< Isigiele 15 >

1 Hina Gode da nama amane sia: i,
Yehova anayankhulanso nane kuti,
2 “Dunu egefe! Efe da ifala abuli defebela: ? Waini efe ea amoda da iwila ifala abuli defebela: ?
“Iwe mwana wa munthu, kodi mtengo wamphesa umapambana bwanji mtengo wina uliwonse? Nthambi zake zimapambana bwanji nthambi ina iliyonse.
3 Amo efega liligi noga: i hamoma: bela: ? Amoga liligi gosagimusa: ma: go hamoma: bela: ?
Mtengo umene uja nʼkupangira chiyani? Kodi anthu angathe kupangira chikhomo chokolekapo zinthu zawo?
4 Waini efe da lalu didimu fawane defele gala. Amo ea bidi da nei dagoi amola dogoa da genosuia: i galea, amoga liligi hamomu ganoma: bela: ?
Taonani, ndi nkhuni chabe zosonkhera moto. Ukaponyedwa pa moto monga nkhuni ndi kuyaka mbali zonse ndi kusanduka makala, kodi ungagwiritsidwe ntchito ina iliyonse?
5 Amo liligi da hame neiya amolawane amoga liligi hamomu hamedei. Be laluga nebeba: le, baligiliwane hamedei ba: sa.”
Ngati pamene unali wosapsa sukanatheka kuwugwiritsa ntchito, nanga bwanji utapserera ndi moto, adzawugwiritsa ntchito bwanji?
6 Wali, Ouligisu Hina Gode da amane sia: sa, “Dunu da efe amo iwilaga lale, gobesea, amo defele, Na da Yelusaleme fi dunu fadegale,
“Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Mtengo wamphesa ndidzawuponya mʼmoto monga ndimachitira ndi mitengo ina ya ku nkhalango. Momwemonso ndidzachita ndi anthu a ku Yerusalemu.
7 amola ilima se dabe imunu. Ilia da lalu afae amoba: le hobea: i dagoi. Be amomane, lalu eno da ili nene dagomu. Na da ilima se bidi iasea, Na da Hina Gode dia da dawa: mu.
Ndidzawalanga pamenepo ngakhale iwo atuluka pa moto, motowo udzawatenthabe. Ndipo pamene ndidzatsutsana nawo, mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
8 Ilia da Nama fa: no bobogelalu yolesi. Amaiba: le, Na da ilia soge gugunufinisimu.” Ouligisudafa Hina Gode da sia: i dagoi.
Ine ndidzasandutsa dziko kukhala chipululu chifukwa anthu akhala osakhulupirika, akutero Ambuye Yehova.’”

< Isigiele 15 >