< Isigiele 46 >

1 Ouligisudafa Hina Gode da amane sia: sa, “Ganodini dibifufu ea gusudili logo ga: su da hawa: hamosu eso gafeyale amoga ga: si dialebe ba: ma: mu. Be Sa: bade eso amola Oubi Gaheabolo Lolo Nabe eso amoga doasima: mu.
“Ambuye Yehova akuti, Chipata chakummawa cha bwalo lamʼkati chizikhala chotseka pa masiku asanu ndi limodzi ogwira ntchito, koma chizitsekulidwa pa tsiku la sabata ndi pa tsiku la chikondwerero cha mwezi watsopano.
2 Ouligisu hina da gadili dibifufu amoga asili, logo holei sesei amoga golili sa: ili, amola gobele salasu dunu da ea ohe iasu amo gogo gobele salasea amola Hahawane Gilisili Olofole Iasu gobele salasea, e da logo holei mosomo ifa amoga dafulili lelumu. E da logo holei amogai nodone sia: ne gadolalu, bu gadili masunu. Logo ga: su da mae ga: sili dialeawane, daeya galu ga: simu.
Mfumu izilowa podzera mʼkhonde la mʼkati la chipata pochokera kunja, nʼkudzayima pafupi ndi nsanamira yapakhomo. Ansembe apereke nsembe yake yopsereza ndi nsembe yake yachiyanjano. Mfumuyo ipembedze pa chiwundo cha pa chipatacho kenaka nʼkutuluka. Koma chipatacho asachitseke mpaka madzulo.
3 Sa: bade huluane amola Oubi Gaheabolo Lolo Nabe huluane, amogai dunu huluanedafa da logo holei midadi, Hina Godema beguduli amola Ema nodone sia: ne gadoma: mu.
Anthu a mʼdziko azipembedza pamaso pa Yehova pa khomo la chipata chimenechi pa masiku a sabata ndi pa tsiku la mwezi watsopano.
4 Sa: bade esoga, ouligisu hina da Hina Godema, sibi mano gafeyale amola sibi gawali afae (huluane da foloai, noga: idafa) amo gogo gobele salimusa: , gaguli misa: mu.
Nsembe yopsereza imene mfumu iyenera kupereka kwa Yehova ikhale motere: pa tsiku la Sabata izipereka ana ankhosa aamuna asanu ndi mmodzi wopanda chilema, ndiponso nkhosa yayima yopanda chilema.
5 Sibi gawali afae afae amo gilisili gobele salimusa: , e da 14 gilogala: me gala: ine gaguli misa: mu. Amola sibi mano afae afae amo gilisili gobele salimusa: , e da ea hanaiga udigili iasu ima: mu. E da 14 gilogala: me gala: ine afae afae gaguli masea, amoga 3 lida olife susuligi gilisili gaguli misa: mu.
Pamodzi ndi nkhosa yayimuna, mfumu izipereka nsembe ya chakudya yokwanira efa imodzi. Pamodzi ndi ana ankhosa, mfumu izipereka monga ikufunira kutero. Iperekenso hini imodzi ya mafuta pa efa iliyonse ya tirigu.
6 Oubi Gaheabolo Lolo Nabe e da wahadebe bulamagau gawali, amola sibi mano gafeyale amola sibi gawali afae (huluane foloai noga: idafa) amo gobele salimusa: gaguli misa: mu.
Pa tsiku la mwezi watsopano mfumuyo ipereke mwana wangʼombe wamwamuna, ana ankhosa asanu ndi mmodzi ndiponso nkhosa yayimuna, zonsezi zopanda chilema.
7 E da musa: iasu gala: ine amola olife susuligi amo defele gilisili ima: mu.
Ipereke efa imodzi ya tirigu pa ngʼombe yayimuna iliyonse ndiponso efa ina pa nkhosa yayimuna iliyonse. Pa ana ankhosa ipereke tirigu monga ikufunira kutero. Pamodzi ndi efa ya tirigu, ipereke hini imodzi ya mafuta.
8 Ouligisu hina da logo holei sesei fisili, ea ganodini misi logo amoga bu gadili masa: mu.
Pamene mfumu ikulowa, izidzera mʼkhonde lamʼkati la chipata chakummawa, izitulukiranso pomwepo.
