< Isigiele 28 >
1 Hina Gode da nama amane sia: i,
Yehova anandiyankhula nati:
2 “Dunu egefe! Daia hina bagade ema, Na, Ouligisudafa Hina Gode, da ema amane sia: sa, amo ema adosima, ‘Di da gasa fifili, di da ‘gode’ dina: sia: sa. Di da ‘gode’ defele, dia fisu da: iya fili amola hano wayabo bagade huluane da dia fisu sisiga: sa, amo dina: di sia: sa. Di da ogogole,’ na da ‘gode’ sia: sa, be di da ‘gode’ hame. Di da osobo bagade dunu fawane.
“Iwe mwana wa munthu, iwuze mfumu ya ku Turo mawu a Ine Ambuye Yehova akuti, “‘Iwe ndi mtima wako wodzikuza umanena kuti, ‘Ine ndine mulungu; ndimakhala pa mpando wa mulungu pakati pa nyanja.’ Koma ndiwe munthu chabe osati mulungu, ngakhale ukuganiza kuti ndiwe wanzeru ngati mulungu.
3 Di da dia asigi dawa: su da Da: niele ea asigi dawa: su baligisa, amo dia dawa: sa. Di da dunu huluane ilia wamolegei hou ba: sa, amo disu dawa: lala.
Taona, ndiwedi wanzeru kupambana Danieli. Ndipo palibe chinsinsi chobisika kwa iwe.
4 Dia dawa: lai amola hahamosu dawa: amoga hawa: hamobeba: le, di da gouli amola silifa bagade lale, bagade gagui agoane ba: sa.
Mwa nzeru zako ndi kumvetsa kwako unadzipezera chuma ndipo unasonkhanitsa golide ndi siliva mʼnyumba zosungira chuma chako.
5 Di da bidi lasu hou hamobeba: le, muni baligili lalu. Di da dia bagade gagui hou dawa: beba: le, hidale dawa: lala.
Ndi nzeru zako zochitira malonda unachulukitsa chuma chako ndipo wayamba kunyada chifukwa cha chuma chakocho.
6 Be wali, Na, Ouligisudafa Hina Gode, da amane sia: sa,’ Dia da dia dawa: lai da ‘gode’ ea dawa: lai defele gala dawa: beba: le,
“‘Choncho Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Popeza umadziganizira kuti ndiwe mulungu,
7 Na da ougi nimi bagade ha lai dunu dima doagala: musa: oule misunu. Ilia da dia liligi noga: iwane di da dia dawa: lai amola hahamosu dawa: amoga lai, amo huluane wadela: lesimu.
Ine ndidzabwera ndi anthu achilendo, anthu ankhanza, kuti adzalimbane nawe. Adzakuthira nkhondo kuti awononge zonse zimene unazipeza ndi nzeru zako, ndipo adzawononga kunyada kwakoko.
8 Ilia da di medole legele, hano wayabo bagadega sanasimu.
Iwo adzakuponyera ku dzenje ndipo udzafa imfa yoopsa mʼnyanja yozama.
9 Ilia da di famusa: masea, di da ‘na da gode’ sia: ma: bela: ? Amo esoha, di medole legesu dunu odagi gadenesea, di da ‘gode’ hame be osobo bagade dunu fawane esala, amo noga: le dawa: mu.
Kodi udzanenabe kuti, ‘Ine ndine mulungu,’ pamaso pa iwo amene akukupha? Iwe udzaoneka kuti ndiwe munthu chabe, osati mulungu, mʼmanja mwa iwo amene akukuphawo.
10 Di da wa: me ea bogoi amo defele, Gode Ea hou hame lalegagui ga fi dunu ilia lobo da: iya bogomu. Na, Ouligisudafa Hina Gode, da ilima amo hamoma: ne sia: beba: le, ilia da di medole legemu.”
Udzafa imfa ya anthu osachita mdulidwe mʼmanja mwa anthu achilendo. Ine ndayankhula zimenezi, akutero Ambuye Yehova.’”
