< Mousese Ea Malasu 4 >

1 Amalalu, Mousese da Isala: ili dunuma amane sia: i, “Dilia da sema huluane na da waha dilima olelelala, amo huluane nabawane hamosea, dilia da esalumu, amola dilia soge amo dilia aowalali ilia Hina Gode da dilima iaha, amo dilia da gesowale fimu.
Mverani inu Aisraeli, malangizo ndi malamulo amene ndikuphunzitseni. Muwatsatire kuti mukhale ndi moyo ndi kuti mulowe ndi kutenga dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu akukupatsani.
2 Na sema dilima olelesa amoga eno sema mae gilisima, amola amoga mae fadegama. Na da Hina Gode Ea sema dilima i dagoi. Amo huluane nabima.
Musawonjezere pa zimene ndikukulamulirani ndipo musachotserepo, koma muwasunge malamulo a Yehova Mulungu wanu amene ndikukupatsani.
3 Dilisu da Hina Gode Ea hou Bio Goumia ba: i dagoi. E da dunu huluane amo da ogogosu ‘gode’ Ba: ile amoma nodone sia: ne gadosu, amo huluane gugunufinisi dagoi.
Inu munaona ndi maso anu zimene Yehova anachita ku Baala-Peori. Yehova Mulungu wanu anawononga aliyense amene anatsata Baala wa ku Peori pakati panu.
4 Be nowa da dilia Hina Godema fa: no bobogesu hou hame fisi da wali esoga esala.
Koma inu nonse amene munagwiritsitsa Yehova Mulungu wanu mukanali ndi moyo mpaka lero.
5 Na da na Hina Gode nama hamoma: ne sia: i defele, sema huluane dilima olelei dagoi. Dilia da wali Ga: ina: ne soge doagala: le, gesowale fimu. Amo ganodini, amo sema huluane nabawane hamoma.
Taonani, ndakuphunzitsani malangizo ndi malamulo monga Yehova Mulungu wanga anandilamulira kuti inuyo muwatsatire mʼdziko limene mukulowa ndi kulitengali.
6 Dilia amo sema mae yolesili nabawane hamosea, dilia da eno osobo bagade fi dunu ilima, dilia bagade dawa: su hou olelemu. Ilia da amo sema nabasea, ilia da amane sia: mu, ‘Amo Isala: ili dunu da bagade. Ilia asigi dawa: su hou da bagadedafa.’
Muwasunge mosamalitsa pakuti zimenezi zidzaonetsa nzeru zanu ndi kuzindikira kwanu kwa anthu a mitundu ina, amene adzamva za malangizo onsewa nati, “Ndithudi, mtundu waukulu uwu ndi wa anthu anzeru ndi ozindikira.”
7 Ninia da fidisu hanai galea o se nabasea, ninia Hina Gode da nini fidimusa: gadenene esala ba: sa. Ninia da Ema fidima: ne wele adosea, E da hedolo fidimusa: maha. Eno dunu fi huluane, amola bagadedafa fi huluane, da agoaiwane Gode hame gala.
Mtundu wina wa anthu ndi uti umene uli waukulu chomwechi, woti ukhoza kukhala ndi milungu yawo pafupi monga mmene alili Yehova Mulungu wathu ndi ife nthawi zonse pamene tipemphera kwa Iye?
8 Na da wali sema moloidafa amola noga: idafa dilima olelei. Eno dunu fi huluane fonobahadi amola bagadedafa, huluane da agoaiwane sema hame gala.
Ndipo ndi mtundu uti mwa mitundu ya anthu umene ndi waukulu chotere kuti nʼkukhala ndi malangizo ndi malamulo olungama ngati malamulo amene ndikuyika pamaso panu lero?
9 Dawa: ma! Ha: esaloma! Dilia da osobo bagadega esalea, dilia siga ba: i liligi mae gogolema. Dilia mano amola dilia aowa ilima olelema.
Inu mungosamala ndi kudziyangʼanira kwambiri nokha kuti musayiwale zimene maso anu aona. Musalole kuti zichoke mʼmitima mwanu pa moyo wanu wonse. Zimenezi muziphunzitse kwa ana anu ndi zidzukulu zanu ngakhale mʼtsogolo.
