< Mousese Ea Malasu 19 >
1 Hina Gode da dunu fi amo da wali soge amo E da dilima iaha amo ganodini esala, amo E da gugunufinisimu. Amasea, dilia da ilia moilai bai bagade amola ilia diasu huluane lale, amo ganodini fimu.
Yehova Mulungu wanu akadzawononga anthu amene dziko lawo akukupatsani, ndipo inu mukawapirikitsa ndi kukhazikika mʼmizinda ndi mʼnyumba zawo,
mukapatule mizinda itatu imene ili pakati pa dziko lomwe Yehova Mulungu akukupatsani kukhala lanu.
3 Amo fa: no, dilia da amo soge fifili, soge udiana agoane ilegema. Amo udiana afae afae soge dogoa ganodini moilai bai bagade afae ilegema. Amasea, dunu da mae ougili giadofale dunu eno medole legesea, e da hehenane amo moilai bai bagade ganodini gaga: su ba: mu.
Mudzakonze misewu ndi kuligawa patatu dzikolo limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani ngati cholowa chanu, kuti aliyense wopha munthu akhoza kuthawirako.
4 Dunu afae da dunu eno ema ha lai dunu hame be dunu eno mae ougili giadofale medole legesea, e da amo moilaiga hobeale ahoasea, gaga: su ba: mu.
Ili ndi lamulo lokhudza munthu amene wapha mnzake mosazindikira osati mwadala, nathawira kumeneko kupulumutsa moyo wake. Ndi munthu amene wapha mnzake mosazindikira, popanda maganizo oyipa.
5 Fedege sia: agoane, dunu aduna da iwilaga ifa aba ahoasea, afae da ifa abasea goahei ea dialuma da da: ba: ga duga: gala: le eno dunu medole legesea, ifa abasu dunu da hobeale Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade udiana amo afaega masunu da defea.
Mwachitsanzo, munthu atapita ku nkhalango ndi mnzake kukadula mitengo, ndiye posamula nkhwangwa kuti adule mtengo, nkhwangwa ikhoza kuguluka nʼkukagwera mnzake uja nʼkumupha. Munthu ameneyo akhoza kuthawira ku umodzi mwa mizindayo napulumutsa moyo wake.
6 Moilai bai bagade udiana ilegemu da defea. Be moilai bai bagade afae fawane ilegesea, dunu da amoga hobeale ahoasea logo sedade ba: mu. Amasea, maga: me dabe imunu dunu da amo dunu baligisia, ougiba: le medole legemu. Be amo da defea hame. Bai amo dunu da ougiba: le o hanaiba: le ea na: iyado hame medole legei be mae ougili giadofale fawane medoi.
Kupanda kutero ndiye kuti wolipsira akhoza kumuthamangitsa mwaukali ndi kumugwira ngati mtunda utalika, ndipo akhoza kumupha ngakhale kuti sanayenera kufa popeza sanaphe mnzake mwadala.
7 Amaiba: le, na da dilima sia: sa. Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagade udiana ilegema.
Ichi ndi chifukwa chake ndikukulamulani kuti mudzipatulire nokha mizinda itatu.
8 Dilia Hina Gode da dilia aowalali ilima ilegele sia: i defele dilia soge bu bagade hamosea, amola dilima imunu ilegele sia: i soge huluane dilima i dagosea,
Ngati Yehova Mulungu wanu akulitsa malire anu monga analonjezera pa malumbiro ndi makolo anu, nakupatsani dziko lonse monga analonjezera,
9 dilia moilai bai bagade udiana eno ilegema. (Dilia da na sia: i liligi huluane noga: le nabasea amola dilia Hina Godema asigisia amola Ea olelesu defele esalea, E da amo soge dilima imunu.)
chifukwa chotsatira bwino malamulo onse amene ndikukuwuzani lero, kukonda Yehova Mulungu wanu ndi kuyenda mʼnjira zake nthawi zonse, ndiye kuti mukuyenera kupatula mizinda itatu yowonjezera.
10 Wadela: i hame hamosu dunu da udigili bogosa: besa: le, amola dilia da soge Hina Gode da dilima iaha amo ganodini wadela: i hame hamosu dunu udigili medole legesa: besa: le, Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilale bai bagade ilegema.
