< Da:i Dione Dawa:i Olelesu 11 >

1 Dia muni amo ga fi ilia bidi lasu hou hamoma: ne ima. Eso enoga di da muni dabua eno ligi ba: mu.
Ponya chakudya chako pa madzi, udzachipezanso patapita masiku ambiri.
2 Dia muni dabua eno ligi ba: ma: ne, sogebi bagohame amoga bidi lasu hou hamoma. Bai di da dima se nabasu hou misunu hame dawa:
Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu, pakuti sudziwa ndi tsoka lanji limene likubwera pa dziko.
3 Ifa da habodili muwane dasea, e da ea sa: i sogebi amogaiwane dialumu. Mu mobi da nabai galea, gibu da sa: imu.
Ngati mitambo yadzaza ndi madzi, imagwetsa mvula pa dziko lapansi. Mtengo ukagwera cha kummwera kapena cha kumpoto, ndiye kuti udzagonera kumene wagwerako.
4 Di da ouesaleawane, fo amola gibu ea hou defele fawane hawa: bugimusa: dawa: sea, di da hamedafa bugimu amola hamedafa gamimu.
Amene amayangʼana mphepo sadzadzala; amene amayangʼana mitambo sadzakolola.
5 Gode da liligi huluane hahamoi. Amola di da mano dudubu gaheabolo hahamobe abula agui uda ea hagomo ganodini amo hame dawa: , amo defele di da Gode Ea hamobe hamedafa dawa:
Momwe sudziwira mayendedwe a mphepo, kapena momwe mzimu umalowera mʼthupi la mwana mʼmimba mwa amayi, momwemonso sungathe kudziwa ntchito za Mulungu, Mlengi wa zinthu zonse.
6 Di da hahabe ha: i manu bugima! Amola daeya amolawane bugima! Di da amo bugi da noga: le heda: mu o bugi amoga afae da noga: le heda: sa amola oda da wadela: mu amo di da hamedafa dawa:
Dzala mbewu zako mmawa ndipo madzulo usamangoti manja lobodo, pakuti sudziwa chimene chidzapindula, mwina ichi kapena icho, kapena mwina zonse ziwiri zidzachita bwino.
7 Wali esoha amo hahawane nodomu da defea.
Kuwala nʼkwabwino, ndipo maso amasangalala kuona dzuwa.
8 Ode huluane dia esalebeba: le, nodoma. Habowali di da esalea, noga: le dawa: ma. Dia bogole dialumu eso da dia esalebe eso baligi ba: mu. Fa: no misunu hou amoma nodomu da hamedei.
Munthu akakhala wa zaka zambiri, mulekeni akondwerere zaka zonsezo, koma iye azikumbukira masiku a mdima, pakuti adzakhala ochuluka. Chilichonse chimene chikubwera ndi chopanda phindu.
9 Ayeligi dilia! Dilia ayeligi eso amoga hahawane nodoma! Dilia da goi gogawane nodoma! Dilia hanaiga hamoma! Be dawa: ma! Dilia hamobe huluane amoga Gode da fofada: nanu, dabe imunu.
Kondwera mnyamata iwe, pamene ukanali wamngʼono, ndipo mtima wako usangalale pa nthawi ya unyamata wako. Tsatira zimene mtima wako ukufuna, ndiponso zimene maso ako akuona, koma dziwa kuti pa zinthu zonsezo Mulungu adzakuweruza.
10 Dilia hou huluane ba: sea, mae da: i dioma amola se nabasea, mae dawa: ma! Dilia da eso bagahame fawane goi esalumu.
Choncho uchotse zokusautsa mu mtima mwako, upewe zokupweteka mʼthupi mwako, pakuti unyamata ndi ubwana ndi zopandapake.

< Da:i Dione Dawa:i Olelesu 11 >