< Gadili Asi 4 >

1 Amalalu, Mousese da Hina Godema amane adole i, “Be Isala: ili dunu da na sia: dafawaneyale hame dawa: sea amola na sia: hame nabasea, na da adi hamoma: bela: ? Ilia da Di da nama hame misi amo sia: sea, na da adi hamoma: bela: ?”
Mose anayankha, “Aisraeliwo sakandikhulupirira ndipo sakandimvera. Iwowo adzati, ‘Yehova sanakuonekere iwe.’”
2 Amaiba: le, Hina Gode da ema amane adole ba: i, “Dia loboga gagui da adila: ?” E bu adole i, “Amo da dagulu.”
Ndipo Yehova anamufunsa nati, “Nʼchiyani chili mʼdzanja lakolo?” Mose anayankha kuti, “Ndodo.”
3 Hina Gode da amane sia: i, “Amo dagulu osoboga ligia guduma!” Mousese da ligia guduli, dagulu da afadenene bu sa: ya: be hamoi. Amalalu, Mousese da beda: iba: le amoga hobea: i.
Yehova anati, “Tayiponya pansi.” Mose anayiponya pansi ndipo inasanduka njoka ndipo anayithawa.
4 Amalalu, Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Defea! Dia lobo ligia guduli, sa: ya: be ea la: go gaguli gaguia gadoma.” Amaiba: le, Mousese da ea lobo ligia guduli, sa: ya: be gaguli, sa: ya: be da bu afadenene dagulu ba: i.
Kenaka Yehova anati kwa iye, “Igwire mtchira.” Ndipo Mose anayigwira mchira njokayo ndipo inasandukanso ndodo mʼdzanja lake.
5 Hina Gode da amane sia: i, “Di da Isala: ili dunu ba: ma: ne amo hou hamoma. Ilia da Hina Gode amo ilia aowalalia Gode, A:ibalaha: me, Aisage amola Ya: igobe ilia Gode, da dima misi dagoi, ilia da amo dafawaneyale dawa: ma: ne amo hou hamoma.”
Yehova anati, “Ukachite zimenezi ndipo akakukhulupirira kuti Yehova, Mulungu wa makolo awo, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isake ndi Mulungu wa Yakobo, wakuonekera iwe.”
6 Hina Gode da Mousesema eno amane sia: i, “Dia lobo amo dia abula ganodini wamo salima.” Mousese da Gode Ea sia: i defele hamoi. E da ea lobo bu duga: le, amo da aiya bagade moloba: agoai ba: i. (‘lebelosi’ oloi).
Yehova anatinso, “Pisa dzanja lako mʼmalaya akowo.” Choncho Mose anapisa dzanja lake mʼmalaya ake ndipo pamene analitulutsa, linali la khate kuchita kuti mbuu ngati ufa.
7 Amalalu, Hina Gode da amane sia: i, “Dia lobo bu dia abula ganodini wamo salima.” E da agoane hamoi. E lobo bu duga: le, aiya huluane da bahoi dagoi ba: i amola ea lobo gadofo da ea da: i hodo eno defele ba: i.
Yehova anati, “Tsopano pisanso dzanja lako mʼmalaya.” Mose anapisanso dzanja lakelo mʼmalaya ake ndipo atalitulutsa, linali labwinobwino, ngati thupi lake lonse.
8 Hina Gode da amane sia: i, “Ilia da dia hidadea hamoi musa: hame ba: su hou amo dafawaneyale hame dawa: sea, ilia da amo hou ba: sea, dia sia: dafawaneyale dawa: mu.
Tsono Yehova anati “Akakapanda kukukhulupirira, osalabadira chozizwitsa choyambacho, akakhulupirira ndithu chifukwa cha chozizwitsa chachiwiricho.
9 Be ilia amo musa: hame ba: su hou aduna ba: sea, dia sia: dafawaneyale hame dawa: sea, defea, Naile Hano amoga hano lale, hafoga: i osoboga sogadigima. Amasea, hano da afadenene, bu maga: me hamoi dagoi ba: mu.”
Koma ngati sakakhulupirira zizindikiro ziwiri izi kapena kukumvera, ukatunge madzi a mu mtsinje wa Nailo ndi kuwathira pa mtunda powuma ndipo madziwo adzasanduka magazi.”
10 Be Mousese da amane sia: i, “Hame mabu, Hina! Dia na mae asunasima! Na da sia: noga: le adole imunu hame dawa: Di da nama sia: beba: le, na hou da hame afadenei. Na sia: da noga: i hame, dioi bagade gala.”
