< 2 Hou Olelesu 36 >

1 Yuda fi dunu da Yousaia egefe Youaha: se, amo Yuda hina bagade ilegele, Yelusalemega ema susuligi sogadigili, mogiligai.
Tsono anthu a mʼdzikomo anatenga Yehowahazi mwana wa Yosiya namuyika kukhala mfumu mu Yerusalemu mʼmalo mwa abambo ake.
2 Youaha: se da lalelegele, ode 23 esalu, muni Yuda hina bagade hamoi. E da Yelusaleme moilai bai bagadega esala, oubi osodayale agoane Yuda fi ouligilalu.
Yowahazi anali wa zaka 23 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa miyezi itatu.
3 Idibidi hina bagade Nigou da Youaha: se gagulaligili, e da Yuda dunu ema silifa defei 3,000 gilo amola gouli 30 gilo dabe ema ima: ne logei.
Mfumu ya Igupto inamuchotsa pa udindo wa ufumu mu Yerusalemu ndipo inakhometsa msonkho dziko la Yuda wa makilogalamu 3,400 asiliva ndi agolide.
4 Hina bagade Nigou da Yousaia egefe eno Ilaiagime, amo Yousaia bagia Yuda hina bagade hamoi. E da Ilaiagime ea dio afadenene, bu Yihoiagimi dio ema asuli.
Mfumu ya Igupto inakhazika Eliyakimu, mʼbale wake wa Yehowahazi kukhala mfumu ya Yuda ndi Yerusalemu ndipo anasintha dzina la Eliyakimu kukhala Yehoyakimu. Koma Neko anatenga Yowahazi mʼbale wake wa Eliyakimu ndi kupita naye ku Igupto.
5 Yihoiagimi da lalelegele, ode 25 esalu, e da muni Yuda hina bagade hamoi. E da Yelusaleme moilai bai bagadega esala, ode gidayale agoane Yuda fi ouligilalu. Yihoiagimi da Hina Godema wadela: le hamoi.
Yehoyakimu anali wa zaka 25 pamene anakhala mfumu, ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka 11. Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova Mulungu wake.
6 Yihoiagimi da Yuda fi ouligilaloba, Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese da Yuda soge doagala: le, golili sa: ili, hasali. E da Yihoiagimi gagulaligili sia: inega lagili, Ba: bilone sogega hiouginana asi.
Nebukadinezara, mfumu ya ku Babuloni anachita naye nkhondo ndipo anamumanga ndi zingwe zamkuwa ndi kumutenga kupita naye ku Babuloni.
7 Nebiuga: denese da Debolo Diasu noga: i liligi eno amo suguli, Ba: bilone sogega gaguli asili, ea hina bagade diasu ganodini ligisi.
Nebukadinezara anatenganso zipangizo za ku Nyumba ya Yehova kupita nazo ku Babuloni ndipo anaziyika mʼnyumba ya Mulungu wake kumeneko.
8 Yihoiagimi ea hamonanu huluane amola ea wadela: idafa hou hamonanu da “Isala: ili amola Yuda fi hina bagade Ilia Hamonanu Meloa” amo ganodini dedene legei. Yihoiagimi da bogole, egefe Yihoiagini da e bagia Yuda hina bagade hamoi.
Zochitika zina za pa ulamuliro wa Yehoyakimu, zinthu zonyansa zimene anachita ndi zonse zinapezeka kuti zinali zomutsutsa zalembedwa mʼbuku la mafumu a Israeli ndi Yuda. Ndipo Yehoyakini mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
9 Yihoiagini da lalelegele, ode 18 agoane esalu, e da muni Yuda hina bagade hamoi. E da Yelusaleme moilai bai bagadega esala, oubi udiana agoane Yuda fi ouligilalu. Yihoiagini amolawane Hina Godema wadela: le hamoi.
Yehoyakini anali ndi zaka 21 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa miyezi itatu ndi masiku khumi. Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova.
