< A:imose 7 >
1 Na da esala ba: i amo ganodini Ouligisudafa Hina Gode ba: i. Isala: ili hina bagade ea gisi da noi dagoi amola gisi da bu heda: lebe amo esoga Hina Gode da danuba: wa: i bagadedafa hamonanebe ba: i.
Zimene Ambuye Yehova anandionetsa ndi izi: Yehova ankasonkhanitsa gulu la dzombe nthawi imene gawo la zokolola za mfumu linali litakololedwa kale ndipo mbewu zachiwiri zinali zitangoyamba kumera kumene.
2 Na esala ba: i amo ganodini, na da danuba: mola: ya: i liligi huluane soge ganodini amo na dagoi ba: i. Amalalu, na da amane sia: i, “Ouligisudafa Hina Gode! Dia fi ilia hou gogolema: ne olofoma! Ilia da habodane esaloma: bela: ! Ilia da fonobahadi amola gasa hame!”
Dzombelo litadya zomera zonse za mʼdzikomo, Ine ndinafuwula kuti, “Ambuye Yehova, khululukani! Kodi Yakobo adzapulumuka bwanji? Iye ndi wofowoka kwambiri!”
3 Hina Gode da Ea asigi dawa: su afadenene, amane sia: i, “Dia esala ba: i amo da dafawane hame ba: mu.”
Kotero Yehova anakhululuka. Yehovayo anati, “Izi sizidzachitika.”
4 Ouligisudafa Hina Gode da nama esala ba: su eno olelei. E da Ea fi dunu se dabe iasu ima: ne, lalu didilalu. Lalu da hano wayabo bagade osobo hagudu diala amo nei dagoi. Amalalu, lalu da osobo bagade amola amo nemusa: muni nenanu.
Zimene Ambuye Yehova anandionetsa ndi izi: Ambuye Yehova ankayitana malawi a moto kuti alange anthu. Motowo unawumitsa nyanja yakuya ndi kupsereza dziko.
5 Amalalu, na amane sia: i, “Hame mabu! Ouligisudafa Hina Gode mae! Dia fi da habodane esaloma: bela: ? Ilia da fonobahadi amola gasa hame!”
Tsono ine ndinafuwula kuti, “Ambuye Yehova, chonde ndikukupemphani, lekani! Kodi Yakobo adzapulumuka bwanji? Iye ndi wofowoka kwambiri!”
6 Hina Gode da bu Ea asigi dawa: su afadenene, amane sia: i, “Amo amola da hame ba: mu.”
Kotero Yehova anakhululuka. Ambuye Yehova anati, “Izinso sizidzachitika.”
7 Ouligisudafa Hina Gode da nama esala ba: su eno olelei. Amo ganodini na da Hina Gode dobea gagui (amo da ogoma efe ilegesu amoga defei) amo dafulili lelebe ba: i. Ea lobo ganodini, ogoma efe ilegesu dialebe ba: i.
Zimene Iye anandionetsa ndi izi: Ambuye anayima pambali pa khoma lomangamanga, mʼmanja mwake muli chingwe chowongolera khoma.
8 E da nama amane adole ba: i, “A: imose! Di da adi ba: sala: ?” Na da bu adole i, “Na da ogoma efe ilegesu ba: sa!” Amalalu, E da nama amane sia: i, “Amoga Na da dima olelesa. Na fi dunu da dobea noga: le hame ilegele gagui defele esala. Na da ilima se dabe iasu ima: ne Na asigi dawa: su bu hame afadenemu.
Ndipo Ambuye anandifunsa kuti, “Amosi, nʼchiyani ukuonachi?” Ine ndinayankha kuti, “Chingwe chowongolera khoma.” Ndipo Yehova anati, “Taona, Ine ndikuyika chingwe chowongolerachi pakati pa anthu anga, Aisraeli; sindidzawalekereranso.
9 Aisage egaga fi ilia nodone sia: ne gadosu sogebi huluane da wadela: lesi dagoi ba: mu. Isala: ili soge hadigi sogebi huluane da wadela: lesi dagoi ba: mu. Na da hina bagade Yelouboua: me ea fi hina bagade hou huluane wadela: lesi dagomu.”
