< 2 Hina 1 >

1 Isala: ili hina bagade A: iha: be da bogoi. Amogalu fa: no Moua: be soge fi dunu da Isala: ili fi ilima odoga: i.
Atamwalira Ahabu, Mowabu anawukira Israeli.
2 Isala: ili hina bagade A: ihasaia da ea hina bagade diasu Samelia ganodini, amo da: iya gadonini osoba gudu gala: la sa: ili, se bagade nabi. Amaiba: le, e da sia: adola ahoasu dunu amo Filisidini soge ganodini Egelone moilai bai bagade fi ilia ogogosu ‘gode’ Ba: ilesibabe, ema e da uhima: bela: le o hame uhima: bela: le, amo adole ba: ma: ne asunasi.
Ndipo Ahaziya anagwa kuchokera pa khonde la chipinda chake chammwamba ku Samariya, ndipo anavulala kwambiri. Choncho iye anatuma amithenga nawawuza kuti, “Pitani mukafunse kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni, ngati ndichire matendawa.”
3 Be Hina Gode Ea a: igele dunu da Disiabe balofede dunu Ilaidia, e da amo adola ahoasu dunu ilima amane adole ba: ma: ne sia: i, “Dilia da abuliba: le Egelone fi ilia ‘gode’ Ba: ilesibabe amo ea fada: i sia: naba ahoabela: ? Bai Isala: ili soge ganodini Gode hame esala, dilia dawa: sala: ?
Koma mngelo wa Yehova anawuza Eliya wa ku Tisibe kuti, “Nyamuka, pita ukakumane ndi amithenga a mfumu ya ku Samariya ndipo ukawafunse kuti, ‘Kodi popeza kulibe Mulungu ku Israeli, nʼchifukwa chake inu mukupita kukafunsa nzeru kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni?’
4 Hina bagade A: ihasaiama amane sia: ma, ‘Hina Gode da amane sia: sa, Di da dia se nabi amo mae uhini, di da bogomu.’” Ilaidia da Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i defele hamoi.
Tsono Yehova akuti, ‘Iweyo sudzadzuka pa bedi wagonapo. Udzafa ndithu!’” Ndipo Eliya ananyamuka.
5 Amaiba: le, sia: adola ahoasu dunu ilia da hina bagadema buhagi. Hina bagade da amane sia: i, “Dilia abuliba: le buhagibala: ?”
Amithenga aja atabwerera kwa mfumu, mfumuyo inawafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mwabwerera?”
6 Ilia bu adole i, “Ninia da logoa dunu gousa: le, e da nini dima buhagili misini, Hina Gode dima sia: i liligi dima adoma: ne sia: i. Hina Gode da amane sia: i, ‘Di da abuliba: le Egelone fi ilia ‘gode’ Ba: ilesibabe amo ea fada: i sia: naba ahoabela: ? Bai Isala: ili soge ganodini Gode hame esala, dilia dawa: sala: ? Di da dia se nabi amo mae uhini, di da bogomu.’”
Iwo anayankha kuti, “Munthu wina anabwera kudzakumana nafe, ndipo anatiwuza kuti, bwererani kwa mfumu imene inakutumani ndipo mukayiwuze kuti, ‘Yehova akuti, kodi popeza kulibe Mulungu ku Israeli, nʼchifukwa chake mukupita kukafunsa nzeru kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni? Tsono sudzadzuka pa bedi wagonapo. Udzafa ndithu!’”
7 Hina bagade A: ihasaia da ilima amane adole ba: i, “Dunu e da haboda: i ganabela: ?”
Mfumu inafunsa amithengawo kuti, “Kodi munthu amene anabwera kudzakumana nanuyo ndi kukuwuzani zimenezi amaoneka bwanji?”
8 Ilia bu adole i, “E da ohe gadofoga hamoi abula ga: ne amola bulamagau gadofoga bulu ga: i ba: i.” Hina bagade da ha: giwane adole i, “Go da Ilaidia goa!”
Iwo anayankha kuti, “Munthuyo anavala zovala zaubweya ndi lamba wachikopa mʼchiwuno mwake.” Mfumu inati, “Munthu ameneyo ndi Eliya wa ku Tisibe.”
9 Amalalu, e da dadi gagui ouligisu dunu afae amola dadi gagui dunu 50 agoane Ilaidia lala masa: ne asunasi. Dadi gagui ouligisu dunu da asili, ba: loba, Ilaidia da agolo da: iya esalebe ba: i. E da Ilaidiama amane sia: i, “Gode Ea hawa: hamosu dunu! Hina bagade da di gudu sa: ima: ne sia: sa.”
Pamenepo mfumu inatuma mtsogoleri wa ankhondo ndi anthu ake makumi asanu kwa Eliya. Mtsogoleriyo anapita kwa Eliya, amene anali atakhala pamwamba pa phiri, ndipo anati, “Munthu wa Mulungu, mfumu ikuti, ‘Tsikani!’”
