< Gadili Asi 33 >

1 Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Di amola dunu fi amo di da Idibidi sogega gadili masa: ne oule misi. Amo sogebi yolesili, soge amo Na da A: ibalaha: me, Aisage amola Ya: igobe iligaga fi amola ilima imunu ilegele sia: i, amoga masa.
Ndipo Yehova anati, “Chokani pa malo ano, iwe ndi anthu amene unawatulutsa mʼdziko la Igupto. Pitani ku dziko limene ine ndinalonjeza ndi lumbiro kwa Abrahamu, Isake ndi Yakobo kuti, ‘Ine ndidzalipereka kwa zidzukulu zanu.’
2 Na da a: igele dunu dilima logo olelemusa: asunasimu. Amola dilia da amo sogega fima: ne, Na da Ga: ina: naide, A:moulaide, Hidaide, Belesaide, Haifaide amola Yebusaide, amo dunu fi huluane sefasimu.
Ndipo ndidzatumiza mngelo patsogolo panu kuthamangitsa Akanaani, Aamori, Ahiti, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi.
3 Dilia da soge noga: idafa, fedege agoane amo ganodini dodo maga: me amola agime hano da hano agoane yogodaha, amoga ahoa. Be Na da dili hame sigi masunu. Bai dilia da dogo gawamaga: i dunu, amola Na da dili logoga dafawanedafa fanelegesa: besa: le, hame masunu.”
Pitani ku dziko loyenda mkaka ndi uchi. Koma ine sindidzapita nanu, chifukwa anthu inu ndinu nkhutukumve ndipo nditha kukuwonongani mʼnjiramo.”
4 Isala: ili dunu da amo sia: nabaloba, da: i dioiba: le dinanu. Ilia da se nababeba: le, bu hame nina: hamoi.
Anthu atamva mawu owopsawa, anayamba kulira ndipo palibe anavala zodzikometsera.
5 Bai Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Isala: ili dunuma adoma, ‘Dilia da hame nabasu dunu. Na da fa: bihadi fawane dili oule ahoa ganiaba, Na da dafawane dili medole legela: loba. Wali dilia nina: hamoi igi noga: i huluane fadegama. Na da fa: no dilima adi hamoma: beyale dawa: ma.”
Pakuti Yehova anali atanena kwa Mose kuti, “Awuze Aisraeli kuti, ‘Inu ndinu nkhutukumve.’ Ngati ine ndipita ndi inu kwa kanthawi, nditha kukuwonongani. Tsopano vulani zodzikometsera zanu ndipo ine ndidzaganiza choti ndichite nanu.”
6 Amaiba: le, Isala: ili dunu da Sainai Goumi yolesili, fa: no bu hame nina: hamoi.
Kotero Aisraeli anavula zodzikometsera zawo pa phiri la Horebu.
7 Eso huluane Isala: ili dunu da ilia Abula Diasu gaguloba, Mousese da Gode Ea Abula Diasu (Da: bena: gele) amo abula diasu gilisisu gadili fonobahadi sedagawane gagusu. Ilia da amo Abula Diasu, “Hina Gode Ea amo ganodini Esalebe Diasu” amo dio asuli. Nowa da Hina Godema sia: sa: imusa: dawa: loba, e da amoga ahoasu.
Tsono Mose ankatenga tenti ndi kukayimanga kunja kwa msasa chapatalipo, ndipo ankayitcha “tenti ya msonkhano.” Aliyense wofuna kukafunsa kanthu kwa Yehova amapita ku tenti ya msonkhano kunja kwa msasa.
8 Mousese da Gode Ea Abula Diasuga ahoanoba, dunu huluane da ilia abula diasu holeiga lelebe ba: su. Ilia da Mousese ea Gode Ea Abula Diasu ganodini golili dasu ba: su.
Ndipo nthawi ina iliyonse imene Mose amapita ku tenti anthu onse amanyamuka ndi kuyimirira pa makomo amatenti awo, kumuyangʼana Mose mpaka atalowa mu tentimo.
9 Mousese da ganodini golili sa: i dagoi ba: loba, mumobi da gudu sa: ili, Da: bena: gele ea logo holeiga dialebe ba: su. Amalalu, Hina Gode da mumobi haguli amoga Mousesema sia: dalebe ba: su.
Mose akamalowa mu tenti, chipilala cha mtambo chimatsika ndi kukhala pa khomo pamene Yehova amayankhula ndi Mose.
10 Dunu huluane da mumobi Gode Ea Abula Diasu logo holei amoga dialebe ba: loba, ilia da hedolowane begudusu.
Nthawi zonse anthu akaona chipilala cha mtambo chitayima pa khomo la tentiyo amayimirira ndi kupembedza, aliyense ali pa khomo la tenti yake.
11 Hina Gode da Mousesema sisima hodole, dunu da ea na: iyadoma sia: daha amo defele sia: dasu. Amalalu, Mousese da bu Isala: ili abula diasu gilisisu amoga buhagisu. Be Mousese ea ayeligi fidisu, amo Yosiua (Nane egefe) da Gode Ea Abula Diasuga esalusu.
