< Mousese Ea Malasu 6 >

1 “Amo da sema huluane dilia Hina Gode da na dilima olelema: ne sia: i. Dilia soge dilia wali gesowale fimu amo ganodini, amo sema nabawane hamoma.
Awa ndi malamulo, malangizo ndi ziphunzitso zimene Yehova Mulungu wanu anandilamula kuti ndikuphunzitseni kuti mukawatsatire mʼdziko limene mukuwolokera Yorodani kuti mukalitenge,
2 Dilia amola diligaga fi, da amo soge ganodini ode bagohame esaloma: ne, dilia Hina Gode Ema nodoma, amola Ea sema na da wali dilima iaha amo nabawane hamoma.
kuti inuyo, ana anu, ndi zidzukulu zanu mʼtsogolomo mudzaope Yehova Mulungu wanu moyo wanu wonse posunga malangizo ndi malamulo ake onse amene ndinakupatsani inu kuti musangalale ndi moyo wautali.
3 Isala: ili dunu! Amo sema noga: le nabima amola hamoma. Amasea, dilia da hahawane ba: mu amola dilia da gasa bagade fi hamone amola dilia aowalali ilia Hina Gode Ea sia: defele, amo soge noga: idafa amo ganodini esalumu
Mvera Israeli ndipo usamalitse kuchita malamulowa kuti zinthu zikuyendere bwino mʼdziko ndi kuti muchuluke kwambiri mʼdziko loyenda mkaka ndi uchi monga momwe Yehova Mulungu wa makolo anu anakulonjezerani.
4 Isala: ili fi! Noga: le dawa: ma! Hina Gode E fawane da ninia Gode.
Tamvani inu Aisraeli, Yehova Mulungu wathu, Yehova ndi mmodzi.
5 Dilia dogo huluane amoga, dilia a: silibu huluane amoga amola dilia gasa huluane amoga, dilia Hina Godema asigima.
Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu zako zonse.
6 Amo hamoma: ne sia: i na da wali eso dilima iaha, amo maedafa gogolema.
Malamulo amene ndakupatsani lero ayenera kukhala mu mtima mwanu.
7 Dilia mano ilima olelema. Amo sema noga: le dawa: ma: ne, eso huluane amo sema dilia lafidili sia: ma - dilia moilaiga esalea, ga ahoasea, helefisia amola hawa: hamosea, dawa: ma: ne sia: ma.
Muziwaphunzitsa mwachangu kwa ana anu. Muzikamba za malamulowa pamene muli mʼnyumba zanu, pamene mukuyenda mʼnjira, pamene mukugona ndi pamene mukudzuka.
8 Sema dedei amo dilia lobo amoga la: gima amola dilia odagiga dawa: ma: ne legema.
Muwamange ngati zizindikiro pa manja anu ndi kuwamangirira pa zipumi zanu.
9 Dilia moilai logo holei mimogodi ifa amoga amo sema dedema amola dilia gagoi logo ga: su amoga dedema.
Muwalembe pa mphuthu za nyumba zanu ndi pa zipata zanu.
10 Dilia Hina Gode da dilia aowalali A: ibalaha: me, Aisage amola Ya: igobe ilima hahawane imunu sia: i, amo defele, E da dilima soge amoga da bagade gagui moilai bai bagade (amo dilia loboga hame gagui) amo dilima imunu.
Pamene Yehova Mulungu wanu akukulowetsani ndi kukupatsani dziko limene analumbirira makolo anu Abrahamu, Isake ndi Yakobo, dziko lokhala ndi mizinda ikuluikulu imene inu simunamange,
11 Amo ganodini, diasu da liligi dilia hame ligisi amoga nabaiwane ba: mu. Dilia da hano nasu uli dogoi dilia da hame dogoi amo ba: mu. Amola waini sagai amola olife ifa sagai amo dilia da hame sagai ba: mu. Hina Gode da dili amo soge ganodini oule ahoasea, amola dilia da sadi dagoi ba: sea,
nyumba zodzaza ndi zinthu za mitundu yonse zimene inu simunayikemo, zitsime zimene inu simunakumbe, minda ya mpesa ndi mitengo ya olivi zimene inuyo simunadzale, tsono mukadya ndi kukhuta,
12 Hina Gode mae gogolema. Dilia da musa: Idibidi soge ganodini udigili hawa: hamosu dunu esalu amola Hina Gode da dili gaga: i.
samalani kuti mungayiwale Yehova amene anakutulutsani ku Igupto, kukuchotsani mu ukapolo.
13 Dilia Hina Godema beda: ma! Ema fawane nodone sia: ne gadoma. Amola hahawane hou o liligi imunusa: ilegesea, Ea Dioba: le fawane hamoma.
