< 1 Sa:miuele 27 >
1 Da: ibidi da hisu amane sia: i, “Eso afae enoga Solo da na fane legemu. Na hamomu noga: idafa da Filisidini dunu ilia sogega hobeale masunu. Amasea, Solo da Isala: ili soge ganodini na hogolalu yolesimu, amola na da gaga: i dagoi ba: mu.
Davide anaganiza mu mtima mwake nati, “Tsiku lina ine ndidzaphedwa ndi Sauli. Palibe chabwino ndingachite, koma kuthawira ku dziko la Afilisti. Kotero Sauli adzasiya kundifunafuna mʼdziko lonse la Israeli, ndipo ndidzapulumuka.”
2 Amaiba: le, Da: ibidi ea 600 dadi gagui dunu ilia da amo galuwane Ga: de moilaia hina bagade A: igise (Ma: ioge egefe) ema asi.
Choncho Davide ndi anthu 600 amene anali nawo anachoka napita kwa Akisi mwana wa Maoki mfumu ya ku Gati.
3 Da: ibidi, ea dunu amola ilia sosogo fi huluane da Ga: de moilaiga ha: ini fi. Da: ibidi da ea uda aduna amo Ahinoua: me, (Yeselielega fi uda) amola Gamele amoga misi uda A: biga: ile, Na: iba: le ea didalo, amo ela oule asi.
Davide anakhala ndi Akisi ku Gati pamodzi ndi ankhondo ake, aliyense ndi banja lake. Davide ali ndi akazi ake awiri, Ahinoamu wa ku Yezireeli ndi Abigayeli wa ku Karimeli, mkazi wamasiye wa Nabala.
4 Solo da Da: ibidi Ga: de moilai bai bagadega hobea: i nababeba: le, e da Da: ibidi hogolalu yolesi.
Sauli anamva kuti Davide wathawira ku Gati, ndipo sanamufunefunenso.
5 Da: ibidi da A: igisema amane sia: i, “Di da na sama galea, na amo ganodini esalumusa: moilai fonobahadi nama ima. Na da ani moilai bai bagade amo ganodini esalumu da hamedei galebe.”
Kenaka Davide anawuza Akisi kuti, “Ngati ndapeza kuyanja pamaso panu mundipatse malo dera limodzi la dziko lanu kuti ndizikhala kumeneko. Mtumiki wanu adzakhala mu mzinda waufumu chifukwa chiyani?”
6 Amaiba: le, A:igise da Sigala: ge moilai ema i. Amohaganini, Yuda hina bagade dunu ilia da gebewane Sigala: ge moilai bai bagade gagulala.
Choncho tsiku limenelo Akisi anamupatsa Zikilagi ndipo mzindawo wakhala wa mafumu a Yuda mpaka lero.
7 Da: ibidi da Filisidini soge amo ganodini oubi 16 agoane esalu.
Davide anakhala mʼdziko la Afilisti kwa chaka chimodzi ndi miyezi inayi.
8 Amo esoga, Da: ibidi amola ea gegesu dunu ilia da Gisie, Gesi amola A: malege fi dunu (amo da amo soge ganodini gebewane esalu) ilima doagagala: lu. E da ilia sogega doagagala: lu asili, Sie soge baligili, Idibidi sogega doaga: su.
Tsono Davide ndi anthu ake ankapita kukathira nkhondo Agesuri, Agirizi ndi Aamaleki. (Mitundu ya anthu imeneyi kuyambira kale inkakhala mʼdziko la pakati pa Suri ndi Igupto).
9 E da dunu amola uda huluane fane lelegele dagole, amalu ilia sibi, bulamagau, dougi, ga: mele amola abula amolawane sasamogene gaguli asi. Amalu e da A: igisema buhagisu.
Davide ankati akathira nkhondo dera lina, sankasiya munthu wamoyo, mwamuna kapena mkazi, koma ankatenga nkhosa, ngʼombe, abulu, ngamira ndi zovala, pambuyo pake nʼkubwerera kwa Akisi.
10 Amalalu, A:igise da ema adole boba: lusu, “Di da waha habidili doagala: la asibala: ?” Amola Da: ibidi da ema e da Yuda ga (south) sogega o Yilamiele fi ilia sogega o Ginaide fi ilia esalebe sogega doagala: musa: asi, amo bu adole iasu.
Akisi akafunsa kuti, “Kodi lero unapita kukathira nkhondo kuti?” Davide ankayankha kuti, “Ndinapita kukathira nkhondo kummwera kwa Yuda,” mwinanso ankanena kuti, “Ndinapita ku dziko la Ayerahimeeli” kapenanso ankanena kuti, “Ndinapita ku dziko la Akeni.”
11 Da: ibidi ea hou da, e da dunu amola uda huluanedafa fane lelegelalusu. Amalalu, dunu asili, Ga: de fi ilima Da: ibidi ea houdafa hamoi olelemu da hamedafa galu. Da: ibidi da Ga: de sogega esaloba, amo hou gebewane hamonanusu.
Davide sankasiya mwamuna kapena mkazi wamoyo kuti akafotokozere anthu a ku Gati zochitikazo kuopa kuti opulumukawo akhoza kudzanena kuti “Davide watichita zakutizakuti.” Tsono izi ndi zimene Davide ankachita pamene ankakhala mʼdziko la Afilisti.
12 Be A: igise da Da: ibidi ea hou da moloidafa dawa: beba: le, hisu amane sia: i, “Hina: dunu fi Isala: ili ilia da Da: ibidi bagadewane higabeba: le, e da eso huluane na hawa: hamosa gebewane esalumu.”
Akisi ankamukhulupirira Davide ndipo ankati mu mtima mwake, “Davide wadzisandutsa munthu woyipa kwambiri pakati pa anthu ake omwe, Aisraeli. Tsono adzakhala mtumiki wanga mpaka kalekale.”