< Gadili Asi 38 >

1 Ohe iasu gobesimusa: e da aga: isia ifa lale, oloda hamoi. Amo da gagili agoane ea la: di fe defei da 2.2 mida amola la: di fe da 2.2 mida. Ea gadodili heda: su da 1.3 mida ba: i.
Anapanga guwa lansembe zopsereza lamatabwa amtengo wa mkesha. Linali lofanana mbali zonse. Msinkhu wake masentimita 137, mulitali mwake masentimita 229, mulifupi masentimita 229.
2 E da oloda ea hegomai biyaduyale gadili amoga bulamagau ea ‘hono’ agoane heda: musa: hamoi. Ilia da oloda amoga noga: le madelagi dagoi ba: i. Amo huluane e da balasega dedeboi.
Anapanga nyanga imodziimodzi pa ngodya zake zinayizo, kotero kuti nyangazo ndi guwalo zinali chinthu chimodzi, ndipo anakuta guwalo ndi mkuwa.
3 E da sefe amola nasubu gilisi amo fadegama: ne, ofodo hamoi. Amola ‘safala’, ofodo, ma: go amola bianoi ofodo amo lalu gaguli masa: ne, amo huluane balasega hamoi.
Anapanganso ziwiya zamkuwa izi zogwirira ntchito pa guwalo: miphika, mafosholo, mabeseni owazira magazi, ngowe zokowera nyama ndi zosonkhezera moto.
4
Anapanga sefa yachitsulo chamkuwa ya guwa lansembelo kuti ikhale mmunsi mwa khoma la guwa lansembelo, kuchokera pansi mpaka pakati pa khoma la guwalo.
5 E da nasubu amo gudu sa: ima: ne, gigiadamoi hamoi. E da amo liligi oloda ea gadodili legesu hagudu amo oloda ea bada sagai amoga lala: gilisi. E da oloda ea hegomai biyaduyale gala amoga gasisalasu oloda gaguli masa: ne lala: gilisi.
Anapanga mphete zamkuwa zinayi ndipo anazilumikiza ku ngodya zinayi za sefa ija kuti zigwire nsichi zonyamulira.
6 E da amo oloda gaguli masa: ne, aga: isia ifa aduna hamoi. E da amo ifa aduna balasega dedeboi.
Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndipo anazikuta ndi mkuwa.
7 E da amo ifa gasisalasu oloda la: di la: di hamoi, amo ganodini sali. E da oloda amo aga: isia ifa da: fe amoga gagili agoane hamoi.
Iwo analowetsa nsichizo mʼmphetemo mbali zonse ziwiri za guwalo kuti azinyamulira. Guwalo linali lamatabwa ndi logoba mʼkati mwake.
8 E da balase dodofesu ofodo amola ea balase bai hamoi. Uda da Hina Gode Ea Abula Diasu Holeiga hawa: hamonanu amo ilia daiya ba: su lale, amoga ofodo hamoi.
Anapanga beseni lamkuwa lokhala ndi miyendo yamkuwanso kuchokera ku magalasi oyangʼanira nkhope a amayi amene ankatumikira pa chipata cha tenti ya msonkhano.
9 E da Da: bena: gele Abula Diasu amo gagomusa: abula gagoi hamoi. E da ga (south) la: di guga amoga abula noga: idafa ea sedade defei 44 mida amo hamone gosagisi.
Kenaka anapanga bwalo la chihema. Mbali yakummwera inali yotalika mamita 46 ndipo kunali nsalu yotchinga yofewa yosalala yolukidwa bwino.
10 E da amo abula gosagisimusa: golasu ifa balasega hamoi 20 amola bai salasu balasega hamoi 20 amola hamoi dagoi. Golasu ifa amoga ma: go amola bulufalegei dududawalo agoane da silifa amoga hamoi ba: i.
Anapanganso mizati makumi awiri, matsinde makumi awiri amkuwa ndi ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.
