< 2 Hou Olelesu 26 >

1 Amalalu, Yuda fi dunu da A: masaia egefe Asaia, amo ilima hina bagade hamoma: ne ilegei. Amogala, ea lalelegei ode da 16 agoane ba: i.
Kenaka anthu onse a ku Yuda anatenga Uziya amene anali wa zaka 16, namuyika kukhala mfumu mʼmalo mwa Amaziya abambo ake.
2 (Ea ada bogole, fa: no, Asaia da Ila: de moilai bai bagade bu fedelale, amo buga: le gagui.)
Iye anamanganso mzinda wa Eloti ndi kuwubwezeranso ku Yuda abambo ake atamwalira.
3 Asaia da lalelegele, ode 16 esalu, e da muni Yuda hina bagade hamoi, amola e da Yelusaleme moilai bai bagadega esala, ode 52 agoanega Yuda fi ouligilalu. Ea ame da Yelusaleme moilai bai bagade uda, ea dio amo Yegoulaia.
Uziya anali wa zaka 16 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 70. Dzina la amayi ake linali Yekoliya wa ku Yerusalemu.
4 E da ea ada ea hou defele, Hina Gode hahawane ba: ma: ne, molole hamoi.
Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Amaziya abambo ake.
5 Ea Gode Ea Sia: fada: i sia: su dunu (Segalaia) da esaloba, e da mae fisili, Hina Godema noga: le fa: no bobogei. Amola Gode da ema hahawane dogolegele hamoi.
Iye anapembedza Mulungu nthawi ya Zekariya, amene ankamulangiza za kuopa Mulungu amene anamupatsa chipambano.
6 Asaia da Filisidini dunuma gegemusa: asi. E da moilai bai bagade amo Ga: de, Ya: bene amola A: siedode, ilia gagoi mugului dagoi. Amola A: siedode gadenene amola Filisidini soge huluane ganodini, gagili sali moilai bai bagade gaguli gagai.
Iyeyo anapita kukachita nkhondo ndi Afilisti ndipo anagwetsa makoma a Gati, Yabine ndi Asidodi. Ndipo kenaka anamanganso mizinda ya pafupi ndi Asidodi ndi malo ena pafupi ndi Afilisti.
7 Gode da e fidiba: le, e da Filisidini dunu, A:la: be fi dunu ilia da Geba: iele soge ganodini esalu, amola Miunaide fi dunu huluane hasasali.
Mulungu anamuthandiza polimbana ndi Afilisti ndi Aarabu amene amakhala ku Guri-Baala ndiponso polimbana ndi Ameuni.
8 Asaia da A: mone fima dabe ima: ne, seselala lai. Asaia da nimi bagade hamoiba: le, dunu huluane amola Idibidi dunu da ea hou lalaba asi.
Aamoni ankabweretsa msonkho kwa Uziya ndipo mbiri yake inamveka mpaka ku malire a dziko la Igupto chifukwa anali wamphamvu kwambiri.
9 Asaia da Yelusaleme gagili sali amo bainasima: ne hamoi. E da Hegomai Logo Ga: su, Fago Logo Ga: su amola dobea fei sisigagala: i, amoga diasu gado gagagula heda: i.
Uziya anamanga nsanja ku Yerusalemu ku Chipata Chapangodya, ku Chigwa cha Chipata ndi pokhotera mpanda, ndipo anayikamo chitetezo.
10 E amolawane da ohe fofole sogega diasu gagili sali gado gagagula heda: i. Amola hano wayabo bagohame dogoi. Bai e da guma: dini agolo sogea amola umia amogai ohe fofoi bagohame ouligisu. E da hawa: hamone manusa: obenai bagadeba: le, e da dunu ilima agolo sogea waini sagama: ne amola nasegagi sogea bugili moma: ne, fada: i sia: ne iasu.
Iye anamanganso nsanja ku chipululu ndi kukumbanso zitsime zambiri chifukwa anali ndi ziweto zambiri mʼmbali mwa phiri ndi ku zigwa. Iye anali ndi anthu amene ankagwira ntchito mʼminda yake ndiponso mʼminda yake ya mphesa mʼphiri ndi malo achonde, pakuti ankakonda nthaka.
11 E da dadi gagui wa: i gegemusa: momagei bagadedafa galu. Dadi gagui wa: i ea hou amola idi amo sia: dedesu dunu Yiaiele amola Masa: ia ela dedene legesu. Ela ouligisu dunu da Ha: nanaia (e da hina bagade eagene dunu).
Uziya anali ndi gulu lankhondo lophunzitsidwa bwino, lokonzekera kupita ku nkhondo mʼmagulu monga mwa chiwerengero chawo chimene mlembi Yeiyeli ndi Maaseya anasonkhanitsa motsogozedwa ndi Hananiya mmodzi mwa akuluakulu a mfumu.
12 Asaia ea dadi gagui wa: i ouligisu dunu ilia idi da 2,600 agoane.
Chiwerengero chonse cha atsogoleri a mʼmabanja oyangʼanira anthu ochita nkhondo chinali 2,600.
13 Iliha dadi gagui dunu ilia idi da 307,500 agoane. Ilia huluane da hina bagade ea ha lai dunuma gegemusa: momagei.
Pansi pa ulamuliro wawo panali asilikali 307,500 ophunzitsidwa nkhondo, gulu lamphamvu lothandiza mfumu kulimbana ndi adani ake.
14 Asaia da ea dadi gagui dunu ilima da: igene ga: su, goge agei, dialumagene ga: su habuga, da: igene ga: su bulu, oulali, dadi amola ga: muga: dadia gala: su gele, amo ilima iafui.
