< 2 Hina 12 >

1 Isala: ili hina bagade Yihiu da Isala: ili soge ode fesuale ouligilalu, Youa: se da muni Yuda hina bagade hamoi. E da Yelusaleme moilai bai bagade ganodini esala, ode 40agoanega Yuda fi ouligilalu. Ea ame da Biasiba moilai uda galu, ea dio amo Sibia.
Mʼchaka chachisanu ndi chiwiri cha Yehu, Yowasi anakhala mfumu, ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka makumi anayi. Amayi ake anali Zibiya wa ku Beeriseba.
2 Youa: se ea esalusu huluane amoga, Hina Gode hahawane ba: ma: ne hou hamonanusu. Bai gobele salasu dunu Yihoida da hou noga: idafa ema olelei.
Yowasi anachita zolungama pamaso pa Yehova masiku onse amene wansembe Yehoyada ankamulangiza.
3 Be e da Gode Ea hou hame lalegagui dunu ilia ogogosu ‘gode’ma nodone sia: ne gadosu sogebi, amo hame wadela: lesi, amola amogawi Yuda fi dunu mogili da ohe amola gabusiga: manoma gobele sasalilalu.
Komabe sanachotse malo opembedzerapo mafano ndipo anthu anapitiriza kupereka nsembe ndi kufukiza lubani ku malo opembedzerako mafanowo.
4 Youa: se da gobele salasu dunu ili ema misa: ne sia: ne, ilia da muni amo da Debolo diasuga gobele salimusa: lai, amola hahawane udigili iasu muni, amo huluane momagele lelegema: ne sia: i.
Yowasi anati kwa ansembe, “Tolerani ndalama zonse zimene zimaperekedwa monga chopereka chopatulika ku Nyumba ya Yehova, ndalama zonse zamsonkho wa munthu aliyense, ndalama zomwe munthu amapereka akalonjeza ndiponso ndalama zimene munthu amapereka mwaufulu ku Nyumba ya Yehova.
5 Gobele salasu dunu afae afae ilia da muni ouligisu dunu ilia muni ilima i amoga lale, ilia da Debolo liligi wadela: lesi amo ba: sea, bu hahamoma: ne, Youa: se ea sia: i.
Wansembe aliyense alandire ndalamazo kuchokera kwa abwenzi ake, ndipo zigwiritsidwe ntchito yokonzera chilichonse chimene chipezeke kuti ndi chowonongeka mʼnyumbayo.”
6 Be Youa: se ea ouligibi ode23 agoane da doaga: loba, gobele salasu dunu ilia da bu hame hahamobeba: le, Debolo Diasu da hame hahamoi dialebe ba: i.
Koma pofika chaka cha 23 cha ufumu wa Yowasi, ansembewo anali asanakonze nyumbayo.
7 Amaiba: le, Youa: se da Yihoida amola gobele salasu dunu huluane ema misa: ne sia: ne, amola ilima amane adole ba: i, “Dilia da abuliba: le Debolo Diasu bu hame hahamosala: ? Wali weganini, dilia muni lai amo mae modalegema! Dilia amo muni noga: le ouligima: ne, ouligisu dunuma ima.”
Choncho Mfumu Yowasi inayitanitsa wansembe Yehoyada ndi ansembe ena ndipo inafunsa kuti, “Chifukwa chiyani simukukonza malo owonongeka a mʼnyumbayi? Musasungenso ndalama zina zochokera kwa abwenzi anu, koma muzipereke kuti akonzere nyumbayi.”
8 Gobele salasu dunu ilia da amane hamoma: ne sia: i, amola ilila: da Debolo Diasu bu hame hahamomu sia: i.
Ansembe anavomera kuti salandiranso ndalama kuchokera kwa anthu ndipo kuti sindiwo amene ati akonzenso nyumbayo.
9 Amalalu, Yihoida da gagili lale, ga: lu da: iya gelabo doasili, gagili oloda bega: ligisi. Amo gagili da Debolo Diasu ea logo holei heda: su lobodafadini dialebe ba: i. Debolo Diasu logo holeiga gobele salasu hawa: hamosu dunu da, dunu amo da nodone sia: ne gadomusa: misi, ilia muni lale, gagili ganodini salasu.
Koma wansembe Yehoyada anatenga bokosi ndipo anabowola chivundikiro chake. Anayika bokosilo pambali pa guwa lansembe, kudzanja lamanja la aliyense amene akulowa mʼNyumba ya Yehovayo. Ansembe amene ankalondera pa khomopo ankaponya mʼbokosi ndalama zonse zimene ankabwera nazo ku nyumba ya Yehova.
10 Ilia da amo gagili ganodini muni bagade ba: loba, hina bagade ea sia: dedesu dunu amola Gobele Salasu Hina dunu ela da misini, silifa fage lai amo idili, amola ea dioi defei ba: su.
Nthawi zonse akaona kuti mʼbokosimo muli ndalama zambiri, mlembi wa mfumu ndi mkulu wa ansembe ankabwera ndipo ankawerenga ndalama zomwe anthu ankabwera nazo ku Nyumba ya Yehova ndi kuziyika mʼmatumba.