10 Woufo oubi doaga: loba, hina bagade Nebiuga: denese da Yihoiagini gagulaligili, Ba: bilone sogega hiouginana asi. E da noga: idafa liligi huluane Debolo Diasu ganodini galu, amo huluane lale, Ba: bilone sogega gaguli asi. Amalalu, Nebiuga: denese da Yihoiagini ea adabi Sedegaia amo Yuda fi amola Yelusaleme fi ilia hina bagade hamoi.
Nthawi ya mphukira, mfumu Nebukadinezara inayitanitsa Yehoyakini ndipo inapita naye ku Babuloni, pamodzi ndi ziwiya zamtengowapatali za mʼNyumba ya Mulungu wa Yehova, ndipo anayika Zedekiya malume wake kukhala mfumu ya Yuda ndi Yerusalemu.
11 Sedegaia da lalelegele, ode 21 agoane esalu, e da muni Yuda hina bagade hamoi. E da Yelusaleme moilai bai bagadega esalu, ode gidayale agoane Yuda fi ouligilalu.
Zedekiya anali ndi zaka 21 pamene ankakhala mfumu, ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka 11.
12 Hina bagade Sedegaia da Hina Godema wadela: le hamoi. E da gasa fili, Hina Gode Ea sia: ne iasu balofede dunu Yelemaia, amo ea sia: hame nabi.
Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova Mulungu wake ndipo sanadzichepetse yekha pamaso pa mneneri Yeremiya amene ankayankhula mawu a Yehova.
13 Hina bagade Nebiuga: denese da logebeba: le, Sedegaia da Gode Ea Dioba: le ema hame odoga: mu ilegele sia: i. Be Sedegaia da ema odoga: i. E da gasa fili, Isala: ili Hina Godema bu sinidigimu higa: i galu.
Iye anawukiranso mfumu Nebukadinezara amene anamulumbiritsa mʼdzina la Mulungu. Iyeyo anali wosamva ndipo anawumitsa mtima wake. Sanatembenukire kwa Yehova Mulungu wa Israeli.
14 Amola Yuda fi ouligisu dunu, gobele salasu dunu, amola dunu huluane, ilia da ilima sisiga: i fifi asi defele, loboga hamoi ogogosu ‘gode’ liligi nodone sia: ne gadobeba: le, Debolo Diasu amo Hina Gode da Hadigi dialoma: ne ilegei, amo nigima: i.
Kuwonjezera apo, atsogoleri onse a ansembe ndi anthu ena anapitirapitira kukhala osakhulupirika, kutsatira machitidwe onse onyansa a mitundu ina ndi kudetsa Nyumba ya Yehova Mulungu wawo, imene anayipatula mu Yerusalemu.
15 Ilia aowalalia Hina Gode da ili amola Debolo Diasu gaga: musa: hanaiba: le, balofede dunu ilima sisama: ne gebewane asunahoasu.
Yehova, Mulungu wa makolo awo, ankatumiza mawu kwa iwo kudzera kwa amithenga ake kawirikawiri, chifukwa ankawamvera chisoni anthu ake ndi malo ake okhalapo.
16 Be ilia da Gode Ea adola ahoasu dunuma lasogole oufesega: su, amola Gode Ea sisasu hame nabasu. Amalalu, Hina Gode Ea ilima ougi da heda: le, amoga hobeamu hamedei ba: i.
Koma iwo ananyoza amithenga a Mulungu, anapeputsa mawu awo ndipo ankaseka aneneri ake mpaka anawutsa mkwiyo wa Yehova pa anthu ake ndipo panalibenso mankhwala owachiritsa.
17 Amaiba: le, Hina Gode da Ba: bilone hina bagade ili doagala: musa: ne asunasi. Nebiuga: denese da Yuda ayeligi dunu amo Debolo Diasu ganodini ili medole legei. E da dunu huluane, ayeligi amola da: i hamoi, dunu o uda, oloi gala o dagumui, amo huluanema hame asigi. Gode da dunu huluane Nebiuga: denese ea lobo da: iya iasi.