10 Dilia da Sainai Goumia Hina Gode amo Ea midadi lelu. E da nama amane sia: i, ‘Dunu fi huluane gilisima. Na hanai da Na dima sia: mu liligi ilia huluane nabimu. Amasea Na da ilima nabasu hou olelemu. Ilia da osobo bagadega esalea, Nama nabasu hou hamomu da defea. Amola ilia da ilia manoma Nama beda: su hou olelemu da defea.’
Kumbukirani tsiku limene munayimirira pamaso pa Yehova Mulungu wanu ku Horebu, pamene anati kwa ine, “Sonkhanitsa anthu pamaso panga kuti amve mawu anga ndi kuti aphunzire kundilemekeza mʼmoyo wawo onse mʼdzikomo ndi kuti ana awo aziwaphunzitsa zimenezi.”
11 Dilia da asili goumi ea baiga lelu. Goumi da bunumai mobi bagade amoga dedeboi dagoi amola lalu bagade ea gona: su da muagado heda: i. Amo hou dilia manoma olelema.
Munabwera pafupi ndi kuyima pa tsinde pa phiri pamene phirilo limayaka moto umene umafika mpaka kumwamba. Panalinso mtambo wakuda ndi mdima wambiri.
12 Hina Gode da lalu ganodini esalebe, amoga E da dilima sia: i. Dilia da Ea sia: nabi be hodo hame ba: i. Amo amola dilia manoma olelema.
Kenaka Yehova anayankhula nanu kuchokera mʼmotowo. Inu munamva mawu ake okha koma simunamuone pakuti panali mawu chabe.
13 Hina Gode da dilima logo olelei. Dilia da Gousa: su amo E da dilima hamoi amo noga: le fa: no bobogema: ne, Hamoma: ne Sia: i Nabuane Gala E da gele gasui aduna da: iya dedei amo nabawane hamoma E sia: i. Amo sia: huluane dilia manoma olelema.
Iye anakuwuzani Malamulo Khumi omwe ndi pangano lake limene anakulamulirani kuti mutsatire. Ndipo anawalemba malamulowo pa mapale awiri a miyala.
14 Hina Gode da nama dilima sema huluane soge wali dilia gesowale fimu amo ganodini fa: no bobogemu amo dilima olelema: ne sia: i.”
Ndipo Yehova anandilamula nthawi imene ija kuti ndikuphunzitseni malangizo ndi malamulo amene muyenera kutsata mʼdziko limene mutenge mukawoloka Yorodani.
15 Mousese da eno amane sia: i, “Hina Gode da Sainai Goumia lalu amo ganodini esalebe dilima sia: noba, dilia da hodo hame ba: i. Amaiba: le, dilia hahawane esaloma: ne, noga: le dawa: ma!
Tsiku limene Yehova anayankhula nanu ku Horebu mʼmoto uja, simunaone thupi lake. Choncho mudziyangʼanire nokha mosamalitsa,
16 Wadela: le hamomusa: dilia loboga hamoi ‘gode’ agoaila: liligi maedafa hamoma.
kuti musasokonezeke ndi kudzipangira nokha fano kapena chifanizo cha mtundu uliwonse, kaya chokhala ngati mwamuna kapena ngati mkazi,
17 Dunu agoai o uda agoai o ohe fi o sio o
kaya chokhala ngati nyama iliyonse ya pa dziko lapansi kapena mbalame iliyonse yowuluka mlengalenga.
18 sania o menabo agoaiwane liligi amoma sia: ne gadomusa: , mae hedofale hamoma.
Kapena cholengedwa chilichonse choyenda pa nthaka kapena nsomba ya mʼmadzi akuya.
19 Amola dilia da eno ilia dafama: ne olelesu nabasea, liligi dilia da mu amo ganodini ba: sa amoma mae nodone sia: ne gadoma. Amo da eso amola oubi amola gasumuni. Hina Gode da amo liligi osobo bagade fifi asi gala ilima i dagoi.
Ndipo pamene muyangʼana kumwamba muona dzuwa, mwezi ndi nyenyezi, zonse zakumwambazo musakopeke kuti muzigwadire ndi kumapembedza zinthu zimene Yehova wapereka kwa anthu a mitundu yonse pa dziko lapansi.
20 Be dilia da hisu. Dilia da Idibidi soge ganodini lalu bagade defele ganodini esalu. Amoga Hina Gode da dili fadegai. E da dilia Ea Fidafa (wali dilia da Ea Fidafa esala) amo hamoma: ne dili gadili oule asi.
