< 2 Hou Olelesu 29 >

1 Hesigaia da lalelegele ode 25 gidigiloba, Yuda fi ilia hina bagade hamoi. E da Yelusaleme moilai bai bagade esala, Yuda fi ode 29 agoanega ouligilalu. Ea ame da Abaidia (Segalaia idiwi).
Hezekiya anali wa zaka 25 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 29. Dzina la amayi ake linali Abiya mwana wa Zekariya.
2 E da ea aowa Da: ibidi defele, Hina Gode ba: ma: ne, moloidafa hou hamonanu.
Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Davide abambo ake.
3 Hesigaia ea bai muni ouligi ode gidigili, ode eno amo, oubi agega, e da Debolo Diasu logo doasili, logo ga: su dodoa: i.
Pa chaka choyamba cha ulamuliro wake, iye anatsekula zitseko za Nyumba ya Yehova ndipo anazikonza.
4 E da gobele salasu dunu amola Lifai fi dunu mogili, Debolo gusudili gagoi ganodini gilisi.
Iye analowetsamo ansembe ndi Alevi ndipo anawasonkhanitsa ku bwalo lakummawa
5 Amogawi, e da ilima amane sia: i, “Dilia huluane nigima: fadegama: ne, hano ulalu, Gode Ea hawa: hamomusa: momogili gagama. Amola dilia aowalalia Hina Gode Ea Debolo Diasu, amoga ledo liligi huluane fadegale, bu modale ligiagama.
ndipo anati: “Mverani, inu Alevi! Dziyeretseni tsopano ndiponso muyeretse Nyumba ya Yehova Mulungu wa makolo anu. Muchotse zodetsa zonse ku malo opatulika.
6 Ninia aowalalia, da Hina Godema baligi fa: su, amola amo hou E da higa: i ba: su. Ilia da E fisiagai, amola sogebi Ea esalebe amo baligi fa: su.
Makolo athu anali osakhulupirika ndipo anachita zoyipa pa maso pa Yehova Mulungu wathu ndi kumusiya Yehovayo. Iwo anatembenuka ndi kusiya malo okhalako Yehova ndi kumufulatira.
7 Ilia da Debolo logo ga: i amola gamali huluane ha: ba: doma: ne yolesi. Ilia da Isala: ili Hina Gode Ea Debolo Diasu ganodini, gabusiga: manoma hame gobele sali, amola Ema ohe hame gobele sali.
Iwowo anatsekanso zitseko zapakhonde ndi kuzimitsa nyale. Sanafukize lubani kapena kupereka nsembe zopsereza ku malo opatulika a Mulungu wa Israeli.
8 Amaiba: le, Hina Gode da Yuda fi amola Yelusaleme fi ilima ougi galu. Amola ilima se iasu ba: beba: le, dunu huluane da fofagadigi amola bagade beda: i. Amo hou huluane dilia dawa:
Kotero, Yehova anakwiyira Yuda ndi Yerusalemu. Iye anawasandutsa chinthu chochititsa mantha, choopsa ndiponso chonyozedwa monga momwe mukuonera ndi maso anuwa lero lino.
9 Ninia ada huluane da gegesu ganodini medole lelegei dagoi ba: i. Ninia uda amola mano huluane mugululi, ga oule asi ba: i.
Ichi nʼchifukwa chake makolo athu anaperekedwa ku lupanga ndipo nʼchifukwa chake ana athu aamuna ndi aakazi ndi akazi athu ali ku ukapolo.
10 Be wali, na da Isala: ili Hina Godema, gousa: su hamoma: ne ilegei dagoi. Amalu, E da ninima bu hame ougimu.
Tsono ine ndikuganiza zochita pangano ndi Yehova Mulungu wa Israeli, kuti mkwiyo wake woopsawu utichokere.
11 Nagofelali! Mae aligima! Dilia da Ema gabusiga: manoma gobele salima: ne, amola dunu huluane Ema nodone sia: ne gadosu hou bisima: ne, Isala: ili Hina Gode da dili ilegei dagoi.”
Ana anga, musanyalanyaze tsopano, pakuti Yehova wakusankhani kuti muziyima pamaso pake ndi kumutumikira Iye, kugwira ntchito pamaso pake ndi kufukiza lubani.”