Ankati akadziwa kuti ndalamazo zilipo zingati, ankazipereka kwa anthu amene ankayangʼanira ntchito yokonza nyumbayo. Ndalamazo ankalipira anthu amene ankagwira ntchito yokonza Nyumba ya Yehova, amisiri a matabwa ndi amisiri omanga nyumba,
12 Ilia da amo muni ea idi defele dedene, ilia amo muni Debolo Diasu hawa: hamosu ouligisu dunu ilima iasu. Amo dunu ilia da diasu gagusu dunu, gele goudasu dunu amola gele dadamusu dunu, ilima iasu. Amola ilia da ifa gaga: i, amola gele gadelalesa: i, amo bu hahamoma: ne, amola eno hawa: hamoma: ne, amo dabe iasu.
amisiri a miyala ndiponso anthu ophwanya miyala. Iwo ankagula matabwa ndi miyala yosema yokonzera Nyumba ya Yehova ndipo ankalipira zinthu zonse zofunika pokonzanso nyumbayo.
13 Be amo muniga ilia da silifa faigelei, ofodo, dalabede, gamali gesosu liligi, amola eno silifa o gouli liligi huluane, amo hahamobe dunu iligili muni hame iasu.
Koma ndalama zomwe anthu ankabwera nazo ku nyumbayo sanagulire siliva wopangira mabeseni, zozimitsira nyale, mbale zowazira magazi, malipenga kapena ziwiya zina zilizonse zagolide kapena zasiliva za ku Nyumba ya Yehova.
14 Muni huluanedafa da Debolo Diasu wadela: i buga: le hawa: hamosu dunu, iligili bidi imunusa: amola amo gagumu liligi fawane amo muniga lidisu.
Ndalamazi anazipereka kwa anthu antchito amene anazigwiritsa ntchito yokonzera nyumbayo.
15 Amo hawa: hamosu dunu ilia da moloidafa dunu. Amaiba: le, ilia da amo muni ea asi hou dedene legele hogomu hamedei ba: i.
Koma sanawafunse kuti afotokoze kagwiritsidwe ntchito ka ndalama zolipira amene ankagwira ntchito, chifukwa anthuwo ankagwira ntchitoyo mokhulupirika kwambiri.
16 Be muni amo Yuda dunu da wadela: i hou dabe gobele salasu iasu hamoma: ne i, amo da gagili ganodini hame salasu. Bai amo muni da gobele salasu dunu ilia: galu.
Ndalama zomwe zinkaperekedwa pa nsembe yopepesera machimo ndi nsembe yoperekedwa chifukwa cha tchimo sanabwere nazo ku Nyumba ya Yehova pakuti zinali za ansembe.
17 Amogalu, Silia hina bagade Ha: sa: iele da Ga: de moilai bai bagade doagala: le, hasali. Amalu, e da Yelusaleme doagala: musa: ilegei.
Pa nthawi imeneyo, Hazaeli, mfumu ya Aramu anapita kukathira nkhondo mzinda wa Gati nawulanda. Kenaka Hazaeli anatembenuka kupita kukathira nkhondo mzinda wa Yerusalemu.
18 Yuda hina bagade Youa: se da iasu liligi huluane amo e bisili hina bagade Yihosiafa: de amola Yihoula: me amola A: ihasaia ilia Hina Godema imunusa: ilegei, amola hisu iasu, amola gouli huluane Debolo Diasu amola hina bagade diasu ganodini dialu, amo huluane lale, hina bagade Ha: sa: iele ema iasi. Amalalu, Ha: sa: iele da ea dadi gagui wa: i, amo Yelusaleme fisili, masa: ne sia: i.
Koma Yowasi mfumu ya Yuda anatenga zinthu zonse zopatulika zomwe anazipatula Yehosafati, Yehoramu, ndi Ahaziya abambo ake, mafumu a Yuda ndi mphatso zonse zomwe iye mwini anazipereka: golide yense amene anapezeka mʼnyumba yosungiramo chuma cha mʼnyumba ya Yehova ndi zomwe zinali mʼnyumba ya mfumu, nazipereka kwa Hazaeli mfumu ya Aramu. Pamenepo iye anachoka ku Yerusalemuko.
19 Hina bagade Youa: se ea hamoi eno huluane da “Yuda hina bagade Ilia Hamonanu Meloa” amo ganodini dedene legei.
Ndipo ntchito zina za Yowasi ndi zonse zimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Yuda?
Akuluakulu ake anamuchitira chiwembu ndi kumupha ku Beti Milo, pa njira yotsikira ku Silo.
21 Hina bagade Youa: se ea eagene ouligisu dunu ilia da e medomusa: wamo sia: hahamoi. Ouligisu dunu aduna, amo Yosaga (Simia: de egefe) amola Yihosaba: de (Siouma egefe) ela da Sila sogega ahoasu logoa, diasu amo da osobo gasa: le lelegela heda: i Yelusaleme gusudili dialu, amo diasua Youa: se fane legei. Ilia da Youa: se amo hina bagade uli dogosu sogebi, Da: ibidi Moilai Bai Bagade ganodini, uli dogone sali. Youa: se egefe A: masaia da e bagia hina bagade hamoi.
Yozakara mwana wa Simeati ndi Yehozabadi mwana wa Someri atumiki ake anamukantha nafa. Ndipo anamuyika mʼmanda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide. Ndipo Amaziya mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.

< 2 Hina 12 >