< Eseda 8 >

1 Amo esoga, hina bagade Segesisi da hina bagade uda Esedama, Yu ilia ha lai dunu Ha: ima: ne ea gagui liligi huluane Eseda igili i. Eseda da hina bagade Segesisima amane adoi, “Modigai da na sosogo fi dunu.” Amalalu, Segesisi da Modigai ea odagia sia: ma: ne logo doasi.
Tsiku lomwelo mfumu Ahasiwero anamupatsa mfumukazi Estere nyumba ya Hamani, mdani wa Ayuda. Ndipo Mordekai anafika pamaso pa mfumu, popeza Estere anamuwuza ubale wawo.
2 Hina bagade da ea lobo sogo gasisalasu amo duga: le, (e da amo musa: Ha: ima: nema i, be bu samogei) Modigaima i. Eseda da Modigaima, Ha: ima: ne ea musa: gagui liligi amo ouligima: ne sia: i.
Mfumu inavula mphete yake yodindira imene analanda kwa Hamani ndipo Estere anamusankha Mordekai kukhala woyangʼanira nyumba ya Hamani.
3 Amalalu, Eseda da hina bagade ema bu adole ba: i. E da ea emo gadenene gala: la sa: ili, dinana ha: giwane amane sia: i, “Hina bagade! Ninia ha lai dunu, Ha: ima: ne (A: iga: ge egaga fi dunu) da Yu dunu fi huluane medole legemusa: ilegei. Be ea wadela: i ilegesu, di hedofama!”
Estere anayankhulanso ndi mfumu ndipo anadzigwetsa pa mapazi ake. Uku akulira iye anapempha mfumu kuti iletse choyipa, makamaka chiwembu chimene Hamani Mwagagi anakonza kuti awononge a Yuda.
4 Hina bagade da ea galiamo gouliga hamoi amo ema disiagaiba: le, Eseda da wa: legadole, amane sia: i,
Ndipo mfumu inamuloza Estere ndi ndodo yake yagolide ndipo Estere anadzuka ndi kuyima pamaso pake.
5 “Hina bagade noga: idafa! Di da hanai galea, amola di da nama asigi galea, di da Ha: ima: ne ea wadela: i sia: i ilegei amo hedofama. Ha: ima: ne (Ha: mida: ida egefe amola A: iga: ge egaga fi dunu) e da Yu dunu huluanedafa dia fifi asi ganodini esalebe, amo medole legemusa: sia: i.
Iye anati, “Ngati chikomera mfumu ndi kukukondweretsani, ngati pempho langa muliona kuti ndi loyenera ndi kuti mukondwera nane tsono mfumu ilole kuti lamulo lilembedwe kusintha mawu a mʼmakalata amene Hamani mwana wa Hamedata, Mwagagi, anatumiza ku zigawo zonse za mfumu. Paja Hamani analemba kuti Ayuda onse awonongedwe.
6 Ilia da na fi dunu amola na sosogo fi huluane medole legei ba: sea, na da adi hamoma: bela: ?”
Kodi ndingapirire bwanji pamene ndi kuona tsoka likugwera anthu a mtundu wanga? Ndingapirire bwanji pamene abale anga akuwonongedwa?”
7 Amalalu, hina bagade Segesisi da hina bagade uda Eseda amola Yu dunu Modigai elama amane sia: i, “Hodoma! Ha: ima: ne da Yu dunu medole legemusa: ilegeiba: le, na da e fuga: ma: ne hegoa: nesi dagoi. Amola ea liligi gagui amo na da Eseda ema i dagoi.
Mfumu Ahasiwero anamuyankha mfumukazi Estere ndi Mordekai Myuda kuti, “Ndapereka nyumba ya Hamani kwa Estere ndipo Hamaniyo amupachika kale pa mtanda chifukwa anafuna kuwononga Ayuda.
8 Be sia: da Besia hina bagade ea dioba: le sia: i, amola amo sia: dedei da hina bagade ea lobo sosoga gasisalasu amoga bu hamoi, amo sia: afadenemu da hamedei. Be alia hanaiga, Yu dunuma meloa dedene imunu da defea. Ali da na dioba: le dedenanu, na lobo sogoga gasisalasu amoga bu hamoma.”
Tsono inu awiri, lembani za Ayudawo monga mufunira. Mulembe mʼdzina la mfumu ndipo musindikize chizindikiro cha mphete ya mfumu popeza kuti cholembedwa mʼdzina la mfumu ndi kusindikizidwa ndi chizindikiro cha mphete ya mfumu sichingasinthidwe.”
9 Amo hou da eso 23 amola oubi osoda (Sifane oubi) amoga ba: i. Modigai da hina bagade ea sia: dedesu dunu ema misa: ne sia: si, ili da ea sia: amo eagene ouligisu amola hina dunu fifi asi gala 127 soge amo da Inidia sogega asili Suda: ne amoga doaga: i, ilima iasima: ne, meloa dedema: ne sia: i. Amo sia: da fifi asi gala hihi ilia sia: defele dedene, amola Yu dunu ilia sia: defele dedene ilima iasima: ne sia: i.