12 Lifai fi dunu amogai esalu, ilia dio da: - Sosogo Fi Lifai fi dunu amogai esalu Gouha: de...Ma: iha: de (Amasa: iai egefe) amola Youele (A: salaia egefe) Milalai...Gisia (Simina egefe) amola Idini (Youa egefe) Gesione...Youa (Simina egefe) amola Idini (Youa egefe) Elisa: ifane...Simili amola Yiaiele A: isa: fe...Segalaia amola Ma: danaia Hima: ne...Yihaiele amola Simiai Yediudane...Siema: ia amola Asaiele
Ndipo Alevi awa anakonzeka kugwira ntchito: Kuchokera ku banja la Kohati, Mahati mwana wa Amasai ndi Yoweli mwana wa Azariya; kuchokera ku banja la Merari, Kisi mwana wa Abidi ndi Azariya mwana wa Yehaleleli; kuchokera ku banja la Geresoni, Yowa mwana wa Zima ndi Edeni mwana wa Yowa;
kuchokera kwa zidzukulu za Elizafani, Simiri ndi Yeiyeli; kuchokera kwa zidzukulu za Asafu, Zekariya ndi Mataniya;
kuchokera kwa zidzukulu za Hemani, Yehieli ndi Simei; kuchokera kwa zidzukulu za Yedutuni, Semaya ndi Uzieli.
15 Amo dunu da ilia Lifai fi dunu eno gilisili, ilia huluane nigima: dodofei. Amalalu, hina bagade ea hamoma: ne sia: i defele, ilia da Hina Gode Ea Sema defele, bai muni Debolo Diasu nigima: dodofei.
Atasonkhanitsa abale awo ndi kudziyeretsa, iwo anapita kukayeretsa Nyumba ya Yehova, monga inalamulira mfumu, potsatira mawu a Yehova.
16 Gobele salasu dunu da Debolo Diasu nigima: dodofemusa: , Debolo diasua golili sa: i. Adi liligi da Gode Ea Sema dedei ganodini olelei, nigima: ba: loba, ilia gadili gaguli asi. Amogawi, Lifai fi da amo liligi lale, moilai hamega gadi gaguli asili, Gidalone Fagoga ligisi.
Ansembe analowa ku malo opatulika a Yehova kukayeretsako. Anatulutsira ku bwalo la Nyumba ya Yehova chilichonse chodetsedwa chimene anachipeza mʼNyumba ya Yehova. Alevi anatenga zimenezo ndi kupita nazo ku chigwa cha Kidroni.
17 Ilia da amo hawa: , oubi age amola eso agega muni hamonana, eso godo amoga dagoi. Ilia Debolo Diasu amola higamuni nigima: dodofei. Amalalu, ilia da eso eno godoane hawa: hamonanu, Debolo da Godema nodone sia: ne gadoma: ne, momagei dagoi ba: i.
Iwo anayamba mwambo woyeretsawu tsiku loyamba la mwezi woyamba ndipo pa tsiku lachisanu ndi chitatu la mweziwo anafika pa khonde la nyumba ya Yehova. Tsono anachita mwambo woyeretsa Nyumba ya Yehova ija masiku asanu ndi atatu, ndipo anamaliza pa tsiku la 16 mwezi woyamba.
18 Lifai fi dunu da hina bagade Hesigaiama amane sia: ne iasu, “Ninia da Debolo Diasu, liligi huluane ganodini diala, gobele salimusa: oloda, agi ga: gi legemusa: fafai amola amo hawa: hamomusa: liligi, amo huluane nigima: dodofei dagoi.
Ndipo anapita kwa mfumu Hezekiya ndi kukafotokoza kuti, “Ife tayeretsa Nyumba ya Mulungu yonse, guwa lansembe zopsereza ndi ziwiya zake zonse, ndiponso tebulo limene timayikapo buledi wopatulika pamodzi ndi zinthu zake zonse.
19 Hina bagade A: iha: se da Godema baligi fa: iba: le, Debolo liligi bagohame gaguli asi. Be amo huluane, ninia da bu lale, gaguli misini, nigima: dodofele, bu momodale ligiagai. Wali, amo liligi huluane da Hina Gode Ea oloda midadi diala.”
Takonza ndi kuyeretsa zinthu zonse zimene mfumu Ahazi anazichotsa mwa kusakhulupirika kwake pamene anali mfumu. Taziyika kutsogolo kwa guwa la Yehova.”
20 Hina bagade Hesigaia da mae aligili, Yelusaleme mimogo dunu huluane gilisili, Debolo Diasua oule asi.
Mmamawa tsiku linalo, mfumu Hezekiya inasonkhanitsa pamodzi akuluakulu a mu mzindawo ndipo inapita ku Nyumba ya Yehova.
