< Gadili Asi 21 >

1 Hina Gode da eno amane sia: i, “Isala: ili dunuma amo hamoma: ne sia: i olelema;
“Uwawuze Aisraeli malamulo awa:
2 Di da Hibulu udigili hawa: hamosu dunu bidi lasea, e da ode gafeyale amoga dia hawa: hamomu. Ode fesu amoga, e da hahawane halegale ahoanoma: ne, ea logo doasima. E da dima dabe hame ima: mu.
“Mukagula kapolo wa Chihebri, azikugwirirani ntchito zaka zisanu ndi chimodzi. Koma mʼchaka cha chisanu ndi chiwiri muzimumasula, ndipo asalipire kanthu.
3 E da dia hawa: hamosu lasea uda hamelai galea, e da ahoasea, uda mae lalewane masunu. Be e da dia hawa: hamosu lasea udalai galea, defea, e da ahoasea uda amola oule masunu.
Ngati anabwera yekha, amasulidwenso yekha. Koma ngati anali ndi mkazi pamene ankabwera, mkaziyo apite nayenso.
4 Ea ouligisu dunu da ema uda ia galea, amo e da amo udama dunu mano o uda mano lalelegesea, amo uda amola ea mano da ea hina ea: Udigili hawa: hamosu dunu hi fawane da fisili masunu.
Ngati bwana wake amupatsa mkazi ndipo mkaziyo anabereka ana aamuna kapena aakazi, mkazi ndi anawo adzakhala a bwanayo ndipo mwamuna yekhayo ndiye adzamasulidwe.
5 Be amo udigili hawa: hamosu dunu da ea ouligisu dunu, ea uda amola ea mano amoma e da asigi amola e da udigili halegale ahoanumu higa: i amo sia: sea,
“Koma ngati kapoloyo alengeza kuti, ‘Ine sindikufuna kumasulidwa chifukwa ndimakonda mbuye wanga, mkazi wanga ndi ana,’
6 amasea, ea ouligisu dunu da amo dunu sia: ne gadosu diasuga oule masunu. Amogai, ouligisu dunu da amo udigili hawa: hamosu dunu logo holei mimogodi ifa dafulili leloma: ne sia: ma: mu. Amasea, ouligisu dunu da amo dunu ea ge gala: mu. Amo ilegei hamoi dagoiba: le, udigili hawa: hamosu dunu da ea ouligisu dunu mae fisili, eso huluane amaiwane dialumu.
mbuye wakeyo abwere naye kwa Yehova. Abwere naye pa chitseko kapena pa mphuthu zachitseko ndipo abowole khutu lake ndi chitsulo. Ndipo iye adzakhala kapolo wake moyo wake wonse.
7 Be dunu da idiwi udigili hawa: hamoma: ne bidi lasea, idiwi da ode fesu amoga dunu ilia hou defele, halegale hame masunu.
“Ngati munthu agulitsa mwana wake wamkazi kukhala mdzakazi, mwanayo asamasulidwe monga achitira ndi akapolo aamuna.
8 Dunu eno da amo a: fini uda la: musa: bidi lasea, be fa: no e da higasea, e da amo uda ga fi dunuma bu bidi lamu da sema bagade. E da amo uda ea adama fawane bu bidi lama: mu. Bai e da amo udama asigiwane hame hamoiba: le.
Koma ngati mkaziyo sakukondweretsa bwana wake amene wamusankha kuti amukwatire, amulole kuti awomboledwe. Bwanayo alibe mphamvu zomugulitsa kwa anthu achilendo, chifukwa iyeyo waphwanya pangano lake lomukwatira iye.
9 Dunu da egefe lama: ne, udigili hawa: hamosu a: fini amo bidi lasea, e da amo a: fini idiwi defele noga: le ouligima: mu.
Ngati anamusankha kuti akhale mkazi wa mwana wake, ayenera kumusunga ngati mwana wake wamkazi.
10 Dunu da uda aduna lasea, e da ea musa: lai udama ha: i manu amola abula ema asigi hou e da musa: ema i defele, bu ima: mu.
Ngati akwatira mkazi wina, asamumane woyambayo chakudya ngakhale chovala ndipo apiritirize kugona naye ngati mkazi wake.
11 Be e da amo hou hame hamosea, e da ea musa: uda hahawane udigili masa: ne sia: ma: mu. E da bidi hamedafa lamu.
Koma ngati sangathe kumuchitira zonsezi, ndiye amuleke apite popanda kulipira kanthu.
12 Nowa dunu da dunu eno fanelegesea, amo dunu fanelegema.
“Munthu aliyense amene amenya mnzake namupha, iyenso ayenera kuphedwa.