Muchite zimenezi kuti musakhetse magazi wosalakwa mʼdziko lanu limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani ngati cholowa, ndipo kuti musapezeke ndi mlandu wokhetsa magazi.
11 Be dunu afae da ougiba: le amola hanaiba: le ema ha lai dunu medole legesea amola ea maga: me da ahoa, amasea e da Dabe Fasa: besa: le Gaga: su Moilai bai bagadega hi esalusu gaga: musa: ahoasea,
Koma ngati munthu adana ndi mnzake namubisalira panjira nʼkumuvulaza mpaka kumupha, nathawira ku umodzi mwa mizindayi,
12 amo dunu hi moilai asigilai dunu ilia da e da ilima misa: ne sia: mu. Amasea, ilia da medole bogoi dunu amo ea fi dabe iasu dunu ema imunu. Amola amo dunu da fasu dunu medole legemu.
akuluakulu a mu mzinda wake akamugwire ndi kumubwezera ku mzinda wake namupereka kwa wolipsira kuti aphedwe.
13 Agoai dunuma mae asigima. Amo fasu dunu da Isala: ili fi ganodini esalumu hamedei. Dilia da hahawane hou ba: ma: ne, amo dunu medole legema.
Osamumvera chisoni. Muyenera kuchotsa tchimo lokhetsa magazi wosalakwa mu Israeli kuti zinthu zizikuyenderani bwino.
14 Dilia na: iyado dunu ea soge alalo amo mae afadenema. Amo ilegei ilia da musa: hemonega soge amo dilia Hina Gode da dilima iaha amo ganodini hamosu.
Musamasunthe mwala wa malire anu ndi mnzanu amene anayikidwa ndi makolo anu pa cholowa chimene mulandire mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.
15 Dunu afae fawane da ba: i dagoiba: le, dunu da wadela: le hamoi dagoi mae sia: ma. Ba: su dunu aduna o amo idi baligi ilia da wadela: i hou hamoi ba: i dagoi sia: sea fawane fofada: ma.
Mboni imodzi siyokwanira kupeza munthu kuti ndi wolakwa pa mlandu uliwonse umene wapalamula. Nkhani itsimikizike ndi umboni wa anthu awiri kapena atatu.
16 Be dunu afae da eno dunu gugunufinisimusa: , ogogole e da wadela: i hamoi dagoi sia: sea,
Ngati mboni yonama ifuna kunamizira munthu mlandu,
17 ela da Gode Ea ilegei sogebi amoga asili, gobele salasu dunu amola fofada: su dunu (amo esoga ilegei), ilia da amo dunu ilima fofada: mu.
anthu awiri okhudzidwa ndi mlanduwo ayenera kuyima pamaso pa Yehova pali ansembe ndi oweruza amene ali pa ntchito pa nthawiyo.
18 Fofada: su dunu da amo hou noga: le fofada: mu. Be amo dunu da ogogole ea na: iyado Isala: ili dunu amo wadela: musa: sia: i dagoi ba: sea,
Oweruza afufuze bwinobwino, ndipo ngati zatsimikizika kuti mboniyo ndi yabodza, yopereka umboni wonama pa mʼbale wake,
19 e da se nabasu amo se nabasu eno dunuma e da ogogoi defele lamu galu, amo lamu. Amasea, dilia da wadela: i hou fadegamu.
ndiye kuti amuchitire iyeyo zimene anafuna kuchitira mʼbale wakezo. Muyenera kuchotsa choyipa pakati panu.
20 Amo hou, dunu huluane da nabimu. Amasea, ilia da beda: iba: le, agoai wadela: i hou bu hamedafa ba: mu.
Anthu ena onse adzamva zimenezi nachita mantha, ndipo choyipa choterechi sichidzachitikanso pakati panu.
21 Amo hou amoma mae asigima. Dunu da eno dunu medole legesea, amo dunu medole legema. E da eno ea si wadela: sea, ea si amola wadela: ma. Eno ea bese gusia, ea bese guma. Eno ea emo wadela: sea, ea emo wadela: ma.
Osachita chisoni, moyo uzilipira moyo, diso kulipira diso, dzino kulipira dzino, dzanja kulipira dzanja ndi phazi kulipira phazi.