“Malo achipembedzo a Isake adzawonongedwa ndipo malo opatulika a Israeli adzasanduka bwinja; ndidzagwetsa nyumba ya Yeroboamu ndi lupanga langa.”
10 A: masaia, Bedele gobele salasu dunu, da Yelouboua: me (Isala: ili hina bagade) ema sia: ne iasi amane, “A: imose da di wadela: ma: ne dunu huluane ilima hohonone sia: daha. Ea sia: da ninia soge fi huluane wadela: lesimu.
Pamenepo Amaziya wansembe wa ku Beteli anatumiza uthenga kwa Yeroboamu mfumu ya Israeli kuti, “Amosi akukuutsirani chiwembu pakati pa Aisraeli. Dziko silingalekerere zonena zake zonsezo.
11 E da amane sia: daha, ‘Yelouboua: me da gegesu ganodini bogomu. Isala: ili fi dunu huluane da ilia sogega fadegale, ga soge amo ganodini mugululi asi dagoi ba: mu.’”
Pakuti zimene Amosi akunena ndi izi: “‘Yeroboamu adzaphedwa ndi lupanga, ndipo Israeli adzapita ndithu ku ukapolo, kutali ndi dziko lake.’”
12 Amalalu, A:masaia da A: imosema amane sia: i, “Balofede dunu! Ouiya: ma! Eno hame! Di Yuda sogega buhagili, amogai dia sia: olelema. Ilia fawane da dia sia: beba: le, bidi imunu da defea.
Ndipo Amaziya anawuza Amosi kuti, “Choka, mlosi iwe! Bwerera ku dziko la Yuda. Uzikalosera kumeneko ndipo anthu a kumeneko azikakudyetsa.
13 Be Bedele moilai guiguda: ba: la: lusu sia: bu mae sia: ma. Bai amo sogebi da Isala: ili hina bagade ea nodone sia: ne gadosu sogebi amola Isala: ili fi ilia Debolo sogebi.”
Usanenerenso ku Beteli, chifukwa kumeneko ndi malo opatulika a mfumu ndiponso ndi malo a nyumba yachipembedzo yaufumu.”
14 A: imose da bu adole i, “Na da bidi lama: ne ba: la: lusu hou hame hamosa. Na da sibi ouligisu dunu amola figi ifa ouligisu dunu.
Amosi anayankha Amaziya kuti, “Ine sindine mneneri kapena mwana wa mneneri; koma ndine woweta ziweto, ndiponso mlimi wa nkhuyu.
15 Be Hina Gode da na sibi ouligisu hawa: hamosu fisili, ea fi Isala: ili dunuma fa: no misunu hou olelema: ne sia: i.
Koma Yehova ananditenga ndikuweta nkhosa ndipo anati, ‘Pita ukanenere kwa anthu anga Aisraeli.’
16 Amaiba: le, wali Hina Gode Ea sia: nabima! Di da nama na da ba: la: lusu fisili, Isala: ili dunuma dadousa gagabosu sia: bu mae hamoma: ne sia: sa.
Tsono imva mawu a Yehova. Iwe ukunena kuti, “‘Usanenere zotsutsa Israeli, ndipo siya kulalikira motsutsa nyumba ya Isake.’”
17 Amaiba: le, A:masaia, Hina Gode da dima amane sia: sa, ‘Dia uda da di fisili, udigili moilai bai bagade ganodini ea da: i dunuma udigili bidi lamu. Amola dia mano huluane gegesu ganodini medole legei dagoi ba: mu. Dia soge da fifili, eno dunuma i dagoi ba: mu. Amola disu da Gode Ea hou hame lalegagui ga soge amo ganodini bogomu. Amola Isala: ili dunu da dafawane ilia sogega fadegale, eno sogega mugululi asi dagoi ba: mu.”
“Tsono zimene akunena Yehova ndi izi: “‘Mkazi wako adzasanduka wachiwerewere mu mzindamu, ndipo ana ako aamuna ndi aakazi adzaphedwa ndi lupanga. Munda wako udzayezedwa ndi chingwe ndi kugawidwa, ndipo iwe mwini udzafera mʼdziko la anthu osapembedza Mulungu. Ndipo Israeli adzatengedwa ndithu kupita ku ukapolo, kutali ndi dziko lake.’”