Mose anati kwa Yehova, “Chonde Ambuye, chikhalire ine ndakhala munthu wosatha kuyankhula bwino. Ngakhale tsopano pamene mukundiyankhula, lilime langa ndi lolemera. Ndine wachibwibwi.”
11 Be Hina Gode da ema bu adole i, “Nowa da osobo bagade dunuma lafi iahabela: ? Nowa da dunu ge ga: i o sia: hamedei hamosala: ? Nowa da dunu ba: ma: ne si iaha o mae ba: ma: ne si dofosala: ? Amo da Ni fawane. Na fawane da Hina Gode!
Yehova anati kwa iye, “Kodi anapatsa munthu pakamwa ndani? Ndani amasandutsa munthu kuti akhale wosayankhula kapena wosamva? Ndani amapanga munthu kukhala wopenya kapena wosaona? Kodi si Ine Yehova?
12 Di wali masa! Na da dia sia: fidimu amola di adole ima: ne, Na da dima sia: imunu.”
Tsopano pita, Ine ndidzakuthandiza kuyankhula ndipo ndidzakulangiza zoti ukanene.”
13 Be Mousese da bu adole i, “Hame mabu, Hina! Eno dunu asunasima.”
Koma Mose anati, “Chonde Ambuye, pepani, tumani wina kuti akachite zimenezi.”
14 Amo sia: nababeba: le, Hina Gode da Mousesema ougi galu. E amane sia: i, “Defea! Dia ola Elane (Lifai fi dunu) amo dawa: ma. Ea sia: da noga: iwane Na dawa: E da wali di yosia: musa: logoga manebe. E da di hahawane ba: mu.
Kenaka Yehova anamupsera mtima Mose ndipo anati, “Kodi suli ndi mʼbale wako Aaroni wa fuko la Levi? Ine ndikudziwa kuti iye amayankhula bwino. Iye wanyamuka kale kudzakumana nawe ndipo adzasangalala akadzakuona.
15 Di sia: musa: dawa: i, amo ema sia: ma. Na da alia sia: be amo fidimu amola ali da eno dunu olelema: ne, alima sia: olelemu.
Iwe udzayankhula naye ndi kumuwuza mawu oti akanene. Ine ndidzakuthandizani kuyankhula nonse awirinu ndi kukulangizani zoti mukachite.
16 E da dia lafi defele esalebe ba: mu. E da Isala: ili dunu ilima dia sia: olelemu. Amasea, di da Hina Gode defele, e da sia: adole imunusa: ema olelemu.
Iye akayankhula kwa anthu mʼmalo mwako. Iye adzakhala wokuyankhulira ndipo iweyo udzakhala ngati Mulungu kwa iye.
17 Di ahoasea, amo dagulu gaguli masa. Di da amo daguluga musa: hame ba: su hou hamomu.”
Koma utenge ndodo imene ili mʼdzanja lakoyo kuti ukachite nayo zizindikiro zozizwitsa.”
18 Amalalu, Mousese da esoa: Yedelouma asili, amane sia: i, “Na da na fi Idibidi soge ganodini amo ilia hou ba: la masunu da defeala: ?” Yedelou da defea sia: ne, Mousesema hahawane ‘asigibio’ sia: i.
Tsono Mose anabwerera kwa Yetero, mpongozi wake ndipo anati kwa Iye, “Chonde ndiloleni kuti ndibwerere ku Igupto kwa anthu anga kuti ndikaone ngati ali moyo.” Yeteri anati, “Pitani mu mtendere.”
19 Mousese da Midia: ne soge ganodini esaloba, Hina Gode da ema amane sia: i dagoi, “Dia Idibidi sogega buhagima. Dunu huluane da di fanelegemusa: dawa: i amo da bogoi dagoi.”
Nthawiyi Yehova anali atamuwuza kale Mose ku Midiyani kuti, “Bwerera ku Igupto, pakuti anthu onse amene amafuna kukupha aja anamwalira.”
20 Amaiba: le, Mousese da idua amola egefe aduna amo dougi amoga fila heda: ma: ne hamone, Idibidi sogega doaga: musa: oule asi. Mousese da dagulu amo Gode da gaguli masa: ne sia: i, amo gaguli asi.
Kotero Mose anatenga mkazi wake ndi ana ake aamuna, ndipo anawakweza pa bulu nayamba ulendo wobwerera ku Igupto. Ndipo anatenga ndodo ya Mulungu ija mʼdzanja lake.