Koma inuyo, Yehova anakutengani ndi kukutulutsani mʼngʼanjo yosungunulira zitsulo, ku Igupto kuti mukhale anthu olandira chuma chake monga mmene mulili tsopano.
21 Dilia houba: le, Hina Gode da nama ougi galu. E da nama moloiwane olelei, na da Yodane Hano mae degele, soge noga: idafa E da dilima iaha amo ganodini hamedafa masunu.
Yehova anakwiya nane chifukwa cha inu, ndipo analumbira kwathunthu kuti sindidzawoloka Yorodani ndi kulowa mʼdziko labwinolo limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani inu ngati cholowa chanu.
22 Na da guiguda: bogomu amola hano hamedafa degemu. Be dilia da amo hano degemu amola amo soge noga: idafa gesowale fimu.
Ine ndifera mʼdziko lino, sindiwoloka Yorodani. Koma inu mwatsala pangʼono kuwoloka ndi kukatenga dziko labwinolo.
23 Be dawa: ma! Dilia gousa: su amo Hina Gode da dilima hamoi amo mae gogolema. E da dilima loboga hamoi ‘gode’ liligi maedafa hedofama, amo sema noga: le fa: no bobogema: ne sia: i.
Samalani, musayiwale pangano limene Yehova Mulungu wanu anapangana nanu ndipo musadzipangire nokha fano la chinthu chilichonse chimene Yehova Mulungu wanu waletsa.
24 Bai dilia Hina Gode da lalu bagade defele esala. E da Hi sogebi lamu hanai dunu, ilima bagade higalala.
Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi moto wonyeketsa ndipo ndi Mulungu wansanje.
25 Dilia da amo soge ganodini ode bagohame esalu, mano amola aowa lai dagoi ba: sea, amo esoga amola wadela: i loboga hamoi ‘gode’ liligi ea hodo defele mae hamoma. Bai amo hou Hina Gode Ea siga da wadela: idafa ba: sa, amola E da mi hanamu.
Mukadzakhala nthawi yayitali mʼdzikomo ndi kubereka ana ndi kukhala ndi zidzukulu ndipo mukadzasokonekera ndi kupanga fano la mtundu uliwonse, nʼkumachita zoyipa pamaso pa Yehova Mulungu wanu ndi kumukwiyitsa,
26 Na da wali fedege agoane mu amola osobo bagade, dilima ba: su dunu defele adosa. Dilia da na sia: noga: le hame nabasea, dilia fi da amo soge ganodini eso bagahame fawane esalebe, hedolowane alalolesi dagoi ba: mu. Dilia da soge Yodane Hano la: idi amo dilia da waha gesowale fimu soge amo ganodini ode bagahame fawane esalumu. Dilia fi da dafawanedafa gugunufinisi dagoi ba: mu.
ine ndi kuti kumwamba ndi dziko lapansi zikhale mboni lero zokutsutsani kuti mudzawonongedwa msanga ndipo mudzachotsedwa mʼdziko limene mutenge mukawoloka Yorodani. Simudzakhalitsa kumeneko koma mudzawonongedwa ndithu.
27 Hina Gode da dilia eno fifi asi gala amo ganodini esaloma: ne galadigimu. Amo ganodini dilia dunu da bagahame fawane esalumu.
Yehova adzakubalalitsani pakati pa anthu ena. Ochepa okha pakati panu ndi amene adzapulumuke pakati pa anthu a mitundu ina kumene Yehova adzakupirikitsireniko.
28 Amo ga fifi asi gala ilia soge ganodini esalea, dilia da ogogosu ‘gode’ liligi, osobo bagade dunu ilia loboga hamoi liligi amoga hawa: hamomu. Amo liligi da ifa amola igi, amoga hamoi. Ilia siga hame ba: sa, hame naba, ha: i manu hame naha amola miga hame naba ba: sa.
Kumeneko mudzapembedza milungu ya mitengo ndi miyala yopangidwa ndi anthu, imene singaone kapena kumva kapena kudya kapena kununkhiza.
29 Amo ga fifi asi gala ganodini dilia da dilia Hina Gode hogoi helemu. Dilia da dilia dogo amola asigi dawa: su huluane amoga hogoi helesea, dilia da E bu ba: mu.
Mukanali komweko, ngati mudzamufunafuna Yehova Mulungu wanu mudzamupeza koma ngati mutamufunafuna ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.