21 Ilia da hina bagade ea sosogo fi, amo ilia wadela: i hou fadegama: ne, amola Debolo Diasu nigima: dodofema: ne, bulamagau gawali fesuale, sibi fesuale, sibi mano fesuale amola goudi fesuale oule asi. Hina bagade Hesigaia da gobele salasu dunu (Elane egaga fi dunu) amola ilia amo ohe oloda da: iya gobele salima: ne sia: i.
Iwo anabweretsa ngʼombe zazimuna zisanu ndi ziwiri ndi nkhosa zazimuna zisanu ndi ziwiri, ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri, mbuzi zazimuna zisanu ndi ziwiri monga nsembe zoperekedwa chifukwa cha tchimo la ufumu, la malo opatulika ndi Yuda. Tsono mfumu inalamula ansembe, zidzukulu za Aaroni, kuti apereke zimenezi pa guwa lansembe la Yehova.
22 Gobele salasu dunu da bisili bulamagau gawali medole lelegei. Amo bagia sibi medole lelegei amalu sibi mano medole lelegei. Ilia da amo gobele salasu liligi afae afae ea maga: me oloda da: iya fogagaga: la: i.
Choncho anthuwo anapha ngʼombe zazimunazo ndipo ansembe anatenga magazi ake ndi kuwawaza pa guwa lansembe, kenaka anapha nkhosa zazimuna zija ndipo anawaza magazi ake pa guwa lansembe; anaphanso ana ankhosa aja ndipo anawaza magazi ake pa guwa lansembe.
23 Fa: no fisimusa: , ilia goudi amo hina bagade amola eno Godema nodone sia: ne gadosu dunu ilima oule asi. Ilia da ilia lobo goudi ilia dialuma da: iya ligisi.
Mbuzi zoperekedwa chifukwa cha tchimo zija zinabweretsedwa pamaso pa mfumu ndi anthu onse, ndipo anasanjika manja awo pa izo.
24 Amalalu, gobele salasu dunu da goudi medole lelegele, ilia maga: me amo Isala: ili fi dunu ilia wadela: i hou fadegama: ne, oloda da: iya soga: si. Bai hina bagade ea hamoma: ne sia: i, da Isala: ili dunu huluane ilia wadela: i hou fadegama: ne, Wadela: i Hou Dabe Ima: ne amola Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne gobele salasu hamoma: ne sia: i.
Kenaka ansembe anapha mbuzizo ndipo anapereka magazi ake pa guwa, kuti ukhale mwambo wofafanizira machimo a Aisraeli onse, pakuti mfumu inalamula kuti nsembe yopsereza ndi yopepesera machimo zichitike chifukwa cha Aisraeli onse.
25 Hina Gode da musa: Da: ibidi ea balofede dunu Ga: de amola balofede dunu Na: ida: ne amo ela lafidili hamoma: ne sia: si Da: ibidima sia: i. Amo hamoma: ne sia: si defele, hina bagade Hesigaia da hamoi. E da Lifai dunu, ilia sani baidama amola edado fasu, amo gaguli Debolo Diasu ganodini leloma: ne sia: i.
Iye anayika Alevi mʼNyumba ya Yehova ali ndi ziwaya za malipenga, azeze ndi apangwe potsata lamulo la Davide, Gadi mlosi wa mfumu ndi mneneri Natani. Pakuti Yehova ndiye analamula zimenezi kudzera mwa aneneri.
26 Ilia gesami hea: lala dusu liligi da hina bagade Da: ibidi ea musa: dusu liligi agoai ba: i. Amola gobele salasu dunu da dalabede gaguli aliligi.
Kotero Alevi anayima okonzekera atanyamula zoyimbira za Davide ndiponso ansembe atanyamula malipenga awo.
27 Hesigaia da sia: beba: le, ilia da Wadela: i Hou Dabe Ima: ne gobele salasu Godema iamisi. Muni gobele salalalu, dunu huluane da Hina Godema nodosa gesami hea: i. Amola gesami hea: lala dusu liligi dunu da dalabede fulaboi, amola eno gesa: mi hea: lala dusu liligi dui.
Hezekiya analamulira kuti apereke nsembe zopsereza pa guwa. Pamene amayamba kupereka nsembezo, kuyimbira Yehova kunayambikanso, pamodzi ndi malipenga ndi zipangizo zoyimbira za Davide mfumu ya Israeli.
28 Dunu huluane amogai gilisi da Godema nodone sia: ne gadosu amola gesami hea: su amoga momadelai. Gesami hea: lala dusu dunu da dunanobawane, gobele salasu liligi da nei dagoi ba: i.
