< Gadili Asi 18 >

1 Mousese esoa: Yedelou (Midia: ne gobele salasu dunu) da Gode da Mousese amola Isala: ili fi dunu Idibidi sogega gadili oule misini, noga: le fidisu, amo huluane nabi.
Yetero wansembe wa ku Midiyani amenenso anali mpongozi wa Mose, anamva zonse zimene Mulungu anachitira Mose ndi anthu ake a Aisraeli ndi mmene Yehova anawatulutsira mʼdziko la Igupto.
2 - Amaiba: le, e da Mousesema sofe misi. E da Mousese idua Siboula (Mousese da musa: e Midia: ne sogega fisi) amola ea mano aduna amo Gesiome amola Elia: isa oule misi. (Mousese da musa: sia: i dagoi, “Na da Midia: ne soge ganodini ga fi esala.” Amaiba: le, e da egefema Gesiome (ga fi dunu) dio asuli. E da eno sia: i, “Na ada ea Gode da fidibiba: le, na da Idibidi hina bagade amoga hame fanelegei ba: i. Amaiba: le, egefe eno amoma e da Elia: isa [Gode da na fidilala] amo dio asuli.)
Mose atamubweza Zipora, mkazi wake, Yetero, mpongozi wake anamulandira
3
mwana wake wamkaziyo pamodzi ndi ana ake aamuna awiri. Mose anamupatsa mwana wachisamba dzina loti Geresomu popeza anati, “Ndakhala mlendo mʼdziko lachilendo.”
4
Ndipo mwana wake wachiwiri anamupatsa dzina loti Eliezara, pakuti anati, “Mulungu wa makolo anga anali thandizo langa. Iye anandipulumutsa ku lupanga la Farao.”
5 Mousese da wadela: i hafoga: i soge hadigi goumi gadenene amogai esalu. Amoga, Yedelou da Mousese idua amola egefela oule misi.
Yetero, mpongozi wa Mose pamodzi ndi ana a Mose aamuna awiri ndi mkazi wake anabwera kwa Mose ku chipululu pa phiri la Mulungu kumene Mose anamanga misasa.
6 E da mae doaga: le, Mousesema sia: adole iasi.
Yetero anali atatumiza uthenga kwa Mose kuti, “Ine Yetero, mpongozi wako, ndikubwera ndi mkazi wako ndi ana ake awiri.”
7 Amaiba: le, Mousese da ema yosia: musa: asili, ema beguduli amola nonogoi. Ela, “Di da hahawane esalala: ?,” sia: nanu, ela da Mousese ea Abula Diasu ganodini golili sa: i.
Kotero Mose anatuluka kukakumana ndi mpongozi wake ndipo anawerama ndi kupsompsona. Atalonjerana anakalowa mu tenti
8 Mousese da Yedelouma Hina Gode Ea hou hamobe Felouma amola Idibidi dunuma amola Isala: ili dunu gaga: ma: ne amo huluane olelei dagoi. E da Isala: ili dunu logoga ahoanebe se nabasu amola Hina Gode Ea fidisu huluane olelei.
Mose anafotokozera mpongozi wake zonse zimene Yehova anamuchita Farao ndi Aigupto chifukwa cha Israeli komanso zowawa zonse anakumana nazo mʼnjira. Mose anafotokozanso momwe Yehova anawapulumutsira.
9 Yedelou da amo sia: huluane hahawane nabi.
Yetero anakondwa kwambiri atamva zabwino zonse zimene Yehova anachitira Aisraeli powapulumutsa mʼdzanja la Aigupto.
10 E amane sia: i. “Hina Godema nodoma! E da di amola Ea fi huluane noga: le fidi. E da ili Felou amola Idibidi dunu ilima gaga: ne, ilia se iasu diasu logo doasi dagoi. Godema nodoma!
Iye anati, “Alemekezeke Yehova amene wakupulumutsani mʼdzanja la Aigupto ndi Farao. Wapulumutsanso anthuwa mʼdzanja la Aigupto.
11 Idibidi dunu da Isala: ili dunuma higale hamobeba: le, Hina Gode da amo hou hamoi dagoi. Amaiba: le, Hina Gode Ea hou da eno ‘gode’ liligi ilia hou bagade baligisa, amo na da wali dawa:”
Tsopano ndikudziwa kuti Yehova ndi wopambana milungu ina yonse, pakuti anachita izi kwa amene ananyoza Israeli.”
12 Amalalu, Yedelou da gobele salasu ohe amo mae fifili gogo gobemusa: , Godema imunusa: gaguli misi. Amola e da eno gobele salasu liligi gaguli misi. Elane amola Isala: ili fi ouligisu dunu huluane da Yedelou gilisili, Godema nodone sia: ne gadomusa: , sema lolo manusa: asi.
Ndipo Yetero, mpongozi wa Mose anapereka nsembe yopsereza ndi nsembe zina kwa Mulungu. Aaroni ndi akuluakulu onse a Israeli anabwera kudzadya chakudya pamodzi ndi mpongozi wa Mose pamaso pa Mulungu.
13 Aya esoga, Mousese da Isala: ili dunu fi ilia sia: ga gegesu liligi fofada: nanu. E da hahabe fofada: nanu, mae yolesili gasimu galu.
Mmawa mwake, Mose anakhala pa mpando kuti aweruze milandu ya anthu. Anthu anayima momuzungulira kuyambira mmawa mpaka madzulo.
14 Yedelou da Mousese ea hawa: hamosu bagade ba: beba: le, amane adole ba: i, “Di abuliba: le disu amo dia fi dunu agoane fidisala. Disu da hamonana amola dunu huluane eso huluane hahabe asili gasi, dima fofada: musa: lela.”
