< 1 Sa:miuele 21 >

1 Da: ibidi da Ahimelege (gobele salasu dunu) Noube moilai bai bagadega esalu, amoga asi. Ahimelege da hisu yaguguli ema gousa: musa: misini, amane adole ba: i, “Di da abuliba: le disuwane goeguda: misibala: ?”
Davide anapita ku Nobi kwa wansembe Ahimeleki. Ahimelekiyo ankanjenjemera pamene ankamuchingamira, ndipo anafunsa kuti, “Muli nokha chifukwa chiyani? Chifukwa chiyani mulibe wokuperekezani?”
2 Da: ibidi da bu adole i, “Na da hina bagade ea hamobegawane goeguda: misi. E da na hamoma: ne asunasi we enoma mae sia: ma: ne sia: i. Be na dunu oda ni ilegei sogea nama doaga: ma: ne adosi.
Davide anayankha Ahimeleki kuti, “Mfumu yandituma zinthu zina ndipo yandiwuza kuti, ‘Munthu aliyense asadziwe za zimene ndakutumazo.’ Kunena za anthu anga, ndawawuza kuti tikakumane pamalo pena pake.
3 Di da adi ha: i manu ganabela: ? Di da nama agi gobei biyale galea o eno liligi gagui galea, nama ima.”
Kodi muli ndi chakudya? Patseniko malofu a buledi asanu, kapena chilichonse muli nacho.”
4 Ahimelege da amane sia: i, “Na da agi ga: gi gobei udigili dialebe hame. Be Godema gobele salimusa: sema liligi fawane gala. Dia dunu da uda fisili, gilisili hame golai galea, defea digili moma.”
Koma wansembeyo anamuyankha Davide kuti, “Ine ndilibe buledi wamba woti ndikupatseni. Koma pali buledi wachipembedzo yekha. Ngati anthu amene muli nawo sanagone ndi akazi awo mukhoza kudya.”
5 Da: ibidi da bu adole i, “Defea! Na dunu da uda fisili, gilisili hame golai. Ninia da eso huluane hina bagade ea hawa: hamoma: ne ahoasea, sema defele udama hame doaga: sa. Wali hamobe da bagadeba: le, ninia da ledo mae hamoma: ne, amo sema baligili dawa: sa.”
Davide anayankha kuti, “Kunena zoona sitinakhudzane ndi mkazi monga timachitira nthawi zonse tikakhala pa ulendo. Anthu anga salola kudziyipitsa ndi mkazi ngakhale pa ulendo wamba. Nanji lero tili pa ulendo woterewu!”
6 Amaiba: le, gobele salasu dunu da sema agi ga: gi gobei amo Da: ibidima i. Bai sema agi gobei Godema ianu, (amo da gaheabolo agi gobei legema: ne, musa: agi ga: gi da sema fafai amoga fadegai ba: i) amo fawane dialebe ba: i.
Choncho wansembe uja anamupatsa buledi wachipembedzo popeza kunalibeko buledi wina aliyense koma yekhayo amene amaperekedwa kwa Yehova. Uyu ndi amene anachotsedwa tsiku limenelo kuti ayikepo wina wotentha.
7 (Solo ea laigebo fofoi bisilua ouligisu dunu, Idome soge dunu ea dio amo Douege, da amo esoha amogawi esalu. Bai e da Gode Ea sema hawa: hamosu hamoma: ne misi.)
Koma tsiku limenelo mmodzi wa antchito a Sauli anali pomwepo kudikirira kuti achite mwambo wa chipembedzo mʼnyumba ya Mulungu. Munthuyu dzina lake anali Doegi Mwedomu, munthu wamphamvu pakati pa abusa a Sauli.
8 Da: ibidi da Ahimelegema amane sia: i, “Di da goge agei o gegesu gobihei sedade nama imunu ganoma: bela: ? Hina bagade da nama hedolowane masa: ne sia: beba: le, na da gegesu gobihei o gegesu liligi eno gagumu hamedei ba: i.”