13 Be e da mae ougili giadofale eno dunu medosea, e da hobeale, Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade amoga masunu da defea. Na da amo Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade ilegemu. Amogai, e da se nabasu hame ba: mu.
Koma ngati sanachite dala, ndipo Mulungu analola kuti zichitike, iyeyo athawire ku malo kumene ndidzakupatsani.
14 Be dunu da ougiliwane dunu eno fanelegesea, amo dunu medole legema. E da Na oloda hi gaga: ma: ne hobeasea, ema mae asigima. Amo fanelegesu dunu medole legema.
Koma ngati munthu akonza chiwembu ndi kupha mnzake mwadala, ameneyo muchotseni ngakhale ku guwa langa lansembe ndipo aphedwe.
15 Nowa da ea ada o ea ame amo fasea, amo medole legema.
“Munthu aliyense amene amenya abambo ake kapena mayi ake ayenera kuphedwa.
16 Nowa da dunu amo bidi lamusa: o udigili hawa: hamosu dunu hamoma: ne gasa fili gagulaligisia, amo dunu fanelegema.
“Munthu aliyense amene aba munthu mnzake, ndi kukamugulitsa, kapena kumangomusunga, ayenera kuphedwa.
17 Nowa da ea ada o ame elama gagabusu aligima: ne sia: sea, amo fanelegema.
“Aliyense amene atemberera abambo ake kapena amayi ake ayenera kuphedwa.
18 “Dunu da gegesea, amola dunu afae da dunu eno ea lobo usunawane fasea o igiga fasea, be amo dunu da hame bogosea, ema se nabasu mae ima. Be dunu e da fai dagoi, amo da ea debea da: iya golasea, be fa: no e da dagulu gaguiwane gadili ahoanebe dawa: sea, dunu da ema fai amo e da ea hawa: hamosu bidi oloiba: le fisi, amo huluane ema imunu. Amola e da amo dunu noga: le ouligimu. E da uhinisi dagoiba: le fawane ouligisu yolesimu.
“Ngati anthu awiri akangana ndipo wina amenya mnzake ndi mwala kapena nkhonya koma wosamupha, womenyedwayo akadwala nagona pa bedi,
kenaka nachira ndi kuyamba kuyenda ndi ndodo kutuluka kunja kwa nyumba yake, ndiye kuti womenya mnzakeyo sadzayimbidwa mlandu. Komabe adzayenera kulipira womenyedwayo chifukwa cha nthawi imene anagona pa bedi ija, ndiponso ayenera kumusala mpaka atachiritsitsa.
20 Dunu da ifa lale, ea udigili hawa: hamosu dunu o uda amo fabeba: le, udigili hawa: hamosu da hedolowane bogosea, amo dunuma se nabasu ima.
“Ngati munthu amenya kapolo wake wamwamuna kapena mdzakazi ndi ndodo, kapolo uja ndikufa chifukwa cha kumenyedwako, munthuyo ayenera kulangidwa.
21 Be amo udigili hawa: hamosu dunu o uda da eso afae o aduna esalu bogosea, ouligisu dunuma se nabasu mae ima. E da ea bidi lai amo fisi dagoiba: le, amo da ema se nabasu defele lai gala.
Koma ngati kapolo uja akhala ndi moyo tsiku lonse kapena masiku awiri, ndiye kuti mbuye uja asalangidwe chifukwa kapolo ndi chuma chake.
22 Dunu da gilisili gegesea, amola uda abula agui da se nababeba: le, mano ea hagomo ganodini gala amo fisisia, be eno se hame nabasea, dunu da se nabasu i amo da amo uda egoa ea sia: defele dabe imunu. Be fofada: su dunuma fofada: nanu, dabe imunu.
“Ngati anthu akumenyana ndi kupweteka mayi woyembekezera, mayiyo napita padera, koma osavulala, wolakwayo ayenera kulipira chilichonse chimene mwamuna wake wa mkaziyo adzalamula ndipo bwalo lamilandu lavomereza.
23 Be amo uda hi da se bagade nabasea, dabe da esalusu fisi amo defele esalusu dabe imunu.
Koma ngati wavulazidwa kwambiri, ndiye malipiro ake adzakhala motere: moyo kulipa moyo,
24 Si wadela: sea, wadela: su dunu ea si dabe duga: ma. Bese gusia, dabe ea bese guma. Lobo o emo wadela: sea, amo dunu defele dabema.
diso kulipira diso, dzino kulipira dzino, mkono kulipa mkono, phazi kulipa phazi.
25 Laluga gia: sia, dabe gia: sima. Fa: gi o fofonomasu hamosea, dabe defele ima.
Kutentha ndi moto kulipa kutentha ndi moto, bala kulipa bala, mkwingwirima kulipa mkwingwirima.