9 Dunu ilia da lolo nabe amoga Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: masea, ilia da ga (north) logo holeiga golili sa: ili, sia: ne gadoi dagosea, ilia da ga (south) logo holeiga amoga gadili masa: mu. Amola ilia da ga (south) logo holeiga golili sa: ili, sia: ne gadoi dagosea, ga (north) logo holeiga ga masa: mu. Ilia da ilia misi logo amoga bu ga masunu da sema bagade.
“Anthu a mʼdzikomo akabwera kudzapembedza Yehova pa masiku a chikondwerero, ngati munthu alowera pa chipata chakumpoto atulukire chipata chakummwera. Munthu wolowera chipata chakummwera, atulukire chipata chakumpoto. Munthu asatulukire pomwe walowera, koma atulukire pa chipata choyangʼanana nacho.
10 Dunu eno da ganodini golili dasea, ouligisu hina dunu, e amola da ganodini sa: imu. Amola, ilia da gadili ahoasea, e amola galu gadili masunu.
Mfumu izidzakhala pakati pawo. Anthu akamadzalowa mfumu idzalowa nawo. Anthu akamadzatuluka mfumu idzatuluka nawo.
11 Lolo Nabe eso huluane amoga Gala: ine Iasu gobele salasu da bulamagau gawali o sibi gawali amoga gilisimusa: gagoma 14 gilogala: me. Amola sibi mano gilisimusa: da sia: ne gadosu dunu ea hanaiga imunu. Gala: ine Iasu gobele salasu afae afae amoga olife susuligi3lida gilisima: ma.
“Pa masiku achikondwerero ndi pa masiku ena osankhidwa, zopereka za chakudya zikhale zokwanira efa imodzi pamodzi ndi ngʼombe yayimuna iliyonse, efa imodzinso ndi nkhosa yayimuna, koma pa mwana wankhosa apereke monga angathere. Iperekenso hini imodzi ya mafuta pa efa iliyonse.
12 Ouligisu hina da Hina Godema udigili gobele salasu imunusa: dawa: sea, (amo da mae dadega: le gogo gobele salasu o Hahawane Gilisili Olofole Iasu gobele salasu), ilia da e golili sa: ima: ne, ganodini dibifufu ea gusudili logo doasimu. E da Sa: bade eso gobele salasu hou defele hamomu. Amasea, e da ga ahoasea, ilia da logo ga: mu.
Pamene mfumu ikufuna kupereka chopereka chaufulu kwa Yehova, kaya ndi nsembe yopsereza kapena zopereka za chiyanjano, ayitsekulire chipata chakummawa. Iyo ipereke nsembe yopsereza kapena zopereka zake za chiyanjano monga imachitira pa tsiku la Sabata. Kenaka ituluke ndipo mfumuyo itatuluka, atseke chitsekocho.
13 Hina Gode da amane sia: sa, “Hahabe huluane, dilia da ode afae gidigi sibi mano (foloai amola noga: idafa fa: gi hamedei, olo hamedei) amo Hina Godema gogo gobele salima. Amo da eso huluanedafa hamoma: mu.
“Tsiku lililonse nthawi ya mmawa azipereka kwa Yehova mwana wankhosa wa chaka chimodzi.
14 Amola falaua 2 gilogala: me amo olife susuligi amoma gilisili, hahabe huluane gobele salima: mu. Amo gobele salasu malei da eso huluane, mae fisili, dialumu.
Pamodzi ndi nyamayo aziperekanso mmawa uliwonse chopereka cha chakudya chokwanira chimodzi mwa zigawo zisanu ndi chimodzi za efa. Aziperekanso chimodzi mwa zigawo zitatu za hini ya mafuta okandira ufa wosalala. Chopereka cha chakudya chimenechi chiziperekedwa kwa Yehova nthawi zonse mwa lamulo.
15 Sibi mano, amola falaua, amola olife susuligi da hahabe huluane, mae fisili, Hina Godema gobele salaloma: mu.
Motero azipereka mwana wankhosa ndi chopereka cha chakudya ndi mafuta mmawa uliwonse kuti zikhale nsembe zopsereza za tsiku ndi tsiku.