Yehova anabweretsa mfumu ya anthu a ku Babuloni, imene inapha anyamata awo ndi lupanga ku malo opatulika, ndipo sanasiye kaya mnyamata kapena mtsikana, wamkulu kapena wokalamba. Mulungu anapereka onsewo kwa Nebukadinezara.
18 Nebiuga: denese da Debolo Diasu liligi amola hina bagade amola eagene ouligisu dunu ilia liligi huluane susuguli, Babilone sogega gaguli asi.
Iye ananyamula kupita nazo ku Babuloni zipangizo zonse za mʼNyumba ya Yehova Mulungu wawo, zazikulu ndi zazingʼono zomwe, ndi chuma cha mʼNyumba ya Yehova ndiponso chuma cha mfumu ndi akuluakulu ake.
19 E da Debolo Diasu amola moilai bai bagade huluane ulagili, amola moilai bai bagade gagoi mugululi sali.
Iwo anayatsa moto Nyumba ya Mulungu, ndipo anagwetsa makoma a Yerusalemu. Anatentha moto nyumba zonse zaufumu ndipo anawononga chilichonse chimene chinali chofunika.
20 Amalu, e da dunu hame bogoi esalu, amo huluane Ba: bilone sogega hiouginana asi. Amogawi, ilia da e amola egaga fi dunu ilia udigili hawa: hamosu dunu esalu, amogainini Besia hina bagade da gasawane heda: i.
Iye anagwira ukapolo anthu otsala amene anapulumuka ku lupanga ndi kupita nawo ku Babuloni, ndipo anakhala antchito ake ndi ana ake mpaka pamene ufumu wa Peresiya unakhazikitsidwa.
21 Amaiba: le, Hina Gode Ea balofede dunu Yelemaia ea lafidili sia: i amo huluane dafawane hamoi dagoi ba: i. E da amane sia: i galu, “Ilia Sa: bade ode helefisu hame hamobeba: le, Isala: ili soge da ode 70 agoane udigili hamedei soge agoai dialebe ba: mu.”
Dziko linakondwera ndi masabata ake. Pa nthawi yonse ya chipasuko chake nthaka inapuma, mpaka zaka 70 zinakwana pokwaniritsa mawu a Yehova amene anayankhula kudzera mwa Yeremiya.
22 Ode bisili amoga Sailase da Besia soge ouligisu, Hina Gode Ea balofede dunu Yelemaia ema musa: sia: i liligi da amo defele doaga: i dagoi ba: i. Hina Gode da Sailase ea asigi dawa: su olelebeba: le, Sailase da ea fidisu dunuma ilia da sia: amo dedene, ea soge amo ganodini dunu huluane nabima: ne idili ima: ne sia: i. Ea sia: da agoane dedei,
Mʼchaka choyamba cha Koresi mfumu ya Peresiya, pofuna kukwaniritsa mawu a Yehova amene anayankhula kudzera mwa Yeremiya, Yehova anakhudza mtima wa mfumu ya Peresiya kuti alengeze mu ufumu wake wonse ndipo anazilemba:
23 “Na, Sailase, Besia hina bagade da dilima amane hamoma: ne sia: sa. Hina Gode, Hebene amoga Hina esala, E da na osobo bagade fifi asi gala huluane ilima hina esaloma: ne hamoi dagoi. Amola E da na Yelusaleme moilai bai bagade Yuda soge ganodini amoga Ea Debolo diasu gaguma: ne ilegei. Defea! Dilia Gode Ea fi dunu huluane amoga masa! Amola Gode da dili sigi ahoanumu da defea.” Sia ama dagoi
Chimene mfumu Koresi ya Peresiya ikunena ndi ichi: “Yehova, Mulungu wakumwamba wandipatsa ine mafumu onse a dziko lapansi ndipo wandisankha kuti ndimumangire Nyumba ya Mulungu ku Yerusalemu ku Yuda. Aliyense wa anthu ake pakati panu, Yehova Mulungu wake akhale naye, ndipo apite.”

< 2 Hou Olelesu 36 >