< Isigiele 9 >

1 Na da Gode Ea Isala: ili ha lai dunuma wele sia: be nabi, amane, “Yelusalemema se dabe imunu dunu! Dilia goeguda: misa! Dilia gegesu liligi amo gaguli misa.”
Pambuyo pake Yehova anandiyankhula mofuwula kuti, “Bwerani pafupi, inu odzalanga mzindawu, aliyense ali ndi chida chake mʼmanja.”
2 Amo galuwane, dunu gafeale gala da Debolo diasu logo ga: i gadi (north) amo gadili misi. Ilia defegagale gegesu liligi gaguli misi. Amo iliga afae da dunu abula ahea: iai ga: ne, dedesu liligi gaguli manebe ba: i. Ilia huluane misini, balase oloda amo bega: dadafulili lelefulu.
Ndipo ndinaona anthu asanu ndi mmodzi akubwera kuchokera ku chipata chakumtunda chimene chimaloza kumpoto, aliyense ali ndi chida choopsa cha nkhondo mʼdzanja lake. Pagulu pawopa panali munthu wovala chovala chabafuta, atatenga zolembera pambali pake. Iwo analowa ndi kuyima pambali pa guwa lamkuwa.
3 Isala: ili Gode Ea nenemegi hadigi da esalebe liligi ougia galebe, amo da: iya dialebe ba: i. Gode Ea hadigi da amoga heda: le, Debolo logo holeiga aligila asi. Hina Gode da abula ahea: iai ga: i dunu ilima amane wele sia: i,
Tsono ulemerero wa Mulungu wa Israeli unakwera kuchokera pamwamba pa akerubi, pamene unali, ndipo unafika pa chiwundo cha Nyumba ya Mulungu. Pamenepo Yehova anayitana munthu amene anavala chovala chabafuta uja amene anatenga zolembera pambali pake
4 “Yelusalemedi golili asili, nowa dunu da moilai amo ganodini wadela: i hou hamonanebe amo ba: beba: le da: i dioi galea, amo ea odagigia, ilegele dedema.”
ndipo anamuwuza kuti, “Pita mu mzinda wonse wa Yerusalemu ndi kuyika chizindikiro pamphumi pa anthu amene akumva chisoni ndi kulira chifukwa cha zinthu zonse zonyansa zimene zikuchitika mu mzindamo.”
5 Amalalu, Gode da dunu eno ilima sia: be na nabi, “Amo dunu moilaidi ahoanebe ilima fa: no bobogema. Dunu huluane medole legema. Mae asigili, huluanedafa medole legema.
Kenaka ndinamva Yehova akuwuza anthu ena aja kuti, “Mutsateni mu mzinda wonse ndipo mukakanthe aliyense mopanda kumvera chisoni kapena chifundo.
6 Dunu da: i, amola ayeligi amola uda a: fini amola ame amola mano huluanedafa, medole legema. Be nowa da ea odagigia ilegele dedei galea, amo mae medole legema. Na Debolo diasua muni medole legema!” Amaiba: le, ilia da Yelusaleme ouligisu dunu Debolo diasua lelefulu, amo hidadea medole lelegei.
Mukaphe kotheratu anthu okalamba, anyamata ndi atsikana, makanda ndi akazi koma musakakhudze wina aliyense amene ali ndi chizindikiro. Muyambire ku Nyumba yanga yopatulika.” Motero iwo anayamba ndi akuluakulu amene anali kutsogolo kwa Nyumba ya Mulungu.
7 Gode da ilima amane sia: i, “Debolo diasu amo ledo fima: ne hamoma. Bogoi da: i hodo bagohame ea gagoi ganodini afagogoma. Hawa: hamoma!” Amaiba: le, moilai amo ganodini, ilia da muni dunu medole lelegelalu.
Ndipo Yehova anawawuza kuti, “Ipitsani Nyumba ya Mulungu ndipo mudzaze mabwalo ake ndi anthu akufa. Pitani.” Choncho iwo anapita nayamba kupha anthu mu mzinda monse.
8 Medole legesu da hamonanoba, nisu fawane lelu. Na da midadi odagi guduli, diasa: ili, ha: giwane wele sia: i, “Ouligisudafa Hina Gode! Di da Yelusaleme fi dunu ilima baligili ougiba: le, Di da Isala: ili dunu hame bogoi esalebe, amo huluanedafa medole legema: bela: ?”
Pamene iwo ankapha anthu, ine ndinatsala ndekha. Tsono ndinadzigwetsa chafufumimba ndi kufuwula kuti, “Aa, Ambuye Yehova! Kodi mwawakwiyiratu anthu a ku Yerusalemu motero kuti mudzawononga kotheratu anthu onse otsala ku Israeli?”
9 Gode da bu adole i, “Isala: ili fi dunu amola Yuda fi dunu ilia da wadela: i hou baligilidafa hamoi. Ilia Isala: ili soge huluane amo ganodini, medole legesu hou bagade hamosu. Amola Yelusaleme amo ganodini wadela: i hou bagade heda: i. Ilia da ogogole agoane sia: sa, ‘Hina Gode da ninia soge fisi dagoi, amola E da ninia hou hame ba: sa.’
Iye anandiyankha kuti, “Tchimo la Aisraeli ndi Yuda ndi lalikulu kwambiri; dziko ladzaza ndi zophana ndipo mu mzinda mwadzaza ndi zosalungama. Iwo akunena kuti, ‘Yehova walisiya dziko lake; Yehova sakuona.’
10 Be Na da ilima hame asigimu. Ilia da eno dunuma hamoi, amo defele Na da ilima dabe imunu.”
Choncho sindidzawamvera chisoni kapena kuwaleka, koma Ine ndidzawalanga potsata zochita zawo.”
11 Amalalu, ahea: iai abula ga: i dunu da Hina Godema buhagili, amane olelei, “Na da Dia sia: i didili hamoi dagoi.”
Ndipo munthu wovala chovala chabafuta uja atatenga zolembera pambali pake anadzafotokozera Yehova kuti, “Ndachita monga munandilamulira.”

< Isigiele 9 >