Mpongozi wa Mose ataona zonse zimene iye amawachitira anthu anati, “Nʼchiyani chimene mukuwachitira anthuwa? Nʼchifukwa chiyani mulipo nokha woweruza, pamene anthu onsewa ayimirira kuyambira mmawa mpaka madzulo?”
15 Mousese da amane sia: i, “Na da agoane hamomu da defea. Dunu ilia da Gode Ea hanai amo dawa: musa: gini nama maha.
Mose anamuyankha kuti, “Chifukwa anthuwa anabwera kwa ine kudzafunsa zimene Mulungu akufuna.
16 Dunu aduna da sia: ga gegesu galea, ela da nama maha. Amasea, na da elama afae da moloi amola eno da giadofai amo elama olelesa. Amola na da Gode Ea hamoma: ne sia: i elama olelesa.”
Ngati munthu akangana ndi mʼbale wake, onse awiri amabwera kwa ine, ndipo ine ndimawaweruza. Ndimawawuzanso malamulo a Mulungu ndi malangizo ake.”
17 Amalalu, Yedelou da amane sia: i, “Di da giadofale hamosa.
Mpongozi wa Mose anayankha kuti, “Zimene mukuchitazi si zabwino.
18 Di da dia da: i hodo amola eno dunu ilia da: i hodo wadela: mu. Disu hamomu da hamedei.
Ntchitoyi ndi yayikulu kuposa mphamvu zanu. Inu simungathe kuyigwira nokha. Inu pamodzi ndi anthuwa amene amabwera kwa inu mudzatopa.
19 Na da dima fada: i sia: noga: i imunu. Amasea, Gode da di fidimu. Di da dunu ilia sia: ga gegesu nabimu amola Gode amola ili dogoa agoane alofesu dunu esalumu da defea.
Tsono tamverani ndikulangizeni, ndipo Mulungu akhale nanu. Inu muziwayimirira anthuwa pamaso pa Mulungu, ndipo mikangano yawo muzibwera nayo kwa Iye.
20 Di da Gode Ea hamoma: ne sia: i ilima olelemu amola ilia habodane esalumu amola hawa: hamosu ilima olelemu amo huluane da defea.
Aphunzitseni mawu ndi malangizo a Mulungu. Aphunzitseni mmene ayenera kukhalira ndi zimene ayenera kuchita.
21 Be amo baligili, di da dunu noga: i bagade dawa: su dunu ilegele, ilia da dunu huluane ilima ouligisu hina dunu ilegemu da defea. Ilia dunu fi idi 1000 amola dunu fi idi 100 amola idi 50 amola idi 10 amola ilima ouligisu hina ilegema: mu. Godema beda: i dunu fawane lama amola dunu da hano suligisu hou hame dawa: dunu, amo fawane ilegema.
Koma sankhani amuna odziwa ntchito yawo, anthu owopa Mulungu, anthu odalirika amene amadana ndi kupeza phindu mwachinyengo. Tsono muwayike kuti akhale oyangʼanira anthu motere: atsogoleri a anthu 1,000, ena a anthu 100, ena a anthu 50 ndi ena a anthu khumi.
22 Ilia mae yolesili fofada: su ouligisu dunu agoane hawa: hamoma: mu. Hou da gasa bagade ba: sea, ilia da di hahamoma: ne, dima adola misunu da defea. Be liligi fonobahadi ilisu da fofada: mu da defea. Ilia da dia dioi bagade liligi gilisili gaguli ahoasea, dia dioi liligi da bu fofoi ba: mu.
Tsono amenewa aziweruza anthu nthawi zonse. Mlandu uliwonse waukulu azibwera nawo kwa inu, koma mlandu waungʼono aziweruza okha. Izi zidzachititsa kuti ntchito yanu ipepuke, popeza mudzagwira ntchito mothandizana.
23 Di da Gode Ea sia: defele agoane hamosea, di da bogomuwane hele hame nabimu amola dunu huluane da ilia sia: ga gegei huluane hahamoi dagoi ba: sea, ilia diasuga hahawane masunu.”
Ngati mutsatira malangizowa monga mmene Mulungu wakulamulirani ndiye kuti simudzafowoka ndipo anthu onsewa adzapita kwawo mu mtendere.”
24 Mousese da Yedelou ea olelesu nabi dagoi.
Mose anamvera mpongozi wake ndi kuchita zonse zimene iye ananena.
25 E da Isala: ili fi amoga noga: i dawa: su dunu ilegei. E da dunu idi 1000 amola idi 100 amola idi 50 amola idi 10 ilima ouligisu hina dunu ilegei.
Iye anasankha amuna odziwa bwino ntchito zawo ndipo anawayika kuti akhale atsogoleri, oyangʼanira anthu motere: atsogoleri a anthu 1,000, ena a anthu 500, ena a anthu makumi asanu ndi ena a anthu khumi.
26 Ilia da mae yolesili fofada: su ouligisu hawa: hamosu. Gasa bagade fofada: su, ilia da Mousesema ia misi. Be ilisu da fonobahadi liligi hahamoi.
Iwowa ankaweruza anthu nthawi zonse. Milandu yovuta ankabwera nayo kwa Mose, koma yosavuta ankayiweruza okha.
27 Amalalu, Mousese da Yedelouma “asigibio” sia: nanu, Yedelou da hi diasuga buhagi.
Kenaka Mose analola kuti mpongozi wake, Yetero anyamuke kubwerera ku dziko la kwawo.

< Gadili Asi 18 >