< 1 Sa:miuele 19 >

1 Solo da egefe Yonada: ne amola ea ouligisu dunu huluane ilima e da Da: ibidi fane legemusa: sia: ilegei. Be Yonada: ne da Da: ibidima bagade dogolegei galu.
Sauli anawuza mwana wake Yonatani ndi nduna zake zonse kuti aphe Davide. Koma Yonatani amamukonda kwambiri Davide.
2 Amaiba: le, Yonada: ne da Da: ibidima amane sia: i, “Na ada da di fane legemusa: logo hogolala. Aya hahabe noga: le dawa: ma! Wamoaligisu soge hogole, amogawi esaloma!
Choncho anawuza Davide kuti, “Abambo anga Sauli akufuna kukupha. Tsono uchenjere. Mmawa upite ukabisale ndipo ukakhale komweko.
3 Na da ada ani asili, dia wamoaligi dialebe amo gadenene aligili, dimadi sia: na adama sia: mu. Na da dima hamomu sia: nabasea, amo dima adomu.”
Ine ndidzapita ndi kukayima pafupi ndi abambo anga ku munda kumene iwe ukabisale. Ndipo ndidzayankhula ndi abambo anga za iwe ndipo chilichonse chimene ndikamve ndidzakuwuza.”
4 Yonada: ne da Soloma Da: ibidi ea hou nodone olelei. E amane sia: i, “Ada! Dia hawa: hamosu dunu Da: ibidima mae giadofale hamoma. E da dima giadofale hamedafa hamoi. Be e da dima giadofale mae hamone, e da dima fidisu hou baligili bagadedafa hamoi.
Tsono Yonatani anakanena zabwino za Davide kwa abambo ake Sauli ndipo anati, “Mfumu musachimwire mtumiki wanu Davide, sanakuchimwireni, koma amakuchitirani zabwino kwambiri.
5 E da ea esalusu mae dawa: le, Goulaia: de fane legei. Amalalu, Hina Gode da Isala: ili fi ilia baligili hasalasimusa: hamonesi. Di da amo ba: loba, nodoi. Amaiba: le, di da abuliba: le hame giadofasu dunu amo bai hamedenewane fane legemusa: dawa: bela: ?”
Iye anayika moyo wake pa chiswe pamene anapha Mfilisiti uja. Choncho Yehova anachita zazikulu popambanitsa Aisraeli pa nkhondo. Inu munaona zonsezo ndipo munakondwera. Nanga nʼchifukwa chiyani mukufuna kuchimwira munthu wosalakwa pofuna kupha Davide?”
6 Solo da Yonada: ne ea sia: nababeba: le, dafawaneyale dawa: i. E da Hina Gode Ea Dioba: le, Da: ibidi ea hame fane legemu ilegele sia: i.
Sauli anamvera mawu a Yonatani ndipo analumbira kuti, “Pali Yehova, Davide sadzaphedwa.”
7 Amaiba: le, Yonada: ne da Da: ibidi wele guda: le, Solo ea sia: i liligi huluane ema adole i. Amalalu, e da Da: ibidi amo Soloma oule asili, Da: ibidi da ea musa: hamoi defele bu Solo ea hawa: hamosu.
Pambuyo pake Yonatani anayitana Davide namuwuza zonsezi. Choncho Yonatani anabwera naye Davide kwa Sauli ndipo ankamutumikira Sauliyo monga kale.
8 Filisidini dunu amola Isala: ili dunu da bu gegei. Da: ibidi da ilima doagala: le, ilima noga: le hasalasibiba: le, Filisidini dunu da hobeale afia: su.
Panabukanso nkhondo ina ndipo Davide anapita ndi kukamenyana ndi Afilisti. Iye anawakantha mwamphamvu kotero kuti Afilisti anathawa.
9 Ha afaega, wadela: i a: silibu Hina Godemadi misi da Soloma aligila sa: i. E da hi diasua goge agei hi loboa gaguli esalu, amo Da: ibidi da amoga ea sani baidama dusa esalu.
Tsiku lina mzimu woyipa uja unafikanso pa Sauli. Nthawi imeneyi nʼkuti Sauli uja ali mʼnyumba mwake, mkondo uli mʼdzanja lake ndi Davide akuyimba zeze,
10 Solo da ea goge agei amoga Da: ibidi dobeala bobodole danoma: nesimusa: gala: le ba: i. Be Da: ibidi da giadofale, goge agei da dobea damana nudasi. Da: ibidi da hame ludiba: le, hobeale asi.
Sauli anafuna kumubaya Davide ndi kumukhomera kukhoma, koma Davide anapewa mkondowo kotero Sauli anakabaya pa khoma. Usiku womwewo Davide anathawa.
11 Amogala gasiawane, Solo da Da: ibidi ea diasu ba: lesili hahabe fama: ne, hawa: hamosu dunu asunasi. Da: ibidi idua Maiga: le da ema amane sisa: i, “Di da wali gasia hame hobeale dasea, aya medole legei dagoi ba: mu.”
Usiku womwewo Sauli anatumiza anthu ku nyumba ya Davide kuti akamubisalire ndi kumupha mmamawa. Koma Mikala mkazi wake anamuchenjeza nati, “Ngati usiku uno supulumutsa moyo wako, mawa udzaphedwa.”
12 Maiga: le da Da: ibidi fo misa: ne agenesi gelabodi amoga gudu asunasia guduli, e da hobea: i.
Choncho Mikala anamutulutsira Davide pa zenera, ndipo anathawa ndi kupulumuka.
