< Gadili Asi 8 >

1 Amalalu, Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Felouma masa! Ema amane sia: ma, “Hina Gode da amane sia: sa, ‘Na dunu fi di gagui amo Nama nodone sia: ne gadomusa: fisidigima.
Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Ukamuwuze Farao kuti, Lolani anthu anga kuti apite, akandipembedze.
2 Di da higasea, Na da dia sogega se iasimu. Soge huluane da guama amoga dedeboi dagoi ba: mu.
Ndipo ngati simulola kuti apite Ine ndidzalanga dziko lonse la Igupto polidzaza ndi achule.
3 Naile Hano da guama amoga nabaidafa ba: mu. Amasea, guama da hano yolesili, dia diasu amola dia debea amoga heda: mu. Ilia da dia eagene ouligisu dunu amola ilia diasuga masunu. Amola ilia dilia ha: i manu ofodo amola gobele nasu amo ganodini ba: mu.
Mtsinje wa Nailo udzadzaza ndi achule. Achulewo adzatuluka ndi kukalowa mʼnyumba yaufumu, ku chipinda chogona ndi pa bedi lako, mʼnyumba za nduna zako ndi pa anthu ako ndi mophikira buledi ndiponso mopangira bulediyo.
4 Ilia da di, dia fi dunu amola dia ouligisu dunu ilima soagala: le, fila heda: mu.
Achulewo adzakulumphira iwe ndi anthu ako ndiponso nduna zako.”
5 Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Di Elanema ea dagulu lale, hano amola hano logo amola hano wayabo huluane amo da: iya ea dagulu ligia gadoma: ne sia: ma. Guama da heda: le, Idibidi soge huluane dedeboma: ne sia: ma.”
Ndipo Yehova anati kwa Mose, “Uza Aaroni kuti, ‘Loza ndodo yako ku mitsinje, ku ngalande ndi ku zithaphwi ndipo pakhale achule pa dziko lonse la Igupto.’”
6 Amalalu, Elane da ea dagulu hano da: iya ligia gadoi. Amola guama da heda: le, Idibidi soge huluane dedeboi.
Kotero Aaroni analoza dzanja lake pa madzi a ku Igupto, ndipo achule anatuluka nadzaza dziko lonse la Igupto.
7 Be Felou ea fefedoasu dawa: dunu da ilia hou hamobeba: le, guama da heda: i.
Koma amatsenga anachita zinthu zomwezo mʼmatsenga awo. Iwonso anatulutsa achule mʼdziko lonse la Igupto.
8 Felou da Mousese amola Elane misa: ne sia: i. E da elama amane sia: i, “Alia Hina Godema E da amo guama sefasima: ne sia: ne gadoma. Amasea, na da dia fi ilia da Godema gobele salasu hou hamoma: ne, logo doasimu.”
Kenaka, Farao anayitanitsa Mose ndi Aaroni ndipo anati, “Pemphera kwa Yehova kuti achulewa achoke kwa ine ndi anthu anga, ndipo ine ndidzalola kuti anthu anu apite kukapereka nsembe kwa Yehova.”
9 Mousese da bu adole i, “Na da di, dia ouligisu dunu amola dia fi dunu amo fidima: ne hahawane Godema sia: ne gadomu. Na sia: ne gadoma: ne, di eso ilegema. Amasea, guama huluane da fadegale, Naile Hano amo ganodini fawane guama ba: mu.”
Mose anati kwa Farao, “Inu mungonditchulira nthawi imene mukufuna kuti ndikupempherereni, nduna zanu pamodzi ndi anthu anu kuti achule achoke mʼnyumba zanu ndi kuti atsale okhawo ali mu mtsinje wa Nailo.”
10 Felou da bu adole i, “Dia na fidima: ne, aya sia: ne gadoma!” Mousese da amane sia: i, “Dia adole ba: i defele na da hamomu. Amasea, ‘gode’ eno ninia Hina Gode defele da hamedafa gala, amo di da dawa: mu.
Farao anati, “Mawa.” Mose anamuyankha kuti, “Chabwino zidzakhala monga mwaneneramu, kuti mudzadziwe kuti palibe wina wofanana ndi Yehova Mulungu wathu.
11 Di, dia eagene ouligisu dunu amola dia fi huluane da guama afia: i dagoi ba: mu. Naile Hano ganodini fawane da guama ba: mu.
Achule adzachoka mʼnyumba yanu, mʼnyumba za nduna zanu pamodzi ndi za anthu anu. Koma adzatsala mu mtsinje wa Nailo basi.”