Muziopa Yehova Mulungu wanu ndi kumutumikira Iye yekha, ndipo muzilumbira pa dzina lake.
14 Eno ogogosu ‘gode’ liligi (amoma eno fi dunu dili fi sisiga: le esala da sia: ne gadosa), amoma maedafa nodone sia: ne gadoma.
Musamatsatire milungu ina, milungu ya anthu ena okuzungulirani,
15 Be dilia da amo liligima nodone sia: ne gadosea, Gode Ea ougi bagade da dilima lalu agoane doagala: mu amola dilia da gugunufinisi dagoi ba: mu. Bai dilia Gode dili amola gilisili esala da eno liligi Ea sogebi lamu bagadewane higasa.
pakuti Yehova Mulungu wanu amene ali pakati panu, ndi Mulungu wansanje ndipo adzakukwiyirani kwambiri ndi kukuwonongani, kukufafanizani mʼdziko.
16 Dilia da Masa sogega Godema ado ba: su hou hamoi. Agoaiwane bu mae hamoma.
Musamuyese Yehova Mulungu wanu monga munachitira ku Masa.
17 Sema huluane E da dilima i amo noga: le hamoma.
Onetsetsani kuti mukusunga malamulo a Yehova Mulungu wanu, malangizo ake ndi zikhazikitso zake zimene anakulamulirani.
18 Adi hou Hina Gode da moloi amola noga: i sia: sea, amo hou dilia hamoma. Amasea, dilia da hahawane ba: mu. Dilia da soge noga: i amo Hina Gode da dilia aowalali ilima imunu ilegele sia: i, amo dilia da amo gesowale fimu defele ba: mu.
Chitani zoyenera ndi zabwino pamaso pa Yehova, kuti zikuyendereni bwino ndi kuti mukhoza kukalowa ndi kulanda dziko labwinolo limene Yehova analonjeza molumbira kwa makolo anu,
19 Amola Gode Ea dilima ilegele sia: i defele, dilia da dilima ha lai dunu amo gadili sefasimu.
kupirikitsiratu adani anu onse, monga Yehova wanenera.
20 Fa: nohobea, dilia mano da dilima amane adole ba: mu, ‘Ninia Hina Gode da abuliba: le amo sema huluane nabawane hamoma: ne sia: bela: ?’
Mʼtsogolo muno, ana anu akadzakufunsani kuti, “Kodi tanthauzo la ndondomeko, malangizo, zikhazikitso ndi malamulo amene Yehova Mulungu wathu anakulamulani nʼchiyani?”
21 Amasea, ilima amane adoma, ‘Ninia da Idibidi hina bagade dunu ea udigili hawa: hamosu dunu esalu. Be Hina Gode da Ea gasa bagade amoga nini gaga: i.
Inu mudzawawuze kuti, “Ife tinali akapolo a Farao ku Igupto, koma Yehova anatitulutsa ku Igupto ndi dzanja lamphamvu.
22 Ninia siga ninia ba: i dagoi. E da musa: hame ba: su hou Ea gasa bagade amoga hamoi. E da Idibidi dunu beda: ma: ne, ilima, ilia eagene ouligisu dunu amola Idibidi hina bagade amoma hamoi.
Ifeyo tikuona Yehova anatumiza zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa, zazikulu ndi zoopsa, pa Aigupto ndi Farao pamodzi ndi banja lake lonse.
23 E da nini Idibidi sogega fisili masa: ne, amo nini guiguda: amo soge E da ninia aowalali ilima imunu ilegele sia: i, amo ninima imunusa: oule misi.
Koma anatitulutsa kumeneko ndi kutilowetsa kuno natipatsa dziko limene analonjeza mwa lumbiro kwa makolo athu.
24 Amalalu, ninia Hina Gode da ninima amo sema huluane nabima: ne amola Ema beda: ma: ne sia: i. Amane hamonanu, E da eso huluane ninia fi noga: le ouligimu amola ninia mae ha: ne bagade gaguiwane esaloma: ne fidimu.
Yehova anatilamula kuti tizimvera malamulo onsewa, kuti tizimuopa kuti zinthu zizitiyendera bwino pa moyo wathu monga momwe zilili leromu.
25 Ninia da mae yolesili, Gode Ea sema ninima i amo huluane noga: le nabasea, E da ninima hahawane ganumu.’”
Ndipo ngati tisamala kumvera malamulo onsewa pamaso pa Yehova Mulungu wathu monga momwe anatilamulira ife, chimenecho chidzakhala chilungamo chathu.”

< Mousese Ea Malasu 6 >