bagade! Amo moilai bu gagusia amola amoea gagoi dagosea, Yu fi dunu da dima su muni iasu hou fisimu, amola dia su labe da ebelemu agoai ba: mu.
Kuwonjeza apo amfumu mudziwe kuti ngati amalize kumanganso mzindawu ndi kukonzanso makoma ake, adzaleka kukhoma msonkho, kulipira ndalama zakatundu olowa mʼdziko kapena msonkho wina uliwonse, ndipo chuma cha thumba la ufumu chidzachepa.
14 Di da nini huluane ouligisa. Amaiba: le, agoai hou doaga: mu ninia higa: i ba: mu. Ninia agoane dawa: ,
Popeza tsono ife timadya nawo kwa mfumu sitiyenera tizingoonerera zinthu zochititsa mfumu manyazi. Nʼchifukwa chake tikutumiza uthenga kwa inu a mfumu kuti mudziwe zonse.
15 di da dia fidisu dunu ilima ilia meloa dedei dia aowalali ilia dedei, amo ganodini hogoma: ne sia: ma. Di agoane hamosea, Yelusaleme soge dunu da eso huluane mae fisili, hame nabasu hou hamosu di da ba: mu. Ilia gasa fi hou hamobeba: le, hina bagade amola soge ouligisu dunu da se bagade nabi amola ili ouligimu gasa bagade ba: i. Amaiba: le, amo moilai bai bagade da wadela: lesi dagoi ba: i.
Choncho pachitike kafukufuku mʼbuku la mbiri yakale ya makolo anu. Mʼbuku la mbiri zakale mudzapezamo ndi kuwerenga kuti mzinda umenewu ndi waupandu, wosautsa mafumu ndi nduna zamʼmadera zomwe. Kuyambira kale wakhala ukuwukira ulamuliro uliwonse. Nʼchifukwa chake mzinda umenewu anawuwononga.
16 Amaiba: le ninia da agoane dawa: Ilia da amo moilai bai bagade amola ea gagoi bu gagusia, di hina bagade, da Guma: dini Iufala: idisi soge ouligimu hamedeiwane ba: mu.” Ilia da amo meloa Adasegesisi ema dedene i.
Tsono tikukudziwitsani amfumu kuti ngati mzinda umenewu umangidwanso ndi makoma ake nʼkutsirizidwanso ndiye kuti inu simudzalamuliranso chigawo cha patsidya pa Yufurate.
17 Adasegesisi da ilima dabe meloa amane dedene i, “Dilia! Lihame (eagene hina dunu), Simisai (soge dedesu dunu) amola ela fidisu dunu Samelia soge amola Guma: dini Iufala: idisi soge amo ganodini esala. Asigi sia: sia: sa!
Mfumu inatumiza yankho ili: Mkulu wa gulu lankhondo Rehumu, mlembi Simisai ndi anzanu onse amene akukhala ku Samariya ndi mʼzigawo zina zonse za Patsidya pa Yufurate. Landirani moni.
18 Dilia nama meloa dedene iasi amo na sia: alofele iasu dunu da afadenene, nama idili i.
Kalata imene munatumiza ija yawerengedwa bwino lomwe pamaso panga.
19 Na sia: beba: le, na fidisu dunu da aowalali ilia meloa dedei amo hogolala ba: i. Dafawane! Musa: amola amo fa: no, Yelusaleme fi dunu da hina bagade ilia sia: hame nabasu, amola amo ganodini hame nabasu dunu amola nimi bagade dunu bagohame ba: su.
Ine nditalamula kuti afufuze nkhaniyi kwapezekadi kuti mzinda umenewu uli ndi mbiri yowukira mafumu ndi kuti zaupandu ndi zowukira zinkachitikadi mʼmenemo.
20 Gasa bagade Ba: bilone hina dunu da Yelusaleme amola Guma: dini Iufala: idisi soge huluane ouligisu. Ilia da su (da: gisi) muni amo dunuma lasu.
Mafumu amphamvu akhala akulamulira Yerusalemu ndi chigawo chonse cha Patsidya pa Yufurate. Iwo ankalandira msonkho ndi kulipira ndalama zakatundu olowa mʼdziko pa kanthu kena kalikonse.
21 Amaiba: le, amo dunuma ilia Yelusaleme bu gagusu go fisima: ne sia: ma. Na da bu gaguma: ne sia: sea fawane, ilima bu gaguma: ne sia: ma.
Tsopano inu khazikitsani lamulo kuti anthu amenewo asiye ntchitoyo, asamangenso mzindawo mpaka ine nditalamula
22 Ilia da na hou bu wadela: sa: besa: le, amo sia: hedolo adoma!” Adasegesisi da amo meloa dedene iasi.
Musachedwe kuchita zimenezi. Kodi ine ndingalole bwanji kuti zowononga zotere zikule ndi kupweteka ine mfumu?
23 Sia: alofele iasu dunu da amo meloa Lihame amola Simisai amola ela fidisu dunu ilima idili i. Ilia da Yelusalemega hedolo asili, Yu dunu ilia moilai bai bagade gagusu logo hedofai dagoi.
Kalata ya mfumu Aritasasitayi itangowerengedwa pamaso pa Rehumu ndi Simisai mlembi uja, ndi anzawo onse, iwo anapita msangamsanga ku Yerusalemu kukawaletsa Ayuda aja mwamphamvu kuti asapitirire ntchito yawo.
24 Debolo diasu bu gagusu logo da hedofaiba: le, ilia da hame hawa: hamosu. Amalalu, hina bagade eno ea dio amo Da: liase da Besia soge ouligisu hou lai. E da ode aduna ouligilalu,
Motero ntchito yomanga Nyumba ya Mulungu ku Yerusalemu inayimitsidwa mpaka chaka cha chiwiri cha ulamuliro wa Dariyo mfumu ya ku Perisiya.

< Esela 4 >