21 Hina Gode da bu Mousesema amane sia: i, “Di da wali Idibidi sogega buhagimuba: le, di da Idibidi hina bagade (Felou) ba: ma: ne, musa: hame ba: su hou dia hamoma: ne Na da dima gasa i, amo huluane hamoma. Be na da Felou ea dogo igi agoane hamomu. Amaiba: le, e da Na fi dunu ilia gadili masunu logo hame doasimu.
Yehova anati kwa Mose, “Ukaonetsetse kuti wachita pamaso pa Farao zodabwitsa zonse zimene ndayika mphamvu mwa iwe kuti ukachite. Koma Ine ndidzawumitsa mtima wake kotero kuti sadzalola anthuwo kuti apite.
22 Amasea, di da ema amane sia: ma, ‘Hina Gode da amane sia: sa; Isala: ili da Na magobo mano.
Ndipo iwe ukati kwa Farao, ‘Yehova akuti, Israeli ali ngati mwana wanga wachisamba.’
23 Na da dima nagofe Nama nodone sia: ne gadomusa: gadili masa: ne, logo doasima: ne sia: i. Be di da higa: i galu. Amaiba: le, Na da wali dia magobo dunu mano fanelegemu.’”
Choncho ndikuti, ‘Mulole mwana wanga apite kuti akandipembedze. Koma ngati ukana, Ine ndidzapha mwana wako wachisamba.’”
24 Mousese da Idibidiga doaga: musa: logoga ahoanoba, sogebi afae amogai ouesalu golai. Amogai, Hina Gode da ema misini, Mousese fanelegemusa: dawa: i.
Pambuyo pake Mose ali mʼnjira, pamalo wogona, Yehova anakumana naye, ndipo anafuna kumupha.
25 Be Mousese idua Siboula da debesu sua: ne, egefe gadofo damuni, amo Mousese ea emo da: iya ligisi. Gadofo damusu hou dawa: beba: le, e da Mousesema amane sia: i, “Di da nama maga: me egoa agoane galebe!” Amaiba: le, Hina Gode da Mousese hame fanelegei.
Koma Zipora anatenga mwala wakuthwa nachita mdulidwe mwana wake ndipo khungulo analikhudzitsa pa mapazi a Mose. Iye anati “Zoonadi, kwa ine ndiwe mkwati wamagazi.”
Choncho Yehova anamuleka Mose wosamupha. Pa nthawiyo, Zipora anati, “Mkwati wa magazi,” ponena za mdulidwe.
27 Be Hina Gode da Elanema amane sia: i dagoi, “Di wadela: i hafoga: i soge amoga masa. Amogai, di Mousese gousa: ma.” Amaiba: le, e da hadigi goumi (Sainai Goumi) amogai Mousese gousa: i. E da Mousese gousa: le, nonogoi.
Yehova anati kwa Aaroni, “Pita ku chipululu ukakumane ndi Mose.” Iye anapitadi nakakumana ndi Mose pa phiri la Mulungu namupsompsona.
28 Amalalu, Mousese da Hina Gode ea adoi huluane (E da Idibidi sogega buhagima: ne sia: i) amo Elanema olelei. Amola musa: hame ba: su hou Hina Gode da e hamoma: ne sia: i, amo Elanema olelei.
Kenaka Mose anamufotokozera Aaroni chilichonse chimene Yehova anamutuma kuti akanene. Anamufotokozera za zizindikiro zozizwitsa zimene anamulamulira kuti akazichite.
29 Amaiba: le, Mousese amola Elane ela da Idibidi sogega asi. Amogai, ilia da Isala: ili ouligisu dunu huluane gilisi.
Mose ndi Aaroni anapita kukasonkhanitsa pamodzi akuluakulu onse a Aisraeli.
30 Elane da ilima hou huluane Hina Gode da Mousesema sia: i amo ilima olelei. Dunu huluane ba: ma: ne, Mousese da musa: hame ba: su hou huluane hamosu.
Ndipo Aaroni anawafotokozera zonse zimene Yehova ananena kwa Mose. Anachita zizindikirozo pamaso pa anthu onse,
31 Amalalu, Isala: ili dunu fi da dafawaneyale dawa: i. Ilia Hina Gode da ilima misi dagoi amola ilia se nabasu huluane E da ba: i dagoi, amo dafawaneyale dawa: i. Amo dawa: beba: le, ilia da beguduli, Godema nodone sia: ne gadoi.
ndipo anakhulupirira. Iwo atamva kuti Yehova anadzawayendera ndi kuti waona mmene akuzunzikira, anaweramitsa mitu pansi napembedza.

< Gadili Asi 4 >