12 Amalalu, Mousese amola Elane da Felou yolesili, asili Hina Gode da guama sefasima: ne, Ema sia: ne gadoi.
Mose ndi Aaroni anachoka, ndipo Mose anapemphera kwa Yehova kuti achotse achule amene anatumiza kwa Farao.
13 Hina Gode da Mousese ea sia: ne gadoi defele hamoi. Guama huluane diasu amola gagoi amola ifabi amo ganodini esafulu da bogogia: i dagoi.
Ndipo Yehova anachita zomwe Mose anapempha. Achule amene anali mʼnyumba, mʼmabwalo ndi mʼminda anafa
14 Idibidi dunu da guama bogoi amo gilisili ligisi biba heda: i dialu. Soge huluane da gaha bagade nabi.
Aigupto anawunjika achulewo milumilu ndipo dziko linanunkha.
15 Be Felou da guama bogoi dagoi ba: beba: le, ea dogo da bu igi agoane hamoi. Hina Gode Ea sia: i defele, e da Mousese amola Elane ela sia: hame nabi.
Koma Farao ataona kuti zinthu zinayambanso kukhala bwino, anawumitsanso mtima wake ndipo sanamverenso mawu a Mose ndi Aaroni, monga momwe Yehova ananenera.
16 Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Di Elanema amane sia: ma. E da ea daguluga osoba fama. Amasea osobo su Idibidi soge huluane amo ganodini da afadenene mimini ba: mu.”
Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Uza Aaroni kuti akweze ndodo yake ndi kumenya fumbi la pa nthaka, ndipo fumbilo lidzasanduka nsabwe pa dziko lonse la Igupto.”
17 Amaiba: le, Elane da ea daguluga osobo fai. Osobo su Idibidi soge ganodini huluane da afadenene mimini hamoi. Ilia da dunu amola ohe fi amo da: iya fila heda: le dedeboi dagoi.
Iwo anachita momwemo, ndipo pamene Aaroni anakweza ndodo yake ndi kumenya fumbi, nsabwe zinafika pa munthu aliyense ndi pa ziweto. Fumbi lonse la mʼdziko la Igupto linasanduka nsabwe.
18 Idibidi fefedoasu dunu da gasa fili mimini hamomusa: hamonanu. Be hamedei. Mimini da bagohame soge huluane ganodini ba: i.
Koma amatsenga atayesa kupanga nsabwe mwa matsenga awo, analephera. Ndipo nsabwezo zinali pa munthu aliyense ndi pa ziweto zawo.
19 Idibidi fefedoasu dunu da Felouma amane sia: i, “Gode Hi da amo hou hamoi.” Be Felou ea dogo da ga: nasi hamoi. E da Hina Gode Ea sia: i defele, Mousese amola Elane ela sia: hame nabi.
Amatsenga anati kwa Farao, “Izi wachita ndi Mulungu.” Koma mtima wa Farao unali wowumabe ndipo sanamvere zonena za Mose ndi Aaroni monga momwe Yehova ananenera.
20 Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Hahabedafa, Felou da Naile Hano amoga ahoanumu. Di ema ba: la masa. Ema amane sia: ma, ‘Hina Gode da agoane sia: sa, Na fi dunu da Nama nodone sia: ne gadomusa: , di ili ga masa: ne fisidigima.
Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Mmawa, upite ukakumane ndi Farao maso ndi maso pamene azidzapita ku madzi ndipo ukanene kuti, ‘Yehova akuti, Lola anthu anga kuti apite akandipembedze.
21 Na da dima sisasa. Di da fisidigimu higasea, Na da dima se nabasu imunu. Na da fane dima amola dia eagene ouligisu dunuma amola dia fi dunu huluane ilima asunasimu. Idibidi dunu ilia diasu huluane da fane amoga nabai ba: mu. Amola Idibidi soge osobo huluane da fane amoga dedeboi dagoi ba: mu.
Koma ngati suwalola anthu anga kuti apite, Ine ndidzatumiza pa iwe ntchentche zoluma ndi pa nduna zako ndi anthu ako ndi mʼnyumba zanu. Mʼnyumba za Aigupto mudzadzaza ntchentche zoluma. Ngakhale pa nthaka pamene akhalapo padzadzaza ndi ntchentche zoluma.’”
22 Be Gousiene amo Na fi ilia esalebe soge amoga Na da fane hame asunasimu. Di da Na, Hina Gode, da amo hou hamonanebe dawa: ma: ne, Na da Na fi amola dia fi hisu ba: sa. Amo musa: hame ba: su hou da aya ba: mu.”