26 Dunu da ea udigili hawa: hamosu dunu o uda amo ea si fabeba: le si wadela: sea, e da dabe ima: ne amo udigili hawa: hamosu uda o dunu amo hahawane halegale masa: ne logo doasima: mu.
“Ngati munthu amenya wantchito wake wa mwamuna kapena mdzakazi wake pa diso ndi kuliwononga, wantchitoyo amasulidwe ngati malipiro a diso lake.
27 E da fabeba: le bese wadela: sea, e da amo udigili hawa: hamosu dunu o uda amoma dabe ima: ne ea logo doasima: mu.
Ndipo ngati agulula dzino la wantchito wamwamuna kapena mdzakazi, wantchitoyo amasulidwe ngati malipiro a dzino lake.
28 “Bulamagau gawali da ea bese amoga dunu fabeba: le dunu da bogosea, amo bulamagau gawali igiga fanelegema. Ea hu amo mae moma. Be ea ouligisu dunu ema se nabasu mae ima.
“Ngati ngʼombe ipha munthu wamwamuna kapena wamkazi ndi nyanga yake, iponyedwe miyala ndipo nyama yake isadyedwe. Ndipo mwini ngʼombeyo asayimbidwe mlandu.
29 Be amo bulamagau gawali da musa: mae fisili dunuma doagala: musa: dawa: lalu ganiaba amola ea ouligisu dunu da sisasu nabalu, amo bulamagau gagoi ganodini hame ouligisu, amo bulamagau da ea besega dunu fanelegesea, bulamagau igiga medole legema amola ea ouligisu dunu fanelegema.
Koma ngati ngʼombeyo inali ndi chizolowezi chogunda anthu ndipo mwini wakeyo anachenjezedwa koma iye sanayimange ndipo yapha mwamuna kapena mkazi, ngʼombeyo iponyedwe miyala ndipo mwini wakeyo aphedwenso.
30 Be eno dunu da bulamagau ouligisu amo ea esalusu gaga: musa: muni dabe imunu da defea sia: sea, defea, e da muni bagade huluane ima: ne sia: ma.
Koma ngati wauzidwa kuti alipire, iye apereke zimene wauzidwazo kuti awombole moyo wake.
31 Bulamagau gawali da dunu mano o uda mano fanelegesea, amo sema da defele diala.
Lamulo ili ligwirenso ntchito ngati ngʼombeyo yagunda mwana wamwamuna kapena wamkazi.
32 Bulamagau gawali da udigili hawa: hamosu dunu o uda fanelegesea, bulamagau ea ouligisu dunu da hawa: hamosu dunu o uda ea ouligisu amoma silifa fage muni 30 agoane imunu. Be bulamagau gawali amo igiga gala: le, medole legema.
Ngati ngʼombeyo yagunda kapolo wamwamuna kapena mdzakazi, mwini ngʼombeyo apereke masekeli makumi atatu a siliva kwa mwini kapoloyo, ndipo ngʼombeyo iponyedwe miyala.
33 Dunu afae da uli dogoi amo ea ga: lu fadegasea, o e da uli dogone ga: lu hame figisia amola bulamagau gawali o dougi da amo ganodini bosona dasea,
“Munthu akasiya dzenje lapululu kapena akakumba dzenje koma wosaphimbapo, ndipo ngʼombe kapena bulu nʼkugweramo,
34 e da ohe ea ouligisu amoma muni dabe defele imunu. Be e da ohe medoi, amo gagumu.
mwini dzenjelo amulipire mwini chiweto chakufacho koma iye atenge chiwetocho.
35 Dunu afae ea bulamagau gawali da dunu eno ea bulamagau gawali fanelegesea, amo dunu aduna da bulamagau gawali hame bogoi amo bidi lale, muni amo afafane, afae da la: di lamu eno da eno la: di lamu. Ela da bulamagau bogoi amo ea hu dadega: le, la: di la: di lamu.
“Ngati ngʼombe ya munthu wina ipha ngʼombe ya mnzake, ngʼombe yamoyo ija igulitsidwe ndipo anthu awiriwo agawane pakati ndalama yake. Achite chimodzimodzi ndi ngʼombe yakufa ija.
36 Be amo bulamagau gawali da musa: mae fisili, eno bulamagau doagala: musa: dawa: lala ganiaba amola ea ouligisu dunu da gagoi ganodini hame ouligisu, amo dunu da bogoi bulamagau ouligisu dunuma bulamagau gawali esala imunu. Be e da bulamagau bogoi amo manusa: lamu.
Koma zikadziwika kuti ngʼombeyo inali ndi khalidwe logunda, ndipo mwini wake samayitsekera mʼkhola, mwini ngʼombeyo alipire ngʼombe ina yamoyo koma atenge yakufayo.”

< Gadili Asi 21 >