11 E da amo defele ga (north) la: di guga amoga hamoi.
Mbali yakumpoto inalinso yotalika mamita 46 ndipo inali ndi mizati makumi awiri, matsinde amkuwa makumi awiri, ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.
12 Guma: dini, e da abula ea defei da 22 mida amo golasu ifa nabuane gala amola bai nabuane gala, amoga gosagisi.
Mbali yakumadzulo inali yotalika mamita 23 ndipo inali ndi nsalu yotchinga, mizati khumi ndi matsinde khumi. Inalinso ndi ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.
13 Gusudili amo da logo holei ea sogebi gagoi da guma: dini defele 22 mida defei ba: i.
Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, inalinso yotalika mamita 23.
14 Logo holei da dogoa ba: i. Ea la: diga da gagoi abula 6.6 mida defei ba: i. Eno la: diga da amo defele ba: i. Abula da la: di golasu ifa udiana amola bai udiana amoga gosagisi ba: i. La: di da amo defele ba: i.
Mbali imodzi yachipata kunali nsalu yotchinga yotalika mamita asanu ndi awiri, mizati itatu ndi matsinde atatu,
polowera mʼbwalo panali nsalu yotchinga ya mamita asanu ndi awiri pamodzi ndi mizati itatu ndi matsinde atatu.
16 Abula huluane amo gagomusa: gosagisi da abula noga: i ahea: ya: i amoga hamoi dagoi.
Katani yonse yotchinga kuzungulira chihema inali yofewa, yosalala ndi yolukidwa bwino.
17 Gagoi golasu ifa huluane da silifa dagulu bulufalegei agoane gilisili disi dagoi ba: i.
Matsinde amizati anali amkuwa. Ngowe ndi zingwe za mizati zinali zasiliva, ndipo pamwamba pa mizatiyo anakutapo siliva. Choncho mizati yonse ya bwalolo inalumikizidwa ndi zingwe zasiliva.
18 Logo holeidafa da abula 9 mida la: di amola 2 mida gado heda: i la: di amo defei amoga hamoi. Amo abula amoga sibi hinabo mola: ya: i, oga: iyei amola yoi amoga amuni ba: i.
Nsalu yotchinga ya pa chipata inali yamtundu wa mtambo, yapepo ndi yofiira, yofewa yosalala ndi yopangidwa ndi anthu aluso. Nsaluyo inali yotalika mamita asanu ndi anayi, molingana ndi nsalu zotchinga bwalo. Msinkhu wake unali masentimita 229,
19 Amo abula da golasu ifa biyaduyale gala amola ilia bai biyaduyale gala amoga gosagisi ba: i. Ilia ma: go amola habuga dududawalo agoane da silifa amoga hamoi.
pamodzi ndi mizati yake inayi ndi matsinde amkuwa anayi. Ngowe ndi zingwe zake zinali za siliva, ndipo pamwamba pake pa mzati anakutapo ndi siliva.
20 Abula Diasu amola gagoi ilia golasu ifa sagasu da balasega hamoi dagoi ba: i.
Zikhomo za chihema ndi zina zonse zozungulira chihemacho zinali zamkuwa.
21 Hina Gode Ea Hadigi Abula Diasu amo ganodini igi gasui aduna amo da: iya da Gode Ea Sema nabuane gala dedei dagoi ba: i. Abula diasu liligi hamomusa: gini, Mousese da liligi lama: ne dedene legema: ne sia: i. Lifai fi dunu da amo dedene legei. Ilia ouligisu dunu da Elane egefe Idama galu. Ouli liligi lai amo ilia defei da hagudu dedei diala.
Chiwerengero cha zipangizo zimene anagwiritsa ntchito popanga chihema, chihema chaumboni, zimene Mose analamulira Alevi kuti alembe motsogozedwa ndi Itamara mwana wa Aaroni, wansembe, chinali ichi:
22 Bisa: liele (Uli egefe amola He ea aowa - Yuda fi dunu) da Hina Gode Ea liligi hamoma: ne sia: i amo huluane hamoi dagoi.
Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huzi wa fuko la Yuda anapanga chilichonse Yehova analamulira Mose,
23 Ea fidisu dunu, Ouhoulia: be (Ahisama: ge egefe - Da: ne fi dunu) da ouli, igi amola ohe gadofo amoga dedesu hou dawa: su. E da hawa: hamoma: ne, osa: le dedesu dawa: i amola abula amoga sibi hinabo mola: ya: i, oga: iyei amola yoi amo amunasu hou dawa: i.
pamodzi ndi Oholiabu mwana wa Ahisamaki, wa fuko la Dani, wa luso la zopangapanga ndi kulemba mapulani, ndi wopanga nsalu zolukidwa bwino za mtundu wa mtambo, yapepo ndi zofiira, zofewa ndi zosalala.
24 Gouli huluane amo Hina Godema Ea Hadigi Abula Diasu gaguma: ne iasu ea dioi defei (Amo da dioi defeidafa amoga ba: i) da 1,000 gilogala: me ba: i.
Golide yense wochokera ku nsembe yoweyula amene anagwiritsa ntchito pa ntchito yonse yopanga malo wopatulika anali wolemera makilogalamu 1,000 potsata miyeso ya kumalo wopatulika.
25 Silifa amo ilia Isala: ili dunu afae afae ilima lai ea dioi defei (amo amola ilia da dioi defeidafa amoga ba: i) da 3,430 gilogala: me ba: i.
Siliva wochokera ku gulu lonse la anthu anali wolemerera makilogalamu 3,430, potsata miyeso ya ku malo wopatulika.
26 Ilia da dunu ilia idi defele dunu huluane afae afae ilima lai. Amola ilia da dioi defeidafa amo esoga ilia da ilegei amoga dioi defei ba: i. Ilia da Isala: ili dunu idisia dunu ode 20 lalelegei amola amo baligi da idi 603,550 ba: i.
Munthu aliyense amapereka beka imodzi, kufanana ngati makilogalamu 6, potsata muyeso wa ku malo wopatulika. Kuchokera kwa aliyense amene anawerengedwa kuyambira zaka 20 kapena kuposerapo, amuna onse analipo 603,550.
27 Ilia da silifa mogili, dioi defei 3,400 gilogala: me amo lale, amoga bai 100 agoane gala amo Hadigi Malei Sesei amola ea abula bugima: ne hamoi. Bai afae afae hamoma: ne, ilia da gouli 34 gilogala: me amoga hamoi. Silifa 30 gilogala: me hame lai dialu, amoga Bisa: liele da bulufalegesu dududawalo, golasu ifa ma: go amola golasu ifa habuga hamoi dagoi.
Anagwiritsa ntchito siliva wolemera makilogalamu 3,400 kupanga matsinde 100 a ku malo wopatulika ndi makatani, ndipo makilogalamu 34 kupanga tsinde limodzi.
Makilogalamu otsalawo anagwiritsa ntchito popanga ngowe zamzati kukutira pamwamba pa mizati ndiponso kupanga zingwe zake.
29 Balase amo da Hina Godema modale ligiagale i, amo ea dioi defei da 2,425 gilogala: me ba: i.
Mkuwa ochokera ku nsembe yoweyula unali makilogalamu 2,425.
30 E da amo balase amoga Hina Gode Ea Abula Diasu logo holei ifa amo ea bai, amola balase oloda, ea gigiadomai, oloda ea liligi huluane,
Iwo anawugwiritsa ntchito popanga matsinde a pa chipata cha tenti ya msonkhano, guwa la mkuwa pamodzi ndi sefa yake ndiponso ziwiya zonse,
31 gagoi golasu ifa ilia sagasu bai, Hadigi Abula Diasu ea udidisu ifa amola gagoi ea udidisu ifa, amo huluane e da amo balasega hamoi.
matsinde ozungulira bwalo ndiponso a pa chipata pake, ndi zikhomo zonse za tentiyo ndi matsinde a malo wozungulirapo.

< Gadili Asi 38 >