10 Ilaidia da bu adole i, “Defea! Na da Gode Ea dunu galea, lalu da muagadonini sa: ili, di amola dia dunu fane legei ba: mu.” Hedololewane, lalu da sa: ili, ouligisu dunu amola ea dadi gagui dunu nene dagoi.
Eliya anayankha mtsogoleriyo kuti, “Ngati ndine munthu wa Mulungu, moto utsike kuchokera kumwamba, ukupsereze iwe pamodzi ndi anthu makumi asanu akowo!” Pomwepo moto unatsikadi kuchokera kumwamba ndipo unapsereza mtsogoleriyo pamodzi ndi anthu akewo.
11 Hina bagade da ouligisu dunu eno amola dadi gagui 50 agoane Ilaidiama heda: ma: ne asunasi. Amoga asili, ouligisu dunu da amane sia: i, “Gode Ea dunu! Hina bagade da di wahadafa sa: ima: ne sia: sa!”
Zitachitika izi, mfumu inatumanso mtsogoleri wina pamodzi ndi asilikali ake makumi asanu. Mtsogoleriyo anati kwa Eliya, “Munthu wa Mulungu, zimene mfumu ikunena ndi izi, ‘Tsikani msangamsanga!’”
12 Ilaidia da bu adole i, “Defea! Na da Gode Ea dunu galea, lalu da muagadonini sa: ili, di amola dia dunu fane legei ba: mu.” Hedololewane, lalu da sa: ili, ouligisu dunu amola ea dadi gagui dunu nene dagoi.
Eliya anayankha kuti, “Ngati ndine munthu wa Mulungu, moto utsike kuchokera kumwamba, ukupsereze iwe pamodzi ndi anthu ako makumi asanuwo!” Pomwepo moto unatsikadi kuchokera kumwamba ndipo unapsereza mtsogoleriyo pamodzi ndi anthu akewo.
13 Eno agoane, hina bagade da ouligisu dunu amola dadi gagui dunu 50 agoane asunasi. Ouligisu dunu e da agoloba: le heda: le, Ilaidia ea midadi muguni bugili, ha: giwane amane adole ba: i, “Gode Ea dunu! Di da nama amola na dunuma asigima! Nini mae medole legema!
Ndipo mfumu inatumanso mtsogoleri wachitatu pamodzi ndi asilikali ake makumi asanu. Mtsogoleri wachitatuyu anakwera pa phiripo ndi kugwada pamaso pa Eliya. Iye anayankhula mopemba kuti, “Munthu wa Mulungu, chonde musandiwononge ineyo pamodzi ndi atumiki makumi asanu anuwa!
14 Ouligisu dunu aduna musa: misi amola ilia dunu da muagadodini lalu misini, amo nene dagoi ba: i. Be nama asigima!”
Taonani, moto unatsika kuchokera kumwamba ndi kupsereza atsogoleri awiri pamodzi ndi anthu awo onse. Koma tsopano musawononge moyo wanga!”
15 Hina Gode Ea a: igele dunu da Ilaidiama amane sia: i, “Ali gilisili sa: ima! Amola mae beda: ma!” Amaiba: le, Ilaidia da ouligisu dunu ela A: ihasaia ema asili,
Mngelo wa Yehova anati kwa Eliya, “Pita naye, usamuope.” Choncho Eliya ananyamuka natsika naye limodzi kupita kwa mfumu.
16 ema amane sia: i, “Hina Gode da amane sia: sa, “Di da abuliba: le amo Egelone ‘gode’ Ba: ilesibabe ema ea fada: i sia: nabimusa: , sia: adole ahoasu dunu asunasibala: ? Bai Isala: ili soge ganodini Gode hame esala, di dawa: sala: ? Di da amo hamobeba: le, mae uhini bogomu.”
Eliya anawuza mfumu kuti, “Yehova akuti, ‘Chifukwa chiyani munatumiza amithenga kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni, kukafunsa ngati muti muchire? Kodi mu Israeli mulibe Mulungu woti nʼkukuyankhani funso lanu? Choncho, popeza mwachita izi, simudzadzuka pamene mwagonapo; mudzafa ndithu.’”
17 Hina Gode da Ilaidia ea lafidili sia: i defele, A:ihasaia da bogoi. A: ihasaia da egefelali hame galu. Amaiba: le, eaeya Youla: me da e bagia hina bagade hamoi. E da Yuda hina bagade Yihoula: me (Yihosiafa: de egefe) ea ouligibi ode aduna ouligilalu, Isala: ili hina bagade hamoi.
Motero Ahaziya anafadi, monga mwa mawu a Yehova amene Eliya anayankhula. Tsono popeza Ahaziya analibe mwana, Yoramu analowa ufumu mʼmalo mwake mʼchaka chachiwiri cha Yehoramu mwana wa Yehosafati mfumu ya ku Yuda.
18 Hina bagade A: ihasaia ea hamoi liligi oda amo huluane da “Isala: ili hina bagade Ilia Hamonanu Meloa” amo ganodini dedene legei.
Ntchito zina zonse zimene Ahaziya anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Israeli?

< 2 Hina 1 >