11 Hina Gode da bu nama amane sia: i,
Yehova anandiyankhula kuti:
12 “Dunu egefe! Daia hina bagade da dafamuba: le, gogolole dawa: ma. Na, Ouligisudafa Hina Gode, da amane sia: sa, amo ema adosima, ‘Di da musa: eno dunu dawa: digima: ne, moloidafawane esalu. Di da bagade dawa: su amola ayeligi da: da: loiwane ba: su esalu.
“Iwe mwana wa munthu, imba nyimbo yodandaulira mfumu ya Turo ndipo uyiwuze mawu a Ine Ambuye Yehova akuti, “‘Iwe unali chitsanzo cha ungwiro weniweni, wodzaza ndi nzeru ndi wokongola kwambiri.
13 Di da Gode Ea ifabi amo Idini soge ganodini esalu. Di da igi ida: iwane gala gaga: si amo (lubi amola daimode, douba: se, belole, ganiliane, ya: seba, sa: faia, emelalede amola ganedi). Di da nina: hamoi liligi gouliga hamoi galu. Na da amo liligi dia hahamoi eso amoga digili i.
Iwe unkakhala ngati mu Edeni, munda wa Mulungu. Miyala yokongola ya mitundu yonse: rubi, topazi ndi dayimondi, kirisoliti, onikisi, yasipa, safiro, kalineliyoni ndi berili ndiwo inali zofunda zako. Ndipo zoyikamo miyalayo zinali zagolide. Anakupangira zonsezi pa tsiku limene unalengedwa.
14 Na da a: igele (amoga dunu da beda: i), di sosodo ouligima: ne, amogawi leloma: ne asunasi. Di da Na hadigi goumia esalu, nenema: gi igi ida: iwane dialebe amo ganodini golili ahoasu.
Ndinayika kerubi kuti azikulondera. Unkakhala pa phiri langa lopatulika, ndipo unkayendayenda pakati pa miyala ya moto.
15 Di da dia hahamoi eso amogainini moloidafa hou hamosu. Be di da bu wadela: i hou muni hamosu.
Makhalidwe ako anali abwino kuyambira pamene unalengedwa mpaka nthawi imene unayamba kuchita zoyipa.
16 Di da bidi lasu bagade hamobeba: le, bu ogogosu amola bidi hamoi hamosu. Amaiba: le, Na da di Na hadigi goumi amoga fadegai. Amola a: igele amo da di sosodo ouligi lelu, da di igi nenemigi sogebiga sefasi.
Unatanganidwa ndi zamalonda. Zotsatira zake zinali zoti unachulukitsa zandewu ndi kumachimwa. Choncho ndinakuchotsa ku phiri langa lopatulika. Mkerubi amene ankakulondera uja anakupirikitsa kukuchotsa ku miyala yamoto.
17 Dia ba: su da isisima: goiba: le, di da hidale hamoi. Amola, eno dunu da dima nodoiba: le, di da gagaoui ba: i. Amaiba: le eno hina bagade dunu dawa: digima: ne, Na da di osobo gudu gisalugala: i. Ilia da amo sisasu ba: ma: ne.
Unkadzikuza mu mtima mwako chifukwa cha kukongola kwako, ndipo unayipitsa nzeru zako chifukwa chofuna kutchuka. Kotero Ine ndinakugwetsa pansi kuti ukhala chenjezo pamaso pa mafumu.
18 Di da wadela: ledafa bidi lasu hou hamobeba: le, dia nodone sia: ne gadosu sogebi huluane da ledo bagade ba: i. Amaiba: le, Na da dia moilai huluane laluga ulagisili, nene sa: i dagoi. Dunu huluane wali dima ba: sea, da nasubu fawane ba: sa.
Ndi malonda ako achinyengo unachulukitsa machimo ako. Motero unayipitsa malo ako achipembedzo. Choncho ndinabutsa moto pakati pako, ndipo unakupsereza, ndipo unasanduka phulusa pa dziko lapansi pamaso pa anthu onse amene amakuona.