30 Dilia se bagade nabasea amola na waha sia: i liligi dilia ba: sea, ouesalu, dilia da Hina Godema sinidigili, Ea sia: bu nabimu.
Mukadzakhala pa chipsinjo ndipo zonsezi zikadzakuchitikirani, ndi pamene pambuyo pake mudzabwerera kwa Yehova Mulungu wanu ndi kumumvera Iye.
31 Hina Gode da gogolema: ne olofosu bagade dawa: E da dili hamedafa yolesimu amola dili hame gugunufinisimu. Amola E da gousa: su amo Hisu dilia aowalali ilima hamoi amo hamedafa gogolemu.
Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu wachifundo, Iye sadzakutayani kapena kukuwonongani kapena kuyiwala pangano lake ndi makolo anu, limene analitsimikiza mwa lumbiro.
32 Musa: hemone dilia da hame lalelegei eso amoga Gode da dunu fi osobo bagadega fima: ne hamoi, amo eso ea hou hogoi helema. Osobo bagade soge huluane amo ganodini hogoi helema. Amo bagade hou Gode da waha hamobe da musa: ba: bela: ? Dunu da amo hou hamoi amo nabibala: ? Hame mabu!
Tsopano tafunsani za masiku a mʼmbuyomu, zakale inu musanabadwe, kuyambira tsiku limene Mulungu analenga munthu pa dziko lapansi. Tafufuzani kuyambira kumapeto mpaka mapeto anzake a thambo. Kodi chinachitikako china chachikulu ngati ichi, kapena chinayamba chamvekako chokhala ngati ichi?
33 Dunu fi afae da Gode laluga ilima sia: i dilia defele nabi, amo bu esalebe ba: bela: ? Hame mabu!
Kodi uliponso mtundu wina wa anthu umene unamva mawu a Mulungu akuyankhula kuchokera mʼmoto nʼkukhala ndi moyo monga mwachitira inumu?
34 Eno ‘gode’ liligi da mae beda: iwane dunu fi afae amo eno dunu fi amoga fisili masa: ne, ea fidafa hamoi, dilia Hina Gode da Idibidi soge dilima hamoi defele, eno ‘gode’ da agoane hamobela: ? Hame mabu! Dilia siga ba: ma: ne E da Ea gasa bagadega hamoi. E da olo bagade amola gegesu bagade hamoi. E da musa: hame ba: su dawa: digima: ne olelesu amola beda: su bagade liligi hamoi dagoi.
Kodi alipo mulungu amene anayeserapo kudzitengera mtundu wa anthu kuwachotsa mu mtundu unzake mwa mayesero, zizindikiro zozizwitsa, nkhondo, komanso mwa mphamvu zake zopanda malire, kapena mwa zochita zazikulu ndi zochititsa mantha, monga zimene Yehova Mulungu wanu anakuchitirani ku Igupto inu mukupenya?
35 Hina Gode Hisu da Gode - eno hame - amo dilima olelema: ne, Hina Gode da amane hamoi.
Iye anakuonetsani zonsezi kuti inu muzindikire kuti Yehova ndiye Mulungu, palibenso wina wofanana naye.
36 E da dilima olelema: ne, Hebene soge amoga dilima sia: i. Amola osobo bagadega E da Ea Hadigi lalu dilima olelei, amola amoga dilima sia: i.
Kuchokera kumwamba, Iye anafuna kuti inu mumve mawu ake ndi kuti mukhale osunga mwambo. Pa dziko lapansi anakuonetsani moto waukulu, ndipo inu munamva mawu ake kuchokera mʼmotomo.
37 E da dilia aowalali ilima asigiba: le, dili ilegei, amola Hisu da Ea gasa bagade amoga dili Idibidi soge fisili masa: ne gadili hiougi.
Popeza anakonda makolo anu ndi kusankha adzukulu awo, a pambuyo pawo, anakutulutsani kuchoka ku Igupto ali pakati panu ndi mphamvu yake,
38 Dilia da gusuba: i ahoanoba, E da dunu fi amo ilia idi amola gasa da dili baligi, amo sefasi. Bai E da dili amo ilia soge ganodini (amo da wali dilia soge) oule masunu hanai galu.
kuti akupirikitsireni mayiko akuluakulu ndi amphamvu kuposa inu, ndi kukubweretsani inu ku dziko lawo kuti likhale lanu, monga liliri lero.
39 Amaiba: le, wali eso maedafa gogolema! Hina Gode da Godedafa Hebene ganodini amola osobo bagadega. Eno ‘gode’ da hamedafa.