Nthawi yomweyo, pa tsiku la 23 la mwezi wachitatu wa Sivani, mfumu inayitana alembi ake. Analemba zonse zokhudza Ayuda monga ananenera Mordekai. Analembera akazembe, abwanamkubwa ndi nduna za zigawo 127 kuyambira ku India mpaka ku Kusi. Zimene analamula Mordekai zinalembedwa mʼzilembo za chigawo chilichonse ndi chiyankhulo cha mtundu uliwonse wa anthu. Ayudanso anawalembera mʼmalemba awo ndi chiyankhulo chawo.
10 Modigai da sia: beba: le, ilia da hina bagade Segesisi ea dioba: le dedei, amola Modigai da dedei amoga hina bagade ea lobo sogo gasisalasu amoga bu hamoi. Dunu eno ilia da hina bagade ea hehenasu bagade dawa: hosi, amo da: iya fila heda: le, amo meloa dedei fifi asi gala huluane ilima sagola asi.
Mordekai analemba makalatawo mʼdzina la mfumu Ahasiwero, nawadinda ndi chizindikiro cha mphete ya mfumu. Ndipo anawatumiza ndi anthu amithenga amene anakwera pa akavalo a ufumu othamanga kwambiri obadwa mu khola la ufumu.
11 Meloa dedei da hina bagade da Yu dunu moilai huluane ganodini esala, ilia bu gegemu logo doasi dagoi sia: i. Ilia bu gegemusa: , momagema: ne sia: i. Dadi gagui dunu da adi fifi asi gala amo ganodini ilima doagala: sea, ilia da amo dunuma bu gegene, amo dunu, uda amola mano fane lelegele, ilia liligi huluane lamu da defea, meloa da agoane dedei.
Mʼmakalata amenewa mfumu inalola kuti Ayuda okhala mu mzinda uliwonse akhale ndi ufulu wokumana ndi kudzitchinjiriza komanso kuwononga, kupha ndi kufafaniziratu gulu lililonse la nkhondo la anthu a mtundu uliwonse kapena chigawo chimene chingawathire nkhondo. Ayudawo analoledwa kuwononga gulu lankhondo lija, ana awo ndi akazi awo komanso kuti afunkhe katundu wawo.
12 Meloa dedei da amo hou Besia fifi asi gala huluane amo ganodini, eso13amola oubi fago (A: ida oubi) amoga ba: mu. Amo esoga, Ha: ima: ne da musa: Yu dunu huluane fuga: ma: ne sia: i.
Ayuda analoledwa kuchita zimenezi mʼzigawo zonse za Mfumu Ahasiwero pa tsiku limodzi lokha la 13 la mwezi wa 12, mwezi wa Adara.
13 Amo meloa dedei ilia da sema gaheabolo hamoi sia: i. Amola Yu dunu ilia gegemusa: noga: le momagema: ne, dunu huluanedafa amo nabimu da defea, ilia sia: i. Amasea, ilia da ilima ha lai bu dabema: ne, logo da doasi dagoi sia: i.
Mawu a mʼmakalatawo anayenera kudziwitsidwa kwa anthu a mtundu uliwonse mu chigawo chilichonse kuti ndi lamulo ndithu kwa anthu a mtundu uliwonse ndi kuti Ayuda adzakhale okonzeka pa tsikulo kulipsira kwa adani awo.
14 Hina bagade da sia: beba: le, dunu da hosi da: iya fila heda: le, amo meloa dedei iasima: ne hehenai. Moilai bai Susa amola, amo ganodini ilia da amo sia: dunu huluane nabima: ne olelei.
Atawalamulira a mfumu, amithenga aja anapita nawo makalata mwachangu, atakwera pa akavalo a mfumu. Ndipo lamulolo analiperekanso ku likulu la mzinda wa Susa.
15 Modigai da abula noga: idafa salalu, amola habuga gouliga hamoi figili, hina bagade ea diasu fisili, gadili asi. Amalalu, Susa moilai bai bagade amo ganodini, dunu ilia nodone bagade haia: fusu.
Mordekai anachoka pamaso pa mfumu atavala zovala zaufumu zooneka ngati mtambo ndi zofewa zoyera, chipewa chachikulu cha golide ndi mkanjo wapepo. Ndipo mzinda wa Susa unafuwula mokondwa.
16 Yu dunu da hahawane bagade ba: i. Ilia da beda: i hou fisili, denesi dagoi.
Kwa Ayuda inali nthawi ya nkhope zowala ndi za chimwemwe, chikondwerero ndi ulemu.
17 Moilai huluane amola fifi asi gala huluane amo ganodini, ilia da hina bagade ea sia: dedei amo nababeba: le, Yu dunu da hahawane helefisu amola lolo nasu hamoi. Amola dunu eno mogili da Yu dunu ilima beda: iba: le, ilia fidafa fisili, bu Yu dunu fi ilima gilisi.
Mʼchigawo chilichonse ndi mu mzinda uliwonse, kumene mawu a mfumu onena za lamulo lake anafika, kunali chimwemwe ndi chikondwerero pakati pa Ayuda. Linali tsiku la phwando ndi chikondwerero. Ndipo anthu ambiri a mitundu ina anazitcha Ayuda chifukwa anachita mantha ndi Ayudawo.

< Eseda 8 >