19 Di da bu mae ba: ma: ne, asi dagoi. Amola fifi asi gala huluane da di dawa: i, amo da beda: gia: sa. Bai dima doaga: i hou da ilima doaga: sa: besa: le, ilia da beda: i.”
Anthu onse amitundu amene ankakudziwa akuchita mantha chifukwa cha iwe. Watheratu mochititsa mantha ndipo sudzakhalaponso mpaka muyaya.’”
20 Hina Gode da nama amane sia: i,
Yehova anandiyankhula nati:
21 “Dunu egefe! Saidone moilai bai bagade amoma se ima: ne mimogoa diwaneya udidima!
“Iwe mwana wa munthu, utembenukire ku mzinda wa Sidoni ndipo unenere mowudzudzula kuti,
22 Saidone fi ilima Na, Ouligisudafa Hina Gode da ilia hou olelema: ne amane sia: sa, amo adosima, ‘Saidone! Na da dia ha lai. Na da dima se bidi iasea, dunu eno da Nama nodomu. Na da di amo ganodini esala dunu ilima Na hadigi olelema: ne se bidi iasea, ilia da Na da Hina Gode dawa: mu.
‘Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Ndine mdani wako, iwe Sidoni, ndipo ndidzalemekezedwa chifukwa cha iwe. Anthu adzadziwa kuti Ine ndine Yehova ndikadzakulanga ndi kudzionetsa kuti ndine woyera pakati pako.
23 Na da dima olo iasimu. Amola Na hamobeba: le, maga: me da dia logo ganodini bagade a: iahoabe ba: mu. Eno dunu da la: di huluane amoga misini dima doagala: mu, amola dia fi dunu da medole legei dagoi ba: mu. Amasea, di da Na da Hina Gode dawa: mu.”
Ndidzatumiza mliri pa iwe ndi kuchititsa magazi kuti ayende mʼmisewu yako. Anthu ophedwa ndi lupanga adzagwa mbali zonse. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
24 Hina Gode da amane sia: i, “Fifi asi gala amo Isala: ili sisiga: i, ilia da Isala: ili fi amo higabeba: le, ilima se bagade iasu. Be ilia agoaiwane bu hamedafa hamomu. Amola ilia da Na da Ouligisudafa Hina Gode dawa: mu.”
“‘Nthawi imeneyo Aisraeli sadzakhalanso ndi anthu pafupi achipongwe amene ali ngati nthula zowawa ndi ngati minga zopweteka. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.
25 Ouligisudafa Hina Gode da amane sia: i, “Na da Isala: ili fi dunu amo fifi asi gala amoga, Na da ili afagogoi, amoga lale, ilia sogedafa buhagima: ne oule misunu. Amasea, fifi asi gala huluane da Na da Hadigi dawa: mu. Isala: ili fi dunu da ilia sogedafa amo Na da musa: Na hawa: hamosu dunu Ya: igobema i, amo ganodini esalumu.
“‘Ine Ambuye Yehova mawu anga ndi awa: Nditasonkhanitsa Aisraeli kuchoka ku mayiko kumene anamwazikira, ndidzadzionetsa kuti ndine woyera pakati pawo pamaso pa anthu a mitundu ina. Adzakhala mʼdziko lawo, limene ndinalipereka kwa mtumiki wanga Yakobo.
26 Ilia da amo ganodini hahawane gaga: lewane esalumu. Ilia da diasu gagumu amola waini efe sagamu. Ilia na: iyado fi dunu amo da ilima higasu, ilima Na da se bidi imunu. Amola Isala: ili fi da gaga: i dagoi ba: mu. Amasea, ilia da Na da ilia Hina Gode dawa: mu.”
Adzakhala kumeneko mwamtendere ndipo adzamanga nyumba ndi kulima minda ya mpesa. Adzakhala kumeneko mwamtendere pamene ndidzalange anthu oyandikana nawo, amene ankawanyoza. Motero iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wawo.’”