Vomerezani lero ndipo dziwani mu mtima mwanu kuti Yehova ndiye Mulungu kumwamba ndi pa dziko lapansi. Palibenso wina.
40 Dilia Ea sema huluane na da wali eso dilima olelei, amo nabawane hamosea, dilia amola diligaga fi da hahawane esalumu. Amola dilia da mae fisili, amo soge dilia Hina Gode da dili eso huluane amo ganodini esalalaloma: ne dilima iaha, amo ganodini esalalalumu.”
Sungani malangizo ake ndi malamulo ake amene ndikukupatsani lero lino, kuti zikuyendereni bwino inu ndi ana anu kutsogoloko, ndi kuti mukhalitse mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kwa nthawi zonse.
41 Amalalu, Mousese da moilai bai bagade udiana Yodane Hano eso maba gusudili ilegei.
Kenaka Mose anapatula mizinda itatu cha kummawa kwa Yorodani,
42 Amo moilai bai bagade da Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade. Nowa dunu da ea ha lai dunu hame amomane mae ougili giadofale medole legesea, e da amo moilaiga hobeale ahoasea, maga: me dabe iasu dunu amoga mae medole legele, gaga: su ba: mu.
kumene aliyense amene wapha munthu akhoza kuthawirako ngati wopha munthuyo sanaphe mnzakeyo mwadala ndi maganizo oyipa. Iye akhoza kuthawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi napulumutsa moyo wake.
43 Liubene fi dunu ilia Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade da Bisa (hafoga: i bi da: iya umi sogega dialu). Ga: de fi dunu ilia Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade da Lamode (Gilia: de soge amo ganodini). Amola Eso Mabadili Mana: se fi dunu ilia Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade da Golane (Ba: isia: ne soge amo ganodini).
Mizindayo inali iyi: ku fuko la Rubeni, unali mzinda wa Bezeri ku mapiri a ku chipululu; ku fuko la Gadi, unali Ramoti ku Giliyadi; ndipo ku fuko la Manase, unali Golani ku Basani.
44 Mousese da Gode Ea sema amola Ea olelei huluane Isala: ili dunu fi ilima i.
Awa ndi malamulo amene Mose anapereka kwa Aisraeli.
Izi ndi ndondomeko, malangizo ndi malamulo amene Mose anawapatsa iwo pamene anatuluka ku Igupto.
46 Ilia da Idibidi soge yolesili, fago soge Yodane Hano eso mabe la: ididili Bedebio la: ididili esaloba, amo sema ilima olelei. Amo soge da musa: hina bagade Saihone, A:moulaide ouligisu musa: Hesiabone moilaiga esalu, amo ea soge. Mousese amola Isala: ili dunu fi da Idibidi soge yolesili amo hina bagade dunu hasali.
Anali ku chigwa cha kufupi ndi Beti-Peori mbali ya kummawa kwa Yorodani, mʼdziko la Sihoni mfumu ya Aamori amene ankalamulira ku Hesiboni ndipo anagonjetsedwa ndi Mose ndi Aisraeli pamene ankachokera ku Igupto.
47 Ilia da ea soge gesowale fi amola hina bagade Oge (Ba: isia: ne soge ouligisu, e amola da A: moulaide dunu Yodane Hano eso mabe la: ididili esalu) amo ea soge fedelale fi.
Iye anamulanda dziko lake ndi dziko la Ogi mfumu ya ku Basani. Awa anali mafumu awiri Aamori a kummawa kwa Yorodani.
48 Amo soge da Aloua moilai (Anone Hano bega: dialu) amo oleiga asili Silione Goumi (eno dio Hemone Goumi) amoga doaga: i.
Dziko ili linayambira ku Aroeri cha kumphepete kwa khwawa la Arinoni ku phiri la Siyoni (limeneli ndi phiri la Herimoni),
49 Soge huluane Yodane Hano eso mabe bega: ga (north) asili Bogoi Hano Wayabo doaga: i amola eso mabe amoga asili Bisiga Goumi amoga doaga: i, amo soge huluane da ilia lai soge ganodini dialu.
ndi kuphatikizapo dziko lonse la Araba cha kummawa kwa Yorodani mpaka kukafika ku Nyanja ya Araba, kumunsi kwa Phiri la Pisiga.

< Mousese Ea Malasu 4 >