16 Ouligisudafa Hina Gode da dafawane hamoma: ne sia: sa, “Ouligisu hina da ea soge mogili egefe afae ema udigili iasea, egefe da amo soge gagulaligimu. Amo soge da ea sosogo fi ilia:
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ngati kalonga apereka mphatso chigawo cha cholowa chake kwa mmodzi mwa ana ake, mphatsoyo idzakhala ya ana akewo. Idzakhala yawo chifukwa ndi cholowa chawo.
17 Be ouligisu hina da ea hawa: hamosu dunuma ea soge afae iasea, bu Samogesu Ode doaga: sea, e da amo soge bu samogene, bu hina: soge ba: mu. E amola egefe ilia fawane da amo soge eso huluane gagui dialebe ba: mu.
Koma ngati ipereka mphatso yotere kuchokera pa cholowa chake kwa mmodzi mwa antchito ake, mphatsoyo idzakhala ya wantchitoyo mpaka chaka chaufulu. Pambuyo pake idzabwereranso kwa kalongayo chifukwa cholowa chake ndi cha ana ake.
18 Ouligisu hina da dunudafa ilia soge udigili lamu da sema bagade. E da soge egefe ema imunusa: dawa: sea, e da hi sogedafaga fawane imunu. E da dunudafa amo ilia soge udigili labeba: le, ili banenesimu da sema bagade.”
Kalonga asalande cholowa chilichonse cha anthu, kuwachotsa mʼdera lawo la dziko. Iye apereke kwa ana ake cholowa chawo chochokera pa chuma chakechake, kuti pasapezeke ndi mmodzi yemwe mwa anthu anga wolandidwa chuma chake.’”
19 Amalalu, amo dunu da na sesei amo da ga (north) ba: legai ganodini dibifufu ea ga (south) la: idi diala, amo ea gagili diasuga oule asi. Amo sesei da gobele salasu dunu esaloma: ne, hadigi ilegei. E da sogebi amo da sesei ea gududi la: idi dialebe, nama lobo sogone olei.
Kenaka munthu uja anandidzeretsa pa khomo la pambali pa chipata nandilowetsa ku zipinda za ansembe zoyangʼana kumpoto. Ndipo ndinaona kumeneko malo chakumadzulo kwa zipindazo.
20 E amane sia: i, “Amo sogebiga, gobele salasu dunu da hu amo da wadela: i hou dodofemusa: amola dabe imunusa: , amo gobema: mu amola falaua iasu ga: gima: mu. Bai amo liligi da hadigi amola sema. Amola dunu da amoga se nabasa: besa: le, gadili dibifufu amoga gaguli masunu da hamedei.”
Munthuyo anandiwuza kuti, “Awa ndi malo amene ansembe adzaphikirapo nsembe yopepesera kupalamula ndi nsembe yopepesera machimo. Kumenekonso azidzawotcherako chopereka cha chakudya. Sadzatuluka nazo zoyerazi mʼbwalo lakunja kuopa kuti angapatsireko kuyera anthu ena.”
Pambuyo pake anandilowetsa mʼbwalo lakunja napita nane ku ngodya zinayi za bwalolo. Ndipo ndinaona mʼkati mwa ngodya iliyonse bwalo lina.
22 Amalalu, e da na dibifufu gadili amoga oule asili, nama amo ea hegomai biyaduyale afae afae ganodini, dibifufu fofonobo ea seda defei 20.4 mida amola ea ba: de defei 14.4 mida amoga dialebe ba: i.
Motero pa ngodya zinayi za bwalo panalinso mabwalo ena angʼonoangʼono. Mabwalo amenewa anali ofanana. Mulitali mwake munali mamita makumi awiri ndipo mulifupi mwake munali mamita khumi ndi asanu.
23 Amo dibifufu afae afae da igiga gagoi, amola ea dobea danoma: ne da gobele nasu gasa: i dialebe ba: i.
Kuzungulira mabwalo anayi angʼonoangʼono aja panali mpanda wamiyala, ndi malo asonkhapo moto omangidwa mʼmunsi mwa mpandawo mozungulira.
24 Amo dunu da nama amane sia: i, “Amo da gobele nasu diasu. Amo ganodini Debolo hawa: hamosu dunu da gobele salasu liligi amo dunudafa da iaha, amo gobema: mu.”
Munthuyo anandiwuza kuti, “Izi ndi zipinda zophikiramo. Mʼmenemu anthu otumikira ku Nyumba ya Mulungu adzaphikiramo nyama za nsembe za anthu.”

< Isigiele 46 >