< Isigiele 30 >

1 Hina Gode da nama bu amane sia: i,
Yehova anandiyankhula kuti:
2 “Dunu egefe! Na, Ouligisudafa Hina Gode, Na sia: dunu huluane nabima: ne, amane wele sia: ma, ‘Beda: igia: su eso da mana.
“Iwe mwana wa munthu, nenera ndipo ulengeze zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena. “‘Ufuwule mawu awa akuti, ‘Kalanga, tsiku lafika!’
3 Hina Gode Ea hamomu eso da gadenesa. Amo esoga, soge fifi asi gala da se nabasu ginamei mobi agoai ba: mu.
Pakuti tsiku layandikira, tsiku la Yehova lili pafupi, tsiku la mitambo yakuda, tsiku lachiwonongeko cha mitundu ya anthu.
4 Idibidi soge da gegesu ba: mu. Sudane soge da se nabasu bagade ba: mu. Idibidi soge ganodini, dunu bagohame da medole legei dagoi ba: mu. Ilia liligi huluane amo enoga gegenana lai dagoi ba: mu. Amola ilia soge huluane, wadela: lesi dagoi ba: mu.
Lupanga lidzabwera kudzalimbana ndi Igupto ndipo mavuto adzafika pa Kusi. Pamene anthu ambiri adzaphedwa mu Igupto, chuma chake chidzatengedwa ndipo maziko ake adzagumuka.
5 Amo gegesu ganodini, bidiga lai dadi gagui dunu ilia da eno sogega hiougi (amo soge da Sudane, Lidia, Libia, Ala: ibia, Bade amola Na fi dunu Isala: ili) amo da medole lelegei dagoi ba: mu.’”
Kusi, Puti, Ludi ndi Arabiya yense, Libiya ndiponso anthu a mʼdziko logwirizana naye adzaphedwa ndi lupanga pamodzi ndi Igupto.
6 Hina Gode da amane sia: i, “Idibidi gaga: su dunu huluane, Migidole ga (north) soge amogainini asili, Asawane doaga: le, huluane da medole lelegei dagoi ba: mu. Idibidi hidasu dadi gagui gilisisu da wadela: lesi dagoi ba: mu. Na, Ouligisudafa Hina Gode da sia: i dagoi.
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: “‘Onse othandiza Igupto adzaphedwa ndipo kunyadira mphamvu zake kudzatheratu. Adzaphedwa ndi lupanga kuyambira ku Migidoli mpaka ku mzinda wa Asiwani,’” ndikutero Ine Ambuye Yehova.
7 Idibidi soge da wadela: lesi dagoi, eno soge huluane ilia wadela: su baligisawane ba: mu. Ea moilai huluane da wadela: lesidafa ba: mu.
“‘Dziko la Igupto lidzasanduka bwinja kupambana mabwinja ena onse opasuka, ndipo mizinda yake idzakhala yopasuka kupambana mizinda ina yonse.
8 Na da Idibidi soge laluga ulagisia, amola ea gaga: su dunu huluane medole legei dagoi ba: sea, ilia da Na da Hina Gode dawa: mu.
Nditatha kutentha Igupto ndi kupha onse omuthandiza, pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
9 Amo eso doaga: sea, amola Idibidi soge da wadela: lesi dagoi ba: sea, Na da Sudane mae dawa: le esalebe dunu ilima dusagai da: iya sia: adola ahoasu dunu asunasimu. Ilia sia: nabasea, beda: ga fofogadigimu. Amo eso da mana.”
“‘Nthawi imeneyo ikadzafika, amithenga adzapita mofulumira kuchokera kwa Ine kukaopseza Kusi, iwowo osadziwako kanthu. Ndipo adzada nkhawa pa tsiku limene Igupto adzawonongedwa, chifukwa tsikulo lidzafika ndithu.
10 Ouligisudafa Hina Gode da amane sia: sa, “Na da Ba: bilone hina bagade, Nebiuga: denese, ema e da Idibidi doagala: le, ea bagade gagui hou dagolisima: ne sia: mu.
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Ndidzagwiritsa ntchito Nebukadinezara, mfumu ya ku Babuloni kuti ndithetse gulu lankhondo la Igupto.
11 E amola ea nimi bagade dadi gagui wa: i da soge wadela: musa: misunu. Ilia da gegesu gobihei bagade gaguli, Idibidi doagala: mu. Idibidi soge da bogoi da: i hodo amoga nabai ba: mu.
Iye ndi gulu lake lankhondo, mtundu wa anthu ankhanza kwambiri aja adzabwera kudzawononga dzikolo. Adzasolola malupanga awo kulimbana ndi Igupto ndipo dziko lidzadzaza ndi mitembo.
12 Na da Naile Hano hale hafoga: lesili, Idibidi fi amo wadela: i dunu amoga iagamu. Ga fi dunu da soge huluane gugunufinisimu. Na, Hina Gode da sia: i dagoi.”
Ndidzawumitsa mtsinje wa Nailo ndi kugulitsa dziko la Igupto kwa anthu oyipa. Ndidzagwiritsa ntchito anthu achilendo kuti ndiwononge dzikolo pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo. Ine Yehova ndayankhula.
13 Hina Gode da amane sia: sa, “Na da Memefisi moilai bai bagade ilia loboga hamoi ‘gode’, amola ogogosu ‘gode’ huluane wadela: lesimu. Idibidi ouligisu dunu da hame ba: mu, amola Na da dunu huluane beda: gia: ma: ne hamomu.