Yehova amayankhula ndi Mose maso ndi maso ngati mmene munthu amayankhulira ndi bwenzi lake. Kenaka Mose amabwerera ku msasa koma womuthandiza wake, Yoswa, mwana wa Nuni samachoka pa tentiyo.
12 Mousese da Hina Godema amane sia: i, “Dafawane! Di da nama amo dunu Ga: ina: ne sogega bisili oule masa: ne sia: i. Be nama oule masunu dunu da nowa, amo di nama hame adoi. Di na noga: le dawa: amola na hou hahawane ba: sa, amo Di da adoi dagoi.
Mose anati kwa Yehova, “Inu mwakhala mukundiwuza kuti, ‘Tsogolera anthu awa,’ koma simunandiwuze amene mudzamutuma kuti apite pamodzi nane. Inu mwanena kuti, ‘Ndikukudziwa bwino kwambiri ndipo wapeza chisomo pamaso panga.’
13 Amaiba: le, Di da nama hahawane galea, Dia fa: no hamomu hou nama olelema. Na udigili hame adole ba: sa. Be na da Dia hawa: hamosu noga: le hamoma: ne amola, Di da na hahawane ba: ma: ne, adole ba: sa. Amo dunu fi da Dia dunu fidafa hamoma: ne, Di ilegei dagoi. Amo mae gogolema!”
Ngati mwakondwera nane ndiphunzitseni njira zanu kuti ndikudziweni ndi kupitiriza kupeza chisomo pamaso panu. Kumbukirani kuti mtundu uwu ndi anthu anu.”
14 Hina Gode da amane sia: i, “Na da ani masunu. Na da dima hasalasu hou imunu.”
Yehova anayankha kuti, “Ine ndemwe ndidzapita pamodzi ndi iwe, ndipo ndidzakupatsa mpumulo.”
15 Mousese da bu adole i, “Di da ninia hame sigi ahoasea, Di da amo sogebi fisimusa: nini gadili mae asunasima.
Kenaka Mose anati kwa Yehova, “Ngati inu simupita nafe, musatitumize kuti tipite, kutichotsa pano.
16 Di da nini hame sigi ahoasea, Di da nama amola Dia fi ilima hahawane gala, nowa da dawa: ma: bela: ? Be Di da ninima gilisili ahoasea, dunu huluane da ninia da fi hisu, dunu fi huluane eno amoga afafai, dunu huluane da dawa: mu.”
Kodi wina adzadziwa bwanji kuti inu mwandikomera mtima pamodzi ndi anthu awa ngati simupita nafe? Kodi nʼchiyani chomwe chidzatisiyanitse pakati pa anthu onse amene ali pa dziko lapansi?”
17 Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Na da di noga: le dawa: , amola Na da dima hahawane gala. Amaiba: le, Na da dia adole ba: i defele hamomu.”
Ndipo Yehova anati kwa Mose, “Ine ndidzachita zimene iwe wandipempha chifukwa Ine ndikukondwera nawe, ndikukudziwa bwino lomwe.”
18 Amalalu, Mousese da Ema amane adole ba: i, “Na da Dia hadigi sinenemegi amo ba: mu hanai galebe.”
Kenaka Mose anati, “Tsopano ndionetseni ulemerero wanu.”
19 Hina Gode da bu adole i, “Defea! Na da Na hadigi hou di ba: ma: ne olelemu. Na hadigi Dio amola dima adomu. Na da Gode Hinadafa. Na da nowa dunu gogolema: ne olofomusa: dawa: sea, Na da gogolema: ne olofomu. Nowa dunuma Na da asigima: ne dawa: sea, Na da ema asigimu.
Ndipo Yehova anati, “Ine ndidzakuonetsa ulemerero wanga wonse ndipo ndidzatchula dzina langa lakuti Yehova pamaso pako. Ine ndidzachitira chifundo amene ndikufuna kumuchitira chifundo ndipo ndidzakomera mtima amene ndikufuna kumukomera mtima.”
20 Na da Na odagi dima hame olelemu. Bai nowa Na odagi ba: sea, e da bogomu.
Iye anati, “Koma iwe sungaone nkhope yanga, pakuti palibe munthu amene amaona Ine nakhala ndi moyo.”
21 Be amo gele da Na dafulili diala. Amoga di leloma.
Ndipo Yehova anati, “Pali malo pafupi ndi ine pomwe ungathe kuyima pa thanthwe.
22 Amasea, Na hadigi sinenemegi da baligisia, Na da di gele gelabo ganodini sanasili, Na loboga dedebomu. Amasea, Na da baligimu.
Pamene ulemerero wanga udutsa, ndidzakuyika mʼphanga la thanthwe ndi kukuphimba ndi dzanja langa mpaka nditadutsa.
23 Amasea, Na da Na lobo bu lalegamu. Di da Na baligi ba: mu be Na odagi ba: mu da sema gala.”
Kenaka ine ndidzachotsa dzanja langa ndipo iwe udzaona msana wanga, koma nkhope yanga sidzaoneka.”

< Gadili Asi 33 >