< 1 Sa:miuele 29 >
1 Filisidini dunu da ilia dadi gagui dunu huluane A: ifege moilai bai bagadega gilisi. Amola Isala: ili dunu da si hano Yeseliele Fago ganodini galu, amo gadenene awalia wa: i fi.
Afilisti anasonkhanitsa asilikali awo onse ku Afeki, ndipo Israeli anamanga misasa yawo pa chitsime cha Yezireeli.
2 Filisidini hina bagade biyale gala ilia dadi gagui da (mogili idi 100 amola mogili idi eno amo 1,000) ilia da mogodigili asi. Da: ibidi amola ea dunu da ili baligili hina bagade A: igisema gilisili mogodigili asi.
Pamene atsogoleri a Afilisti ankatsogolera magulu awo ankhondo a miyandamiyanda, Davide ndi ankhondo ake ankayenda pambuyo pamodzi ndi Akisi.
3 Filisidini dadi gagui ouligisu dunu da ili ba: loba, amane adole ba: i, “Amo Hibulu dunu da abuliba: le misibala: ?” A: igise da bu adole i, “Amo da Da: ibidi, Isala: ili hina bagade Solo ea eagene ouligisu dunu afae. E da eso bagohame ani esalu. E da nama misi eso amogainini misini wali eso amoga, na da ea hou amo ganodini giadofasu hamedafa ba: su.”
Tsono atsogoleri a Afilisti aja anafunsa kuti, “Kodi Ahebri awa akufuna chiyani?” Akisi anayankha kuti, “Uyu ndi Davide, mtumiki wa Sauli mfumu ya Israeli. Iye wakhala ndi ine kwa masiku ndithu, kapena titi zaka ndipo kuyambira tsiku limene anachoka kwa Sauli mpaka lero, ine sindinapeze cholakwa mwa iye.”
4 Be Filisidini ouligisu dunu da ougili A: igisema amane sia: i, “Amo dunu da moilai amo dia igili i, amoga buhagima: ne asunasima! E da nini bisili mae gegena masa: ne, ea logo hedofama! E da gegesu ganodini sinidigili, ninima gegesa: besa: le. E da ea hina bagade ea bu ema hahawane ba: ma: ne, ninia dunu fane legema: ne agoane hamosa: besa: le, e buhagima: ne sia: ma.
Koma atsogoleri a ankhondo a Afilisti anamukwiyira Akisi kwambiri ndipo anati, “Mubweze munthuyu kuti abwerere ku malo amene unamupatsa. Iye asapite nafe ku nkhondo kuopa kuti angadzasanduke mdani wathu. Kodi iyeyu adzadziyanjanitsa bwanji ndi mbuye wake? Iyeyutu adzadziyanjanitsa ndi mbuye wake pakupha anthu ali panowa?
5 Bai amo dunu da Da: ibidi. Amola ea hou amoma nodoma: ne, Isala: ili uda da sisiogola gesami amane hea: i, “Solo da 1,000 baligili gale fane legei be Da: ibidi da 10,000 baligili gale fane legei.”
Paja ameneyu ndi Davide yemwe ankamuvinira namuyimbira kuti, “‘Sauli wapha anthu 1,000 koma Davide wapha miyandamiyanda?’”
6 A: igise da Da: ibidi ema misa: ne wele sia: ne, amane sia: i, “Na da Esalebe Isala: ili Gode Ea Dioba: le amane sia: sa. Di da na mae yolesili, dia na fuli gala: su. Di da ani gegemusa: masunu, na da defea. Di da nama misi esoha amogainini, wali eso amoga na da dia hou amo ganodini giadofasu hamedafa ba: su. Be eno Filisidini hina bagade da di hahawane hame ba: sa.
Kotero Akisi anayitana Davide ndipo anamuwuza kuti, “Pali Yehova wamoyo, iwe wakhala wodalirika ndipo chikanakhala chinthu chabwino kuti uzimenya nkhondo pamodzi nane popeza chibwerere iwe kuno ine sindinapeze cholakwa chilichonse ndi iwe. Koma atsogoleri enawa ndiwo sakukufuna.
7 Amaiba: le, ilia dima ougisa: besa: le, di diasuga olofole buhagima.”
Tsono bwerera. Upite mu mtendere kuopa kuti ungachite kanthu kena koyipira atsogoleri a Afilistiwa.”
8 Da: ibidi da bu adole i, “Hina! Na da adi wadela: i hou hamobela: ? Di da dia sia: i defele, na da muni dia hawa: hamoi amogainini misini wali esoha amoga, na hou amo ganodini wadela: i hou hame ba: i galea, di da na ouligisu amola na hina bagadeba: le, na da abuliba: le ani dia ha lai ilima gegena masunu da hamedeila: ?”
Davide anafunsa Akisi kuti, “Kodi ndachita chiyani? Kodi mwapeza cholakwa chotani mwa ine mtumiki wanu chiyambire kukutumikirani mpaka lero? Tsono chifukwa chiyani sindingapite kukamenya nkhondo ndi adani a mbuye wanga mfumu?”
9 A: igise da amane sia: i, “Dafawane! Na da dia sia: i defele dawa: sa! Di da Gode Ea a: igele dunu defele na fuligala: lala. Be hina bagade eno ilia da di nini bisili mae gegena masa: ne sia: sa.
Akisi anayankha kuti, “Ine ndikudziwa kuti ndiwe wangwiro ngati mngelo wa Mulungu. Komabe atsogoleri a ankhondo a Afilisti akuti, ‘Davide asapite nafe ku nkhondo.’
10 Amaiba: le, Da: ibidi! Aya hahabe, dilia huluane Solo yolesili, nama misi dunu da hedolo wa: legadole, hadigibi galu we soge yolesili masa.”
Tsono udzuke mmamawa, pamodzi ndi ankhondo ako amene unabwera nawo, ndipo unyamuke kukangocha.”
11 Amaiba: le, Da: ibidi amola ea dunu da golale, hahabedafa Filisidini sogega doaga: musa: asi. Amola Filisidini dunu da Yeseliele amoga asi.
Choncho Davide ndi anthu ake anadzuka mmamawa kubwerera ku dziko la Afilisti. Koma Afilistiwo anapita ku Yezireeli.