Davide anafunsa Ahimeleki kuti, “Kodi muli ndi mkondo kapena lupanga pano? Ine sindinatenge lupanga langa kapena chida china chilichonse chifukwa zimene andituma amfumu ndi zamsangamsanga.”
9 Ahimelege da bu adole i, “Na da Filisidini dunu Goulaia: de (amo di da Ila fagoga fane legei) amo ea gegesu gobihei fawane gala. Amo da Ifode baligia abulaga lala: gili diala. Di hanai galea, lama. Gegesu liligi eno da hame. Afa gofawane!” Da: ibidi da amane sia: i, “Nama ima! Amo gobihei da noga: idafa. Baligisu liligi da hame gala.”
Wansembeyo anayankha kuti, “Kuno kuli lupanga la Goliati Mfilisiti uja amene unamupha mʼchigwa cha Ela, lakulungidwa mʼnsalu paseli pa Efodi. Ngati mufuna kulitenga, tengani popeza kuno kulibe lina koma lokhalo.” Davide anati, “Palibe lina lofanana nalo. Ndipatseni lomwelo.”
10 Amaiba: le, Da: ibidi da asi. E da Soloba: le hobeale asili, Ga: de moilai bai bagade hina bagade A: igise ema doaga: i.
Tsiku lomwelo Davide ananyamuka kuthawa Sauli ndipo anapita kwa Akisi, mfumu wa ku Gati.
11 Hina bagade A: igise ea eagene ouligisu dunu da ema amane sia: i, “Amo dunu da Isala: ili soge hina bagade Da: ibidi. Amo dunu ea hou olelema: ne, uda da siogolala amane gesami hea: i, ‘Solo da 1,000 baligili gale fane legei, be Da: ibidi da 10,000 baligili gale fanelegei.”
Koma nduna za Akisi zinafunsa mfumuyo kuti, “Kodi uyu si Davide mfumu ya dzikoli? Kodi iyeyu si uja pomuvinira ankayimba kuti, “Sauli wapha 1,000, koma Davide wapha miyandamiyanda?”
12 Da: ibidi da ilia amane sia: dabe nababeba: le, oso dogone beda: i. Amola e da hina bagade A: igiseba: le bagadewane beda: i.
Mawu amenewa anamulowa kwambiri Davide mu mtima ndipo anayamba kuopa kwambiri Akisi mfumu ya ku Gati.
13 Amaiba: le, habogala dunu da e gadenena manebe ba: loba, e da ogogole doulasi elabusu dunu agoane hamosu, amola ilia da e gagulaligili ba: su, be e da bu gagaba: gisu. E da moilai logo ga: su damana udigili dedesu amola lafidi defo sasia: le, mayabo damana bodola: i.
Choncho anasintha makhalidwe ake pamaso pawo, nʼkudzisandutsa ngati wamisala. Iye ankangolembalemba pa zitseko za chipata ndi kumangotuluka dovi, nʼkumayenderera mʼndevu zake.
14 Amaiba: le, A:igise da ea eagene ouligisu dunu ilima amane sia: i, “Ba: ma! Amo dunu da doulasi dagoi. Dilia da abuliba: le e nama oule misibala: ?
Akisi anawuza nduna zake kuti, “Mukumuona munthu uyu kuti ndi wamisala! Nʼchifukwa chiyani mukubwera naye kwa ine?
15 Na da doulasi dunu bagohame ouligisa. Abuliba: le eno agoaiwane nina: diasua guiguda: , nama ougima: ne oule mahabela: ?”
Kodi ine ndikusowa anthu amisala kuti muzibwera naye munthuyu kwa ine kuti azidzachita zamisala zake pamaso panga? Kodi munthu ameneyu nʼkulowa mʼnyumba mwanga?”

< 1 Sa:miuele 21 >