13 Amalu, e da dununa hamoi ogogosu ‘gode’ liligi diasua bugisi amo lale, diaheda: su da: iya diasili, goudi hinaboga hamoi dialuma fugululisili, abula sosonesi.
Kenaka Mikala anatenga fano naligoneka pa bedi nayika pilo wa ubweya wa mbuzi ku mutu kwa fanolo ndipo analifunditsa nsalu.
14 Solo ea dunu da Da: ibidi lala manoba, Maiga: le da ilima amane sia: i, “E da oloi diala.”
Pamene amithenga a Sauli aja anafika kuti akamugwire Davide, Mikala anati, “Davide akudwala.”
15 Be Solo da ea hawa: hamosu dunu ilia siga Da: ibidi oloi dialebe ba: ma: ne bu asunasi. E ilima amane sia: i, “Ea diaheda: su da: iya dialebe, amo goeguda: gaguli misa. Amasea, na da e medole legemu.”
Koma Sauli anatumanso anthuwo kuti akamuone Davide, nati, “Mubwere naye kuno ali pa bedi pomwepo kuti ndidzamuphe.”
16 Ilia da ganodini sa: ili ba: loba, dununa hahamoi liligi amo da goudi hinaboga hamoi busafugululi diasi dialebe ba: i.
Koma pamene anthuwo analowa, anangoona fano pa bedipo ndi pilo wa ubweya wa mbuzi ku mutu kwake.
17 Solo da Maiga: lema adole ba: i, “Di da abuliba: le na ha lai hobeama: ne nama ogogobela: ?” Maiga: le da bu adole i, “Na da e hobeama: ne hame fidisia, e da na fane legemu sia: i.”
Tsono Sauli anafunsa Mikala kuti, “Nʼchifukwa chiyani wandinamiza chotere polola kuti mdani wanga athawe?” Mikala anayankha kuti, “Davide anandiwuza kuti, ‘Ukapanda kutero ndikupha.’”
18 Da: ibidi da hobeale, La: ima sogega, Sa: miuelema asili, Solo ea ema hamoi liligi huluane ema adole i. Amalu, e amola Sa: miuele ela da Na: iode amoma asili esalu.
Choncho Davide anathawa napulumuka. Pambuyo pake anapita kwa Samueli ku Rama nakamuwuza zonse zimene Sauli anamuchita. Kenaka iye ndi Samueli anapita kukakhala ku Nayoti.
19 Solo da Da: ibidi amo da Na: iode sogebi, La: ima soge amo ganodini esalebe nabi.
Sauli anamva kuti, “Davide ali ku Nayoti ku Rama.”
20 Amaiba: le, e da dunu amo Da: ibidi gagula masa: ne asunasi. Ilia da asili ba: loba, Sa: miuele hi ouligili balofede dunu huluane gilisi da hoahoasa gogosa: dalebe ba: i. Amalu, Hina Gode Ea A: silibu Hadigidafa da Solo ea dunu ilima aliligila dabeba: le, ilia amola da momadelale hoahoasa gogosa: dusa: i.
Choncho iye anatumiza anthu kuti akamugwire Davide. Koma anaona gulu la aneneri likulosera ndi Samueli akuwatsogolera. Pomwepo Mzimu wa Mulungu unawafikira ndipo nawonso anayamba kulosera.
21 Solo da amo sia: nababeba: le, e da dunu eno dewane asunasi. Be ilia amola da amanewane momadelale hoahoasa gogosa: dusa: i. E da dunu mogi osoda eno asunasi, be ilia da amanewane hamoi.
Sauli atamva zimenezi anatumizanso anthu ena, koma nawonso anayamba kulosa. Anatumanso anthu ena kachitatu, koma nawonso anayamba kulosa.
22 Amalalu, Solo hi bisili La: ima soge amoga masusa: asi. E da hano si bagade Sigu sogebiga dialu amoga doaga: le, Sa: miuele amola Da: ibidi da habia: le nababa: loba, ela da Na: iode sogega esalayabe nabi.
Pomaliza Sauli mwini wake ananyamuka kupita ku Rama ndipo anafika ku chitsime chachikulu cha ku Seku. Ndipo anafunsa, “Samueli ndi Davide ali kuti?” Munthu wina anamuyankha kuti, “Ali ku Nayoti ku Rama.”
23 Solo da amoga ahoanoba, Gode Ea A: silibu da ema aligila sa: ili, e da hoahoasa gogosa: ahoana, Na: iode sogebiga doaga: i.
Choncho Sauli anapita ku Nayoti ku Rama. Koma Mzimu wa Mulungu unafikanso pa iye ndipo ankalosa akuyenda mpaka anafika ku Nayoti.
24 Solo da Sa: miuele ea si da: iyawane hoahoasa, abula huluane gigisa: le fasili gogosa: lalu, amo esoha amola gasia e da da: i nabado solegadole gebewane dialu. (Amo hou hamobeba: le, fa: no dunu da amane sia: dasu, “Solo da balofede dunu hamobela: ?”)
Nayenso anavula zovala zake nayamba kulosa pamaso pa Samueli. Kenaka anagona wamaliseche tsiku lonse ndi usiku wonse. Nʼchifukwa chake anthu amati, “Kodi Sauli alinso mmodzi wa aneneri?”

< 1 Sa:miuele 19 >