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Ndidzawononga mafano ndi kuthetsa milungu yosema ya ku Mefisi. Simudzakhalanso mfumu mu Igupto, ndipo ndidzaopseza dziko lonse.
14 Na da Idibidi ga (south) soge wadela: lesimu, amola Soua: ne moilai bai bagade gadili (north) diala amo laluga ulagisimu. Na da Idibidi bisilua moilai bai bagade amo Dibisi, amoma se bidi imunu.
Ndidzasandutsa chipululu mzinda wa Patirosi, ndi kutentha mzinda wa Zowani. Ndidzalanga mzinda wa Thebesi.
15 Idibidi gagili sali moilai bai bagade, amo Belusiame da Na ougi ba: mu. Na da Dibisi ea gagui liligi wadela: lesimu.
Ndidzakhuthulira ukali wanga pa mzinda wa Peluziumu, linga lolimba la Igupto, ndi kuwononga gulu lankhondo la Thebesi.
16 Na da Idibidi laluga ulagisimu, amola Belusiame da se bagade nabimu. Dibisi gagoi da mugului dagoi ba: mu, amola moilai da hanoga dedeboi dagoi ba: mu.
Ndidzatentha ndi moto dziko la Igupto; Peluziumu adzazunzika ndi ululu. Malinga a Thebesi adzagumuka, ndipo mzindawo udzasefukira ndi madzi.
17 Hilioubalisi amola Bibisede moilai bai bagade ayeligi dunu da gegesu ganodini bogogia: mu, amola dunu oda da afugili oule asi dagoi ba: mu.
Anyamata a ku Oni ndi ku Pibeseti adzaphedwa ndi lupanga ndipo okhala mʼmizinda yake adzatengedwa ukapolo.
18 Na da Idibidi ilia gasa fili gasa hou wadela: sea, Daha: banisi gagili sali moilai da gasi fawane ba: mu. Mobi ginamei da Idibidi soge dedebomu, amola ea moilai fi dunu huluane da afugili oule asi dagoi ba: mu.
Ku Tehafinehezi kudzakhala mdima pamene ndidzathyola goli la Igupto; motero kunyada kwake kudzatha. Iye adzaphimbidwa ndi mitambo yakuda, ndipo okhala mʼmizinda yake adzapita ku ukapolo.
19 Na da Idibidi fi ilima se bidi agoane iasea, ilia da Na da Hina Gode dawa: mu.”
Kotero ndidzalanga dziko la Igupto, ndipo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”
20 Eso fesu amola oubi age amola ode gida amoga ninia mugululi misi, Hina Gode da nama amane sia: i,
Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri la mwezi woyamba wa chaka chakhumi ndi chimodzi, Yehova anandiyankhula kuti:
21 “Dunu egefe! Na Idibidi hina bagade ea lobo gasa fi dagoi. Dunu afaega ea lobo ili gadole abulaga hame la: gilisi. Amaiba: le, amo uhini amola gegesu gobihei bu gegemusa: gagumu da hamedei.
“Iwe mwana wa munthu, ndathyola dzanja la Farao mfumu ya Igupto. Taona, silinamangidwe kuti lipole, ngakhale kulilimbitsa ndi nsalu kuti lithe kugwiranso lupanga.
22 Amalu, wali, Na, Ouligisudafa Hina Gode, da amane sia: sa, ‘Na da Idibidi hina bagade ema ha lai. Na da ea lobo aduna filisimu - musa: fi lobo amola ele galu filisimu. Amasea, gegesu gobihei bagade da ea lobo gagui habonane sa: imu.
Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti, Ine ndikudana ndi Farao mfumu ya Igupto. Ndidzathyola manja ake onse; dzanja labwino pamodzi ndi lothyokalo, ndipo lupanga lidzagwa mʼmanja mwake.
23 Na da Idibidi fi dunu amo fifi asi gala huluane amoga afagogolesimu.
Ndidzamwaza Aigupto pakati pa mitundu ya anthu ndikuwabalalitsira ku mayiko ambiri.
24 Amasea, Na da Ba: bilone hina bagade ema gasa iawane, Na gegesu gobihei ea lobo da: iya ligisimu. Be Na da Idibidi hina bagade ea lobo fifilisimu. Amola ea ha lai dunu ea midadi, e da gogonomonanu bogomu.
Ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babuloni, ndipo mʼmanja mwake ndidzayikamo lupanga langa. Koma ndidzathyola manja a Farao, ndipo adzabuwula ngati wolasidwa koopsa pamaso pa mfumu ya ku Babuloniyo.
25 Dafawane! Na da ea gasa wadela: lesimu, be Ba: bilone hina bagade ema gasa imunu. Na da ema Na gegesu gobihei iasili, amola e da amoga Idibidi fi dunuma sosiagasea, dunu huluanedafa da Na da Hina Gode dawa: mu.
Ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babuloni, koma manja a Farao adzafowoka. Motero anthu adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzayika lupanga langa mʼmanja mwa mfumu ya ku Babuloni. Ndipo adzaligwiritsa ntchito pothira nkhondo dziko la Igupto.
26 Na da Idibidi fi dunu amo gadili se fasili, ili fifi asi gala huluane amo ganodini esaloma: ne afagogolesimu. Amasea, ilia da Na da Hina Gode dawa: mu.”
Ndidzamwaza Aigupto pakati pa mitundu ya anthu, ndikuwabalalitsira ku mayiko ambiri. Motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”

< Isigiele 30 >