Uziya anawapangira asilikaliwo zishango, mikondo, zipewa zankhondo, malaya ankhondo achitsulo, mauta ndi miyala yogendera.
15 Yelusalemega, ea gegesu hahamosu dunu da liligi amoga ilia da diasu gado gagagula heda: i amola bai bagade gagoi dobea ea hegomaia amoga gele bagade gagala: su, amo hahamoi. Dunu fi huluanedafa da ea nimi bagade hou lalaba asi. Ea gasa da bu bagade heda: i. Bai Gode da e noga: le fidi.
Mu Yerusalemu anapanga makina okonzedwa ndi anthu aluso amene amagwiritsidwa ntchito pa malo otetezera a pa nsanja ndi pa ngodya kuponyera mivi ndi kugubuduzira miyala. Mbiri yake inamveka kutali ndi ponseponse pakuti anathandizidwa kwambiri mpaka anakhala wamphamvu kwambiri.
16 Be hina bagade Asaia da nimi bagade hamonoba, e da gasa fili, hina hou hi ofa: su. Amalalu, e da dafai. E da ea hina Godema odoga: ne, Debolo Diasua golili sa: ili, oloda da: iya gabusiga: manoma gobele salimusa: momagei.
Koma pamene Uziya anakhala wamphamvu kwambiri, kunyada kwake kunamuwononga. Iye sanakhulupirike kwa Yehova Mulungu wake, ndipo analowa mʼNyumba ya Yehova kukafukiza lubani pa guwa lofukizira.
17 Gobele salasu dunu A: salaia amola eno gasa bagade gobele salasu dunu 80 agoane, ilia da hina bagade ea logo hedofamusa: , ea bagia aligili asi.
Wansembe Azariya pamodzi ndi ansembe a Yehova ena 80 olimba mtima anamutsatira.
18 Ilia amane sia: i, “Asaia! Di da Hina Godema gabusiga: manoma gobele salasu hamoma: ne hame ilegei. Elane egaga fifi mabe gobele salasu dunu, ilia fawane da amo hawa: hamoma: ne momogili gagai galu. Amo Hadigi Malei Sesei yolesili, ga masa! Di da Hina Gode se nabima: ne hamoi dagoi. E da dima bu hahawane dogolegele hame hamomu.”
Iwo anatsutsana naye ndipo anati, “Sibwino kuti inu mfumu muzifukiza lubani koma zidzukulu za Aaroni, zimene zinapatulidwa kuti zizifukiza lubani. Chokani pa malo opatulika ano, pakuti inu mwakhala osakhulupirika, ndipo simudzalemekezedwa ndi Yehova Mulungu.”
19 Asaia da Debolo Diasu ganodini oloda bega: , gabusiga: manoma gobele salimusa: hanu wa: i gaguli lelu. E da gobele salasu dunu ilima ougi bagade ba: i. Amogaluwane, ‘lebolosi’ olo da ea odagia madelai dagoi ba: i.
Uziya, amene anali ndi chofukizira mʼmanja mwake wokonzeka kuti afukize lubani, anapsa mtima. Iye anakwiyira ansembewo. Ndipo ansembe aja akuona patsogolo pa guwa lofukizira lubani mʼNyumba ya Mulungu, khate linayamba pamphumi pake.
20 A: salaia amola gobele salasu dunu eno ilia da hina bagade ea odagia sosodola aligili, bagade beda: i. Ilia da e Debolo Diasu fisili masa: ne sesei. E da Hina Gode Ea se iasu lai dagoi, amo dawa: beba: le, hedolowane gadili hobeale asi.
Azariya, mkulu wa ansembe pamodzi ndi ansembe ena onse atamuyangʼana anaona kuti anali ndi khate pamphumi pake, ndipo anamutulutsa mofulumira. Ndipo iye mwini anafulumira kutuluka, chifukwa Yehova anamulanga.
21 Amalu, hina bagade Asaia ea fifi ahoanebe amogalu, e da nigima: madelai dagoi ba: i. E da bu Debolo Diasu ganodini heda: mu hamedei ba: i. Bai Hina Gode Ea Sema defele, amo da ema sema legei galu. E da mae hawa: hamone, hina: diasua udigili esalebe ba: i. Egefe Youda: me da Yuda fi ouligisu.
Mfumu Uziya anali ndi khate mpaka tsiku limene anamwalira. Iye amakhala mʼnyumba ya yekha ngati wakhate, ndipo samalowa mʼNyumba ya Yehova. Yotamu mwana wake ndiye amayangʼanira nyumba yaufumu ndipo ankalamulira anthu a mʼdzikomo.
22 Balofede dunu Aisaia (A: imose egefe) da hou eno amo hina bagade Asaia hamoi, meloa ganodini dedene legei.
Ntchito zina za mfumu Uziya, kuyambira pachiyambi mpaka pa mapeto, zinalembedwa ndi mneneri Yesaya mwana wa Amozi.
23 Asaia da bogole, hina bagade bogoi uli dogosu sogebi Da: ibidi Moilai bai bagadega dogone sali. Be e da ‘lebolosi’ olo madelaiba: le, hina bagade ilia bogoi gele gelabo ganodini hame sali. Egefe Youda: me da e bagia Yuda hina bagade hamoi.
Uziya analondola makolo ake, ndipo anamuyika pamodzi ndi makolo ake ku malo a manda a mafumu, koma osati mʼmanda mwawomo poti anthu anati, “Iyeyu anali ndi khate.” Ndipo Yotamu mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.

< 2 Hou Olelesu 26 >