< 2 Sa:miuele 1 >

1 Solo da bogoloba, Da: ibidi da A: malege fi dunu ilima hasalasilalu, Sigela: ge moilai bai bagadega buhagili, eso aduna esalu.
Atamwalira Sauli, Davide anabwerako kumene anakagonjetsa Aamaleki ndipo anakakhala ku Zikilagi masiku awiri.
2 Amalalu, diahabe goi ayeligi afae da Solo ea fisisu awali diasu amoganini manebe ba: i. Ea da: i dioi dawa: digima: ne, e abula gadelale amola e da osobo ea dialuma da: iya duduli gala: i ba: i. E da Da: ibidima misini, ema nodone dawa: digima: ne osoboga beguduli diasa: i.
Pa tsiku lachitatu munthu wina wochokera ku msasa wa Sauli anafika, zovala zake zitangʼambika ndiponso anali atathira dothi pamutu pake. Atafika kwa Davide, anadzigwetsa pansi, kupereka ulemu kwa Davideyo.
3 Da: ibidi da ema amane adole ba: i, “Di da habogainini misibala: ?” Ayeligi da bu adole i, “Na da Isala: ili ilia ha wa: i fisisu amoganini hobeale misi.”
Davide anamufunsa iye kuti, “Kodi iwe wachokera kuti?” Iye anayankha kuti, “Ine ndathawa ku misasa ya Aisraeli.”
4 Da: ibidi da amane sia: i, “Di da gegei amo hou huluane nama adodole ima.” Ayeligi dunu da amane sia: i, “Ninia dadi gagui dunu da huluane gegesu amoba: le hobeale asi dagoi. Amaiba: le, ninia dunu da bagohame bogogia: i dagoi. Solo amola ea mano Yonada: ne da elegalu bogoi dagoi.”
Davide anafunsa, “Tandiwuza, chachitika ndi chiyani?” Iye anati, “Anthu athawa ku nkhondo ndipo ambiri aphedwa. Sauli ndi mwana wake Yonatani aphedwa.”
5 Da: ibidi da ema adole ba: i, “Di da Solo amola Yonada: ne ela bogoi da habodane dawa: bela: ?”
Ndipo Davide anati kwa mnyamata amene anabweretsa nkhaniyi, “Ukudziwa bwanji kuti Sauli ndi mwana wake Yonatani afa?”
6 Ayeligi da bu adole i, “Na da Giliboua agolo amo da: iya lela ba: i, Solo da ea gogega udidili lelebe ba: i, amola ha lai dunu ilia sa: liode, amola dunu ilia da hosi da: iya fila heda: i amola da gagadenena ahoanebe ba: i.
Mnyamatayo anati, “Zinangochitika kuti ndinali pa phiri la Gilibowa, ndipo Sauli anali komweko ataweramira pa mkondo wake, pamodzi ndi magaleta ndi okwera ake atamuyandikira.
7 Amalu Solo da beba: loba, na ba: beba: le, e da nama wele sia: i. Na da bu ema adole i `Wae! Ada!’
Pamene anatembenuka ndi kundiona ine, iye anandiyitana, ndipo ndinati, ‘Kodi ndichite chiyani?’”
8 E da na nowayale naba ba: i. Na da bu adole i, `Na da A: malege dunu.’
Iye anandifunsa, “Iwe ndiwe yani?” Ine ndinayankha kuti, “Ndine Mwamaleki.”
9 Amalu e da amane sia: i, `Di da guiguda: misini, na fane legema! Na da baligiliwane fane odahida: iba: le, na da bogomu gadenei esala.’
“Kenaka iye anati kwa ine, ‘Bwera pafupi ndipo undiphe! Ndikumva ululu kwambiri, koma ndikanali ndi moyo!’
10 Amaiba: le, na da ema gadenena heda: le, e fane legei dagoi. Bai na dawa: loba ea bogomu asigi dawa: su amo gisigisia, bogomu agoane ba: i. Amanoba na da ea dialuma da: iya habuga amola ea lobofasele fei huluane lale, dima gaguli misi wea!”
“Kotero ndinabwera pafupi ndi kumupha, chifukwa ndinadziwa kuti mmene anagweramo sakanakhalanso ndi moyo. Ndipo ndatenga chipewa chaufumu chimene chinali pamutu pake ndi khoza la pa dzanja lake ndipo ndazibweretsa kwa inu mbuye wanga.”
11 Da: ibidi da da: i dione fofagiba: le, ea abula huluane gagadelai. Amola ea fi dunu ilia da amo defele ilila: abula gagadelai.
Apo Davide ndi anthu onse amene anali nawo anangʼamba zovala zawo.
12 Ilia da Hina Gode Ea fi Isala: ili dunu bagohame amola Solo amola Yonada: ne ilia da bogogia: i amo dawa: beba: le, ilia da ha: i mae nawane didigia: lala soge gasi.
Iwo analira maliro ndi kusala zakudya mpaka madzulo chifukwa cha Sauli ndi mwana wake Yonatani, komanso chifukwa cha gulu la ankhondo la Yehova ndi nyumba ya Israeli, chifukwa anaphedwa ndi lupanga.
13 Da: ibidi da amo sia: gaguli misi ayeligi ema adole ba: i, “Di da nowa fi dunula: ?” E da bu adole i, “Na da A: malege fi dunu, be amomane na da soge dia ouligi amo ganodini esala.”
Davide anati kwa mnyamata amene anabweretsa uthengawo, “Iwe umachokera kuti?” Iye anayankha kuti, “Ine ndine mwana wa mlendo Mwamaleki.”
14 Da: ibidi da ema amane adole ba: i, “Abuliba: le di da Hina Gode Ea ilegei Hina bagade amo fane legemu amo hame beda: bela: ?”