“Koma pa tsikulo ndidzapatula dera la Goseni, kumene kumakhala anthu anga, motero kuti sikudzakhala ntchentche zoluma. Choncho iwe udzadziwa kuti Ine Yehova ndi amene ndikulamulira dziko lino.
Ndidzasiyanitsa pakati pa anthu anga ndi anthu ako. Chizindikiro chozizwitsa ichi chidzachitika mawa.”
24 Hina Gode da fane gilisisu bagohame amo Felou ea diasuga amola eagene ouligisu dunu ilia diasuga asunasi. Fane idimu hamedeidafa misiba: le, Idibidi soge huluane da gugunufinisi dagoi ba: i.
Ndipo Yehova anachita zimenezi: Ntchentche zoluma zochuluka zinalowa mʼnyumba yaufumu ya Farao ndi nyumba za nduna zake. Choncho ntchentche zolumazi zinawononga dziko lonse la Igupto.
25 Amalalu, Felou da Mousese amola Elane ema misa: ne sia: i. E da elama amane sia: i, “Defea! Dilia Hina Godema gobele salasu hou hamoma: ne, Idibidi soge ganodini hamomusa: masa.”
Kenaka Farao anayitanitsa Mose ndi Aaroni nati, “Pitani kaperekeni nsembe kwa Mulungu wanu mʼdziko lomwe lino.”
26 Be Mousese da bu adole i, “Agoane hamosea da moloi hame ba: mu. Ninia ohe fi amo gobele salasu hamoma: ne medole legesea, Idibidi dunu da higa: i ba: mu. Amo hou ninia Idibidi dunu ilia siga ba: ma: ne hamosea, ilia da amo hou higa: iba: le, nini igiga gala: le legemu.”
Koma Mose anati, “Sitingathe kutero pakuti nsembe zathu kwa Yehova Mulungu ndi zowayipira Aigupto. Ngati tipereke nsembe zowayipira Aigupto mʼmaso mwawo, adzatiponya miyala kuti tife.
27 Logo afae fawane gala. Ninia da eso udiana amo wadela: i hafoga: i soge ganodini ga ahoasea, ninia Hina Gode Ea sia: defele, Ema gobele salasu hamomu.”
Ife tiyenera kuyenda ulendo wa masiku atatu kupita ku chipululu kukapereka nsembe kwa Yehova Mulungu wathu monga anatilamulira.”
28 Felou da amane sia: i, “Defea! Dilia Hina Godema gobele salasu hamoma: ne, wadela: i hafoga: i sogega masunu da defea. Be sedagaga mae masa. Amola na fidima: ne Godema sia: ne gadoma.”
Farao anati, “Ine ndikulolani kuti mupite ku chipululu kukapereka nsembe kwa Yehova Mulungu wanu, koma musapite kutali kwambiri. Tsopano ndipempherereni.”
29 Mousese da bu adole i, “Na da ga ahoasea, na da Hina Godema E da fane amo dima, dia eagene ouligisu dunuma amola dia fi huluane ilima fisili sefasima: ne sia: mu. Be di da ninia fi ilia Hina Godema gobele salasu hamoma: ne masunu logo damumusa: , ninima bu mae ogogoma.”
Mose anayankha kuti, “Ine ndikangochoka pano, ndikapemphera kwa Yehova ndipo mawa lomweli ntchentche zoluma zidzachoka kwa Farao, nduna zake pamodzi ndi anthu ake. Koma Farao, onetsetsani kuti musachitenso zachinyengo ndi kuwakaniza anthu kuti asakapereke nsembe kwa Yehova.”
30 Mousese da Felou yolesili asili, Godema sia: ne gadoi.
Choncho Mose anasiyana ndi Farao nakapemphera kwa Yehova.
31 Amola Hina Gode da Mousese ea adole ba: su defele hamoi dagoi. Fane huluane da Felou, ea eagene ouligisu dunu amola ea fi dunu huluane yolesi dagoi. Fane afae esalebe da hamedafa ba: i.
Ndipo Yehova anachita zomwe Mose anapempha: Ntchentche zoluma zinachoka kwa Farao ndi nduna zake ndiponso kwa anthu ake. Palibe ngakhale imodzi yomwe inatsala.
32 Be Felou da bu eno ea dogo ga: nasi hamoi. E da Isala: ili dunu ga fisili masa: ne hame fisidigi.
Koma nthawi imeneyinso Farao anawumitsa mtima wake ndipo sanalole kuti anthu atuluke.

< Gadili Asi 8 >