Anthu onse anawerama pansi ndi kulambira, pamene oyimba amayimba ndi malipenga. Izi zonse zinapitirira mpaka pa mapeto pa nsembe zopsereza.
29 Amalalu, hina bagade Hesigaia amola dunu huluane da muguni buguli, Godema nodone sia: ne gadoi.
Zopereka zitatha, mfumu ndi wina aliyense amene anali naye anagwada pansi ndi kulambira.
30 Hina bagade amola Yuda fi ouligisu dunu da Lifai fi dunuma, ilia da nodone gesami hea: su, amo Da: ibidi amola balofede dunu A: isa: fe ela dedei liligi, amo gesami hea: ma: ne sia: i. Amaiba: le, dunu huluane da hahawane bagade, muguni bugi dialawane, Godema nodone gesami hea: lalu.
Mfumu Hezekiya ndi akuluakulu ake analamulira Alevi kuti atamande Yehova potsata mawu a Davide ndi mlosi Asafu. Kotero anayimba nyimbo zamatamando mokondwera ndipo anaweramitsa mitu yawo ndi kulambira.
31 Hesigaia da dunu gilisi ilima amane sia: i, “Dilia da wali dodofei dagoiba: le, Hina Godema momogili gagai dagoi. Amaiba: le, dilia Hina Godema hahawane nodone ima: ne, Ema gobele salasu liligi gaguli misa. Dunu huluane da ea sia: nabawane hamoi. Mogili da ili hanaiba: le, ohe gobele salimusa: oule mafia: i.
Kenaka Hezekiya anati, “Inu mwadzipereka tsopano kwa Yehova. Bwerani ndipo mufike ndi nsembe ndi zopereka zachiyamiko ku Nyumba ya Yehova.” Choncho anthu onse anabweretsa nsembe ndi zopereka zachiyamiko, ndipo anthu onse amene anali ofuna mu mtima mwawo anabweretsa nsembe zopsereza.
32 Ilia da bulamagau gawali 70 agoane, sibi 100 agoane amola sibi mano 200 agoane, Hina Godema gobele salimusa: gaguli mafia: i.
Chiwerengero cha nsembe zopsereza chimene anthu onse anabweretsa chinali ngʼombe zazimuna makumi asanu ndi awiri, nkhosa zazimuna 100, ana ankhosa aamuna 200 ndipo zonsezi zinali za nsembe yopsereza kwa Yehova.
33 Amola ilia da bulamagau gawali 600 agoane amola sibi 3,000 agoane, amo Godema gobele salimusa: , amola dunu moma: ne, oule misi.
Ziweto zimene zinapatulidwa kukhala nsembe zinalipo ngʼombe zazimuna 600, nkhosa ndi mbuzi 3,000.
34 Gobele salasu dunu da amo ohe huluane medole legemu defele hame ba: i. Amaiba: le, Lifai fi dunu da ilia fidibiba: le, hawa: hamoi da dagoi ba: i. Dagoloba, gobele salasu dunu eno mogili da nigima: dodofei dagoi ba: i. (Lifai fi dunu ilia nigima: dodofesu hou da gobele salasu ilia hou baligisu. Bai gobele salasu dunu mogili da noga: le hame dodofei.)
Koma ansembe anali ochepa kuti asende zonse zopsereza. Choncho abale awo Alevi anawathandiza mpaka ntchito yonse inatha ndipo mpaka ansembe ena atadziyeretsa, pakuti Alevi anachita changu kudziyeretsa kulekana ndi momwe anachitira ansembe.
35 Gobele salasu dunu da ohe gogo gobele sasalibi, amo hou ouligisu. Amola ilia da gobei ohe, amo dunu ilia moma: ne liligi, amoga sefe duga: le, laluma gobele sasalisu. Amola ilia da waini hano amo da ohe gobele salasu gilisili iasu, amogai soga: sisisu. Ilia da agoane Debolo Diasu ganodini, nodone sia: ne gadosu hou bu hemoi.
Panali nsembe zopsereza zochuluka, pamodzi ndi mafuta a nsembe yachiyanjano ndi nsembe yachakumwa imene imachitika pamodzi ndi nsembe yopsereza. Kotero ntchito ya mʼNyumba ya Mulungu inakhazikitsidwanso.
36 Hina bagade Hesigaia amola dunu huluane da hahawane bagade ba: i. Bai Gode da amo hawa: hamosu hedolodafa hamoma: ne, ili noga: le fidi.
Hezekiya ndi anthu onse anakondwera pa zimene Mulungu anachitira anthu ake, chifukwa zinachita mwamsangamsanga.

< 2 Hou Olelesu 29 >