Davide anamufunsanso kuti, “Nʼchifukwa chiyani sunaope kukweza dzanja lako ndi kupha wodzozedwa wa Yehova?”
15 Amalu, Da: ibidi da ea dunu afae misa: ne sia: i, amalu ema amane sia: i, “Goe dunu fane legema!” Amabeba: le, e da amo ayeligi fane legei dagoi.
Kenaka Davide anayitana mmodzi mwa anyamata ake ndipo anati, “Pita ukamukanthe!” Kotero iye anapita kukamukantha, ndipo mnyamata uja anafa.
16 Amola Da: ibidi da A: malege dunu bogolala amo ba: lu, e da amane sia: i, “Di bogoma: ne di fawane olela misi dagoi. Di da Hina Gode Ea ilegei hina bagade amo dia fane legei sia: i dagoiba: le, di fawane da dima bogoma: ne fofada: i dagoi.”
Pakuti Davide anali atanena kwa iye kuti, “Iwe wadzipha wekha. Pakamwa pako pakunena zokutsutsa wekha, pamene unanena kuti, ‘Ine ndapha wodzozedwa wa Yehova.’”
17 Da: ibidi da Solo amola egefe Yonada: ne elama asigili, goe fofagini disu gesami hea: i.
Davide anayimba nyimbo iyi ya maliro, kulira Sauli ndi mwana wake Yonatani.
18 Amola Da: ibidi da amo gesami ilia da Yuda dunu fi huluane ilima olelema: ne sia: i. (Amo gesami da Ya: isia Buga ganodini dialoma: ne dedene legei.)
Ndipo analamula kuti anthu a ku Yuda aphunzitsidwe nyimbo ya maliroyi imene yalembedwa mʼbuku la Yasari:
19 “Isala: ili agolo amo da: iya ninia ouligisu dunu da bogogia: i dagoi. Ninia gasa bagadedafa dadi gagui dunu bagohame da amogai dafane bogoi dagoi.
“Ulemerero wako iwe Israeli, wagona utaphedwa ku zitunda. Taonani amphamvu agwa kumeneko!
20 Ga: de moilai bai bagadega amola Asegelone logoga maedafa adole gama. Filisidini uda ilia hahawane nodosa: besa: le, mae adole gama. Wadela: i fi ilia idiwi ilia gadele osa: besa: le, mae sia: ma.
“Musakanene zimenezi ku Gati, musazilengeze ku misewu ya ku Asikeloni, kuti ana aakazi a Afilisti angasangalale, ana aakazi a osachita mdulidwe angakondwere.
21 Giliboua agolo amoga da gibu amola oubi mogele hamedafa sa: imu da defea. Giliboua bugili nasu soge amoga ha: i manu hamedafa heda: mu da defea. Ninia gasa bagade dadi gagui dunu ilia ibidigi da ilia gogosiasu olelema: ne amogai diafula. Be Solo ea ibidigi da doga: le susuligi amoga legesu, be wali da hame legesa.
“Inu mapiri a ku Gilibowa, musakhalenso ndi mame kapena mvula, kapena minda yobereka zopereka za ufa. Pakuti kumeneko chishango cha munthu wamphamvu chinadetsedwa, chishango cha Sauli sanachipakenso mafuta.
22 Yonada: ne ea dadi da giolasi galu. Be Solo ea gegesu gobihei sedadega mae dawa: le, buluduli fane legele, maga: me bususu dawa: i.
“Pa magazi a ophedwa, pa mnofu wa amphamvu, uta wa Yonatani sunabwerere, lupanga la Sauli silinabwere chabe.
23 Solo amola Yonada: ne ela da noga: idafa amola hahawanedafa galu. Ele galu esalu, amola ele galu bogoi. Ela da buhiba ea hagili ahoasu baligi, amola elea gasa da laione wa: me ea gasa baligi dagoi.
“Sauli ndi Yonatani, pa moyo wawo anali okondedwa ndi okoma mtima, ndipo pa imfa yawo sanasiyanitsidwe. Iwo anali ndi liwiro loposa ziwombankhanga, anali ndi mphamvu zoposa mkango.
24 Dilia Isala: ili uda! Dilia huluane Soloma asigiba: le dadawa: loma. E da dilima abula yoi noga: idafa dilima ga: ma: ne i. Amola e da dili nina: hamoma: ne, gouli amola igi ida: iwane dilima iasu.
“Inu ana aakazi a Israeli, mulireni Sauli, amene anakuvekani zovala zofiira ndi zofewa, amene anakometsera zovala zanu ndi zokometsera zagolide.
25 Ninia gesa: i dadi gagui dunu ilia da dafane bogogia: i. Ilia da gegenana bogogia: i. Yonada: ne da agolo amoga dafane bogoi diala.
“Taonani amphamvu agwa ku nkhondo! Yonatani wagona ataphedwa ku zitunda.
26 Naeya Yonada: ne! Na da diha fofagini disa. Di da na dogolegeidafa galu. Amola di da nama dogolegeidafa galu. Dia nama dogolegesu hou da udama magedasu hou amo da baligili ba: su.
Ine ndikuvutika mumtima chifukwa cha iwe mʼbale wanga Yonatani, unali wokondedwa kwambiri kwa ine. Chikondi chako pa ine chinali chopambana, chopambana kuposa chikondi cha akazi.
27 Gesa: i dadi gagui da dafane bogoi dagoi. Ilia gegesu liligi da udigili fisili, gugunufinisi dagoi ba: sa.”
“Taonani amphamvu agwa! Zida zankhondo zawonongeka!”

< 2 Sa:miuele 1 >